Shehe uyuso wagagada ulariki wake mopanda mantha kusiya anthu akungoombera mmanja

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 5 лип 2024

КОМЕНТАРІ • 156

  • @user-jl6sq3ph1b
    @user-jl6sq3ph1b 5 днів тому +16

    Tayesedwa ndi president wakhaza chakwera ndie timupempha Allah kuti atichosele chakwelayo ameen

  • @HusseinAdamLidezo
    @HusseinAdamLidezo 5 днів тому +10

    Sheikhe ulaliki wanu siukugwilizana ndi ma aya omwe mumatulutsa pakamwa panu, uku ndikugulitsa mawu amulungu, ambuye akumvelen chison Ameen

    • @omardyman8083
      @omardyman8083 5 днів тому

      Analandila ndalama nkhani anaiyamba bwino kukasokoneza kumapeto zachamba

    • @rasulmaulidi2224
      @rasulmaulidi2224 3 дні тому

      zikomo kwambiri m'bale wanga ndimaganiza ngati ndindekha ndimaganiza choncho..ndikufuna number yake ndimuyankhule mwapadela ndi galu wamunthu uyu ali ndidyela simasewera akuyalutsa chisilamu

  • @abdulhameed7808
    @abdulhameed7808 5 днів тому +5

    Basi sitilankhula zambili tingokusungirani ulemu Sheikh Anthu.

  • @NenehMasanje
    @NenehMasanje 5 днів тому +12

    Sheikh mwadya now ndrama

  • @AbdulmajeedJbanda-oz3jv
    @AbdulmajeedJbanda-oz3jv 5 днів тому +3

    7:53 7:53 Chikangawa akupatsani million yinu zaziiiiii nkhanizanu
    Mayeselo aifa muyesa ife sitimaziwaaa,
    Nde imfazake zochita kumugwira munthu pakhosi mwadaladala , kumuombela mfuti mkamwa munthu ,kodi yinu mulankhulabwanj muli ndiwumunthuyinu ,aaa muzichotsela ulemu nokhatuyinu mwangotengana nonse odya ndalama zamagazibasi ,
    Afitiwo alimwetuuuu ati zikuyenda malawi wake utiyo amene mungamunamize lelo ,
    Azibusa muzichotsera ulemu nokha mwamva

  • @SulaimanaJames-b9v
    @SulaimanaJames-b9v 3 дні тому

    Maa Shaa Allah
    May Allah bless this message and make it beneficial

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 5 днів тому +3

    Wadya nawo ndalama zamagazi iwee, usatinamize asilamufe pamodzi ndi amalawife, ifenso ndife asilamutu, mayesero ukunena apawa simayesero ochokeraxkwa ALLAH, awa ndimayesero ochokera kwa satana kudzela kwa chizukulu tudzi chake chotchedwa chakwela ndi boma less lake 😂😂😂😂😂

  • @DeliaKaduya
    @DeliaKaduya 5 днів тому +3

    Odya ndalama zamagazi ngati akumasowa zoyankhula zawo? Allah mukunenayo akuyendereni Sheik😢

  • @MillieMalakam
    @MillieMalakam 5 днів тому +2

    Ameen sheikh Allah ahead u. From Cape Town centre

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 5 днів тому +3

    Chemoto alipomwepo anapha ALLAN WITIKA, anapha chilima kuchikangawa 😂😂😂😂

  • @SteveriaZimba-qs1id
    @SteveriaZimba-qs1id 5 днів тому +1

    Amen and amen uthenga wamphavu ambuye alemekezeke ndipo akhululukire zochimwa zathu

  • @MariamJaffali
    @MariamJaffali 5 днів тому +1

    Naam sheikh ma shaa Allah ulaliki wabwino ndithu ❤❤❤❤

  • @BrownMatonyola-xi3lb
    @BrownMatonyola-xi3lb 3 дні тому

    Mwadya zingati
    Aliyese wanyambita ndalama zoti azizilise za imfa yachilima ndikupepha Yehovah Mulungu wathu amuonetse kiyama akumane ndi mavuto

  • @FebbieMaulidi
    @FebbieMaulidi 5 днів тому +1

    God bless you sheik for unity message ❤

  • @SayidiIshmael
    @SayidiIshmael 3 дні тому

    ❤Allah give you more life and imaan to defending this deen

  • @IshaaakKango
    @IshaaakKango 2 дні тому

    Maashallah sheikh

  • @AbdulmajeedJbanda-oz3jv
    @AbdulmajeedJbanda-oz3jv 17 годин тому

    Aaaa sizomwezija Izi inu asheikh opanda manyazi ,
    Panja peni peni wadya ndalama Za Chikangawa uyu,
    Sali pachilungamo uyu

  • @muhmmadsarwer9527
    @muhmmadsarwer9527 4 дні тому

    Ameen thuma ameen Allah tichotseleni President ameneyu..ndipo tipatseni mtsogoleri wabwino mdziko mwathu muno

  • @abwinoamatani4921
    @abwinoamatani4921 5 днів тому +1

    Mukufuna mutamike. M'nungu tam'nyekule ngulumbira une

  • @mosewallace9717
    @mosewallace9717 3 дні тому

    mweye che kuntamba 🔥🔥

  • @kekeaufi9834
    @kekeaufi9834 5 днів тому +2

    *WA ALYKUM SSALAAM WARAHAMATULLAHI WABARAKATUHU,,,,Inna lillah wa Inna ilayh rajoon*

  • @TWAIBAKBANIES
    @TWAIBAKBANIES 4 дні тому

    Ma vesi ali apa zili kutali tali . Aaaaaaa koma akulu akulu sheikh mudziima pachilungamo komanso ma ves osamawakhitetsa ai

  • @ThivadoartistDyson
    @ThivadoartistDyson 5 днів тому

    Kkkkkkkkkkk wabodza ndiwe ma inovolopu yakutseka pakamwa ya chakwela, zikhale ndi kunkuyu 😂😂😂 waukape ndani sakudziwa.

  • @AbdulmajeedJbanda-oz3jv
    @AbdulmajeedJbanda-oz3jv 5 днів тому +1

    Sheikh awa salibwino akugulitsa mawu aMulungu ndi ntengo wotsika mukankhanthidwa mutsiku lomaliza

  • @AndersonTsoyo
    @AndersonTsoyo День тому

    100% shehe uthenga omanganga dziko

  • @user-fi7ko7bl6f
    @user-fi7ko7bl6f 2 дні тому

    Ili ndiye gulu loyitana chakwela ku Eid atawapasa mbia makwacha mashehe adyera ichoooo!

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 5 днів тому +1

    Usatiipisile Islam yathu iwe wamva , bwanji sukuwalesa makafiir omwe ulinawo pomwepowo kuti azikha okonda anzawo?

  • @AbdulmajeedJbanda-oz3jv
    @AbdulmajeedJbanda-oz3jv 5 днів тому +2

    Mwapatsidwa ndalama

  • @Macsaidi
    @Macsaidi 5 днів тому

    Komabe sitinganame pa chilungamo.
    Saulos Chilima anaphedwa ndi ndege ya boma la mcp

  • @omardyman8083
    @omardyman8083 5 днів тому

    Ndine msilamunso koma sheikh uyu wapochelaapo nkhani anaiyamba bwino kukasokoneza kumapeto akatero anali ku state house

  • @MollenMponya
    @MollenMponya 2 дні тому

    Awa ndye mau ochokwera kwa Mulungu osati Za Anja amaziyesa Okha opambana

  • @PeterThomas-lw3io
    @PeterThomas-lw3io 5 днів тому

    Alhamudulillla sheih my Allah bless you all the time what's a sweet Message like 💋💗 this Marshall ( port Erizabeth SA missionvale

  • @johnarushamasese108
    @johnarushamasese108 5 днів тому +1

    Ana usawi chemwalimu apochele silingwa

  • @doreenkaliati3166
    @doreenkaliati3166 5 днів тому

    God bless you Sheik all the time ❤❤❤❤❤

  • @juntoiman
    @juntoiman 4 дні тому

    Mmmmm sheikh zoona malo molankhula chilungamo pamaso pa anthu muli busy kubisa choona.Pamenepotu padali anzanu koma lero alikyt

  • @JeanKambala-gm1zr
    @JeanKambala-gm1zr 5 днів тому

    Nyasi zenizeni pamaso pamulungu chilungamo mukuchidziwa Shehe iwe. Wadya ndalama

  • @MafumuBanda
    @MafumuBanda 5 днів тому

    Sheikh ilim yanu ndiyochepa mupite mukaphunzirenso, ngati mukuzitenga zinthu za Allah maso mmwamba eeeeee chilango chaukali chkupezani pompo mulipo asakutameni awowo andalewo ndizotsala , ifenso tinaphunzira kwambiri kuposa iweyo xxx

  • @AbouzaidahSayeed
    @AbouzaidahSayeed 5 днів тому

    Kkkkkk sheikh wasanjatu uyu 😅

  • @NuradinaAbrahima-rt9ip
    @NuradinaAbrahima-rt9ip 4 дні тому

    No i was interested ndi ulaliki wanu Sheikh koma kumapetoko mwandionongela data yanga😭😭😭😭

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 5 днів тому +1

    Ine ndine Msilamu, uyu ndi sheikh wa chishiya uyu kafiir weniweni uyu,

    • @HusseinAdamLidezo
      @HusseinAdamLidezo 5 днів тому +1

      Sheikhe wamanyi uyu mbuz

    • @harrisbanda5891
      @harrisbanda5891 5 днів тому

      @@HusseinAdamLidezo zoona angamasinthanise chisilamu ndi ndalama?, bwanji sakulesa asatana anzakewa kuzunza ndikupha anthu mdziko muno ?

  • @trickermussa472
    @trickermussa472 5 днів тому

    Kukangotinyasisila deen yathu mbuzi ya shaikh

  • @marvelousmadzimure1811
    @marvelousmadzimure1811 3 дні тому

    Masha Allah ❤❤❤

  • @Sasha-g3z
    @Sasha-g3z 4 дні тому

    Bas allah awadalotse ndi ulaliki wawow

  • @yassinn5634
    @yassinn5634 4 дні тому

    Msilamu wolakira zau Mulungu osati enewa .Akuti ngati munthu wa mulungu walalika osanyoza president akuti ndiye sadziwa kulalikira. Shame

  • @ZionekaMember
    @ZionekaMember 5 днів тому +1

    Soka kwaiye akupindisa chilungamo popeza akuziyandikisa matako ake kumoto

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 5 днів тому

    Zikhale ng'oma akuwombelanso mmanja pamfundoless zomwe wanena, kodi unamulesa kuti asamaphe ma ruandaniz and Burundians komanso amalawi?.

  • @AbdulmajeedJbanda-oz3jv
    @AbdulmajeedJbanda-oz3jv 17 годин тому

    Inu nde muletsa zoipazooo suyu muyamikira mfiti ,wakuba, musatinyase

  • @Musa-cz1nm
    @Musa-cz1nm 5 днів тому

    Ma shaallah ma shaallah ma shaallah

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 5 днів тому

    Izo mzoona zoti tiziphunzisana zabwino ndikulesana zoyipa, funso kwa iweyo shehe ndiloti;
    Kodi zoipa zomwe akuchita chakwelayo wamulesa?
    Kupha kumene akupha aboma anthu kumalawi kuno wawalesa aboma ako awusiluwo ?,

  • @Randy-er2xo
    @Randy-er2xo День тому

    Thanks shelk potipatsa ulaliki wabwnowu

  • @KasundaAbbasi
    @KasundaAbbasi 5 днів тому

    Ngakhale mawu akewo akupepuka zoyakhula zakeso kumalemelera abusa aja

  • @abwinoamatani4921
    @abwinoamatani4921 5 днів тому

    Mzimu wa Chilima ukunyetseni nonse amene mukugawa ma yellow band ndi inu amene mukudya ma bans

  • @AminahMussah
    @AminahMussah 5 днів тому +3

    sheikh zamanyazitu iziii kufuna kuoneka wabwino pamanso pa pule mwadya zingat

  • @amoschataika7440
    @amoschataika7440 5 днів тому

    Chemoto akhale Kunkuyu😅😅😅😅

  • @AbdulmajeedJbanda-oz3jv
    @AbdulmajeedJbanda-oz3jv 5 днів тому

    Munthu angopha anthu inu mukamuyimile , munthu onyoza chisilamuyo inu mukamuyimile angapilile zimenezo ndani
    Kodi yinu mufuna azakupheleni agogo anu mpamene muzaone? Kuti izi ndizilombo!!!? Aaaaa mwatipsesa mitimatu nsilamu wantundu wanji osadzudzula munthu akupanga zoipa , bwanji simukuyima pa deen ndikulalika chilungamo aaaaa yinu nde mwalalika mophusa bolani abusa aja nawonso yinde anyika koma yinu mwanyanya ,
    Ndipo palibe akutameni kupatula okhawo akulipilani ndalamawo ife ndife asilamu eni eni choipa timadzudzula basi angakhale Allah anamudzudzula ntumiki wake Muhammad ( saw ) sametime atabwera munthu kuzamfutsa koma ntumiki anayang'ana kumbali
    Alkah pompo pompo anamudzudzura awa ndayani aaaaa musatinyase mwamva

  • @FarhaazbashaMdoka
    @FarhaazbashaMdoka 3 дні тому

    Koma ma ayah wa tikugwilitsa ntchito molakwika 😆😆😆😆😆😆👏👏👏👏👏👏

  • @udkconsultancy5567
    @udkconsultancy5567 5 днів тому

    POWERFUL

  • @HalisonSolomon
    @HalisonSolomon 5 днів тому

    SHEIH MWAPALA ULALIKIWANU MUMAFUNA AKUTAMENI A PRESIDENT PALIBE CHANZERU MWAYANKHULAPO APA ALLA WAKE UTIYO ANGAKONDEE NDI ZOMWE AKUCHITA CHAKWERAYO AYI INUSO ALLA AKUONENI

  • @Ishmael376
    @Ishmael376 5 днів тому

    Komati choti muziwe kulankhula boA pamaso pamulungu pomwe chilungamo mukuziwa muziwe kuti akakuwochani

  • @user-ti8ds7iq8z
    @user-ti8ds7iq8z 5 днів тому +1

    Chakwela akusapoter Israel shehe wa mabi

  • @AugustineIshmael
    @AugustineIshmael 5 днів тому

    Naam ena akwiya chifukwa mwayakhula zosephana ndizomwe Iwo akufuna

  • @princedetbozsmallboy1749
    @princedetbozsmallboy1749 5 днів тому

    Awaso nawo aaaaaa zaziiii mazidyani wosatipusitsa

  • @emilynthite6545
    @emilynthite6545 5 днів тому +1

    Apasidwa ndarama alaliki adyela

  • @AnnieKwisanja
    @AnnieKwisanja 5 днів тому

    Akutuma Kodi sheikh wachinyengo iwe nde akupasa zingati ?

  • @AbdulmajeedJbanda-oz3jv
    @AbdulmajeedJbanda-oz3jv 5 днів тому

    7:53 Chikangawa akupatsani million yinu zaziiiiii nkhanizaunu

  • @Hassankazembe-d3o
    @Hassankazembe-d3o 5 днів тому

    Sheikh apatu nanu mwanama kwambiri 😂😂😂😂😂😂

  • @medicoastkzn
    @medicoastkzn 5 днів тому

    Mashala

  • @ChristianMtambalika
    @ChristianMtambalika 5 днів тому

    Anthu muzinena chirungamo osamabisala mukaona omunenayo kuti alipopo mamizimu anthu akuvutika pqmene iweyo ukufunq kukomesera president umenewo moyo oyipa ngati uli sogoleri wapingo ndiwe waboza liuze chirungamo dziko

  • @UseniMailosi
    @UseniMailosi 5 днів тому

    Walykum ssalam wakahmatul llah wabaraktu

  • @KassimIssa-bn3od
    @KassimIssa-bn3od 5 днів тому

    Kmatu musamapange zindu kut akutamen shehe Allah wanji angasangalale ulaliki zimayi sisi kunja osamvala pango 😢😢😢 dini ulindo bas inarilah

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 5 днів тому

    Moses kumkuyu akukuwombela mmanja pamfundoless zakozo, kodi unamulesa kuti asamaphe anthu ngati mmene anaphela ALLAN WITIKA uja?

  • @user-zf7xk8fk5s
    @user-zf7xk8fk5s 5 днів тому +1

    Km Inu sheikh ndinu opanda nzeru apurezident akunyoza chisilam kms amakokomezera nkhondo ku Palestine kut adziwapha asilam zoon Inu kumaim pagulu kwacemera

    • @user-zf7xk8fk5s
      @user-zf7xk8fk5s 5 днів тому

      Ndipo panop asilam akumalaw akuchititsa manyaz chisilam chifukwa chokonda ndalam mmmm zomvetsa chison

    • @HalisonSolomon
      @HalisonSolomon 5 днів тому

      Ndipo sheih uyu watinamizapo wadya nao ndalama za pule malawi sadzathekayi

    • @AbdulmajeedJbanda-oz3jv
      @AbdulmajeedJbanda-oz3jv 5 днів тому

      Alibenzeru uyu

  • @user-fm7yg5yc2c
    @user-fm7yg5yc2c 5 днів тому

    Walaikum salaam warahmatullah wabarakatuh... Innalillah wainna illaih rajiun

  • @AliSinoya
    @AliSinoya 4 дні тому

    Sheikh uyu manyakwa

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg 5 днів тому

    Shehee wadya chamba chanji chakwera Mutu Ngati gwafa😂

  • @CHIFUNDOCHINA-lp9lg
    @CHIFUNDOCHINA-lp9lg 3 дні тому

    Mashallah

  • @user-qs7xw4ph7z
    @user-qs7xw4ph7z 4 дні тому

    Amen

  • @MussaAndreQuenessi
    @MussaAndreQuenessi 5 днів тому

    Chakwera anapha chilima😊

  • @SolomonShaibuh
    @SolomonShaibuh 5 днів тому

    Live from Gaza city

  • @AbdulmajeedJbanda-oz3jv
    @AbdulmajeedJbanda-oz3jv 5 днів тому

    Palibe amene angakutameni yinu bodza zidyani ndalamazo msilamu weni weni akuonani Kuti mwanama akulu ndinu adyela

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg 5 днів тому

    Achina chimoto ndi a MCP ndiwe shehe😂

  • @moosakananji1879
    @moosakananji1879 5 днів тому

    Sheikh awa Malo ngt awa kumafunika Sheikh ayyub azipita kumeneku not awa

  • @mcsellahntv6896
    @mcsellahntv6896 5 днів тому

    Ndiye ulaliki otaninso uwu, mukulalikila ngati simukumva kuwawa bwanji, odya banzi sasowa.

  • @user-jb5yb9wq3y
    @user-jb5yb9wq3y 5 днів тому +1

    Ndalama Za mcp zikuyakhula

  • @bisweckchimphamba8497
    @bisweckchimphamba8497 5 днів тому

    Iwe undithera nthawi ukuwoneka kuti walandila brown envelope

  • @abbasdamsonamini4888
    @abbasdamsonamini4888 4 дні тому

    Naam Ameen thumma Ameen

  • @user-ky8eq5ek1p
    @user-ky8eq5ek1p 5 днів тому

    Bodza pakadalipano akuliyamba ndi Chakwelayo

  • @RobertLuka-wy9cl
    @RobertLuka-wy9cl 5 днів тому

    Ameen

  • @shadrackdrums3536
    @shadrackdrums3536 5 днів тому

    Ulaliki oti sungatingele kumoyo wosatha komaso sungasithe kalikose. Koma anthu akuwombela mmanja. Ulaliki oti mukupanga taget Boni kalindo, Bakili muluzi tv komaso limpopo FM. Ife we are not going to support any usiles speach or teaching like this wadya bamzi shehe.

  • @user-xd1cm7tm7t
    @user-xd1cm7tm7t 5 днів тому

    Chemoto ndinu mwandila ma unforp

  • @HallimaMakwinja
    @HallimaMakwinja 5 днів тому

    Kodi munthu ameyu ndani alinaye number yake sheikh ameneyo ndimuuze kuipa koononga chipembezo chifukwa chandalama

  • @HallimaMakwinja
    @HallimaMakwinja 5 днів тому

    Inu sheikh watu ndithudi si mslamu weniweni awa akuononga chipembezo cha chislamu ndi mbunzi yamunthu

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 5 днів тому

    Iwenso waikila kumbuyo asatana mmalo mowalesa zoipa which means ndiwe kafiir

  • @JumaMboneka
    @JumaMboneka 5 днів тому

    Aise kaya ukumati mwiniwakowe Malawi chani kuyambila lelo ndakutuluka ndakuona kut ndiwe wamanyi ukuchwmelela zimenezi kut sheh walalikila mwamphavu mphavuzake zilikut machende ako aise pamoz ndisheh akowo iwe wamanyi kwabas

  • @MussaAndreQuenessi
    @MussaAndreQuenessi 5 днів тому

    Awapasa ndalama 😮 awa

  • @NchocitoTuaibo
    @NchocitoTuaibo 5 днів тому

    Naam sheh

  • @JamesRoben-dy7bx
    @JamesRoben-dy7bx 5 днів тому

    Uyu anadya kale ndalama uyu komaso ndi wa mcp uyu

  • @abdulllahanubieimran06comanubi
    @abdulllahanubieimran06comanubi 5 днів тому

    Jazackah alla

  • @user-fi7ko7bl6f
    @user-fi7ko7bl6f 2 дні тому

    Shehe my foot 😅😅😅

  • @EmanuelPaul-io2hk
    @EmanuelPaul-io2hk 3 дні тому

    Shehe akufuna chuma chamagazichi eti?