GWEDEGWEDE LERO NDE KUNALI KUGUDULA NDIWO ZAGULU | ZITHUNZI ZA ANDUNA KUNO |

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 10 лип 2024

КОМЕНТАРІ • 35

  • @kadijachilwan967
    @kadijachilwan967 23 дні тому +5

    Apolice amaonjeza nkhanza pansewu😢

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg 23 дні тому +1

    Zikhale ng'oma ma bombasa wagulakoso 😂😂😂 wausilu iwe

  • @giftmasenti5732
    @giftmasenti5732 23 дні тому +1

    A Traffic police ambiri za miyoyo ya anthu alibe nazo ntchito nde ndizimenezo

  • @wilisonbornface4282
    @wilisonbornface4282 23 дні тому

    Live from south Africa cape town

  • @gracemkandawire8769
    @gracemkandawire8769 23 дні тому +2

    Powerful GwedeGwede,,bambo banda

  • @B1Chitatata
    @B1Chitatata 23 дні тому +3

    Salute

  • @CatherineDesire
    @CatherineDesire 23 дні тому +1

    Chipewa cha khwangwala kuteloko amafuna anyemere kaye kuti adutse ndi mwana wodwala ,utsilu dyera

  • @SolomonNjolomole
    @SolomonNjolomole 23 дні тому

    Munadza makosana ❤❤

  • @MerryWayson
    @MerryWayson 23 дні тому

    Sitidya ndale kkkk ndimakunyadilani kwambiri Mibawa TV

  • @ishmaelchirwa9303
    @ishmaelchirwa9303 22 дні тому

    Anduna akutsotsola ulusi pano akuti kuionesa 😂

  • @mathewsmdzanja3276
    @mathewsmdzanja3276 23 дні тому

    I salute mibawa

  • @SurprisedDrumKit-ql7rj
    @SurprisedDrumKit-ql7rj 23 дні тому +1

    Za police mbuzi zaanthu izi kma kuba ndikupempha

  • @AnaffSayamika-uh6vg
    @AnaffSayamika-uh6vg 23 дні тому

    Mumakwana guys 💥

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg 23 дні тому

    😢😢😢😢 apolice apamalawi vuto ndi umphawi anthuni

  • @InnocentnMbale-zq8pk
    @InnocentnMbale-zq8pk 23 дні тому +2

    Kkkk chipanda kuyankhula bwezi ali mumaguza omwewo kkkk

  • @Homeofpeace321
    @Homeofpeace321 23 дні тому

    Nkaka akulembaso MSCE

  • @user-xx4jb9se3z
    @user-xx4jb9se3z 22 дні тому

    Zoonadi apolice amaonjeza

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg 23 дні тому

    Chakwera mumuudzeso kuti opha nzake afeso chifukwa chakwera anapha chilima my boss he call chakwera bull dog😂😂

  • @StevieChikaonda
    @StevieChikaonda 23 дні тому

    Muli ndi mtopola guyz😊

  • @HarryMasamba
    @HarryMasamba 23 дні тому

    Kkkkkkkkkkkkkkkkkkk Komatsu dzina izi

  • @user-gw2zb8pf7n
    @user-gw2zb8pf7n 23 дні тому

    Mwanayo anali ndi 1 month and 3 weeks mgalimoto ndinali MO ine😢

  • @user-eh1mg3ww6d
    @user-eh1mg3ww6d 23 дні тому

    Ndipo apolice akumalawi ndinu otembelekdwa ndipo mukulephela kugwila mbava koma kulimbana ndi athu osalakwa

  • @LucianoKapepuza-sy9wx
    @LucianoKapepuza-sy9wx 23 дні тому

    Nawo a MCP asatile malamulo a gwirizano wawo kuti apite s Utm asogoleke nawo

  • @wilisonbornface4282
    @wilisonbornface4282 23 дні тому

    Steve ndi Selina mativesa kukoma

  • @user-jn7bt1uy5s
    @user-jn7bt1uy5s 23 дні тому

    Mbambande mibawa

  • @dumisanimoyo3152
    @dumisanimoyo3152 23 дні тому

    Tisakubisileni apolice alowa chiwewe kusaka ndalama

  • @user-lc3sw8iz2g
    @user-lc3sw8iz2g 23 дні тому

    Ku malawi zimathera tikufufuza.

  • @NaduMbewe-zz6iw
    @NaduMbewe-zz6iw 23 дні тому

    Kkkkkk

  • @user-bc2mu2ns5n
    @user-bc2mu2ns5n 23 дні тому

    Futso nkhumati kodi sopano kubako mwathana Nako?

  • @CatherineDesire
    @CatherineDesire 23 дні тому

    Va police palibe vomwe vikuchita vimangodziwa kupempha ndrama pamseu ndikumanga mbava yoti anthu aigwira kare anthu eniake,ndipo vitengelepo phunziro mwina vingayambe kugwira ntchito bwino vipewa va mbalevo

  • @MosesShaibu-ee8hn
    @MosesShaibu-ee8hn 23 дні тому

    Madokotalanso ali ndivutolawo munthu akumuwona ali pamzele komakungobwelawinawake wawudindo amakudusila chifukwachani winayusi munthu kodi?

  • @OfwaMwambila
    @OfwaMwambila 23 дні тому

    If u stopped by the police officers on the road in ur 🚗 .who is supposed to follow the other? 4me i don't go out to a police office who stopped me coz i had no intention of stopping.u stop me,u come to me &tell me why you stopped me not me coming to ask u

  • @AlasonPaulo-ht7zb
    @AlasonPaulo-ht7zb 23 дні тому

    Zoonadi Inu muli bwino kwambili

  • @gwatandingo9502
    @gwatandingo9502 23 дні тому +1

    Wanga kufa mwana chifukwa cha wa police wandigwira nayeso adzafera pompo ineyoso natopa nawo mbuzi zimenezo pofunika osamawanyengelera😢😢

  • @WysonYohan
    @WysonYohan 23 дні тому

    Malawi tingogulisa tigawane ndlama bc