KAMLEPO KALUWA BOMA ZOMWE MUKUFUNA KUPANGA NDIKUDZIWA

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 10 лип 2024

КОМЕНТАРІ • 49

  • @MosesTangwe
    @MosesTangwe 20 днів тому +5

    Uku mkuchikweza amputa olakwika, voice imeneyo ikumveka mwa simple koma ili fire😊

  • @user-ux8bc6wy1i
    @user-ux8bc6wy1i 20 днів тому +6

    Even neba ku Zambia they know that we don't have president in Malawi

  • @wittinessnkhokwe
    @wittinessnkhokwe 20 днів тому +6

    Inu a mcp nenani kuti tonse amalawi tichokemo tifune kolowela muone kuti mudzilanulira ndani?

  • @TwalikiWisiki
    @TwalikiWisiki 20 днів тому +1

    Mr Kaluwa i appreciate you,,,you a true gentleman a hero,, if it takes you to go back to your past to resolve this chakwera issue so it be,,

  • @user-pv9uk6sc3w
    @user-pv9uk6sc3w 20 днів тому +3

    You have to take this Government to court for this damage.

  • @HenryLaidon-pl9ly
    @HenryLaidon-pl9ly 20 днів тому +3

    Guys Kamlepo ndi One of True democrat ku Malawi kuno tsopano kodi kuzunza mukumuzuza munthu wobweretsa democracy koma kokoliko ndalama zamisonkho yamphawi zakomadi

  • @luuu22mwanjabala79
    @luuu22mwanjabala79 20 днів тому +3

    Wise man from the North side

  • @FionaKhoma
    @FionaKhoma 19 днів тому +1

    Bora ilili tikachotsa chakwera a police ambili akuyenera kuchotsedwa tchito

  • @amoschataika7440
    @amoschataika7440 20 днів тому +2

    Well said, loud and clear

  • @RobertLuka-wy9cl
    @RobertLuka-wy9cl 20 днів тому +2

    Wise man mr kamulepo ❤❤❤❤❤

  • @user-zy2nh4lj4h
    @user-zy2nh4lj4h 20 днів тому

    Zinazo muzipanga koma za artist fredokiss mukangoesera 😮 malawi tiyatsa mukangopha fredo achinyamata tifafaniza state house

  • @JamayakoJamayako-rv2he
    @JamayakoJamayako-rv2he 20 днів тому +1

    Am agreed with you
    Pipo shud open their eyes
    Wise man

  • @brendamakokola7498
    @brendamakokola7498 20 днів тому +1

    Politics is dirty game

  • @EmmanuelGasiten-fo5dr
    @EmmanuelGasiten-fo5dr 19 днів тому

    Chomwe wachiona wankulu atakhala pansi, mwana olo atakwera mumtengo sangachione. Welcome Big

  • @user-ln3zx6wo4w
    @user-ln3zx6wo4w 20 днів тому +1

    Ndikatundu ameneyu aboma musamutengele masewelo zomwewakambazo ndizoona ndithu

  • @chipilirokalison1334
    @chipilirokalison1334 19 днів тому

    Sizitheka mulungu alipo kumwamba osamara

  • @user-jl6sq3ph1b
    @user-jl6sq3ph1b 19 днів тому

    Amenewo ndie mawu amphamvu mbuzi za police zogwilisidwa ntchito ndi chikangawazo makape amenewo akuti agulidwa ndi mcp gvrt Makamaka mai yolamu nayeso chipawa chosamukhala mutu chija mbuzi ya munthu aziwona makape amenewo mu 2025 wonsewo akathela ku mawulapalibeso kuwakhululukila inshaAllah

  • @JameChome
    @JameChome 20 днів тому

    Ask Bakii Muluzi anamtangwanitsa kooopya 😂😂😂😂😂

  • @NescotNyamwela
    @NescotNyamwela 20 днів тому

    Ine president wanga ndi Dad Bingu wa mutharika kwa ine sanafe i can see kuti anapanga chani. Kma mbuz zinaz zimangozuza amalawi osalakwa anyway sindili ku malawi kma home is best mbuziyi izaziwa kazachopa pamwambapo

  • @Blessings-td4cr
    @Blessings-td4cr 20 днів тому +1

    Boma iliri azitsogoleri mitu sikuyenda bwino why still keeping cellphones of Born kalindo and kamlepo why why Malawi President and the Police why can you please change your decisions why.

  • @temwarachaelkhonje3733
    @temwarachaelkhonje3733 20 днів тому +1

    Aputa olakwika tu....

  • @GeraldChisokeza-er5cf
    @GeraldChisokeza-er5cf 20 днів тому

    Oh no osat Fredo ayi.Komano kukhetsa Mwazi chifukwa Cha mpamdo Kaya Mulungu amaona amakantha

  • @user-jl6sq3ph1b
    @user-jl6sq3ph1b 19 днів тому

    Apolice yakhani kuti umuyaya uja udakalipobe kapena ai?

  • @raytavares2256
    @raytavares2256 20 днів тому

    Collect your phone via the attorneys and high court on releasing it without prejudice and bias. We are praying for you. Ndine kuno ku Great Britain. Yes the late dad Green Ng'oma used to w for Southern Bottles even when they lived in Mzimba before moving to Zingwangwa Blantyre and after ZINGWANGWA THEY MOVED TO ALIMAUNDE AREA 25 LILONGWE. We must all pray for each other and the countries experiencing the political tarmoils.

  • @FionaKhoma
    @FionaKhoma 19 днів тому

    Mcp ikuyenera kuchoka basi ikuzuza athu osarakwa chakwera wakupha ayende basi

  • @MaxWell-d7o
    @MaxWell-d7o 20 днів тому +1

    Pambuyo panu bwana..iponden

  • @AleksaWilliams-qc6cn
    @AleksaWilliams-qc6cn 19 днів тому

    Yooo zilichonchoso 😢

  • @mbewemisoyaanenenji1908
    @mbewemisoyaanenenji1908 20 днів тому

    You fought ngwazi , who are these dogs to fear .

  • @IdahNyasulu
    @IdahNyasulu 20 днів тому +1

    Deal with them bwana kalua

  • @zelliachamboto5744
    @zelliachamboto5744 18 днів тому

    Kulibedi wamuyaya

  • @peterchikwakwa8476
    @peterchikwakwa8476 20 днів тому

    Pena pache MCP tu , mukuonjeza eti!!?? Is this what we wanted? Why why why??

  • @NaduMbewe-zz6iw
    @NaduMbewe-zz6iw 20 днів тому +1

    Zosaesanda

  • @babranzima8120
    @babranzima8120 20 днів тому

    Athu akupha abusa wokopha kodi eeeeee athu akumpoto mwasiye mutha ndinu achakwera ndi azanu wood

  • @MzikaPhiri
    @MzikaPhiri 19 днів тому

    Amen Amen...

  • @CharlesKachipanda-jz9jv
    @CharlesKachipanda-jz9jv 20 днів тому

    Awuzeni makapewa adziwe kuti inu madala madala

  • @user-ss9bj5eh6b
    @user-ss9bj5eh6b 20 днів тому

    chonde bwelerani muzakale bwana tithane nawo anthu oipawa

  • @ShorayChimera
    @ShorayChimera 20 днів тому

    I feel ur pain father 💔

  • @victorauwana7258
    @victorauwana7258 20 днів тому

    Good 👍

  • @EllinaBitto
    @EllinaBitto 20 днів тому +2

    😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭

  • @AgnessMzengo
    @AgnessMzengo 19 днів тому

    Iponden fadah,,,,,

  • @user-kp7le2pu7h
    @user-kp7le2pu7h 20 днів тому

    Wise man❤❤❤

  • @user-fq4kv8dj4t
    @user-fq4kv8dj4t 20 днів тому +3

    Mwaonjeza English enafe sitimva nde izizo muzilankhulako chichewa chifukwa nzatonse amalawi kuti timve

  • @Standwell78
    @Standwell78 20 днів тому

    Chana?? Ayesele

  • @MagaLassi-tg7lj
    @MagaLassi-tg7lj 20 днів тому

    🆓✊

  • @YasinMusa-ym8lp
    @YasinMusa-ym8lp 20 днів тому

    Akupa mcp

  • @MilacleSankhani
    @MilacleSankhani 20 днів тому

    Ask late kamazu about u

  • @HamzaMkwanda-bh8dc
    @HamzaMkwanda-bh8dc 20 днів тому +1

    Wise man