Palibe Chamuyaya Pa Dziko La Pansi - Hon Kamlepo Kalua

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 10 лип 2024
  • On Nyasa VoiceBox, Hon Kamlepo Kalua says nothing is forever. Especially Political Power and Politicians.
    Pa Nyasa VoiceBox, Olemekezeka a Kamlepo Kalua akuti pa Dziko La Pansi Palibe Chamuyaya. Makamaka Mphamvu za Ndale Komanso anthu andale.
    #malawi

КОМЕНТАРІ • 37

  • @user-nf3ik3ff6y
    @user-nf3ik3ff6y 23 дні тому +6

    Good Messnge Mr Kamulepo kaluwa, Chakwela you mast go

  • @user-be5fc3ed1i
    @user-be5fc3ed1i 23 дні тому +3

    Amene kamulepo kalua ndimamziwa ndi ameneyo nthawi yamakezanayo ankayimba nyimbo zamatikitikii tiki tiki zamatikitiki so samalani amcp ndi chakwera wanuyo

  • @CHARLESMASINA-xx5kt
    @CHARLESMASINA-xx5kt 23 дні тому +1

    A great speech sir ...so wise and mature

  • @user-qq3ip1od6i
    @user-qq3ip1od6i 23 дні тому

    We are wit you sir, all the way.... God be wit u n the whole family

  • @user-mh7cc8up4i
    @user-mh7cc8up4i 23 дні тому

    Ulemu wanu Mr kamulepo ambuye akutetezeni Ku khwandwe za MCP we love you ❤

  • @user-eh1mg3ww6d
    @user-eh1mg3ww6d 23 дні тому +1

    Ndipo ndizoonadi apolice akumalawi ziwani kuti mawa limafika ine ndikupepha kuti ualamulilo wakuphau ukazangochoka apolice ose azawachotse tchito mmm ayi

  • @beakab2378
    @beakab2378 23 дні тому

    Viva KK, great message 👍

  • @PrincepreciousMwasangwale
    @PrincepreciousMwasangwale 22 дні тому

    Wise man 😊

  • @princedetbozsmallboy1749
    @princedetbozsmallboy1749 23 дні тому

    Listen is better than beautiful sacrifice, palibe chamuyaya

  • @MadalitsoTamayenda-ez5pj
    @MadalitsoTamayenda-ez5pj 23 дні тому +1

    Yex thus fact becareful ma fon amene anaranda apolice akufune ayikemo ma poison at the end aperekeno what kind of this government am be shame😢😢😢

  • @user-fi7ko7bl6f
    @user-fi7ko7bl6f 23 дні тому

    I salute you Mr K K

  • @SteveAngaMuwellah
    @SteveAngaMuwellah 23 дні тому +1

    Mwaputa olakwika....

  • @Raph-kayRaph-kay-g5v
    @Raph-kayRaph-kay-g5v 23 дні тому

    Respect to you Mr kamulepo

  • @frankiechasokoneza5802
    @frankiechasokoneza5802 23 дні тому

    Bravo Mr kamlepi kaluwa

  • @aubrygrasten1441
    @aubrygrasten1441 23 дні тому

    Great voice sir

  • @AdoptedNaijaBoy
    @AdoptedNaijaBoy 23 дні тому

    Patiently waiting for the day to see cctv footage of the fools mumu police

  • @user-db3mh9wr9v
    @user-db3mh9wr9v 23 дні тому

    This Chakwera must go they take people like fools

  • @lovenesskampira
    @lovenesskampira 23 дні тому

    Ku Malawi si kulilongwe kapena kukasungu hiyaaaa!!!!

  • @frankjolijo
    @frankjolijo 23 дні тому

    Kamulepo Kaluwa🙏🔥👊🔥

  • @user-fi7ko7bl6f
    @user-fi7ko7bl6f 23 дні тому +1

    Tell them the liyaliya😅😅😅

  • @LumbaniNeba-d9n
    @LumbaniNeba-d9n 23 дні тому

    Mawu amphavu Mr Kalua

  • @cacksygustarf6260
    @cacksygustarf6260 23 дні тому

    Tell dem sir agalu amenewa hiyaaa

  • @user-fi7ko7bl6f
    @user-fi7ko7bl6f 23 дні тому

    Hiyaa! Mwanyanya a MCP kwatola amalawi lero mwakumana nazo,muyesa Malawi yu ndi wamanu agalu okupha

  • @MadalitsoTamayenda-ez5pj
    @MadalitsoTamayenda-ez5pj 23 дні тому

    Respect

  • @iamandypandy
    @iamandypandy 23 дні тому

    Mwalasa honourable Kaluwa you should stand for presidency you will get support from Malawians

  • @hanifahmponda8711
    @hanifahmponda8711 23 дні тому

    Aaaa MCP anadzolowela kupha ndi kudzuza anthu mistake tinapanga poyibwedzelatso boma iiii

  • @StevenGoodson-kn7ug
    @StevenGoodson-kn7ug 23 дні тому

    😂😂😂😂 kwachema

  • @juliusnjerengo2610
    @juliusnjerengo2610 23 дні тому +1

    We worn you guys about Chakwera and MCP you didn't listen. Chakwera ndi munthu oipa mtima and he has never been a pastor.

  • @Cathy-oc7vd
    @Cathy-oc7vd 23 дні тому

    You always chase money... thumba mukauma (dry) you make noise.. it has been ur tricks.. you have been always following the party that is ruling kusaka ndalama... ine simungandipusise nawo Mr Kalua...

  • @IsabelMvula-xn8po
    @IsabelMvula-xn8po 23 дні тому

    Kukula kumeneko kkkkkk

  • @finchiadriano
    @finchiadriano 23 дні тому

    Bwanawa alindi umboni kapena akungolumbwalubwa

  • @phillipstamaley7901
    @phillipstamaley7901 23 дні тому

    🤣🤣🤣🤣🤣

  • @inessmsiyambiri8517
    @inessmsiyambiri8517 23 дні тому

    Zoona munthu uyu anathana kale ndi kamuzu ku one party system panonso aszuzinke mmmmmm koma chakwera bwenzi utakhala ndi umuthu pena

  • @user-hm9nc7lz6e
    @user-hm9nc7lz6e 23 дні тому

    Ambuye mutetedzereni penjani kalua mmanja mwa satanic awa chakwera ndi mcp akufuna aononge moyo wace but ladzalo cakwera why moyo wako umakondwa ukamapha anthu popanda kukhetsa mwazi thupi lako kukapwanya tulo silibwera mmaso mwako bwanji osamupha nick chakwera bwanji

  • @johnarushamasese108
    @johnarushamasese108 23 дні тому

    ❤awudzeni chilungamo 🔥

  • @user-kk4uj8ko8k
    @user-kk4uj8ko8k 23 дні тому

    Awuzeni dppppppppppp

  • @crosbyphiri1745
    @crosbyphiri1745 23 дні тому

    Please do not abandon the Lord Jesus Christ for the sake of politics. Please be a true Christian. It's surprising that the former man of God has gone satanic.