zikomo kwambiri m'bale wanga ndimaganiza ngati ndindekha ndimaganiza choncho..ndikufuna number yake ndimuyankhule mwapadela ndi galu wamunthu uyu ali ndidyela simasewera akuyalutsa chisilamu
SHEIH MWAPALA ULALIKIWANU MUMAFUNA AKUTAMENI A PRESIDENT PALIBE CHANZERU MWAYANKHULAPO APA ALLA WAKE UTIYO ANGAKONDEE NDI ZOMWE AKUCHITA CHAKWERAYO AYI INUSO ALLA AKUONENI
Ulaliki oti sungatingele kumoyo wosatha komaso sungasithe kalikose. Koma anthu akuwombela mmanja. Ulaliki oti mukupanga taget Boni kalindo, Bakili muluzi tv komaso limpopo FM. Ife we are not going to support any usiles speach or teaching like this wadya bamzi shehe.
Tayesedwa ndi president wakhaza chakwera ndie timupempha Allah kuti atichosele chakwelayo ameen
Sheikhe ulaliki wanu siukugwilizana ndi ma aya omwe mumatulutsa pakamwa panu, uku ndikugulitsa mawu amulungu, ambuye akumvelen chison Ameen
Analandila ndalama nkhani anaiyamba bwino kukasokoneza kumapeto zachamba
zikomo kwambiri m'bale wanga ndimaganiza ngati ndindekha ndimaganiza choncho..ndikufuna number yake ndimuyankhule mwapadela ndi galu wamunthu uyu ali ndidyela simasewera akuyalutsa chisilamu
Basi sitilankhula zambili tingokusungirani ulemu Sheikh Anthu.
Sheikh mwadya now ndrama
7:53 7:53 Chikangawa akupatsani million yinu zaziiiiii nkhanizanu
Mayeselo aifa muyesa ife sitimaziwaaa,
Nde imfazake zochita kumugwira munthu pakhosi mwadaladala , kumuombela mfuti mkamwa munthu ,kodi yinu mulankhulabwanj muli ndiwumunthuyinu ,aaa muzichotsela ulemu nokhatuyinu mwangotengana nonse odya ndalama zamagazibasi ,
Afitiwo alimwetuuuu ati zikuyenda malawi wake utiyo amene mungamunamize lelo ,
Azibusa muzichotsera ulemu nokha mwamva
Maa Shaa Allah
May Allah bless this message and make it beneficial
Wadya nawo ndalama zamagazi iwee, usatinamize asilamufe pamodzi ndi amalawife, ifenso ndife asilamutu, mayesero ukunena apawa simayesero ochokeraxkwa ALLAH, awa ndimayesero ochokera kwa satana kudzela kwa chizukulu tudzi chake chotchedwa chakwela ndi boma less lake 😂😂😂😂😂
Odya ndalama zamagazi ngati akumasowa zoyankhula zawo? Allah mukunenayo akuyendereni Sheik😢
Ameen sheikh Allah ahead u. From Cape Town centre
Chemoto alipomwepo anapha ALLAN WITIKA, anapha chilima kuchikangawa 😂😂😂😂
Amen and amen uthenga wamphavu ambuye alemekezeke ndipo akhululukire zochimwa zathu
Naam sheikh ma shaa Allah ulaliki wabwino ndithu ❤❤❤❤
Mwadya zingati
Aliyese wanyambita ndalama zoti azizilise za imfa yachilima ndikupepha Yehovah Mulungu wathu amuonetse kiyama akumane ndi mavuto
God bless you sheik for unity message ❤
❤Allah give you more life and imaan to defending this deen
Maashallah sheikh
Aaaa sizomwezija Izi inu asheikh opanda manyazi ,
Panja peni peni wadya ndalama Za Chikangawa uyu,
Sali pachilungamo uyu
Ameen thuma ameen Allah tichotseleni President ameneyu..ndipo tipatseni mtsogoleri wabwino mdziko mwathu muno
Mukufuna mutamike. M'nungu tam'nyekule ngulumbira une
mweye che kuntamba 🔥🔥
*WA ALYKUM SSALAAM WARAHAMATULLAHI WABARAKATUHU,,,,Inna lillah wa Inna ilayh rajoon*
Ma vesi ali apa zili kutali tali . Aaaaaaa koma akulu akulu sheikh mudziima pachilungamo komanso ma ves osamawakhitetsa ai
Kkkkkkkkkkk wabodza ndiwe ma inovolopu yakutseka pakamwa ya chakwela, zikhale ndi kunkuyu 😂😂😂 waukape ndani sakudziwa.
Sheikh awa salibwino akugulitsa mawu aMulungu ndi ntengo wotsika mukankhanthidwa mutsiku lomaliza
100% shehe uthenga omanganga dziko
Ili ndiye gulu loyitana chakwela ku Eid atawapasa mbia makwacha mashehe adyera ichoooo!
Usatiipisile Islam yathu iwe wamva , bwanji sukuwalesa makafiir omwe ulinawo pomwepowo kuti azikha okonda anzawo?
Mwapatsidwa ndalama
Komabe sitinganame pa chilungamo.
Saulos Chilima anaphedwa ndi ndege ya boma la mcp
Ndine msilamunso koma sheikh uyu wapochelaapo nkhani anaiyamba bwino kukasokoneza kumapeto akatero anali ku state house
Awa ndye mau ochokwera kwa Mulungu osati Za Anja amaziyesa Okha opambana
Alhamudulillla sheih my Allah bless you all the time what's a sweet Message like 💋💗 this Marshall ( port Erizabeth SA missionvale
Ana usawi chemwalimu apochele silingwa
Soni jamanja
God bless you Sheik all the time ❤❤❤❤❤
Mmmmm sheikh zoona malo molankhula chilungamo pamaso pa anthu muli busy kubisa choona.Pamenepotu padali anzanu koma lero alikyt
Nyasi zenizeni pamaso pamulungu chilungamo mukuchidziwa Shehe iwe. Wadya ndalama
Sheikh ilim yanu ndiyochepa mupite mukaphunzirenso, ngati mukuzitenga zinthu za Allah maso mmwamba eeeeee chilango chaukali chkupezani pompo mulipo asakutameni awowo andalewo ndizotsala , ifenso tinaphunzira kwambiri kuposa iweyo xxx
Kkkkkk sheikh wasanjatu uyu 😅
No i was interested ndi ulaliki wanu Sheikh koma kumapetoko mwandionongela data yanga😭😭😭😭
Ine ndine Msilamu, uyu ndi sheikh wa chishiya uyu kafiir weniweni uyu,
Sheikhe wamanyi uyu mbuz
@@HusseinAdamLidezo zoona angamasinthanise chisilamu ndi ndalama?, bwanji sakulesa asatana anzakewa kuzunza ndikupha anthu mdziko muno ?
Kukangotinyasisila deen yathu mbuzi ya shaikh
Masha Allah ❤❤❤
Bas allah awadalotse ndi ulaliki wawow
Msilamu wolakira zau Mulungu osati enewa .Akuti ngati munthu wa mulungu walalika osanyoza president akuti ndiye sadziwa kulalikira. Shame
Soka kwaiye akupindisa chilungamo popeza akuziyandikisa matako ake kumoto
Zikhale ng'oma akuwombelanso mmanja pamfundoless zomwe wanena, kodi unamulesa kuti asamaphe ma ruandaniz and Burundians komanso amalawi?.
Inu nde muletsa zoipazooo suyu muyamikira mfiti ,wakuba, musatinyase
Ma shaallah ma shaallah ma shaallah
Izo mzoona zoti tiziphunzisana zabwino ndikulesana zoyipa, funso kwa iweyo shehe ndiloti;
Kodi zoipa zomwe akuchita chakwelayo wamulesa?
Kupha kumene akupha aboma anthu kumalawi kuno wawalesa aboma ako awusiluwo ?,
Thanks shelk potipatsa ulaliki wabwnowu
Ngakhale mawu akewo akupepuka zoyakhula zakeso kumalemelera abusa aja
Mzimu wa Chilima ukunyetseni nonse amene mukugawa ma yellow band ndi inu amene mukudya ma bans
sheikh zamanyazitu iziii kufuna kuoneka wabwino pamanso pa pule mwadya zingat
Ndipo inu zosayenda
Chemoto akhale Kunkuyu😅😅😅😅
Munthu angopha anthu inu mukamuyimile , munthu onyoza chisilamuyo inu mukamuyimile angapilile zimenezo ndani
Kodi yinu mufuna azakupheleni agogo anu mpamene muzaone? Kuti izi ndizilombo!!!? Aaaaa mwatipsesa mitimatu nsilamu wantundu wanji osadzudzula munthu akupanga zoipa , bwanji simukuyima pa deen ndikulalika chilungamo aaaaa yinu nde mwalalika mophusa bolani abusa aja nawonso yinde anyika koma yinu mwanyanya ,
Ndipo palibe akutameni kupatula okhawo akulipilani ndalamawo ife ndife asilamu eni eni choipa timadzudzula basi angakhale Allah anamudzudzula ntumiki wake Muhammad ( saw ) sametime atabwera munthu kuzamfutsa koma ntumiki anayang'ana kumbali
Alkah pompo pompo anamudzudzura awa ndayani aaaaa musatinyase mwamva
Koma ma ayah wa tikugwilitsa ntchito molakwika 😆😆😆😆😆😆👏👏👏👏👏👏
Koma ndalamazi guyz tisamale nazo
POWERFUL
SHEIH MWAPALA ULALIKIWANU MUMAFUNA AKUTAMENI A PRESIDENT PALIBE CHANZERU MWAYANKHULAPO APA ALLA WAKE UTIYO ANGAKONDEE NDI ZOMWE AKUCHITA CHAKWERAYO AYI INUSO ALLA AKUONENI
Komati choti muziwe kulankhula boA pamaso pamulungu pomwe chilungamo mukuziwa muziwe kuti akakuwochani
Chakwela akusapoter Israel shehe wa mabi
Naam ena akwiya chifukwa mwayakhula zosephana ndizomwe Iwo akufuna
Awaso nawo aaaaaa zaziiii mazidyani wosatipusitsa
Apasidwa ndarama alaliki adyela
Akutuma Kodi sheikh wachinyengo iwe nde akupasa zingati ?
7:53 Chikangawa akupatsani million yinu zaziiiiii nkhanizaunu
Sheikh apatu nanu mwanama kwambiri 😂😂😂😂😂😂
Mashala
Anthu muzinena chirungamo osamabisala mukaona omunenayo kuti alipopo mamizimu anthu akuvutika pqmene iweyo ukufunq kukomesera president umenewo moyo oyipa ngati uli sogoleri wapingo ndiwe waboza liuze chirungamo dziko
Walykum ssalam wakahmatul llah wabaraktu
Kmatu musamapange zindu kut akutamen shehe Allah wanji angasangalale ulaliki zimayi sisi kunja osamvala pango 😢😢😢 dini ulindo bas inarilah
Moses kumkuyu akukuwombela mmanja pamfundoless zakozo, kodi unamulesa kuti asamaphe anthu ngati mmene anaphela ALLAN WITIKA uja?
Km Inu sheikh ndinu opanda nzeru apurezident akunyoza chisilam kms amakokomezera nkhondo ku Palestine kut adziwapha asilam zoon Inu kumaim pagulu kwacemera
Ndipo panop asilam akumalaw akuchititsa manyaz chisilam chifukwa chokonda ndalam mmmm zomvetsa chison
Ndipo sheih uyu watinamizapo wadya nao ndalama za pule malawi sadzathekayi
Alibenzeru uyu
Walaikum salaam warahmatullah wabarakatuh... Innalillah wainna illaih rajiun
Sheikh uyu manyakwa
Shehee wadya chamba chanji chakwera Mutu Ngati gwafa😂
Mashallah
Amen
Chakwera anapha chilima😊
Live from Gaza city
Palibe amene angakutameni yinu bodza zidyani ndalamazo msilamu weni weni akuonani Kuti mwanama akulu ndinu adyela
Achina chimoto ndi a MCP ndiwe shehe😂
Sheikh awa Malo ngt awa kumafunika Sheikh ayyub azipita kumeneku not awa
Ndiye ulaliki otaninso uwu, mukulalikila ngati simukumva kuwawa bwanji, odya banzi sasowa.
Ndalama Za mcp zikuyakhula
Iwe undithera nthawi ukuwoneka kuti walandila brown envelope
Naam Ameen thumma Ameen
Bodza pakadalipano akuliyamba ndi Chakwelayo
Ameen
Ulaliki oti sungatingele kumoyo wosatha komaso sungasithe kalikose. Koma anthu akuwombela mmanja. Ulaliki oti mukupanga taget Boni kalindo, Bakili muluzi tv komaso limpopo FM. Ife we are not going to support any usiles speach or teaching like this wadya bamzi shehe.
Chemoto ndinu mwandila ma unforp
Kodi munthu ameyu ndani alinaye number yake sheikh ameneyo ndimuuze kuipa koononga chipembezo chifukwa chandalama
Inu sheikh watu ndithudi si mslamu weniweni awa akuononga chipembezo cha chislamu ndi mbunzi yamunthu
Iwenso waikila kumbuyo asatana mmalo mowalesa zoipa which means ndiwe kafiir
Aise kaya ukumati mwiniwakowe Malawi chani kuyambila lelo ndakutuluka ndakuona kut ndiwe wamanyi ukuchwmelela zimenezi kut sheh walalikila mwamphavu mphavuzake zilikut machende ako aise pamoz ndisheh akowo iwe wamanyi kwabas
Awapasa ndalama 😮 awa
Naam sheh
Uyu anadya kale ndalama uyu komaso ndi wa mcp uyu
Jazackah alla
Shehe my foot 😅😅😅
Shehe akufuna chuma chamagazichi eti?