Dpp nayo tinatopa nayo nkuona tinayithamangitsa. Mavuto ali mdziko muno solution si dpp. Awa adzawonjezera kusawuka kwa a Malawi kupsola apa. Malawi is going througheconomic problems because dpp mismanaged this country's economy.
Azisogoleli ameneqa onse alandile ma thembelelo kuyambila ana awo komanso zizukulu zawo za ana awo onse amene azadye ndalama zomwe akubasi za anath osauka alandile thembelelo ndibkhate mu zina la yesu....
Ameen ameen abusa. Apa boma palibe koma chizuzo basi kuononga dziko uku. Koma apa pakufunika nkhondo ambuye atithandize.chifukwa ngati afika pomupha chilima ife ationa ngati ndani.koma nkhondo ndimeneyatsala basi
God is speaking to the government of Malawi anayiwala kuti kunja kuno kuli Mulungu, akupembedza ndalama. Mulungu dzukani pa mpando wanu wachifumu mutimenyere nkhondoyi
Powerful words may God continue bless you Fr Mnthalika 🔥
Anthu atengapotu phunzilo ndizovuta zomwe tikuziona chifukwa anthu amati akufuna kuona kusintha ndiye aonatu nyekhweeeeee
Umenewu ndiye utsogoleri munthu wa Mulungu asamaope kuyankhula chilungamo , osati azibusa enawa kungowapatsa ndalama basi kusekelera zopusa , ana anjoka Inu Mulungu akulangani
What a teaching ❤❤❤ impressed me so much waooooo❤❤❤
Father Inu Ambuye azikupasani moyo wautali simuwopa kuyankhula chilungamo
Amen abishop ndipo talira mokwana koma mulungu simunthu safulumira ndipo sachedwa one day is one day mulungu ayakha
A Bishop mwalitha bomali, ndipo kumene ali Chakwera sakugona ndi m'mene mwatulukila ma Bishop. Chakwera ndi boma lake la MCP lalephera tatopanalo.
Dpp nayo tinatopa nayo nkuona tinayithamangitsa. Mavuto ali mdziko muno solution si dpp. Awa adzawonjezera kusawuka kwa a Malawi kupsola apa. Malawi is going througheconomic problems because dpp mismanaged this country's economy.
Borani DPP inali bwino fertilize wunali bwino anthu tinali ndi chakudya mapassport amapezeka palipose kuchoka ku mzuzu mupaka kumangochi ndalama sinali yotha mphamvu panopa wesi
you have spoken man of. God we. are listing God is God. does not. fail
Chilungamo chokhachoka. Zokhumudwitsa wina tinamusankha anali M'busa..koma lero anasanduka ..
Father mumakwanisa ulaliki wanu wabwino kwambiri
Mlungu anamufunsa KAINI nati: alikuti m'bale wako Abele? Nde anati, taona mwazi wake ukundililira ine kunthaka. Zotsatira anali matembelero pa KAINI. Kukhetsa mwazi kumadzetsa tsoka.
Amen , tangovomerezani bwana president tulani pansi udindo nokha mukuona kuti zakukanikani .
Mwaputa nkhondo. Akatorika si anthu wamba. Wina atengapo thembelero
Kumwamba kulande vote yanga
Tsiku lina Mulungu wamva Pemphero lathu
Amen amen a bishop mulungu wathu salephera, Achilima anati mudima or ukule bwanji koma kuzacha ndithu ❤❤
Kuyankhula kwa mphavu,kopanda mantha,osaopa munthu,tiziopa mulungu
🤣🤣🤣🤣 Malawi ikakhala Nyekhwe nde taithamatu🤣🤣🤣🤣🇹🇿
Amen and amen inenso ndipemphelo langa ambuye afute ma vote abale anga zoona zomwe timaziyembekezela sizimenezi ayi
True talking man of God
@@user-mj2te7vl6p Kung'alula
Azisogoleli ameneqa onse alandile ma thembelelo kuyambila ana awo komanso zizukulu zawo za ana awo onse amene azadye ndalama zomwe akubasi za anath osauka alandile thembelelo ndibkhate mu zina la yesu....
Amen
Amen Amen
Abusa awawa MULUNGU awapatse moyo wautali.imfa ya chilima akatolika sakugona ndipo akati apemphere amakhala serious mcp bro apule samalani
Koma muli ndi lawyer? Kkkk
Amen! Father Ambuye azikutetezani.
Ali ndi khutu amve,powerful Massage.
Tiwemphelere atisiye anthu oipawa afe ndithu, mkhwiyo wa ambuye uwakwapule anthu akubawa
Amen jone chilebwe
😂😂 eshi amen
Powerful massage
Pipo shud listen carefully
Powerful message Ambuye akutetezereni ntumiki
Mau ogwila mtima zoona .
Father mupitilize kumuthira fire chakwera,watikwana
Chipan ali nacho ndi mulungu wathu
Amen. Mulungu ndiye omenyera nkhondo ana ake
IWE loya wachani IWE ndi m.malawi ukunva bwanji siya zimenezo
Amen abusa inuyo mumatha
Amen ambuye akudaliseni coz mwaonse azitumiki asakha kukhara cete ngati dziko likuyenda bwino koma mulungu azapeleka cilango coopsa kwa anthu amenewa
Amen and amen mulungu atithandiza kumeneya nkhondo imeneyu
Munthu wamulungu walankhula apa
@@WilliamBandaWili Kung'alula
Yes father God will help us
Anthu amulungu kugwa kwa munthu openphela amalandila nazo Themberelo.
Amen a Bishop.Amenewa Ndiye mau
Palibe zofuna kutchuka chilungamo chinenedwe achulewa a mcp anapha anthu pangoz ya ndege( chilima) ndi ena onse
Ameen ameen abusa. Apa boma palibe koma chizuzo basi kuononga dziko uku. Koma apa pakufunika nkhondo ambuye atithandize.chifukwa ngati afika pomupha chilima ife ationa ngati ndani.koma nkhondo ndimeneyatsala basi
Akuti apule chasanduka choseketsa 😂😂😂for
Zowona ndithu, malawi akufunika ma demo kuti akozeke
Amen mau awa agwile ntchito kwa woipayo kuti Malawi apulumuke
Ifeso talanda bwana😂😂😂😂😂😂
Pano agula mifut malo mogula makhwala zipatalam
Sibas katolika waziwa chomwe chinachitik game yathapo yambani kulongeza 😢😢 anthu amene ziululika lero zayambik
Mateyu 18 vs 18
Yomweyoo ikhake nyimbo ndi chitsogodzo kwa ife
Ulaliki ugwira mtima ndithu🔥
Mwaputa a katolika ndipo simunati muziona, campaign ali mmatchalichi
Amen bishop, ndipo pitilizani
Amen 🙏 father, Mulungu kutetezeni
Mkwiyowutu ukuchedwa. Ine nde ndikuufuna nsanga nsaname
Mulungu alemekezeke, amalawi tikuzunzika kwambili, atithandize potiteteza kwa anthu a nkhanza ngati awa.Ft Mulungu akudaliseni pobwera ndi chilungamo.mwina liwu lanu linveka kwa MULUNGU.
Mawu amalenga. Amen Father
Amen Chakwela you mast go watikwana
Amen man of God
God is speaking to the government of Malawi anayiwala kuti kunja kuno kuli Mulungu, akupembedza ndalama. Mulungu dzukani pa mpando wanu wachifumu mutimenyere nkhondoyi
Powerful message
Amen,nanenso ndayitengako
Amen wathu sameneyo ..
You are the Greatest , Amen !
Wow this is charming
😂😂😂😂eeesh pastor
Chilichonse chili ndinthawi koma na apapa zafikapa Ambuye chitaponi kanthu mwasanga
Kod amalaw mupepela mpaka liti lawyer nde kuti chan
Tathokoza abusa ameneyu musasiye kumudzudzula pali mau amanena kuti :ONDIUZA ANALIPO KOMA KUSAMVELA KWANGA KWANDIPWETEKETSA
Pharaoh watsala pang'ono kuonetsedwa ukulu wa Mulumgu pompano aziona iyeyo kodi sakuona kuti ulemu wake unachoka Kale kale? President wanji omangotukwanidwa mgati chitsiru?
Ameni abusa ine nde sinavotereko ndipoyamba pomwe ili siboma ayi koma kupha anthu
Vote yanga naneso itengedwe
Uthenga uwo siwamasewela mulungu akutetezelen ameni
Amen father 🙌🙌🙌
Amen father
Alleluia Abosa naneso ndi banja Langa ndaitengako mulungu afufute ndithu!!!!
Amen God hear our prayers , rescue Malawi
Ulemu wanu Abusa ❤❤❤❤❤❤
Wakutumani ndimulungu lankhulan mosaopa chifukwa malawi waonongeka ndi chakwela
Mau amphamvu zedi
Ndatenganso nane VOTE yanga
Amen abshop
God be with you
Amen father Amen mau mau
Tikufuna anthu olimba mtima kumalawi kuno ngati fazzala awaa
Uthenga uwuwu ukamufika woipa chikumbu mtima chimugwile
Ine aroma ndimayiziwa ndiyimeneyi kafuseni malemu kamuzu aroma sia mcp
Koma yaa🤝 9:58
Munavotela zisilu kodi nanu
Chakwela azindikile kuti akadzangotuluka boma akutengedwa komaso manganya ndi wa MCP asamatinamizepo apa
Yangaso ndatenga
Mukatenge chinzukwa uko Kuti chilamulire Amalawi mwandilidza😢
Mulungu wanthu ndi lawyer basi
Bishop Amen
Analowa mu Zina la ubusa 😢😢😢osaziwa satana watola joker eeeeee ai chakwela wapweteka Malawian 😭😭
Mumatha kurarika bwino bwana
Amen
Amen Amen
Amen 🙏
Momwemo abishop