Speaking on air like this shows that u r a courageous and cool guy, if I have power like u I could have make something strange in this 🇲🇼straight bcz I feel very pain and Huttered
Ulemu wanu bwana Kalindo. Zonse mwakamba ndi zoona kuti Chakwera apakile adzipita kwawo pamafunika mai Mary Chilima atengepo mbali pa ndale pokhala President wa UTM 🎉🎉🎉🎉🎉🎉
Ife tufuna mai chilima basi. Mai kaliati chonde you are good as the SG or CEO of the party. If you loved Chilima as your boss, please give the G-Z, including all the women, the totality of their moral to vote for change. Dr Mtumbuka, Dr Kabambe, Madam Kaliati and the campaign director including UDF, AFORD, DPP, PP should immediately create an inner circle to help her complain and win the election in 2025. Chonde chonde the G-Z are waiting patiently. We pray for you Bwana THE DC.
Amen akuti mary asayimire ndi azipani za mcp ,,,mary ayimire abale ateteze chuma cha mwamuna wake alimbe mtima basi mulungu yekha ndiyemwe amupatse mphavu, A mcp inu mukudziwa kuti kungoima mary chanu palibe
Mbewu imayambila ku nazale Bon Kalindo ndiye mmodzi yemwe anamupusisa Chilima kuchoka ku DPP kupita ku MCP lelo ifa ya Chilima wapezelapo mtaju wopangilapo business ndipo a Malawi timango pusisidwa zili zonse taiwala kuti Kalindo ndiyemwe anayenda maliseche mu nthawi ya DPP.
Kalindo analowak liti ku MCP ??? Mesa anali limodzi ndi chilimayo mmene amapanga alliance later on mpomwe amadzalengeza kt watulukak nde iwe ukukamba ziti??? Kmaso ngt anamupusisa chilima bola kusiyana mkumuchotsa moyo ngt mmene achitira a MCP
Kulibe olungama akulu, ziri ngati chipulumutso chathu. Odala omwe avomereza machimo awo ndikulapa. Atleast atawona kuipa kwa MCP anamuchenjeza, zinangovuta kuti adamukhulupirira Chakwera mudzina loti ndi m'busa plus new blood in politics. He did not know kusadziwa ndale kwa Chakwera did not mean he is not evil 😢
the DC makina achilungamo koma chikangawa mapaziake kwambili msiyeni masiku amatha ndikugona chikangawa ine ndikanakhala ndiphavu ine ndikanapita kumeneko kukamupha
Okay ngati ndi chincho woyamba kumupha ndiwe mwakondwa poti kulibe chilimayo mukhaulabe anthu opusa inu kumukonda munthu atafa koma umamunena ndiwe satana ndi azakowo shame unto you opposition
Speaking on air like this shows that u r a courageous and cool guy, if I have power like u I could have make something strange in this 🇲🇼straight bcz I feel very pain and Huttered
Always, chulungamo chimapweteka. YUDAS adamupeleka YESU chifukwa cha chulungamo
Ulemu wanu bwana Kalindo. Zonse mwakamba ndi zoona kuti Chakwera apakile adzipita kwawo pamafunika mai Mary Chilima atengepo mbali pa ndale pokhala President wa UTM 🎉🎉🎉🎉🎉🎉
auze ave ine chakwela akundinyasa akutionjeza kupha anthu ngati akupha nkhuku ngati ana wamake Malawi ngati ya kunyumba yakwawo
Ife tufuna mai chilima basi. Mai kaliati chonde you are good as the SG or CEO of the party. If you loved Chilima as your boss, please give the G-Z, including all the women, the totality of their moral to vote for change. Dr Mtumbuka, Dr Kabambe, Madam Kaliati and the campaign director including UDF, AFORD, DPP, PP should immediately create an inner circle to help her complain and win the election in 2025. Chonde chonde the G-Z are waiting patiently. We pray for you Bwana THE DC.
Zoimila mary chilimazi ndie zopusa, let her mourn it's too early. Utm was not formed as a family party.
Thus true, personally I agree with you. Let her mourn her late husband peacefully.
Amen akuti mary asayimire ndi azipani za mcp ,,,mary ayimire abale ateteze chuma cha mwamuna wake alimbe mtima basi mulungu yekha ndiyemwe amupatse mphavu, A mcp inu mukudziwa kuti kungoima mary chanu palibe
Mbewu imayambila ku nazale
Bon Kalindo ndiye mmodzi yemwe anamupusisa Chilima kuchoka ku DPP kupita ku MCP lelo ifa ya Chilima wapezelapo mtaju wopangilapo business ndipo a Malawi timango pusisidwa zili zonse taiwala kuti Kalindo ndiyemwe anayenda maliseche mu nthawi ya DPP.
Kalindo analowak liti ku MCP ??? Mesa anali limodzi ndi chilimayo mmene amapanga alliance later on mpomwe amadzalengeza kt watulukak nde iwe ukukamba ziti??? Kmaso ngt anamupusisa chilima bola kusiyana mkumuchotsa moyo ngt mmene achitira a MCP
@@MzadziWanga pamene ankapita ku MCP anali mwana mbiri ya Gadama samaiziwa zoti kunali Solobala samaziwa ndimaesa ndi Chilima yemwe ankatiuza kuti chisakho cha 2014 Iye ndi amene anagwira ntchito kuti MCP iluze anaiwala?
Kulibe olungama akulu, ziri ngati chipulumutso chathu. Odala omwe avomereza machimo awo ndikulapa. Atleast atawona kuipa kwa MCP anamuchenjeza, zinangovuta kuti adamukhulupirira Chakwera mudzina loti ndi m'busa plus new blood in politics. He did not know kusadziwa ndale kwa Chakwera did not mean he is not evil 😢
the DC makina achilungamo koma chikangawa mapaziake kwambili msiyeni masiku amatha ndikugona chikangawa ine ndikanakhala ndiphavu ine ndikanapita kumeneko kukamupha
We like pple you born kalindo
Koma dzikolino silolamula azimayi Ayi Moti mgwirizano umenewu atatsogolela ameneyuyu ndiyekuti utha kudzakhala ofoka koma Peter Basi
Mnthu wankulu Bon Kalindoo tsopano 🔥🔥
NGATI IMAKANIKA GALIMOTO KULIRA MULIBEMO BATTERY KULIBWANJI NDEGE???? NANGA NDEGEYO IMAGWIRA BWANJI NTCHITO ILIBE ZIPANGIZO ZOKWANIRA???? ALL CONCERNED CITIZENS MUST RESIGN😢😢😢😢😢
Bwana kalindo ipatseni motoo kt buuu
Mary chilima my vote
Mumakwana Mr bon kalindo
Chilungamo chofunika ulemu wanu bwana ✊✊ Bon Kalindo🔥🔥✊
Bwana DS mulungu azikudalisani mukuyesesa kutimenyela ufulu oziwa zobisika
Takondwera kuyikapo mlomo a DC chifukwa sitinakuven
😂😂😂😂😂bon kalindo moto buuuu
Ndipo mai Chilima alimbe mtima alitenge dzikoli
Ndipo rinari read kukavota Mary akuyenera kuzuka bas
Mary Chilima oyeeeee!!
2025 boma
I'm following you Mr Born
From RSA enough is enough tell them
Koma ineyo ndikhare mburi .paja galimoto ya manual ngati iribe battery timakakha ndiye ndegeyo amaikakha .ndichoseni umburi .
😂😂😂 koma DC umaimilira open our door to move forward
Zinazo ndizabwino koma osampasaso dzikoli mkazi kulamulira
BWANA KALINDO ZIMENEZIJA ANACHITA KUKONZA CHAKWERA NDI NDUNA ZAKE.ZOSATHEKA KUTI MUNDEGE MUJA MUNALIBE ZIPANGIZO IYEYO AMAKWERA BWANJI YOPANDA ZIPANGIZO ? INALIBE ZIPANGIZO CHIFUKWA CHOTI ANAKWERA NDI CHIRIMA ? ZOONADI A MALAWI TINANYANYA KUFATSA AKANAKHALA MAIKO ENA UYU CHIKANGAWAYU ATACHOTSEDWA KALE PA MPANDO NDI AFITI ANZAKE A MALAWI KUZOLOWERA KUZUNZIDWA BASI
Awachotsa bwanji athu ena iyenso Ali momwemo
The dc king
Ambiri tichikhala olimba m'tima ngati Bon kalindo bwezi andalewa titawanyenya koma tili ndi mantha Amalawi
Koma pa marry chilimapo mmmm no
ngati sunakhwime sungabwele pa air like that 😂😂😂
Koma pa Mary pokhapo ine sindimavomereza, nzeru za chilima sizingakhale za Mary
Kd za mademo zili pat bwan😢....ifet tikudkil tithese mkwiyo
kalindo amatiyimilira... 🔥
The DC ❤❤❤❤❤
Booon Kalindo the DC
Ine ndagwirizana nazo Mery chilima yemweyo 🥳🥳🥳🥳
We like you. The DC ❤❤❤❤
zoona Malawi ndi dziko lomvetsa chisoni kwambiri koma anthu akuvutika
Long live Mr Bon kalindo, the pangolin❤❤
The DC ❤
Kalindo ndi mpulumutsi ndi tsogolo la Malawi
Meryl ekhayo ndi ayi zikhoza kulowa chibwana
Always listening ur truth boss 🙌 ❤🎉
Yes, Mary is a joke plus others.
Takambanikoni za neef abwana anthutu Ayamba kulandidwa Malo komaso Ndi chakudya mmakukamu
Zoonadi chilungamo chimapweteka
Malawi ndiosamufeladi😢
❤❤❤❤🙏👍👍
Mr president kalindo
Kkkkkkk mumakwana bon kalindo the DC
I hope Malawi will not change coz what i know it's dat, the Malawian they just like money.
Kunkuyu adauza a malawi anati black box adayisunga Malo a safe.kodi black box yomwe kunkuyu akanena KUTI adayisunga ndiyitiyo?
We like you The DC ❤❤❤
Till pambuyo panu Adc
Okay ngati ndi chincho woyamba kumupha ndiwe mwakondwa poti kulibe chilimayo mukhaulabe anthu opusa inu kumukonda munthu atafa koma umamunena ndiwe satana ndi azakowo shame unto you opposition
Akakhala pa nkhate sapheka nkhani iyiyi ikukhunza asogoleli athu omwewo and tinawalemba .ntchito ndife kusonyeza Kuti tikuyenelaso kuwachosapo ndife finish Kuti tizingoyankhula sizitithandizayi Koma tikuyenela kupanga action
Iiiii koma azimai akakulaso mphamvu pena ai , even m'mene amapangila gotani hala , kaliati , Jessie kabwila vela kantukule azimai amenewa ine ndimakhulupilira kuti ulemu umene amawapasa amuna awo si wen wen why ndi azimai okula ntima osafuna kuzichepesa ndie pena azimaiwa aaah enawa sandipasa chilimbikiso kuti nkuwaika pamwamba ife nkumaembekeza kusinthadi eeh osatheka amalowa ufiti onyanyila ndipamene uzaziwe kuti akulu akale akamati mfiti yaikazi si-khululuka umaonela pamenepa kuti m'zoona .
Mumpangitsa Mary kuyamba zokhima sanga khale pa mpando asana tsazike Mpando umeneu Athu Amalodzana
Iyeyu chotchinga chake chinali Chilima yemweyu ndipo anamupha basi.
Pa Mary apo ayi mumuphesa mwana wa Eni ake
Anthaso kumupha merry chilima,,angozisiya
Fire 🔥 🔥🔥 man kkkkkkk
Iwe ndi galu kwambr mesa ndinu nomwe mumati ndege idachita kukoledwa ndi ndege inzake mmwambamo ma battery ako ase
Nbusa ujatu lelo ndi kambuku pano akungo endaenda ngati Wamisala
Kkkkkkkkkk😂😂 mbava chakwera
The nyonyolido mumakwana mumatiimirira
The Mr DC❤❤❤
That’s true their just making business
Awuzen agaluwa azinva
Aboma akuziwa chilichotse
😢
Thanks bro ❤
The bc
Nkhaniyo ndioona coz awa amkat tinawauza asatere apa asinthaso kt samalumikizana chinyengo
Dc❤❤❤😂
May God bless u l thinks its G0d who sent you to fight for the malawians continue
The DC
Zophatikizana tinaesa kale 😅
aboma pantumbo pawo ose
🤣🤣 ana akuzuka.
Misheck
Ndipo ife ndiogona ndithu
Chifyenthe kodi
Koka2 uyu ndiopweteketsa mtima
The b c
😂
😂😂😂
Ulichitesi iwe zindele zimakuvela
Iwe ka sound kali pasipo osamayika ayi zapamtumbo zimenezo ife zopusa ayi tikuyenda okwiya kwiya
😅😅😅
Ppppppp
Mary chilima my vote
We like you. The DC ❤❤❤❤
Misheck