Це відео не доступне.
Перепрошуємо.

Nkhanga zaona Chakwera watumiza Asilikali kuti Akamuphe Peter Muthalika lero.

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 12 лип 2024

КОМЕНТАРІ • 436

  • @johnmpatama1461
    @johnmpatama1461 26 днів тому +25

    This is the beginning of the end of Chakwera government.

    • @user-mr2mh4gq8w
      @user-mr2mh4gq8w 26 днів тому

      AMbuye mutisogolere Peter ndi salimo 91 ambuye mupase I mzimu wachiziwitso

  • @user-ev6bi7jr7g
    @user-ev6bi7jr7g 26 днів тому +25

    Ndiye MCP tikuidziwa ife ndimeneyo ndale zake ndi zakupha

  • @stephankamyata3862
    @stephankamyata3862 26 днів тому +19

    Achisale pls motsongozedwa ndambuye protect our APM

  • @augustMag
    @augustMag 26 днів тому +18

    Kwa APM yekhayo ndiye sangamukwanise dinner and dance ndi imeneyo koma Peter Muthalika yekhayo ku dinnerko Peter Muthalika akudziwa zokachita ifa ya Bingu Muthalika ndi ifa za anthu padege ukumupasa phunziro Peter amandisangalasa ndi omvera malangizo awanthu ngati Inu Amtanyiwa ndi Bakili Muluzi TV 🔥

  • @BrownMainje-sh7hj
    @BrownMainje-sh7hj 26 днів тому +14

    Shame on MCP

  • @ExcitedBreakingWaves-oh3zb
    @ExcitedBreakingWaves-oh3zb 26 днів тому +14

    Ngati iyeyo akuphanso Pieter nayenso ayenera kusogozana naye.

  • @MayamikoBanda-jh8bn
    @MayamikoBanda-jh8bn 26 днів тому +29

    I love the way momwe mumachenjeza Malawi kwa zigawenga . Ndiye nimamutsatilani kwambiri pa UA-cam Kono ku Zambia

    • @MaggieMujuma
      @MaggieMujuma 26 днів тому +1

      Eeeee mayo ndalama yanga ine Peter munthalika iwe ndi Wilson msemanjira iwe anthu okuba inu

    • @chimeraJonathan
      @chimeraJonathan 24 дні тому

      L

  • @AiameAdamo-su1nt
    @AiameAdamo-su1nt 26 днів тому +12

    I'm here following you step by step each and everyday.

  • @PhilipMatolino
    @PhilipMatolino 26 днів тому +15

    Kom guyz chakwera khani ndiyotu wina kungofanso kukhala ma demo anyooo!! Mwatitola mcp kwambiri

  • @KhalideNerve-mu1eq
    @KhalideNerve-mu1eq 26 днів тому +10

    Mission impossible God is watching 😢

  • @KennedyPhiri-h9h
    @KennedyPhiri-h9h 26 днів тому +3

    Thanks for your information Mr Limpopo FM 🙏 we always with you

  • @louisgolden
    @louisgolden 26 днів тому +6

    May Allah protect APM

  • @user-ew4dm8yy3b
    @user-ew4dm8yy3b 26 днів тому +8

    Achisale motsogozedwa nd mulungu please protect apm

  • @chrisschikozera7271
    @chrisschikozera7271 26 днів тому +6

    That's end of mcp in this country again.....God ll protect Amp

  • @lovenessmuthiya3513
    @lovenessmuthiya3513 26 днів тому +6

    May God protect APM

  • @user-be5fc3ed1i
    @user-be5fc3ed1i 26 днів тому +3

    Nyimbo imeneyo ntanyiwa ukamabwera pa Limpopo FM usayisiye chonde Limpopo FM moto kuti buuu 🔥🔥 🔥🔥🔥

  • @JosephyMakunganya
    @JosephyMakunganya 26 днів тому +9

    Apa ndiye alimbana ndi achina chisale 🔥🔥 Malawi wafika posauzana

  • @CharlesMaloya
    @CharlesMaloya 26 днів тому +5

    Chakwela and Rwanda foreigner based in Malawi you will get what you want warning to Rwanda you will see

  • @salimmkumakumakitombi-yc7pw
    @salimmkumakumakitombi-yc7pw 26 днів тому +14

    APM SANGAPITE NGATI CHIWETO .YEMWE UJA MUNAPANGA UJA BANSI .. APM ATUPELE CHIHANA ANTHU AWAWA SANGAPANFIDWE NTINTINI NEVER

  • @AjibuTwalibu
    @AjibuTwalibu 26 днів тому +6

    Mwachita bwino
    Comrade mtanyiwa
    Tili nawenawe sitingakutaye

  • @RobertNedson
    @RobertNedson 11 годин тому

    Ambuye apitilize kukudalitsani 🙏🙏🙏🙏musafooke chonde chonde mulungu ali mbali yanu ndi ife ofuna mtendere ndiochitila chifundo malawi aliyese amen!🙏🙏🙏🙏

  • @AlexMbewe-p7y
    @AlexMbewe-p7y 26 днів тому +6

    NDIPO SIZITHEKA AYI MULUNGU ALI KOMWEKO AMENEUJA SANGAKWANISE CHAKWERA KWAKE KWATHA NDIPO ALI NDI THAWI YOCHEPA MULUNGU AMULANGA ANANGOKHALA BUSA KOMA NDICHIGAWENGA CHACHABECHABE BUT I BELIEVE GOD IS THERE TO PROTECT PETER WA MUTHALIKA

    • @macdonaldkorea2928
      @macdonaldkorea2928 26 днів тому

      Or nkhope ya Chakwerayo ikuchitakuonetsa kut ndinkhandwe yoopsa....asapotilidze.konse aidya malawi yonse

    • @StelliaSangaya
      @StelliaSangaya 22 дні тому

      Zoonad

  • @Emmanuelisraelsimbi
    @Emmanuelisraelsimbi 26 днів тому +2

    Koma ngati mgwirizano watha ndiye tikhale chisankho tu coz utsogoleri wu unasankhidwa pansi pa mgwirizano wa Tonse. Lets vote guys

  • @user-dn3gp6yi4y
    @user-dn3gp6yi4y 26 днів тому +8

    Kumeneko ndiye ku mafelano kuja sopano koma anthu awa akuti bwanji ndi dziko lathu cholinga chawo ndi chani? Komaso asilikali athu angoti ziiiii kumangowonelela dziko likuwinengeka koma zoti abale awo ndi makolo awo ku mamamidziku akuvutika iwowo sakuziwa kodi? Nanga chomwe akumakhalila chete ndi chani ? Chakwela kwake kwatha ife tikufuna mtendele mu dziko musakomedwe ndi ndalama komaso omwe akudya ndalama za magazizi si asikali onse pali omwe akumadya enanu dzukani kutha ndi boma lopusali lakupha la mabodza komaso pa katangale azathu aku mangochi tetedzani PM kumeneko akaziwika anthuwo apondeni or kuwapha kumene np afela zintchito zawo

    • @VeronicaChirwa-ct4os
      @VeronicaChirwa-ct4os 26 днів тому

      Asilikali a Malawi amawoneka kuti ndi opepera safuna kuthandiza Zika za Malawi akowopa kuyimbira anthu akulemekeza zigawenga zi Achina Chakwera

  • @HamzaMkwanda-bh8dc
    @HamzaMkwanda-bh8dc 26 днів тому +4

    We don't have any police in our country

  • @ChifundoNinje
    @ChifundoNinje 26 днів тому +4

    Plz plz achisale amunkhitho plz maso ndinu kt amene mumapeleka chitetezo Kwa Pam

  • @preciouskadembo1932
    @preciouskadembo1932 26 днів тому +2

    Dr Bakili Muluzi amkatuza koma ife aMalawi kusamva

  • @user-tw2zf7bj3e
    @user-tw2zf7bj3e 26 днів тому +13

    May Allah almighty protect Apm 🤲 amiina

  • @ephraimphalawala4720
    @ephraimphalawala4720 26 днів тому +9

    In Jesus name, God protect APM

  • @PeterJames-i8y
    @PeterJames-i8y 26 днів тому +6

    Mulungu amene anapulumutsa shadrec ,Mishec ndi abitinego kuphatikiza Daniel mudzenje lamikango apulumutsenso azitsogoleri amene atsalawa. kuti kudziwike kuti kumwamba kuli mulungu wamoyo amene sagona komaso saphethira amawona chilichose cha pasi pa thambo. mulungu apitilize kuulula zisisi pa ana ake amen.

  • @salimmkumakumakitombi-yc7pw
    @salimmkumakumakitombi-yc7pw 26 днів тому +13

    Uthenga upite kwa Norman chisale .onesetsani kuti chitetedzo chakhwimisidwa pa gate

  • @harrietmkusangombe
    @harrietmkusangombe 26 днів тому +3

    God have mercy on our country

  • @AhmadShariff-bk3rr
    @AhmadShariff-bk3rr 26 днів тому +7

    Mission impossible

  • @OnenessLestas
    @OnenessLestas 26 днів тому +1

    Zamaboza basi mulungu akuwoneni

  • @ephraimphalawala4720
    @ephraimphalawala4720 26 днів тому +4

    Prayer Malawi

  • @user-pv9uk6sc3w
    @user-pv9uk6sc3w 26 днів тому +1

    End of chakwera and MCP, achepa, wapha uja Chilima wakwana basi. Thanks to Limpopo FM.

  • @IbrahimPhiri-ky5jk
    @IbrahimPhiri-ky5jk 26 днів тому +8

    Awili aziwika kale tikuimbolani kuti muziwe zosatila anafika pa asoko ndiye atawapo koma tikuwalondolola anyani amenewa komanso mangochi boys ili paliponse 💯

  • @FrankSpison-o7o
    @FrankSpison-o7o 26 днів тому +4

    Lord have mercy on us

  • @user-bd5kw8oq1r
    @user-bd5kw8oq1r 26 днів тому +3

    Koma apa pali anthu odwala amene amakhulilupilila social media dziko lathadi basi munthu kungodzuka kupanga plan yoyipitsa munthu basi the opposite is true inu ndi amene mukufuna chakwera ataphedwa mu nthawi ya DPP anthu amaphedwa ambili apa lero iliso layipa bndiyetu sankhani yesu osati satana mudzakondwa

  • @PatrickSomanje
    @PatrickSomanje 26 днів тому +2

    I love u mr khanga osawopa ngwilanani manja pls

  • @user-pt8wb4vw6r
    @user-pt8wb4vw6r 26 днів тому +1

    Inu antanyiwa mwina inuyo ndinu mmapha anthu ndiye mzinamizila ena ndinu zizsilu ndi maboza anuwo

  • @GRACIOUSKENAN
    @GRACIOUSKENAN 25 днів тому

    Ntanyiwa ndiwe one, continue ,tilibe asilikali angakhale police, kulibe ndattttiii aaaaaaa !!!!!!
    Agalu alipowo ntchito ndi zigololo bas😰😭😭

  • @vituveggah7619
    @vituveggah7619 26 днів тому +4

    Osazamuphwekesa comrade

  • @AndrewChilambo
    @AndrewChilambo 26 днів тому +2

    Antanyiwa pitilizani kuchenjeza amalawi zazigawenga za mcp

  • @AiwaMedia-sh6vx
    @AiwaMedia-sh6vx 26 днів тому +2

    Limpopo FM and BAKILI MULUZI TV mukuyesetsa ndithu kutitsegula mmaso koma amene alikutsogolo kwathu n'gokhumudwitsa. A Opposition aliko????

  • @GrinTemboh
    @GrinTemboh 26 днів тому +1

    Continue with good news we always listen u ukutimvetsa kukoma ntanyiwa

  • @benjaminjobo3525
    @benjaminjobo3525 26 днів тому +1

    Nyimboyi ndaikonda Antanyiwa cain ndi abelo

  • @tiwongehojaney5873
    @tiwongehojaney5873 25 днів тому +1

    God will protect Peter ❤❤❤😢😢

  • @ThivadoartistDyson
    @ThivadoartistDyson 26 днів тому +2

    Akangopha peter l tell you chakwela we come by the trip cross the country kukathana ndi iweyo alu continue.

  • @kennethkaunda3636
    @kennethkaunda3636 26 днів тому +5

    Can I come to Malawi and show my position to chakwera government?

  • @user-sw8bb3iz7x
    @user-sw8bb3iz7x 25 днів тому

    God protect APM

  • @AleksaWilliams-qc6cn
    @AleksaWilliams-qc6cn 26 днів тому +5

    Yoo alipachintchito eti

  • @BlessMnyenyembe
    @BlessMnyenyembe 26 днів тому +2

    Thanks

  • @AllanKamphata
    @AllanKamphata 26 днів тому +1

    Mwasowa nkhani, akaphe nkhalamba ngati imeneyi

  • @user-vq5fe6mo6o
    @user-vq5fe6mo6o 20 днів тому

    Nipamene wina akt chakwera 😢😢koma zowawa izi menyeren nkhondo Ambuye titan padziko pano

  • @UsenLashid
    @UsenLashid 26 днів тому +1

    Mulungu ndiwamphavu yonse Nothing can happen to them in the name of Jesus

  • @MatemangaMoyo
    @MatemangaMoyo 26 днів тому +1

    Limpopo FM ndi bakili muluzi tv, mulungu akupaseni moyo wautali

  • @Janaphiri
    @Janaphiri 26 днів тому +3

    Munthalika wakuti sangalanulire Dziko la Malawi ali ndi ntchito yanji?
    Za fodya basi Kodi mwasiya za Tea mwayamba za chamba eti

  • @WisdomMaseko-fi5sv
    @WisdomMaseko-fi5sv 26 днів тому +1

    Koma mtanyiwa ndi masewero ako ukuzuza anthu kwabasi ona ena ayamba kale kupempherera APM kkkkk

  • @kensonmbewe6692
    @kensonmbewe6692 24 дні тому

    I think this is a sign that we have so many satanists in Malawi, we need God, anthu afika pongoyankhula zimene akugani as long as it will black mail Chakwera, how can you feel if that happens to your father. Too bad

  • @nyanguoipa6996
    @nyanguoipa6996 26 днів тому +1

    Anthu amenewo asamale mangochi sigawa ma sweet

  • @AREFRIEDNELSON
    @AREFRIEDNELSON 26 днів тому +1

    MCp ndichigawenga kuchokela ma 90s nde wina iziti chakwera Alobwino walowa nzwiwanda wangofika pa misara

  • @ChristopherManase-s1f
    @ChristopherManase-s1f 26 днів тому +1

    Eeeee koma ma cadet muli pa ntchito. Kkkkkk

  • @adrianobrigida3402
    @adrianobrigida3402 26 днів тому +1

    Chigawengacho Chichewa Chakwera chikutseweretsa miyoyo ya wanthu.

  • @kidneyblessingschilinguloj7292
    @kidneyblessingschilinguloj7292 26 днів тому +3

    Keep it up

  • @piliranimalama6090
    @piliranimalama6090 26 днів тому +3

    Anthu ndiye kuwadodatu ndi mabodza

  • @FamousJohnathan
    @FamousJohnathan 26 днів тому +2

    Yanjiru simatani..?

  • @JohnFrank-g6e
    @JohnFrank-g6e 14 днів тому

    Ndi Ana awa zomwe akufuna sizitheka komwe in the name of Jesus

  • @macdonaldkorea2928
    @macdonaldkorea2928 26 днів тому

    Tiyamike kut okonda dziko ngati achina Mtanyiwa alipo ambiri....chifukwa chaichi choipa sichibweredzedwa....a Gadama, Matenje ndiena monga a Chilima ndiena aja akwana, pa Muthalika pokha usayerekedze ndithu iwe Chakwera (kungokhala anthu amagazi basi)
    Bakili Muluzi amkanenatu kut MCP siyoyanjana nayo lero ndiiyo itangolawa mpandowo basi kupha kwadzuka ASAAAAA

  • @cliftondad3816
    @cliftondad3816 25 днів тому

    Zinazi zalowa fodya zinthu.. apa nde trust pa nkhani zanu ndachosa.... Maboza

  • @user-od6eo5zc4h
    @user-od6eo5zc4h 26 днів тому

    Mudzina la yesu christu mnazaleti mutetezelnini Peter mutalika kulikonse komwe kuli iye

  • @christophergibson72
    @christophergibson72 26 днів тому +1

    Inu munthu watha kale uyu mufuna mudanitse basi

  • @JosephyMakunganya
    @JosephyMakunganya 26 днів тому +2

    Nkhope za Rwandans zimadziwika asalowe dara kumeneko

  • @EliasKawuwa
    @EliasKawuwa 26 днів тому +1

    A Ntanyiwa tengani ndi inuyo dzikoli,musawauze azanu kuti atenge koma inuyo, a Bon Kalindo, wa Bakili Muluzi TV,atenge dzikoli,kuti kunyoza,ndikutukwana kusiye, kumangonyoza basi, zambiri zimene mumanena ndizabodza kwambiri, zonse akunena za Peter Muntharika ndi zabodza zimenezo, kungofuna kudzionetsa kuti achina Peter Muntharika awaone kuti akupanga za iwowo,kuti DPP ikadzawina adzawatole,adzadyetse mimba zawo

  • @user-gd6zb2bv8f
    @user-gd6zb2bv8f 24 дні тому

    CHAKWERA tamachita manyazi zinazi popanga, nawenso Manganya ndiwe katukule, Mulungu wakumwamba, achite nanu mwapadera ndipo asakusiyani chonchi

  • @patrickkusailemp3769
    @patrickkusailemp3769 26 днів тому

    Longlive APM ..God is in control !!

  • @ibrahimalex7137
    @ibrahimalex7137 26 днів тому

    We're here my brother ❤

  • @MalawianMediafm97
    @MalawianMediafm97 26 днів тому +1

    🤣🤣🤣🤣 this is Comred ntanyiwa on Lipompo FM

  • @MuhammadBAKILI-kl2mj
    @MuhammadBAKILI-kl2mj 26 днів тому +1

    🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏yomweyo chikangawa

  • @GodifureRifa
    @GodifureRifa 26 днів тому

    Mulungu mumutetezere peter muthalika kulikose komwe apita 🙏🙏🙏

  • @SmileMalanda
    @SmileMalanda 26 днів тому

    Akuluwa misala chani kapena mwaz wachilima nd anthu ena aja zikuwazunguza😂😂😂

  • @NDIZOTHEKABANDA
    @NDIZOTHEKABANDA 26 днів тому +1

    Mabozatu amenewo

  • @mellipherjohn7158
    @mellipherjohn7158 26 днів тому

    mumakwana bwana wanthuu🎉🎉🎉

  • @marryphili5419
    @marryphili5419 25 днів тому

    Shame you chakwera fiti Yopanda manyazi wunapha chilima Pano wayamba kusaka Peter wupha anthu angati iwe

  • @AgnessMita
    @AgnessMita 25 днів тому

    Ambuye akutetezeleni APM

  • @MaureenBanda-t2q
    @MaureenBanda-t2q 26 днів тому +1

    Asiyeni akafa ndiiwowo ili ndi dziko

  • @user-gm3cx2xn9o
    @user-gm3cx2xn9o 23 дні тому

    Inu anthu akungofuna kutchuka ndiye inu muli busy 😂😂😂😂😂

  • @BenjaminCharlie-md3fk
    @BenjaminCharlie-md3fk 22 дні тому

    Umakwana ntanyiwa koma akangopha muntalika nafe tipha ndimiyala chakwerayo

  • @GraceMbengo
    @GraceMbengo 25 днів тому

    We pray for God's intervention. Mission iyi Ambuye alowererepo.

  • @chadreckchibwithala1493
    @chadreckchibwithala1493 26 днів тому +1

    koma mmm ntanyiwa boza ngati mnthu wa nkazi aaaa mnthu oti si wa dpp akagula ticket mnthu wachilendo aaa

  • @kangungufoundation2020
    @kangungufoundation2020 25 днів тому

    Kodi amalawi bingu anakulakwirani chani?? Munamuchotsa mwachipongwe, peter uyu mukuti peter ndimunthu amene munamuchotsa mwa chipongwe again kungoni peter ndi chitsiru akuloranso kuti azapangidwenso chipongwe, saulos chilima zana zanali mumamutukwana limodzi ndi chakwera nde poti lero wamwalira wasanduka wabwino amalawi mulibe nzeru you deserve what is happening and there is no way out until you change, you will reap what you sowing

  • @user-uk1tt7ho9t
    @user-uk1tt7ho9t 26 днів тому

    May Lord for everything please protect our beloved president

  • @CatherineDesire
    @CatherineDesire 22 дні тому

    Asilikali nanuso bwanji otsangomupha iyeyo wakutumani Kodi anzako sakufuna moyo

  • @JabiluWaiti
    @JabiluWaiti 25 днів тому

    Mmmm koma akachoka kwa Peter abwera kwa inu a UDF inunso mukuyenera kukhala osamala

  • @user-kc7sd3te3d
    @user-kc7sd3te3d 26 днів тому +1

    Kodi asirikali athu bwanji ku Malawi uko mwangokhala pheeee 😂😂😂

  • @patrickndojime1632
    @patrickndojime1632 26 днів тому +1

    Koma aPrasident opuma ananenatu kuti Doom sumafayira mkamwatu ndizitu pano tubwelera ku ulamuliro wa chipani chimodzi

  • @user-gm3cx2xn9o
    @user-gm3cx2xn9o 23 дні тому

    Anthu akamatenthedwa zolankhula zake zimakhala ngati zingatheke 😂😂😂😂 mulira simunati

  • @user-je6wk8ew6g
    @user-je6wk8ew6g 26 днів тому

    Moti chikangawa yalusa sikugawanso masweet 🤣🤣🤣🤣 atimaliza

  • @MuhammadBAKILI-kl2mj
    @MuhammadBAKILI-kl2mj 26 днів тому +1

    My bsst ladio station limpopo

  • @user-bh2ei4os8w
    @user-bh2ei4os8w 26 днів тому

    Iyiyi ndiye akufuna Kenya Kenya tsopano 🏹🏹🏹