KU CHIKANGAWA NDIYE KWACHEMA UKU / ZINTHU ZAKE ZOVUTA🙌🙌

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 5 лип 2024

КОМЕНТАРІ • 392

  • @RiannahKaliat
    @RiannahKaliat 7 днів тому +27

    Pempho langa ndilakut ngat chilima anaphedwa ndi anthu ndikut mzimu wake uwakathe ndipo asowe mtendere mpaka kare uwakathe

  • @RiannahKaliat
    @RiannahKaliat 7 днів тому +33

    Imfa ya chilima mpaka lero ikumandivetsa mutu 😢Rip legend

  • @emmanuelmukondia3568
    @emmanuelmukondia3568 8 днів тому +16

    THE best way is you to prepare yourself with God. So that you are right with God.

    • @jamesgondwe6669
      @jamesgondwe6669 6 днів тому

      God, how many times have we consulted God? How come that God fearless countries are more progressive than Malawi? Do you think we really survive death to claim heaven?

  • @user-fd1tu6ku1r
    @user-fd1tu6ku1r 7 днів тому +63

    The problem with Comrade Timothy Mtambo is that He's after Money so He has nothing to do with the development of this Country. He started as an Activist while His aim was to benefit something.

    • @sithandanechirwa6376
      @sithandanechirwa6376 7 днів тому +8

      I also don't trust Timothy but if I overthink about the dearth of SKC makes me think that maybe Timothy lost direction because of the ruling gvnt. His mouth was shut by other elites who takes Malawi to their own hands

    • @HamiltonwaNamuwah
      @HamiltonwaNamuwah 7 днів тому +5

      Ndi galu kwabasi ameneyi Timothy Mtambo

    • @MarthaJafali
      @MarthaJafali 7 днів тому +3

      Timothy mtambo is a betray cos he was betrayed the who malawians some years ago I really don't like this gu

    • @user-nw6ie3xx8b
      @user-nw6ie3xx8b 7 днів тому +2

      I love this brother but dyela

    • @user-zk7jw9up6m
      @user-zk7jw9up6m 7 днів тому

      Zikomo mtambo

  • @EdoJohn46
    @EdoJohn46 7 днів тому +17

    Antambo 😂😂😂 ndikukutengeni ngati ndinu amene mudasongezera dzikuni dzamoto kuti tipse Malawi muno ndiwe galu kwabasi

    • @ThomasShuga
      @ThomasShuga 7 днів тому

      Very true 😢😢

    • @MatiasMbaula
      @MatiasMbaula 6 днів тому

      Very true

    • @MaggieCement
      @MaggieCement 5 днів тому

      Ndipo Inu alibe umuthu uyu za ziiii mesa iye emweyi ndiamene anapangitsa kuti tilowe mudima akuonapanowo galu zedi

    • @wakisamsukwa9918
      @wakisamsukwa9918 3 дні тому

      No matter how long you have gone the wrong road, turn back.
      Turning back isn't an offence

  • @mishecksipolo7153
    @mishecksipolo7153 8 днів тому +13

    That's too bad,and it's evident kuti chilima anachita kuphedwa,it just needs the youth to clean up this mess

    • @AbelSinoya
      @AbelSinoya 7 днів тому +1

      Khala chete God knows ungatenge tsoka😂😂

  • @HarlodAndrewbanda-vf2rd
    @HarlodAndrewbanda-vf2rd 7 днів тому +9

    We're still crawling to get there!! Rest in peace Dr SKC, UTM is a movement

  • @jogechawa6192
    @jogechawa6192 7 днів тому +5

    For the first time I agree with Mtambo .Sitimayenela kusangalala 6th July. Palibe chikukoma

  • @ChimwemweKondowe-nj4lx
    @ChimwemweKondowe-nj4lx 7 днів тому +12

    Mtambo thanks for the vital words.
    We now needs actions against these idiots in the government

    • @rexphiri6951
      @rexphiri6951 7 днів тому +1

      powerful words Mr Mtambo

    • @ancientnkhata1137
      @ancientnkhata1137 7 днів тому

      Only stupid people with commend the selfish and greedy Timothy Mtambo

  • @Extratremendouszeus
    @Extratremendouszeus 7 днів тому +10

    Amtambo...ngat mukufuna kut ife tikukhululukireni ...pitani ku mademo mutibwenzere dziko lathu...anthu akuopa mademo chifukwa alibe support...mabungwe onse chakwera adasiya abale ake mmaudindo

    • @LOKAMJ
      @LOKAMJ 7 днів тому

      Exactly

    • @ancientnkhata1137
      @ancientnkhata1137 7 днів тому +1

      DPP could have finished us . He did the right thing to rescue some of us from DPP. It was oppressing us

    • @InnocentMmanga
      @InnocentMmanga 7 днів тому

      😂😂😂

    • @Extratremendouszeus
      @Extratremendouszeus 7 днів тому +1

      @@ancientnkhata1137 oooooh ...May the curse of Almighty befall who is a lier...and make them the wood of hell fire

  • @priscillamangata4023
    @priscillamangata4023 7 днів тому +9

    Ndikakumbukila ifa yaathu amenewa mtima umawawa

  • @user-ro1pl7rv7z
    @user-ro1pl7rv7z 2 години тому +1

    Sometimes I wish Bakili Muluzi to come back again....
    Ligongo apano indu yayi itupile Draft kwabasi. 😅😅 Yangajenda Ata panondi

  • @SaidiMbawa-st6bj
    @SaidiMbawa-st6bj 7 днів тому +5

    Mtanbo akuyakhula za ndale zikugwilizana bwanji ndi mwambowu

  • @chrisboyce2
    @chrisboyce2 7 днів тому +4

    SKC forever in our hearts 💔🔥 powerful words Comrade Mtambo Osafooka kms Osaopa Dziko ndi lanthu ife kuno Ku Ntcheu tili mbali yanu...

  • @dhaoudhiabedinegomaseko2363
    @dhaoudhiabedinegomaseko2363 2 дні тому +1

    Mtambo mseu wa Rumphi Nyika Chitipa munawukana mesa munkaguba nkumaphwanya zinthu kuti musinthe utsogoleri

  • @user-te4ii6sz2v
    @user-te4ii6sz2v 7 днів тому +5

    We quote more political speeches than prayers. This was not a political rally

    • @JosephHill-fy1bb
      @JosephHill-fy1bb 7 днів тому

      Ntambo is not a pastor.... Just watch pastor's preaching time...

  • @YohanePatrick-lc2lq
    @YohanePatrick-lc2lq 7 днів тому +4

    Man ife amalawi tikufuna dpp enawa abodza ngati iweyo Timothy anakuchosa ku mcp chifukwa cha katangale

  • @user-zf9xs3zj9b
    @user-zf9xs3zj9b 7 днів тому +3

    Wakuba mtambo akutiona ngati amalawi ndife galu anthu mwa sandutsa ndale ndi maliro a Dr saulos chilima 😂😂😂

  • @JafaliAkimu-ll1bf
    @JafaliAkimu-ll1bf 7 днів тому +8

    mtambo walankhula za mzeru kuposa namachende chakwera

  • @WisdomMaseko-fi5sv
    @WisdomMaseko-fi5sv 8 днів тому +9

    Koma tizikukhulupirirani ndithu a Timothy???

  • @ConfidenceBanda-g8k
    @ConfidenceBanda-g8k 7 днів тому +4

    Koma ndipo poletsa kupepherapo ndie nduchitsiludi,mobwereza amene amaletsa kupepherayo nchitsiru

  • @JohnSingano-f1p
    @JohnSingano-f1p 7 днів тому +2

    The voice of a lion always brings confusions

  • @jonathanmalanda7742
    @jonathanmalanda7742 6 днів тому +1

    A Mtambo ikani za mapemphero kuti mzimu wa skc uuse mumtendere

  • @JosephJosab
    @JosephJosab 7 днів тому +4

    Mtambo ndi kape

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg 7 днів тому +9

    More fire mtambo chakwera machende ako😂

  • @user-ub1mw7ce5p
    @user-ub1mw7ce5p 7 днів тому +4

    Well spoken, comrade Mtambo.

    • @KondananiNjakwa
      @KondananiNjakwa 6 днів тому +1

      He has missed the trail. Uyu watha. Ndipo akamati ngati wina amawona ngati wayimisa agenda, atanthawuza kuti munthu wina anachita kuphedwa? Kulankhula kopanda nzeru

    • @KondananiNjakwa
      @KondananiNjakwa 6 днів тому

      Nanga munthu angati anyamata oganiza bwino akumanena wena Lwarwa aaaah guys Mtambo anaganiza bwanji?

  • @SakanjiraRose
    @SakanjiraRose 7 днів тому +1

    I'm getting confused, he is the man who mobilized people to fight a government that was to me far much better than the this one he helped to form.

  • @SteveKumwenda-t3d
    @SteveKumwenda-t3d 7 днів тому +2

    Chitsiru ichi, ndiponso uku sikumapemphero

  • @LulezLele
    @LulezLele 7 днів тому +2

    Kapolo uyu guyz akulubwa chani, mesa udapanganso ufitiwo at dat time kape

  • @MisheckAselo
    @MisheckAselo 7 днів тому +3

    That's true they is nothing to celebrate 60 years, it's like we help chakwera, kumkuyu ndi zikhale ng'oma kudya mitsonkho yanthu. Ayi momwemo 😂

  • @abwinoamatani4921
    @abwinoamatani4921 7 днів тому +2

    A ndale ndabodza kumene. Ndi chifukwa chake olo akuba ndalama zambiri-mbiri akavala amangokhala ngati avala chithumba chaku chigayo

  • @DannielOnions-fy3dc
    @DannielOnions-fy3dc 7 днів тому

    Thanks so much 🙏 keep it up please we need people like 👍 u

  • @ChiletsoChembe
    @ChiletsoChembe 5 днів тому +1

    Amalawi please! Let's pray to God forgive us and punish those who mudder saulos chilima

  • @TnmMpamba
    @TnmMpamba 8 днів тому +1

    Watching live from Salima, Khombedza

  • @AndrewLanken-v3u
    @AndrewLanken-v3u 7 днів тому +1

    He has got nothing to give malawians never

  • @cassimyusuf6683
    @cassimyusuf6683 7 днів тому

    Well spoken comrade mtambo criticism singalephere as Malawian we were born like that, keep it up comrade

  • @user-bq5ev7de1l
    @user-bq5ev7de1l 7 днів тому +4

    Apm my vote ✊

  • @emmanuelmukondia3568
    @emmanuelmukondia3568 8 днів тому +11

    Idol worship

  • @kamangamathias2001
    @kamangamathias2001 7 днів тому +2

    What's the reason of kuwaletsa anthu ku phiri. Kiphiri kuli chani?

  • @AlinafeMuleso
    @AlinafeMuleso 5 днів тому +1

    Ndipo ngati chilima anachita kuphedwa ndi anthu adzakhala osowa ntendere mpaka Ndipo ngati mizimu imakantha yakanthe anthu amenewa

  • @chadreckchibwithala1493
    @chadreckchibwithala1493 7 днів тому +2

    LUWALA ANGASINTHE CHANI MBAVA YA MNTHU

  • @arthurmanyozo1289
    @arthurmanyozo1289 7 днів тому +2

    Give your life to Jesus.The owner of your soul is Jesus

  • @AbdulKhan-j2h
    @AbdulKhan-j2h 7 днів тому +1

    Mpava iyi atidye bawo bwanji Sumatuluka uli nduna pano abakuchosa ukufuna kodwela amalawi timaiwala

  • @MagretIdimu-u7w
    @MagretIdimu-u7w 3 дні тому

    We're heart broken 💔 SKC still remains in our hearts 😢😢😢

  • @LunnahMtambo
    @LunnahMtambo 7 днів тому

    More fire bro ,love from ccter namtambo cp

  • @AustinBornface
    @AustinBornface 7 днів тому +1

    Malawi timakhala ngati tili pa stage tupanga drama kma ayi ndithu ndi action

  • @RitaKainga
    @RitaKainga 7 днів тому

    Zikomo Inu nonse amene mwalimbabe mtima kupanga mwambo uwu though asatana akutchinga,Mulungu wathu ndwabwino,sanalepherepo,imfa iyi ndyovuta kuiiwala

  • @LloydLuwis
    @LloydLuwis 8 днів тому +4

    Keep morefire mr tman

  • @chrisschikozera7271
    @chrisschikozera7271 7 днів тому +1

    Osaoopa ai......ku Malawi kulibe president

  • @EdwinMakwangwala
    @EdwinMakwangwala 6 днів тому +1

    Only God is our rest not this politicians. God help Malawi

  • @AndersonChiponola
    @AndersonChiponola 3 дні тому

    Mtambo ndamene anapangitsa zonse izi palibe chomwe angayankhule Mutu wake sumayenda bwino ameneyo chifukwa anamuchotsa unduna wagwa nayo Mbuzi iyi

  • @user-ie5pc4ox8i
    @user-ie5pc4ox8i 3 дні тому

    Ada awawa bwenz Ali MUNTHU wapamwamba kwambir kma Anapanga zausiru ngat akufuna timukhulukire ayambise mademo

  • @JohnAsendi
    @JohnAsendi 7 днів тому +1

    Antambo vuto chinthu chimozi mumafuna ndalama Chonde muzikhala ngati Born Kalindo chifukwa amati pavute pasavute asayimira amalawi ndipo akuti imila amangidwa amangidwanso pomwe enanu mumatifuna pomwe zakuvutani tikukukuwerenganitu INEYO NDIKUCHALENJA zoti wina aliyese aime payekha kuyambira Apita. Tupele. Raz. Nankhumwa. Shahana. Osati Chakwera Amayi Joyce banda ndi phulezdent Kalindo. Ndiye tikavote masankho mawa mwachilungamo mopanda kubela angawine ndi Kalindo chifukwa ndi amene akuoneka kuti angatithandize osati Ena inu 😁😁😁😁😁😁😁😁😁

    • @inessmsiyambiri8517
      @inessmsiyambiri8517 7 днів тому

      Inuyo

    • @user-ww4ei5fb7d
      @user-ww4ei5fb7d 7 днів тому

      Kalindo ndiolimba mtima, ofunika kumuvotera. 😂

    • @JohnAsendi
      @JohnAsendi 7 днів тому

      @@user-ww4ei5fb7d zoonadi sister osati enawa akuoneka ngati akuti konda koma mmitima mulibe chikondi

  • @KenChitete-pg3ws
    @KenChitete-pg3ws 7 днів тому +2

    Vote yanga yikupita kwa afford

  • @ChilangoNdalama
    @ChilangoNdalama 7 днів тому +2

    Big mtambo timakunyadiran

  • @surgeon1621
    @surgeon1621 4 дні тому

    Malawi has become a very sad country. Everyone is just fighting for their own stomach. A person like Mtambo shouldnt be applauded like that as if he wasnt a minister in this government. What achievement can he show malawians to prove he is a better man for malawians. A lot of people want to use Chilimas death to gain points for themselves and yet they have no substance themselves. Too much sentimentalism without constructive knowledge

  • @user-nf3ik3ff6y
    @user-nf3ik3ff6y 7 днів тому

    Good Messnge Mr Mutambo

  • @user-eh1mg3ww6d
    @user-eh1mg3ww6d 7 днів тому +1

    Akulesa bwanji ma pephelo akuopa chani tiyeni nazo pephelo ndi chida

  • @VincentAndrew-jz2gf
    @VincentAndrew-jz2gf 6 днів тому +1

    Atambo ,Ulibe Zelu unaphetsa Athu Ambili

  • @AlinafeMuleso
    @AlinafeMuleso 5 днів тому

    Imfa yachilima ine sinfidzaiwala mpaka pano ndikulirabe ngati kuti anali bambo wanga amene anabereka ine koma sichoncho Ndipo mzimu wachilima ukuyendayendabe pakati pathu mzimu wachilima ambuye muulandire kumpando wanu wakumparadise

  • @YahayaUndiya
    @YahayaUndiya 7 днів тому +1

    Mpira amauona ndi akunja big bolani osaiwala zimene mukuyankhulazi antambo

  • @WiscotDzombe
    @WiscotDzombe 2 дні тому

    Uku ngat kunari kumapemphelo ngat uyu anari compain amtambowatu safuna Bata Malawi koma kusokoneza

  • @user-wz1or9ud9i
    @user-wz1or9ud9i 6 днів тому

    Mzimu wa chilima awasowetse mtendere anthuwa mpaka anfe amene anapha chilima.

  • @vinceynyone6693
    @vinceynyone6693 7 днів тому

    Viva mtambo Viva🔥👏👏

  • @markjames-v1f
    @markjames-v1f 2 дні тому

    Chomwe mkukanikila kutiyimilira ndichan boss wanga

  • @AlinafeMuleso
    @AlinafeMuleso 5 днів тому

    Munayambira kukonaza dziko mudzamaliza liti komanso palibe chimasintha mumaona ngati umphawi wamalawi ndiye podyera panu komanso polemerera panu palibe chanzeru chkmwe wayankhula mtambo apa

  • @AlinafeMuleso
    @AlinafeMuleso 5 днів тому

    Mtambo mtima wake ndi wadyera mmene wachoka ku MCP akufuna apeze not adzidyera kudzera kwachihanna ndiye in leronso asabwere ndimabodza ake ofuna podyera watipwetekesa ngati dzikoli Lili pamoto nfichifukwa Cha iyeyu ndi galu kwabasi

  • @edsonnyasulu5394
    @edsonnyasulu5394 7 днів тому

    Exactly Andale akale achoke boma achinyamata alamulire dziko nkhalamba ndi mfiti komaso ndiankhaza

  • @abwinoamatani4921
    @abwinoamatani4921 7 днів тому +1

    Dziko la Malawi likuyenda cham'mbuyo

  • @GoodluckMwenifumbo-dk8jk
    @GoodluckMwenifumbo-dk8jk 7 днів тому

    Anthu ambiri osutsa pano ndi a MCP
    Zoona mpaka kuwaopseza amipingo,a MCP mwafikapotu

  • @MarriamBakalie
    @MarriamBakalie 6 днів тому

    Mtambo ndiwe galu kwabasi usamawapusise a 🇲🇼 anthu anakuona kale galu iwe zako zinada kale machende ako osavinidwa mbudzi

  • @SaeedHurzrut
    @SaeedHurzrut 7 днів тому

    chilima wakuba ngati amwalira sangakhale wabwino Ife tonse tikuziwa zimenezo aphana pa gwilozano wawo

  • @taombeedward5026
    @taombeedward5026 5 днів тому +1

    The biggest problem mtamboyu

  • @tiwongehojaney5873
    @tiwongehojaney5873 7 днів тому

    Amtambo naye ine ndinakhumudwa naye ndipo ndinataya chikhulupiriro mwaino mwatulukirano nthawi yonseyi munali momwemotu mu Timbaland wakudayo ndiye pano mukutinamizaso chani apaa iyaaa😊

  • @henryphiri6100
    @henryphiri6100 5 днів тому

    Chilima anaphedwa ndi Zikhale Ngoma,Chimwendo,ndi Kunkuyu.

  • @GibsonBakha
    @GibsonBakha 7 днів тому

    Andale inu musamatiwawitsemutu muma gofuna ndalama agalu inu

  • @MACKDADFFDANIEL
    @MACKDADFFDANIEL 4 дні тому

    Vuto athu kumalawi safuna kumenyela athu ovutika kom mimba zawo zomwe akuyakhula uyu ntambo ngati Ali ndi nzeru chonsecho momwe anali nduna samayakhula PAno anamuchotsa wayamba kuwalalatila athu omwe anawasiya a kugwila ntchito mbuzi ya muthu uyu ndipo ndipo ndiyemwe anapangitsa kut athu azivutika mpaka lelo

  • @HenriqKwilasi2022
    @HenriqKwilasi2022 7 днів тому

    Iwenso ndi mfiti chifukwa ukupanga za ndale mtambo

  • @AngellachifundoMwale
    @AngellachifundoMwale 6 днів тому

    Mumatipangisa ndinu omwe muli ndikuthekela kolamula dzikoli koma chonsecho simutithandiza and iwee ntambo uli nkuyankhula koma osakwanilisa mxiii unduna uja unali pheeeee ife tikuvutika pano fukwa cha nzerru zomwe unatilimbikisa ife kuti tikavotere mcp yet lero ukuti usintha ziko mub 2025 yet wakanika zaziii

  • @MaggieCement
    @MaggieCement 5 днів тому

    Iyeyu anali boma momwemonwapanga chani atinyase apa chifukwa anamuthothamo modzi mwa anthu okhutisa mimba iyeyo aligulu lomwelo hiya zokuba basi😊

  • @CharityKangulero
    @CharityKangulero 7 днів тому

    ❤❤❤ Exactly

  • @user-qs2tx7wt6g
    @user-qs2tx7wt6g 7 днів тому

    Achinyamata ake ati angavele iweyo pathako Pako iweyo unakakhala wa mzelu unakakana undunaaa

  • @YasinAmidu-b7b
    @YasinAmidu-b7b 7 днів тому

    The problem with us is that we are the ones that took evil to lead us

  • @user-lz4kc5ob1t
    @user-lz4kc5ob1t 6 днів тому

    inetu ndimangokuveran anyamata a mcp ndimaziwa kt simunakumane nazo uyo mtambo ngat ndinu madolo kkkkk

  • @user-ok7bq9es3y
    @user-ok7bq9es3y 6 днів тому

    Timothy unali ndi molaro kale iwe because of Msundwe barracks, size yako ndi Chimwendo. Ulibe faz iwe

  • @PeterThomas-lw3io
    @PeterThomas-lw3io 7 днів тому

    Rest in peace 🕊️ chilima anagwira chito yaikulu DPP mu
    2014 ikanafela giya komano chilima anapanga zotheka kuti Peter akhale tsogoleri muchomwechotso mu 2020 wayigwira ntchito yathangata kumuyika Crazy Chakwera akulamulila koma njilu ndikupanga mission plane yakumupha yooohhh Chakwera ngoyipa

  • @LimbikaniMakwandu
    @LimbikaniMakwandu 7 днів тому

    Only chilima not you mtambo RIP CHILIMA

  • @abwinoamatani4921
    @abwinoamatani4921 7 днів тому +1

    Nanunsotu mukutichitsa manyazi, 60 eyes ndekuti chani?

  • @AngellachifundoMwale
    @AngellachifundoMwale 6 днів тому

    I feel hurt mukamaimabr apaa nkumafuna kutinamiza kuti tikuvotereni sibwino unduna wanu inuyo munapangapo chani antambo nde lero muzinena ngati inu anzeru ??? Kutiona kupusa Malawi sichoncho

  • @MorrisMapiri-d6z
    @MorrisMapiri-d6z 5 днів тому

    It's not over until it's over. We shall shut up when we will be satisfied.

  • @SajeFurniture-wj1ue
    @SajeFurniture-wj1ue 2 дні тому

    Nkulu wake yemweyu anatibweretsera mavuto, how can we trust him

  • @user-oc8nj3or6y
    @user-oc8nj3or6y 6 днів тому

    But we needs people who can at least change something in this country 😢😢apart from this government that we have now😢😢

  • @WilliamChopika
    @WilliamChopika 3 дні тому

    God is our side nthawi zonse

  • @Josehimba
    @Josehimba 4 дні тому

    More fire comrade

  • @WilliamTemboh
    @WilliamTemboh 7 днів тому +2

    Km tkukhulupilileniso amtambo kapena mukufuna tindalama plz tell me coz munatpweteketsa

    • @Extratremendouszeus
      @Extratremendouszeus 7 днів тому

      Apitenso pansewu atibwenzere dziko lathu...ndiyemweyu adatipereka

    • @DeliaKaduya
      @DeliaKaduya 7 днів тому +1

      Ndipo ndi yemweyu analisiya dziko ku anthu otamba akewa, apa angotibwenzerapo dziko lathu lakale lomwelija

  • @user-bq8gb7tb1l
    @user-bq8gb7tb1l 7 днів тому +2

    Viva mtambo

  • @iqrahchikwenga8991
    @iqrahchikwenga8991 7 днів тому

    Serious reverse gear ineed

  • @SylvesterHarry-n7c
    @SylvesterHarry-n7c 7 днів тому

    Timothy mtambo adali momwemo adagwiramo ntchito palibe chimene adapanga nduwadyera uyu

  • @AlexanderYovatiKhumalo
    @AlexanderYovatiKhumalo 7 днів тому

    How many Presidents who have ruled Malawi down the line 60 years ? The truth matter's speeking to please peoples ears is simple but what is true?

  • @KondananiNjakwa
    @KondananiNjakwa 6 днів тому

    Mtambo was a Minister anapangapo chani? Amuchosa lero azioneka wanzeru?
    Ndale zopusa izi. 6 July mapemphero anali ku BICC basi.