ANTHU A KU NTCHEU AMULANDILIRA MICHAEL USI CHONCHI POMWE WAFIKA KU NSEMBE YOKUMBUKIRA A CHILIMA

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 4 вер 2024

КОМЕНТАРІ • 153

  • @MarthaBanda-ye4pt
    @MarthaBanda-ye4pt Місяць тому +21

    Ambuye mulimbikitseni mwana wanu Mary Chilima akuvetsa chisoni 😭😭😭

    • @AminahMussah
      @AminahMussah Місяць тому +1

      ndipo amphwa kwambili 😭😭😭😭

    • @henrychawinga4639
      @henrychawinga4639 Місяць тому

      AMEN

    • @mphatsomonjeza4371
      @mphatsomonjeza4371 Місяць тому

      God is with her 🙏🏻

    • @user-vk2ym8ql4k
      @user-vk2ym8ql4k Місяць тому

      Ndipo ine ngati ndilire

    • @AntinHawile-rw9fj
      @AntinHawile-rw9fj Місяць тому

      kulira kosalekeza tikulira nanu mayi mary chilima km ambuye yekha ndiyemwe akuziwa kwezan maso kwa yehova ndpo zonse zizakhala bwino mama😢😢

  • @EsnartGirivin
    @EsnartGirivin Місяць тому +26

    Anthuwatu mmitima mudakali moto olo muntima mwangamu ndangoona mpando wakhala usiwo zandikumbutsa achilima moyo kuwawa😢😢

  • @gracemaluwa4674
    @gracemaluwa4674 Місяць тому +5

    Mai Kaliati pitilizani mtima wanu wabwino ,musasiye Mai Chilima okha munyengo yowawitsayi Amen

  • @NearBanda
    @NearBanda Місяць тому +18

    Mary chilima akumvetsa chisoni koma this word 😢😢😢 continue Resting well skc

    • @TamikaKaponya
      @TamikaKaponya Місяць тому +1

      Ndiponso,ine kulira kundimvetsa chisoni

  • @CharlesChilinde
    @CharlesChilinde Місяць тому +2

    Mzimu AChilima uwuse mumtedere ndi ntchito zonse anati gwirira ngati dziko.
    Koma pamwambo umenewu pali ine azikakhala ndi ine mukuwadziwa nokha Mulungu awa Kathe chifukwa Ali ndi mtima osiyana kwambiri ndi momwe AChilima amakondera anthu awo owa tsatira mu U.T.M.ngati chipani. Mulungu odziwa kusunga ndi tothoza ayang'anire Mai Mary Chilima ndi banja lonse Sa
    ❤❤❤❤❤,, 🎉🎉🎉

  • @nysonchapasuka7270
    @nysonchapasuka7270 Місяць тому +4

    May the hand of Almighty God keep on strengthening you Mary Chilima in this critical situation you are going through. We are still mourning together. We understand that SKC has created a huge gap in your life Mama and other lives too but we must look up to Jesus Christ who has a final say.

  • @Martha-m6e
    @Martha-m6e Місяць тому +9

    Mai Kaliyati pitilizani kufungatira Mary chilima.

  • @doreenkaliati3166
    @doreenkaliati3166 Місяць тому +9

    Marry kumvetsa chisoni mwana wa eni ake mayo ine😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭

    • @WilliamMasula-cb1mg
      @WilliamMasula-cb1mg Місяць тому +2

      I feel sorry for her

    • @TamikaKaponya
      @TamikaKaponya Місяць тому +1

      ​@WilliamMasula-cb1mg kwambiri tu, Dziko lapansi hmmmm

    • @fannyzimba149
      @fannyzimba149 Місяць тому

      Koma ndipo zovetsa chisoni 😭😭😭eish

  • @GladysMwantenga
    @GladysMwantenga Місяць тому +2

    Apa mpomwe nda ziwa mau aja kuti atatanthauza izi😭😭😭pochoka mzako pali malo💔 continue rest in peace DR.chilima

  • @MemoryNyirongo-gt4mn
    @MemoryNyirongo-gt4mn Місяць тому

    Palibe chobisika padziko lapasi zingabisike bwanji zidzaulilika (muuse mumtendere achilima tidzakusowani mpaka kalekale) Amen

  • @ChristinaNyirenda-zb1if
    @ChristinaNyirenda-zb1if Місяць тому +5

    Mulungu ndiwadongosolo azaziona tsiku ndilimoz

  • @TizifaBanda-xn5tm
    @TizifaBanda-xn5tm Місяць тому +1

    Mai kaliati...is the true politician and kholo.ku UTM musadzapange mistake kutaya Mai ameneyu

  • @Raph-kayRaph-kay-g5v
    @Raph-kayRaph-kay-g5v Місяць тому +6

    Koma mmene akuyang'anira patrisiayu pavuta apa

  • @MsondaBanda
    @MsondaBanda Місяць тому +1

    All of us we are still shocked and you will see someone saulting on this shameful time,it's better if you don't have something to say just keep quiet coz this is not a time to play with, this is time for the tears respect is needed

  • @stevenkambuku
    @stevenkambuku Місяць тому

    Koma imfa ya SKC mmmm I am speechless, Mhsrip

  • @DanielJuwawo
    @DanielJuwawo Місяць тому +2

    Mayi kaliati mulungu adzikudalitsan ndithu

  • @SimeonAbraham-u2j
    @SimeonAbraham-u2j Місяць тому +3

    Myambo yokumbukila SKC izichitika mochuluka mpaka Wina chikumbumtima chimuphe ndithu

  • @FanscioDancun
    @FanscioDancun Місяць тому

    This is like bringing tears again

  • @eliaskachali-xn2ve
    @eliaskachali-xn2ve Місяць тому

    Ifa ya skc ma guys ndiyo pweteka paziko la pansi. MCP is a devel goverment.Nkhalani olimba a merry chilima, Kwa ine no vote for mcp mu umoyo wanga wose

  • @JaneMoyo-ws2di
    @JaneMoyo-ws2di Місяць тому

    Corridors of justice shld prevail O, Lord. Rest in peace SKC

  • @augustMag
    @augustMag Місяць тому

    Kwa Mulungu yekha ndiye komwe tingasamire Atate zilimbisani ndikuthokoza Ambuye pukutani misizi ya abale onse amene anataya abale awo pa ngozi imeneyi ya ndege mizimu ya abalewa iunse mumtendere 😭😭😭😭😭😭

  • @rhodahjere8747
    @rhodahjere8747 Місяць тому

    Ambuye limbikisani Mary chilima dzikoli ndowawa 😭😭😭😭😭😭

  • @Fatima-db8ut
    @Fatima-db8ut Місяць тому +1

    Lord have mercy

  • @Melinavituhs-tc8ys
    @Melinavituhs-tc8ys Місяць тому

    Mary khope yake ikadali nchisoni zuchita kuoneka ngatiso alipamalilo lero mzimu wa Saulos Klaus chilima uuse mumtendere ❤️😭😭

  • @SabinaNkhoma-sf7kz
    @SabinaNkhoma-sf7kz Місяць тому +3

    Km ndizowswa kwambiri zandikhudza mary akuvetsa chisoni

  • @DolicahGift
    @DolicahGift Місяць тому

    😭😭 Ambuye pitirizani kuwusamarira mzimu wa mr chirima 😢😢😢

  • @JimmyIsaac-xd4ef
    @JimmyIsaac-xd4ef Місяць тому +1

    Manganya 😭😭 pachoka nzako pali Malo, Ambuye mwalolelanj izii?

  • @FelixBoss-yn9pe
    @FelixBoss-yn9pe Місяць тому +2

    Mmmmm mbola fanzi iyiyi ikuoneka yosasangalala

    • @maulanaallie6194
      @maulanaallie6194 Місяць тому

      Ndye asangalala bwanji mwambo wachisoni ngati umenewu nanu

  • @JaneMoyo-ws2di
    @JaneMoyo-ws2di Місяць тому +1

    Convensiion ngati ingokhala mawa iii.

  • @Adamuson
    @Adamuson Місяць тому

    Azakhari sadaname kutchura bambo a Sikono kuti ndi nkhwari.

  • @felixjoseph8161
    @felixjoseph8161 Місяць тому +1

    Manganya zoona ukumva bwanji muntima mwako pomuona nkazi wanzako akumvetsa chisoni ambuye akukhululukire sukudziwa zomwe ukuchita

    • @NatashaBema
      @NatashaBema Місяць тому

      Mfiti ilibe chisoni anwene

  • @charleskhomolina2385
    @charleskhomolina2385 Місяць тому +3

    😢😢😢Imfa yosayiwalika

  • @BlessingsTembenu
    @BlessingsTembenu Місяць тому +3

    Chifukwa chani awayika moyandikana chonchi? Kulakwa.

  • @user-do2cs8nf4b
    @user-do2cs8nf4b Місяць тому

    Koma dzikoli abale Mulungu pitilizan kuwatonthoza Mai Chilima pamodzi ndi ana awo R I P SKC😭😭

  • @DolothyMussa
    @DolothyMussa Місяць тому

    Mayi chilima mulungu akutothozeni ndipo akupaseni kulimbika mtima muzakaonana nawo mukachita bwino moyo uno muuse mu mtendele achilima misozi siyikutha kuno eshhhhh

  • @user-nj5vu8cd5l
    @user-nj5vu8cd5l Місяць тому

    Guys don't forget that no one knows when you will die, this is by only Him The Lord Almighty

  • @amoschataika7440
    @amoschataika7440 Місяць тому +1

    Yudasi izi ndizomwe umafuna kuti uzikhala pamenepo. Iwe munthu oyipa kwambiri. Nzimu wa Chilima ukukanthe kosalekeza.

  • @doreenkaliati3166
    @doreenkaliati3166 Місяць тому +3

    Rest well Mr Chilima mayo Marry wanga ine usamale ndi usi chonde ndi mfiti yayikulu iyi😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭

  • @user-eh1mg3ww6d
    @user-eh1mg3ww6d Місяць тому +1

    Akuziona ngati Ali pamwamba yudasi akamayenda akuchita kunja nja

  • @YusufIbrahim-w1g
    @YusufIbrahim-w1g Місяць тому +1

    Usi yu ndisimene ankamvuna simenesi mulungu awawone agalu amenewa

  • @vukanifracksonchinkonde7324
    @vukanifracksonchinkonde7324 Місяць тому

    If usi was not eppointed as VP.....would you people continue to say he is yudasi?
    Where the name yudasi has come from? Do not hate someone because you head from someone that he is bad.
    Usi has been with our president the late Dr SKC and we have never heardbof any disloyal.
    It's primitive life to fuel enemity for your personal gain.
    Sorry for all of you who want Usi to fall and also you want him to feel like he is hated and leave utm.when he leaves you will also talk so much nosesnse
    Be civilized guys!!!

  • @JoyceChawawa-og1cj
    @JoyceChawawa-og1cj Місяць тому

    Only Almighty God knows

  • @ChrissieGome
    @ChrissieGome Місяць тому

    Mzimu wa vice president , continue resting in peace

  • @LimbikaniChirwa
    @LimbikaniChirwa Місяць тому

    Zausilu zosezo zitayene , mnavapo wakubanja wa anthu 9 aja akuonesapo action yiliyose yokwiya ,zitayeni zimenezo mngafelezaine

  • @WestonGawaza
    @WestonGawaza Місяць тому +1

    Kupepela amugulisa mzawo mukumuyitanatso nose ndinu akupha

  • @NoelBurton-x1z
    @NoelBurton-x1z Місяць тому +2

    SKC forever ❤

  • @hopembendela
    @hopembendela Місяць тому

    Nkazi wa chilima akunvesa chisoni koma

  • @Biath-m4b
    @Biath-m4b Місяць тому

    Zimene sitimkaembekezela poti Ambuye munalola tilibe mau ife

  • @user-nj5vu8cd5l
    @user-nj5vu8cd5l Місяць тому

    Let's only pray for his soul rest in peace but don't create violence because of his death.love one another something bigger gonna come to our nation

  • @user-zm9nl8zn2b
    @user-zm9nl8zn2b Місяць тому +1

    Kodi zikatero ndiye kuti Manganya adasiya kuchita zitsuzo

  • @ziwani3682
    @ziwani3682 Місяць тому +1

    Rest in peace skc 😭😭

  • @JonathanMsiska
    @JonathanMsiska Місяць тому +1

    Koma tiuzane zoona pano Matinitedi tisiye kuvala aliyese nkhope Yake ikhale poyera.Mukazawona munthu wavala tinitedi kumaso ameyo ndi munthu oyipatsitsa.

  • @Lazarus-qo1sl
    @Lazarus-qo1sl Місяць тому

    We need your mercy our father 😢

  • @manzyhetekele8697
    @manzyhetekele8697 Місяць тому

    RIP SKC😢

  • @mphatsosadiki4983
    @mphatsosadiki4983 Місяць тому +1

    Only God knows😢

  • @cmsanyama200
    @cmsanyama200 Місяць тому +2

    Kutsutsula chilonda chosapola bwanji?

  • @tulimwalwimba6544
    @tulimwalwimba6544 Місяць тому +1

    Chilima! Eish

  • @CharityMhone-uk9ym
    @CharityMhone-uk9ym Місяць тому

    Pa ifa ya chilima manganya samaoneka lero watenga udindo akuoneka kamunthu koipa kapha mnzake chifukwa cha mpando chitsiru

  • @GodsFavourite1
    @GodsFavourite1 Місяць тому +1

    Usi amabisala mu tinted😮

  • @user-yu4np2wq4s
    @user-yu4np2wq4s Місяць тому +2

    Ausiwo kuchibwanoko Ngati apaka ufaaaa 😂😂😂😂😂😂😂

  • @abwinoamatani4921
    @abwinoamatani4921 Місяць тому

    A usi ndiopanda manyazi, kuyandikana ndi Mary

  • @GeoLikwanya-cb9gn
    @GeoLikwanya-cb9gn Місяць тому

    Imfa yosaiwalika ku fuko laMalawi 😭🇲🇼

  • @SolomonBewula
    @SolomonBewula Місяць тому

    Lero nsiku lomwe alengeze zakuchikangawa kod Komatsu alengeze basi lero ausi mmene zinayendela

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg Місяць тому

    Usi ukutaniko uko machende ako anagulisa chilima ulibe manyazi chakwera bwanji wayiopa ntcheu😂😂😂 mapwala ako

  • @JoyceBAllubi
    @JoyceBAllubi Місяць тому

    Ambuye mutonthozeni mwana wanu

  • @user-co3wr3rn4h
    @user-co3wr3rn4h Місяць тому +1

    Yudas wankulu usi kulandilidwa

  • @BornfaceMakamu
    @BornfaceMakamu Місяць тому +1

    Tagochipondan icho

  • @vitumbikomateche
    @vitumbikomateche Місяць тому

    Skc for life

  • @thomasmwitiya1447
    @thomasmwitiya1447 Місяць тому +1

    Yudas kulandiridwa

  • @mosespemba8822
    @mosespemba8822 Місяць тому +2

    Is that KABAMBE I'm seeing?

  • @user-pt8wb4vw6r
    @user-pt8wb4vw6r Місяць тому

    Maboza adpp usi wataniso alomwe inu ngati kwa simkufa ayi zikomo ndipo msasokoneze apa makomenti anu auchisiluwa mesa mwasangalala adpp kuti mavoti anu abwelele kwankhalamba yanu kuti izikapha albino

  • @UsenLashid
    @UsenLashid Місяць тому

    Bambo asikonowo musamale nawo ameneyo ndi mbulu akuoneka ngati muli limodzi Koma Ayi makendulo amuontche munthu woyipa

  • @JaneMoyo-ws2di
    @JaneMoyo-ws2di Місяць тому +1

    Yudasi. Satana kumuona akuyenda ndi miyendo. MHSRIP SKC

  • @DavieKidison
    @DavieKidison Місяць тому

    Zambili tikaziwa tikazaseka maso zinthu zamundale sizimaveseseka pakufunika mzimu wachiziwitso pamalawi anthu tisekule maso

  • @EllenNgoon-nc8vg
    @EllenNgoon-nc8vg Місяць тому +1

    😢😢 koma dziko iri

  • @SteliaKolomba
    @SteliaKolomba Місяць тому

    Ndakumbuka SKC😢😢

  • @Geraldmkwewu
    @Geraldmkwewu Місяць тому

    Manganya yudasi km ukumuwona mery mene akuwonekera agulu lnu nose ndi chikangawa Lazaro aphangaka fiti skcpitilizani kupuma mtendere

  • @AustinBanda-ee6sb
    @AustinBanda-ee6sb Місяць тому

    A Malawi anzanga kuweluzana sibwino chili chonse akudziwa ndi Yahwe kuti zinakhala bwanji ndi chilungamo chizadziwikabe pangatalike maka

  • @user-do2cs8nf4b
    @user-do2cs8nf4b Місяць тому

    Ausi mukumbva bwanji mpando mwakhalilawo zomwe mumafuna ndi zimenezo, Koma mukumbukire kuti lino ndi dziko si inu amuyaya

  • @BillyMhone-jp3kn
    @BillyMhone-jp3kn Місяць тому

    Woyeeeee mama Mary Chilima

  • @FloridaMakwinja-eq2ek
    @FloridaMakwinja-eq2ek Місяць тому

    Chisoni chandigarh
    Usi Akuma bwanji

  • @FELIXMAJAWA
    @FELIXMAJAWA Місяць тому

    anthuwa sakukondwera ndikupezeka Kwa usi mitima yawo ikuwawa ngati ineyo

  • @ChristopherChimbalanga-ez5he
    @ChristopherChimbalanga-ez5he Місяць тому

    Rest in peace SKC 😭😭😭

  • @user-nu1dj3jh7b
    @user-nu1dj3jh7b Місяць тому +3

    Tizakhala osauka ovutikitsitsa padziko lapansi chifukwa chakaganizidwe kathu , tinayenela dzinthu zikachitika tizivomeleza maso athu nkupenya kwamulungu koma osati kumalozana zala.

    • @chumasalanje4705
      @chumasalanje4705 Місяць тому

      Iwe dont say like that its clear USI is the one who plan the death of SKC

    • @GiftKumbweza
      @GiftKumbweza Місяць тому

      Ndife anthu omvetsa chisoni kwambiri.Eti in this age and era amwene

    • @user-rz9rm4cb8x
      @user-rz9rm4cb8x Місяць тому

      Mapwala ambuyako iwe

    • @temwekamlenje4358
      @temwekamlenje4358 Місяць тому

      Akanadikira kaye 40 days a Manganyawo bola kuti alemekeza Mzimu wa anzao udindowo pambuyo.

  • @aafrogarrix
    @aafrogarrix Місяць тому

    KOd uku zimachitikila kutiko

  • @TwalikiWisiki
    @TwalikiWisiki Місяць тому

    Marry maso ndi maso ndi mfiti yomwe idagulitsa mwazi mwamuna wake Ku MCP in exchange for His position,,Marry you are a strong woman trust I wouldn't afford to see USi face to face

    • @mcsellahntv6896
      @mcsellahntv6896 Місяць тому

      Me , I would forget ndine namalira, I could freak out.

  • @AnusaNkhoma
    @AnusaNkhoma Місяць тому

    Mmmmmm😢😢

  • @JaneMasikini
    @JaneMasikini Місяць тому

    Ma comment ali apa eee mphawi kuchulutsa zochita matukutuku aeni ake akubanja azisiya zonse mmanja mwa mulungu koma wina busy kumuloza chala munthu eishh

  • @PatrickViyache
    @PatrickViyache Місяць тому +1

    Dzimu wanu ukawutse muntendele skc❤❤❤❤

  • @user-hh4wn4vf9e
    @user-hh4wn4vf9e Місяць тому +1

    😭😭😭

  • @MisheckAselo
    @MisheckAselo Місяць тому

    Eee koma anthu kumuyang'ana kwakeko yudas 😂

  • @johnkatapeh7182
    @johnkatapeh7182 Місяць тому

    RIP SKC

  • @nishanchiwaya4561
    @nishanchiwaya4561 Місяць тому +2

    Macomentiwo oonesa kuti amalawi mwatopa ndi ulemu😅😅😅😅

  • @RichardKuden
    @RichardKuden Місяць тому

    Dziko ndilovuta ndithu😂😂😂😂😂

  • @chirwaellace1093
    @chirwaellace1093 Місяць тому

    Zakeyu alikonso kodi? Mthira kuwiri yudas

  • @DKMWALE-ew3lp
    @DKMWALE-ew3lp Місяць тому +1

    Tuonela mwachidw

  • @SalaJawali
    @SalaJawali Місяць тому

    Kodi awa alibe akazi awo mene a kumayenda okhamo

  • @user-hx6jl2jq9j
    @user-hx6jl2jq9j Місяць тому

    Nkhalani ntcheru ndi usi uyo ndi fiti

  • @georgeraphael8198
    @georgeraphael8198 Місяць тому

    Mwapeza zonena eeeeee😅😅😅😅😅😅

  • @CamlonLogistics-ju6mb
    @CamlonLogistics-ju6mb Місяць тому

    Mary chilima akufunika mapemphelo

    • @BlessingsTembenu
      @BlessingsTembenu Місяць тому

      Ameneyu anayenera naye kumamupempherela coz Ali munyengo yovuta heavy