A ZIKHALE NG'OMA UKU NDIYE KWATENTHA🙌🙌🙌 TAMVANI MFUNDO ZOMWE ABWELA NAZO

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 10 лип 2024

КОМЕНТАРІ • 540

  • @UseniMailosi
    @UseniMailosi 23 дні тому +22

    Malawi chikangawa party

  • @ackimchindimba9912
    @ackimchindimba9912 23 дні тому +6

    Mudyeleni apapa ndalama ziyamba kuphweka bas ndi kampeniyi tiyeni tiwadyele koma tonse ndikudziwa kuti ndife APM

  • @corretabanda7685
    @corretabanda7685 23 дні тому +11

    Nyama za mmanyumba mwanu. God is good and his eyes can see even in the heart of everyone. It will not work in the Name of Jesus

  • @anniedennis7127
    @anniedennis7127 23 дні тому +11

    Ng'ona zodya anthu zingalamulire anthu

  • @MeleckDennis-vg3bv
    @MeleckDennis-vg3bv 23 дні тому +7

    Zopusa zokhazokha mfiti za anthu,kwanu kwathapo agalu inu

  • @JumaGadaff
    @JumaGadaff 16 днів тому

    Bwana kuvota tidzavota koma dziwani kuti muli ndi mulandu ku chikangawa zikomo mulungu ankhale Nanu amen 🙏🙏🙏🙏

  • @user-wq3dh1ly2o
    @user-wq3dh1ly2o 22 дні тому +3

    Olo patavuta bwanji simungalamulileso dziko la malawi chifukwa munataya chipangano ambuye sangalole kuti mutilamulile anthu akupha inu

  • @user-wu4tl2yn9e
    @user-wu4tl2yn9e 23 дні тому +5

    Before kuvota aliyense azizakumbuka kuchikangawa

  • @Sammy-vb1ed
    @Sammy-vb1ed 23 дні тому +2

    Mudzina la yesu krist ndikupemphera kut uone zowawawa zikhale

  • @BrunoMbewe-xj1yy
    @BrunoMbewe-xj1yy 21 день тому +1

    Ndangothokoza kuti mene mumampephelamo mu Mpephero lanu nonse simuna mutchulemo Yesu khristu.Zaoneka kuti inuyo mwazi wayesu simunauziwe mene munagwilira ntchito, pitilizani kugwira ntchito zakumidimazo.

  • @Gmtmphats124gy
    @Gmtmphats124gy 23 дні тому +5

    Akanakhala kuti mulungu amalanga mpompo mpompo akanakuthilan moto pasokhano wanu omweo

  • @spargomw
    @spargomw 23 дні тому +5

    Zikhale Ng'oma😂😂😂😂 tsitsi muzipesako tisamakugemuleni zonse😂😂

  • @giftmaliwa2385
    @giftmaliwa2385 23 дні тому +6

    Za make Dzana this new generation

  • @juntoiman
    @juntoiman 23 дні тому +7

    Pathako panu nonse Zikhale Ng'oma pantumbo pako wamva

  • @user-cd4df3vg4y
    @user-cd4df3vg4y 23 дні тому +1

    Dzigawenga dzawanthu anthu akupha inuuu ng'ona zomwe mwachita pakupha abale athu asanu ndi anayi aja kuchikangawa dziko lonse lapansi ladziwa choonadi chifukwa ma German aja anenana zonse kuti black box inali ku palace.Ndipo anenaso kuti ndichiwembu chomwe munakonza.Pomwe inu muli pheee kufuna kutiuza bodza, ife tadziwa kale ndipo muyaluka

  • @sanlakedickson6780
    @sanlakedickson6780 23 дні тому +3

    ana asatana awa Mzimu wa chilima ukuvutitsani

  • @user-sh1rj3ol3t
    @user-sh1rj3ol3t 23 дні тому +2

    But tu Laz has failed Malawians way more than APM

  • @ephraimmbiza9727
    @ephraimmbiza9727 21 день тому

    Most important thing is that you know yourself that you will not come back in government

  • @AminaPhiri-pp9tw
    @AminaPhiri-pp9tw 23 дні тому +1

    Mukumbukeni chilima amene munamupha uja azikhale ng.oma ndipo zimu wake ukufinyeni ndipo khalira pomwe

  • @user-eg8wx8oi5z
    @user-eg8wx8oi5z 22 дні тому +1

    Now it makes sense kod nkhumbai Nd mtumbuka eti😂😂

  • @sharifujoe7633
    @sharifujoe7633 22 дні тому

    Uyu sikhale ngoma same like idi ameen

  • @EphraimNaveya-hz1du
    @EphraimNaveya-hz1du 15 днів тому

    Za ziiiiiii afiti simungazawine muli ndi magazi kale

  • @kinggasperagain
    @kinggasperagain 23 дні тому +1

    Kweni Malawi inasoka ivinthe kuwina waka nbwe chikurya waka ndalama

  • @lawrencekauwa8005
    @lawrencekauwa8005 22 дні тому

    Kkkkkkk,,,, to be a supporter 🙌

  • @user-fi7ko7bl6f
    @user-fi7ko7bl6f 23 дні тому +3

    Mukuzinamiza agalu Inu za kumachende, azimai nonse Nyini zanu zamanu,mugawane nonse phwala limodzi limodzi agalu okupha

  • @HassanMbalaka-gb5sv
    @HassanMbalaka-gb5sv 23 дні тому +1

    Palinyimbo inayake amat paulendooo paulendooo aaaayeee paulendoooo. Awakwao kwantha

    • @BittonRashid
      @BittonRashid 22 дні тому +1

      Aye aye paulendo tulinkwaula tulinkwaula kkkkkkk mfundo

  • @LindaNkwazi
    @LindaNkwazi 20 днів тому

    U r still remembering chikangawa

  • @Fatima-f5c
    @Fatima-f5c 23 дні тому +7

    Misokhano yanuyo muzipangila m,manyumba mwanumo Koma kunjaku ndithu tikugendani 2025 iwa alia

  • @Extratremendouszeus
    @Extratremendouszeus 22 дні тому

    Dziko linaola...nduna yosapesa😅😅😅😅😅😅

  • @PaulMwaona-kh1fj
    @PaulMwaona-kh1fj 23 дні тому +1

    Ubwino wake achinyamata alipo ambili kunjaku,apapa pachulukana makolo otamba

  • @AleksaWilliams-qc6cn
    @AleksaWilliams-qc6cn 22 дні тому

    Adyeren vote ndimumtima bas

  • @ChilangoNdalama
    @ChilangoNdalama 22 дні тому

    Suiona vote yanga Chaka chamawa ndangokudyera aise

  • @BeliLikhola
    @BeliLikhola 17 днів тому

    muuzeni chilungamo ameneyo, chigawenga ameneyo

  • @joyahmedjoma4615
    @joyahmedjoma4615 22 дні тому

    Ine kunkhara iwe president bola ndifele kokuno ku south Africa wallah wosantha kuyankhura ngat iwe paliolo lenu mwenjo

  • @user-fq4kv8dj4t
    @user-fq4kv8dj4t 23 дні тому +1

    Chikoka mulibemo olo nzozo mbola maturity mbola eeesh mudyeleni

    • @CatherineDesire
      @CatherineDesire 23 дні тому

      ,🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤸🤸🤸🤸🤸mama ine ndakomoka

  • @hopembendela
    @hopembendela 23 дні тому

    Kkkkkkkkkk manganya mukunva koma ati ndiwe mwana osapola panchombotu udziona

  • @LekkttarKhembo-or1tx
    @LekkttarKhembo-or1tx 20 днів тому

    Zitsiru za Malawi zikhale chakwera nonse ndinu osadura ndipo mumanukha kabudula mwanumo mukutinyasa tu

  • @giftjamali8204
    @giftjamali8204 23 дні тому +3

    Ngati mungapezeko bombaaaa ndipatseni nkaphulikire nawo Limonziiii

  • @georgemponda
    @georgemponda 23 дні тому

    Mbuli izi😂😂😂😂 Zikhalebg'oma nde panja penipeni

  • @Blessings-td4cr
    @Blessings-td4cr 22 дні тому

    Mpake muzipangira munyumba campaign,,, chibadwireni mfiti sindinkaidziwa ,,koma Malawi tiona zithu.

  • @MusaKazembe-b1d
    @MusaKazembe-b1d 19 днів тому

    They are not even ashamed 😮

  • @rabisonpias5131
    @rabisonpias5131 23 дні тому

    “Akuti kumabwera ndalama “ ndalama za misonkho yanu zomwe zija ndi zimenezo. M’malao momagura mankhwala mzipatalaa , akungotafuna ndi Ma families awo

  • @IssacMateyo
    @IssacMateyo 23 дні тому

    Amuna mutu wake ometa ngati chiboliwo Muthu osokonezayo zazi

  • @millionsenenje5010
    @millionsenenje5010 23 дні тому

    Mr Kamuyambeni ndiinu bambo wanga koma pena pake mhhhhhhh

  • @DeliaKaduya
    @DeliaKaduya 23 дні тому

    Azimai opusa inu mxiew, kuziwachera achamanu ife tidakagonabe,
    Kuvotera MCP kuli ngati kuyenda maliseche koma utavala panti, mpakaso zikhale nkukhaka VP ndiye zamapipotu! Shupiti zanu

  • @FlavourWitnesszitha
    @FlavourWitnesszitha 23 дні тому +2

    5:39 your time is over mwalephela,komanso azikhale ng'oma ovala ma sult amwanawo😅😅😅😂😂😂mukamuuze chakwera pamtumbo pake

  • @wisdomwizzie9944Jahblessevery1
    @wisdomwizzie9944Jahblessevery1 23 дні тому

    Ngat u MP amugwesa gwesa ana zaka zambirimbiri lero nkumat Vp kkkkkk mudyeleni ameneyo ine olo ya u MP sazaiwonaso kuno

  • @user-ee6be5kl5o
    @user-ee6be5kl5o 23 дні тому

    Ndiye. MCP aaaaa!!!!! Mwauponda ndithu2025 muziona kwanu kwatha anthu anakupatsani mpata koma mwalephera zinthu muzaka 4 amalawi sangapa
    nge misiteki kawiri

  • @MisheckAselo
    @MisheckAselo 23 дні тому

    Ndimamva chisoni ndi anthu apanda nzeru ndikumanamiza anthu, mwaba zakwana azikhale ng'oma 😮

  • @GraceZumazuma
    @GraceZumazuma 23 дні тому

    Chikangawa party, okupha Inu muganiza asakudziwa ndani

  • @WhiteRichard-cw2fo
    @WhiteRichard-cw2fo 23 дні тому

    Zikhale Ng'oma muti chani apaa tiyeni uko 😂😂😂

  • @GanizaniKamvazaana
    @GanizaniKamvazaana 20 днів тому

    Aaaa dzitsiru dza athu kunamizana kukhwapa kwanu nonse

  • @user-wd9yd1bg9n
    @user-wd9yd1bg9n 23 дні тому +3

    Zikhareyo akutha kuona kuti mmmm apa pavuta , olo zikhaleyo sanafune kubwera

  • @user-uc9qk7ci2v
    @user-uc9qk7ci2v 23 дні тому +1

    Taonani zinkhopezo ungokhala ngatinsonkhano wa afititu

  • @JuniorHala-vf9ov
    @JuniorHala-vf9ov 23 дні тому

    Viskulu vinu kwacha ninkhuni mpakana kupemphela pamusonkhano apo naumo wanthu wakutambulila namwe kuzomelezganga kwacha chitima chikukolana kweni in fact Mose imwe mukukondwa na mcp Mavi yinu

  • @FrancisNyayi
    @FrancisNyayi 23 дні тому

    My pipo tiyenda bwanji 😢 koma able

  • @alfrededwinmadziataika5869
    @alfrededwinmadziataika5869 23 дні тому

    Sapesa Adana ndimadzi..😮😮😮😮😮

  • @user-le9su3mt7r
    @user-le9su3mt7r 23 дні тому

    Chikangawa party mbuzi hiziiiii

    • @amosnyongo6565
      @amosnyongo6565 23 дні тому

      Pemphero lanu silingafike kumwamba afiti inu

  • @alboxenzambabanda7230
    @alboxenzambabanda7230 21 день тому

    Time to see chiterera

  • @zondanitzulumusicfly.5202
    @zondanitzulumusicfly.5202 23 дні тому

    Adziwa kuti babiloni is falling.

  • @isaihmagani5697
    @isaihmagani5697 18 днів тому

    Apa akunena zoona Zikhale Pali zambiri zakhara zuchitika, nde kusankha mwachibwana MCP pa mpando itha kuchokapo

  • @FrancoKaunga-rq2ki
    @FrancoKaunga-rq2ki 23 дні тому

    Zikhale ngoma nkhope ngati kazizi mfwiti zawanthu! Kwacha kwacha 😂zakale kale. Kasi nkhumeta uli uko zikhale ngoma?

  • @MsondaBanda
    @MsondaBanda 22 дні тому

    Kumpoto kulije development, kufuma kale awo wangazenga kumpoto nimbani? No dpp, no udf , no utm, pali vifukwa apo,

  • @user-mq2or1lz8h
    @user-mq2or1lz8h 23 дні тому

    😢😢😢😢oooh he has confirmed that this is serious business 😢😢😢rip SKS

  • @HopeMakoka
    @HopeMakoka 23 дні тому

    Akabwerstsa ndalamazo landirani guys Koma zodzalamuliranso awa mmmmmm Kumwamba kudzatsika pansi

  • @user-oo7pe7pw8u
    @user-oo7pe7pw8u 22 дні тому

    Busy kuphemberela mzanu wachumakale kusiya kusiphemberela weka inu simufuna utendere komaso mukuganisa Kuti osewo maganiso Anu angakale amodzi mukunama kovota simuzakala gulu chocho

  • @IshumaliMakajunior
    @IshumaliMakajunior 22 дні тому

    Ndipo lnu mukanadziwa mene tikuvera

  • @user-im7sc2my4w
    @user-im7sc2my4w 23 дні тому

    Angokunyenga angokunyenga ,,angokunyenga angokunyenga angokunyenga 😂😂😂😂😂

    • @ShadreckJim
      @ShadreckJim 23 дні тому

      Kkkkkkkkkkk

    • @Allan-bk1
      @Allan-bk1 23 дні тому

      😂😂😂😂😂😂😂😂 koma ndaseka

  • @CannyMpehla-d1s
    @CannyMpehla-d1s 22 дні тому

    koma malawi waoladi ng'omaso ikhale vp kkkkkkkk

  • @TroubleKatsala-jp2li
    @TroubleKatsala-jp2li 23 дні тому

    Anthuwa apengamisala simukuona zimene akuchita tiyeni tiwadyele koma vote osawapatsa

  • @EllenPhiri-xt8pt
    @EllenPhiri-xt8pt 22 дні тому

    Mbamva ndi afiti awa sangawine tangonani anthu ndi anthu amabanja mwawo okhaokha amenewo

  • @user-ot8no9ex2z
    @user-ot8no9ex2z 23 дні тому

    Azakuvoterani ndi ambuyanu ndithu nsonkhani umakhala ndi anthu awiliwo kuousatu uko bwanji manyazi zimvereni chisoni

  • @ChimwemweJuwao
    @ChimwemweJuwao 17 днів тому

    Haha koma ndiye mukungooneka Mano okhatu kuli kuda Kwa athu kumeneko ndye kwati mukufuna u vice Muthu ukafuna kufa umankhotha makutu kaye

  • @VictoriaWilly
    @VictoriaWilly 23 дні тому

    Kunamizana ndi kosavuta, zinamizanani

  • @WilliamblackvPaul
    @WilliamblackvPaul 23 дні тому +2

    Kwinaku ndingatukwane

    • @user-yb3su3hi9f
      @user-yb3su3hi9f 23 дні тому

      Ofunika kuwatukwana kumene. Onsewo panyero pawo

  • @BrightNyoni-yd4ip
    @BrightNyoni-yd4ip 22 дні тому

    Gulu iwe usamaseweletsa dzina la yesu nkhumba iwe

  • @SolomonNjolomole
    @SolomonNjolomole 23 дні тому +1

    Akulu awa ndi achitsilu kwambiri ndi azizawo onsewo kumeneko

  • @JackNagoli
    @JackNagoli 23 дні тому

    Let them talk guys ndipo apange ma plan awowo km ubiwno wake malawi siwaathu atatu tiyeni tikakumane chaka chamawa basi khani ndi vote not to talk too much angochedwa nazo

  • @ChikumbutsoDzukwa
    @ChikumbutsoDzukwa 23 дні тому

    Munamizana udya Galu amawawa muziona this is new generation

  • @YohaneChitseko
    @YohaneChitseko 22 дні тому

    Manje mapephero amene chabe mulungu sangamve anthu okupha ngati inu

  • @Sammy-vb1ed
    @Sammy-vb1ed 23 дні тому

    Azikhaleo kwaona nkhopeyo ngati muru wamanyi afisi 😂😂😂😂😂😂.

  • @ChrissySalimu
    @ChrissySalimu 23 дні тому

    Wooooooooooooooooooooo

  • @FrancisNyayi
    @FrancisNyayi 23 дні тому

    Mayo mayo chitumbuka sitikunva yankhurani chichewa

  • @CharlesMongola-jw7sk
    @CharlesMongola-jw7sk 22 дні тому

    Pepani mfundo zanu zopusazo musaphenso Manganya,afiti inu

  • @chrisboyce2
    @chrisboyce2 23 дні тому

    Umphawi ndi matenda Zoonadi ( ife kuno ku Ntcheu sitikupanga nawo zimenezi popeza ABIYENI ndi aja munatichotsera aja ...)

  • @pacharokoloviko1694
    @pacharokoloviko1694 21 день тому

    Mayankhulidwe ake amenewa anthu aphanako uku

  • @WilliamBandaWili
    @WilliamBandaWili 23 дні тому

    Mmmmm izo ndi ng'ona zikuruzikuru zikudyani

  • @JohnAsendi
    @JohnAsendi 23 дні тому

    Palibemukukamba ndiye kukanpeniko akuyankhula kwake kumeneko 😂😂😂😂 tinka zaka koma lelo tikuti tasala ndi amwezi canpen DPP sheweeee

  • @TopoTopo-bm4vw
    @TopoTopo-bm4vw 23 дні тому

    😂😂😂😂 tango mdyelani ndalamazo azakhumudwa ameneyo

  • @McfrankJackson
    @McfrankJackson 23 дні тому

    Aaaaaaa aa kkkkkkk 😂😂😂 Malawi politics inalowa madzi 😂😂

  • @StanleyChirwa-d6b
    @StanleyChirwa-d6b 23 дні тому

    😂😂😂 koma ndaseka kwacha kapena kwada

  • @FrankHaruni
    @FrankHaruni 23 дні тому

    😂😂😂😂 awande manyiwo😅😅😅😅

  • @user-hl3st3cc4v
    @user-hl3st3cc4v 23 дні тому

    Kodi khope zimenezo zikuyakhula apazi pamodzi ndi zikhale ng,oma zamasana kapena zautsiku mmmmm anthu andalama olo kuwezuka

    • @user-hm9nc7lz6e
      @user-hm9nc7lz6e 23 дні тому

      Ndi zausiku mumuone or zikhameyo khope yace ngati chidzukwa

  • @thondoyaenterprise3795
    @thondoyaenterprise3795 23 дні тому

    Chimphongo , chonenepa , cha kuda , chilibiiii chi ZIKHALE N'GOMA.

  • @Sammy-vb1ed
    @Sammy-vb1ed 23 дні тому

    The savage politicians, we as malawians we don't need you anymore. Anthu atsankho, kupha komanso katangale.

  • @Eric-gb9ms
    @Eric-gb9ms 23 дні тому

    Nanu inu makolo anthu siyani ndi kutengeka ndi mbamva izii mukuzinamiza mukamati 2030 nkhondo izabuka mudziko lanthu serious anyani inu

  • @user-yc5uc6oh6u
    @user-yc5uc6oh6u 22 дні тому

    Usi afela za eni😂

  • @phanueltalekana5416
    @phanueltalekana5416 23 дні тому

    Mukhaletu ndima ghost voters mwinatu😂😂😂

  • @mollymasangano473
    @mollymasangano473 23 дні тому

    Kutereko Mwadya zibazi,A UTM mwawamva mawuwo apephere Zikhale Ng"oma adzakhale vice President koma kuli kale Vice President Usi ,(Mang'anya) zayambiranso AMalawi tidziphuzira phuziiro,Chitozo Chomwe amawona Malemu Saulosi Chilima,UTM why don't you make a heavy discussion by conducting early elections izi sizitisunga.

  • @BenjaminMtima
    @BenjaminMtima 23 дні тому

    Akulu mwatopa eti. Muziponya zanzeru mwamva