Це відео не доступне.
Перепрошуємо.

Lero mwamuona Yudas Skariyot Yemwe adampereka Yesu (Born Kalindo)!!

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 11 лип 2024

КОМЕНТАРІ • 74

  • @IyahMohyoh
    @IyahMohyoh Місяць тому +6

    Ine si mzika ya Malawi, koma ndinkakhala zaka 13 mu dziko, ndipo ndidzahkalanso. Ndinkamuuza anthu poyambira chaka cha dzana kuti njira imodzi yokutithandiza kugonjetsa ndiye ndi yomweyi. UTM atengane ndi DPP, komwe a Chilima anachokera. Maso anga amanyowa ndikamameera zinkhani zikuchitika. Mlengi wathu atitsogolere mu nkhondoyi. Zikamatentha kumenya zitadzakoma kugonjetsa. Without confidence one and ones are twice defeated in this race of life(Marcus Garvey). Moto iyake basi. Kusengezeratu mwa kathithi. Love an peace. Best wishes 11 thousand km away from you my people. Ndimakunyadirani kwambiri❤❤❤

    • @MalawianCamera
      @MalawianCamera  Місяць тому

      @@IyahMohyoh wow that's nice
      Where are you from?

    • @IyahMohyoh
      @IyahMohyoh Місяць тому

      @@MalawianCamera I am from Russia

    • @MalawianCamera
      @MalawianCamera  Місяць тому

      @@IyahMohyoh Oooh okay wow your Chewa is perfect

    • @user-sy5wd3hn9y
      @user-sy5wd3hn9y Місяць тому

      😂 inuo ndakaz kpn amuna?

    • @MalawianCamera
      @MalawianCamera  Місяць тому +1

      @@user-sy5wd3hn9y musanafuse Mafuso ameneo mutumize kaye connection fee ku Malawian Cameras 😂😂😂

  • @charlesjimu
    @charlesjimu Місяць тому +6

    I don't support any idea of making Alliances with Dpp because both Dpp and MCP is ruled by people of same ideology of the one party system. I think the good think UTM can do is to rebuild party with its new ideology but for the coming 10 years. It should have the long term goals by encouraging and promoting new ideas among youths who will be more voters in 2030 while expanding their presence in the parliament.

  • @PhillipjuniorGogoda
    @PhillipjuniorGogoda 29 днів тому +2

    more fire DC🔥🔥🔥🔥🔥🔥

  • @PatKabiya-hy3vm
    @PatKabiya-hy3vm Місяць тому +3

    Alimbikitsen a UTM Mr Kalindo... palibeso mavuto amene akumane nawo..bola alliance yathapo...let them keeping forward that's all..✊

  • @ZebronTembo-u6p
    @ZebronTembo-u6p Місяць тому +1

    Koma kalindo anakonza ifetinkaona Kuti awa awa analindi cholinga because munthu amalandila malangizo aabwana ke Koma uyu Mmmm anati escariot uyu😂😂😂 aziona next step

  • @MirriamKambale
    @MirriamKambale 29 днів тому +1

    Bon Kalindo alibe mbali that's one thing about him I like amangotulutsa mabvuto wambalizonse ndiku ng'alula iye wautali azabweranso ndiina. Mumisala yakeyi mulinso mfundozina zabwino andalenu tolanimo zothandizazo wamisalatu adaona nkhondo the dddd cccc 😂

  • @user-qn2nu4xs9i
    @user-qn2nu4xs9i Місяць тому +4

    Easy...easy....tawaona kale...ticheza nawo ...zaozo sizitheka!😊😊😊😊😊..anthu ali maso

  • @MarkManyowa
    @MarkManyowa Місяць тому +8

    For Presidency Born Kalimdo ☘️🇹🇿🔥🔥

  • @EbenTechnologies-xq5op
    @EbenTechnologies-xq5op Місяць тому +5

    UTM, Aford, PP should merge their parties to defeat MCP

  • @user-lc3sw8iz2g
    @user-lc3sw8iz2g Місяць тому +6

    A UTM ngati akufuna Congress igwe ndiye kuti agwile tchito ndi DPP.
    Chifukwa Second term ya MCP idzapanga zokuti UTM ithe.

    • @viennasamuel2976
      @viennasamuel2976 Місяць тому

      Ndipo zoonadi kungowamvetsa kuwawa a mcp atuluke

    • @isaihmagani5697
      @isaihmagani5697 28 днів тому

      Sunganene kuti DPP igwire ntchito ndi UTM

  • @joebrown1158
    @joebrown1158 Місяць тому +8

    To be honest Malawian the government is no longer existed there's no government to rule Malawi how is going to be the Parliament without the alliance of the government because that government was formed because of alliance

  • @IyahMohyoh
    @IyahMohyoh Місяць тому +3

    Tsogolo lathu lowala ili mmanja wathu, Mlengi wathu atitsogolere . Kwacha dzukani, tulo ndi lokama, koma ufulu ndi mtendere ndi zithu za mtengo wa patali.

  • @AllySafali
    @AllySafali Місяць тому

    Mayine big man kuzatulukila ndikung'alula mwanyooo God bless u Mr kalindo

  • @user-uv5rf4zt5q
    @user-uv5rf4zt5q Місяць тому +1

    Federal system of government is the only way to go.

  • @williamsalexmbonga
    @williamsalexmbonga Місяць тому

    Nde mukufuna Dr Usi apange risign iwe ndi Mbuzi Winiko eti

  • @alexanderlipenga1330
    @alexanderlipenga1330 Місяць тому +1

    Ine phee kumastand no more recycled politicians be it UDF, MCP, AFORD, DPP, PP, PDP, UTM. We want achinyamata tilamule tokha. NRC for the prosperous Malawi

  • @AubreyChiyaya-ty8ge
    @AubreyChiyaya-ty8ge Місяць тому +4

    Gwesani MCP please kaloweni ku DPP

  • @RamadanShafisha
    @RamadanShafisha Місяць тому

    Kalindo azimutsatila ndimbuli zizake

  • @lyiemax
    @lyiemax Місяць тому

    Honestly speaking from our beloved president, the Dddddd Cccccc!!!! 🔥🔥🔥

  • @MadalitsoChinkhonyo
    @MadalitsoChinkhonyo Місяць тому +5

    Zimenezo nde ayi ku dpp tinachokako basi iwowo ngati akufuna abwele ku utm basi dpp inati khakaza ife sitiyifuna

    • @IyahMohyoh
      @IyahMohyoh Місяць тому +1

      Mwerani mayi Mary Chilima analankula dzulo kuti siyani chidani za ku mbuyo.u kuti tigonjetse anthu oyipa. Koma kufunika nkumalungalira mwozama.

    • @viennasamuel2976
      @viennasamuel2976 Місяць тому

      Ndipo wandiyankhulila bwino Mary

  • @user-do2cs8nf4b
    @user-do2cs8nf4b Місяць тому +1

    UTM bwererani komwe munachokera zakale zapita zatsala zatsopano, ndipo kutsogoloko mudzautenga mpando waupresident bola kulimba mtima

  • @lastonkandiyado4526
    @lastonkandiyado4526 Місяць тому

    Manganya ndiye yudasi sikailoti

  • @RickMahangano
    @RickMahangano 28 днів тому

    The mouth of the voice less, i@the rest of the followers, we like your updates,

  • @franknyasulu7328
    @franknyasulu7328 Місяць тому

    The only way for utm is to unite with DPP afford and udf , ldont think among this for partys can make alliance with mcp , most malawians want the alliance of DPP utm afford and udf

  • @user-hm9nc7lz6e
    @user-hm9nc7lz6e Місяць тому +6

    Zoona autm bwererani ku dpp ndi komwe munacokera

  • @danielmsowoya9107
    @danielmsowoya9107 Місяць тому

    Politics is a game that needs proper strategy. In politics there is no permanent enemy. In my personal opinion, it can be wise enough to gang with DPP if DPP can accept it. Otherwise united we stand divided we fall.

  • @eliasemmamoyo8225
    @eliasemmamoyo8225 Місяць тому

    Ukatelo uziza tukwanaso musogolo muno ndiwe yemwe winiko munthu osaziwika nzochita zomwe uwasiye a utm apange zinthu mwantima pansi wanva winiko wamanyi iwe

  • @FisherAction
    @FisherAction Місяць тому

    DPP Must change your bad behavior lets try Aford mix leaders don't forget mr Chihana please

  • @user-ro1pl7rv7z
    @user-ro1pl7rv7z Місяць тому +1

    Pachibale pawo

  • @FlechaChipeta
    @FlechaChipeta 27 днів тому

  • @sanlakedickson6780
    @sanlakedickson6780 Місяць тому

    booooon kalindoooooooo❤

  • @kangungufoundation2020
    @kangungufoundation2020 Місяць тому

    Chimene chavuta ku malawi ndi ufiti ndi nsanje, akupaseni inu u president tiwone ngati mungakane

  • @anifoiuene6301
    @anifoiuene6301 Місяць тому +1

    Koma nzoona kuti abambo amenewa (chakwera) anali m busa ?? Nanga ndi m busa wanji uyu osanva chisoni ndi nkhosa zake zomwe

    • @lillynhlema9656
      @lillynhlema9656 Місяць тому

      He was a fake pastor....adakakhqla mbusa weniweni sinmbwezi atajoina ndale

  • @hanifahmponda8711
    @hanifahmponda8711 Місяць тому +1

    Aaa amalawi nsitilalola kuti voti opanda ma ID ansadzalembetse voti PAPO BOLANI IDZALEPHELEKE VOTE TIDZAWONE MENE AWONONGELA ZA ID IDZI OSUTSA WADZELU.ANGALOLE ABOMA KULENGEDZA KUTI OPANDA ID ASALEMBETSE VOTE OTSUSA NDIKUMVUMELA AKUDZIWA KUTI KUMWELA NDI KU POTO ANTHU AMBILI ALIBE MA ID DZIZAPANGA DZIWONETSELO ZA DZIKO LOSE KAYA AKUDALILA MAI YOLAMU TIDZAKOMANA KUTSEWU KOKO MCP IDZACHOKE NASI 2025 za ID ayiiiiiiiiiiiiiiiiiiiii TAKANA A MALAWI

    • @IyahMohyoh
      @IyahMohyoh Місяць тому

      @@hanifahmponda8711 Bruto alipo 20 chakuti thousand, anthu 20 chakuti million.ndiye angalimbe mwotani?

  • @marthansaliwa7732
    @marthansaliwa7732 Місяць тому +4

    UTM ikhale paokha basi. Masanzi akasanzidwa sadyedwanso. UTM isayang'ane 2025 koma izikonzekeretse za 2030. Migwirizanoyi ndiyakupha. Munthu sakhutitsidwa ndi ma udindo.

  • @languitoneelias9972
    @languitoneelias9972 Місяць тому

    Mumalimbana ndi chilima presdent wa utm ali moyo mwamukambila zambili lero wamwalira walowa manganya mwayambanso kodi munakhala bwanji inu

  • @amontchuwa6876
    @amontchuwa6876 Місяць тому

    Mr pule Bon kalindo

  • @PeterMajamanda
    @PeterMajamanda Місяць тому

    I know what is Ndale and how

  • @IsaacKulongwe-ol5mx
    @IsaacKulongwe-ol5mx Місяць тому

    Only madness in u kalindo

  • @doreenkaliati3166
    @doreenkaliati3166 Місяць тому

    Iwensotu ndi wabodza pena ndimkakukhulupilira koma apa ndiye ai mwataika kodi siwe umkati DPP siboma labwino umkasogolera mademo iwe lero ukuwaudza anthu kuti abwelere ku dpp uzi sizoona suuja umkanena kuti pita akupha malubino lero ukuti tiyeni ku dpp iwe ndakuona ndiwe nthera kuwiri sopano uyu musamamumvere bola UTM ipange gwilidzano ndi Aford osati dpp zaugalu basi or azaludze palibe vuto

    • @user-dm2fs6hf1b
      @user-dm2fs6hf1b Місяць тому

      Ayi koma mcp is too much they failed what development has mcp done, devaluation fertilizer in dpp time was at 25000 now 95000 can't to see the different killing and intimidation. Sankakwanitsa zonse koma awawa angokwanitsa ma speech koma pa ground 0 pa 100

  • @OwenWalter-nz7uo
    @OwenWalter-nz7uo Місяць тому

    The DC

  • @GiftMwaungulu
    @GiftMwaungulu Місяць тому

    alliance ai zakamika

  • @user-xt2gu9yt9q
    @user-xt2gu9yt9q Місяць тому

    Trapesi ndi Tambo nde gwelo mavuto akumalawi athu oipa kwambili koma ayi mcp yaonjedza

  • @ZebronTembo-u6p
    @ZebronTembo-u6p Місяць тому

    😂😂😂

  • @EllinaBitto
    @EllinaBitto Місяць тому

    Ing¹alule basi❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤

  • @yahgoshen5815
    @yahgoshen5815 Місяць тому

    Now in Malawi it is just dramas

  • @vukanifracksonchinkonde7324
    @vukanifracksonchinkonde7324 Місяць тому

    Propaganda yanu yoti if a utm tipite ku Dpp zikuvutani.....iwe paja ndiwa Dpp.....we can't go back to egypt

  • @AubreyTrust
    @AubreyTrust Місяць тому

    Kuying,alula kweni kwin kkkkkkkk kom

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg Місяць тому

    Manganya ndi fiti size anafupika dzose ndi dzelu dzomwe

  • @RamadanShafisha
    @RamadanShafisha Місяць тому

    Kalindo ndiwe wa Dpp uzachita manyazi 2025 ukunamiza amalawi Dpp sidzalowaso m'boma ndichipani chakupha ulibe zelu kalindo

    • @marryphili5419
      @marryphili5419 Місяць тому

      Wuzachita manyazi ndiweyo bro

    • @RamadanShafisha
      @RamadanShafisha Місяць тому

      @@marryphili5419 zosenzi mukukangalika kunyoza Mcp ndinu alomwe

  • @dalitsonjewa4868
    @dalitsonjewa4868 Місяць тому

    Wamisala uyu😮😮😮😮

  • @user-nq9bg8zo4v
    @user-nq9bg8zo4v Місяць тому

    Dpp no no president wake utiyo?