Yudas Iscaritots cannot be taken seriously. I am waiting for the convention. If this guy will be endorsed that will be my last day as a UTM member and am going back to DPP.
Dr Usi must be aware of what he is doing, ili ndi Dziko. Akapanga masewela awa ndi mathero ake. Ayenela kudzukuta Mmene. Chililima ankamusankhila U VP. Uyu thembelero limupeza Akapanga masewela.
Anthu amene akumunena Michael usi alibe nzeru ndichifukwa chake tizivutika nthawi zonse, tili busy kuyankhula za imfa ya chilima kumutenga chilima innocent pamene chilima anali gulu la chakwera remember the birds of same feathers flock together, chilima was not innocent, the president that was innocent and was killed by the citizens of Malawi was bingu wamutharika, alipo mwa inu amene akumukumbuka bingu pa zabwino zonse zimene anachita??? After that inu amalawi munapanga chani bingu wa mtharika?? Lero muli busy kutukwana chakwera amene munamulowesa nokha kumuchosa Peter mwa chipongwe do you think malawians will go unpublished, mzimu omwe wakwiya ndi wa bingu not chilima and if you are not careful chakwera akhala mpaka 2030 just for your punishment chifukwa sindikuwona wanzeru mwa onse omwe akuzitcha omenyera ufulu. Truth is bitter koma ndakuuzani chilungamo sinthani khalidwe amalawi, dziko lathu tikuliwononga tokha chifuwa cha dyera ndi kusaganiza
A president akowo ngongole yo nthawi yonseyi saamapeleka bwanj? Nde mwakambilana lelo fukwa iweyo wabwela pampandopo? Is tht what u want to tell us? Hmmmmmm ayi ndthu may SKC’s soul keep resting in peace😢
Zikakhala ndalamazo tilandila nawoo koma Micheal usi ndi Chakwela mukagwere tsitikumvotelani malawi wake sii waleroyi ayi, wagwa nayo iwe galu wamuthu iwe
Watha ameneyo mphamvu zake zatha pamene skc adalowa manda,chilegwalegwa kapeta ngongole last minute,njara chani? Mfiti chedza ndizitsiru zizako koma for ma y nod z not bc,udampeleka dzako iwe woyipa kobasi ine nditenga nawo koma vote yanga nyooo
KOMA USI PAMATAKO PAKO WAVA ,KODI ANTHU ALI APA NDI A UTM UKUFUNA UTANI NAO KOD ,PALIBEPO WA MCP APA AI KODI USI ULI KU UTM MWINA KU MCP UFATU IWEYO NDI NDALE ZAKO ZOPUSAZO
Ine kuno ku Ntcheu ndinalandira kale 1M yangongole koma sindibweza chifukwa ndadya Misonkho yanga iyaaa!! ndipo ndapangitsa kale passport Next month ulendo wa ku Capetown Ukandipezera kuti Manganya
Kavutikeni adhara ....kukhale kunyadira kumeneko south to.....pitani UK or tipezeni Ku USA kuno 😂😂😂😂😂😂 anthu koma ...you are pathetic my guy better ukanayamba business ndikubweza you could get opportunity yoti uzatenge ndalama yambili
I have liked the speech of the VP. Whoever is against him has his own challenges but I stand to watch his speech. God is our true judge.
Uyu sanachenjere bwino wafa chilima iye anali phee mbuyomu chadza ndiyani a usi tsopano .
Ndipo ndizowonadi
Mmafuna atani Chilima alipo?@@GospelSoldiers-sr7np
Ndipo inu mmmm
16:43 16:45
Michael usi Muthu oipa kwambiri. Ukanaziwa kuti maloto anga sanaphelezele sibwenzi ukupanga zimenezi. Koma Mulungu akulanga pa zomwe ukuchitazi
Walakwanji Michael
mulungu akulange iwe munthu opada chinsoni.
Ndalama yavuta odi ndilandile ngongole yosabweza ine komaso kulavotera chipani chakumtima kwanga😂😂😂
Ngongole yopelekedwa last time koma yudasi
Convention ija ikufunika ndipo ichitike mwachangu😂😂 awawa apite ku MCP 😂😂
Usachita sanje musiyen agwire ntchito ya dziko jealous down please
Changu changu kaya akalowera pati
Chofunika kulandila ndalamazo koma osavotela
😂😂😂ndalamazo atipatse
100percent
Upresident ukukuyenera bwana usi
Yudas Iscaritots cannot be taken seriously. I am waiting for the convention. If this guy will be endorsed that will be my last day as a UTM member and am going back to DPP.
Then ndiwe wa DPP aise 😂
Osangopita ku DPP ko lero lomwe bwa
Manganya ndi kapolo wachakwera
This mn will bring change in this world , reason he knows how to deal with poor people , belive me , lets just give him chance
😂😂😂😂😂😂😂😂😂 Are you sure 😂😂😂😂😂?
U don't think in your mind
Ine munthu uyu ndinkonda kwambiri... osamalankhula ngat kulibe mawa...usi ndi munthu amene amalankhula akudziwa kt kuli mawa....❤❤❤❤❤❤ Powerful vp....more ❤❤❤❤❤❤
Choka apa ndiwe galu 🐕🐕🐕kwabasi tamuoneleni ndevu zake bodza ukunenali Zachison Kupemtaso ndevu ngt malemu Chilima mmm zachison 😂😂😂😂😂
awa tawathamangiseni achisiru
Km usi nkanakudziwa komwe ukhra nkanabwera kudzakithokoza pokhapa ......nzakutha izi....aliyese adzafika pando wakuweluza...powerful
Ndipo akydziwa
Madhala Usi 😂🔥🔥🔥 inu ndi one bwana
Pola pola ngati ukujabura
So interesting. Why kuyitanira ngongole lero? Kudya katatu lero after 4 years? Ayi sankiyu
Mulungu alemekeze potipatsa S VP Dr Usi.wodzichepetsa
Koma iwe manganya ambuye akuone zedi ufiti ulipo MO ndithu
Koma musamayiwale Mr Don't trust Malawian alingat mbuzi sachedwakuiwala manganya wagundika kuwabwatika muzamukumbukila ntanyiwa ndi Mr Don't trust pa Limpopo FM
Idont blame this guy I blame pple who crap fr him shame
Mumakwana big Mr vp
Anthu mukuputsitsidwa heavy😂😂
Ngongole akatenga kodi awagule ndani umphawi ngati umenewo anthu akufuna ndi njala bwerani ku Nsanje mudzawone mene akuvutika minda yawo madzi okha okha
Uyuyu ndi wanzeru koma wafika nthawi yovuta koma mwa iyeyu muli utsogoleli kuposa enawa
Michael Usi pamodzi ndi agalu amzako a MCP Tamvani idzi" . Inuyo pakadali panopa palibe chomwe mungatichitire a MALAWI ife kuti Tiyiware dza momwe munamuphera CHILIMA Pamodzi ndi An'thu 8 womwe munawapha ngati Njoka aja, . Anthu woyipa wopanda manyazi, Wopanda chisoni , Wopanda umun'thu ..
Mutu ngati ngwime (bwampini)Mcheal usi umandinyansa heavy
Bwanaaa tabwerani kuno ku immigration mudzamuone uyuuuu! Akupanga mwanotu uyuuuu kuno. Tabwerani muli mu Blantyre mommuno.
Zoona kumaombera m'manji zimenezi koma abale munthu zatheka ndithu
Ndipo abale zachison 😢
Munthu sungamazichemelele kuti ine ndimaziwa kupempha, umenewo ndiye uchitsiru.
Inenso I'm feeling uncomfortable with that words ,mpakana kumadzichemelera ndikupepha
😂😂😂😂😂 zaziii ndiye chikukukochanu chonamiza anthu kuti muwapasandarama zangongore zaziii zenizeni kupotoife sikufuna ayi iwe usi kagaru iwe
Chikangawa iwe munthu oyipa iwe
anati saziyankha ngati KSC koma akupanga zotsutsana ndizomwe ananena, munthu oipa
Dr Usi must be aware of what he is doing, ili ndi Dziko. Akapanga masewela awa ndi mathero ake.
Ayenela kudzukuta Mmene. Chililima ankamusankhila U VP. Uyu thembelero limupeza Akapanga masewela.
Ndipu ameneyo ngati Akutuluka muchipani cha UTM mlungu amulange
Kampeniyoooo munali kt nthawi Yoseyi osatipatsa ngongoleyo munyaaa
NGONGOLE YA FERTILIZEEEEEEEEEEEEER MWABWEZAAAA
Gwape oipa chikangawa party
Mache... Ake tikumufuna ndichakwelayo tizamugendeee
Madzi achita katondo, manganya ukudziwapo kathu za ifa ya Chilima
Ngongole ndi imeneyo koma anthu wo business yake iti ndi m'mene ndlama ya Malawi iliri panomu nde adziwinapo chani
Palibe chomwe anganene chifukwa mwini wake panalibe zomwe ankanena, ndiye apapa Dr Usi walakwa chiyani,Ndipo akunena zoona kuti pakhale kugwilizana onse azipsni zimenezo ndiye zofunika
Kazitape Ngati iwe
Munthu oipa iwe usi ngati chikangawa choka.rip my president skc
😮😊 ndipo mu ofesi anthu akuwonjeza zoona tizivutika ngati misokho simaperekedwa... Tamayendaniso ma company muziwona momwe maliporo akukharira.
Munthu amene angachenje ziko lino ndi mozi yekha basi bhon kalindo president wa anthu awuphawi..manganya alibe phavu becoz Ali pasi pachakwela ...
everyday basi nkhani izikhala yokuti "ndinkavala makabudula awiri, thako nkumaonekela" basi? awa ndiye phala lenileni. AChilima mudatisiyilanji?
Uyu akupanga Za chipani chake cha odya zake
Akut abwana ngt wina anapereka abwana ake inu sazakuperekan???wina akuziona ngt dolo km dkila tsku lako likubwera 😂😂❤
Koma Fada katundu wakwiratu kongolero mukunama kwambiri musuzitsa anthu.
Mndiyakhe ndani president wa UTM now
Zikutathauzanji zimenezo abale
Koma amalawi sitizaphunzila munthu uyu mkamwa mwake palibe fundo
You have too late,usi unali kuti nthawi yonseyi and I have no time to give u my vote Mr chikangawa
Galu iwe tizingokhalira kumva za matako akowo, pereka ndalamayo koma vote yako kulibe
Et chilima pot wandiuza zonse mowe tingapangile campain then ndimuphe ine ndzapanga zimene wandiuzazo😆😆😆galu kwabas 😂ndevu szinali choncho🤣🤣
Zooona usi. Auzeeee kt mau alionse ankamwa mwawo amene Ali olipa Mulungu adzawerengera mulandu....tsiku Lina adzaweluzidwa.
Zigawenga inu MCP ndichipaninso?
Mbuzi yaimuna phongo usi
Kkkkkkkkk koma ati ali ndi ukadaulo opempha maiko akuja (masikini wamkulu)😂😂😂😂
MCP yabisala mwamanganya kt atonthoze anthu akhale bata pa zokwiya za SKC
Fundo imodzi imodzi kulionse angapite mmmmmmm😢😢😢😢
Usi ndichitsiru cha MCP. Wapanga chani iweyo gwape? Tikaonana ku convention
Chadza ndi yani a Usi. SKC wamwalira lero busy. Mmmmmmmmh. Njawala sakunama" mkango ukafa fisi sangalere ana"
Yunda sikalioti chikangawa party
Akubw inu mukugura mavote panyopanu
Eya tipaseni ngongoleyo kkk
Anthu amene akumunena Michael usi alibe nzeru ndichifukwa chake tizivutika nthawi zonse, tili busy kuyankhula za imfa ya chilima kumutenga chilima innocent pamene chilima anali gulu la chakwera remember the birds of same feathers flock together, chilima was not innocent, the president that was innocent and was killed by the citizens of Malawi was bingu wamutharika, alipo mwa inu amene akumukumbuka bingu pa zabwino zonse zimene anachita??? After that inu amalawi munapanga chani bingu wa mtharika?? Lero muli busy kutukwana chakwera amene munamulowesa nokha kumuchosa Peter mwa chipongwe do you think malawians will go unpublished, mzimu omwe wakwiya ndi wa bingu not chilima and if you are not careful chakwera akhala mpaka 2030 just for your punishment chifukwa sindikuwona wanzeru mwa onse omwe akuzitcha omenyera ufulu. Truth is bitter koma ndakuuzani chilungamo sinthani khalidwe amalawi, dziko lathu tikuliwononga tokha chifuwa cha dyera ndi kusaganiza
Tachokani apa kodi iwe uyimira pati dikira tione convention ukagwa ngati atakulabade tiona uzasowa mtendere my friend Chima chopanda Zimu woyera sichikoma olo aturo oil kutota njeeee
Tambwali weni weni manganya
Pitizani masewero osati vp simukukwana
Uku mwangogwelako koma siphatso yanu, inu koma ma drama mumatha. Munalemela kale koma kusakhutisidwa. Zinazi umangoona wadziputa😮
Malawian are malawian indeed😂😂😂😂😂😂😂😂😂
Manganya mwanama zaka 4 ambuyanuwo apangachani
A president akowo ngongole yo nthawi yonseyi saamapeleka bwanj?
Nde mwakambilana lelo fukwa iweyo wabwela pampandopo?
Is tht what u want to tell us? Hmmmmmm ayi ndthu may SKC’s soul keep resting in peace😢
Mugendeni ndi miyala
Anamizana ndi chakwera wakeyo,Need siyochiitira Campaign
Zikakhala ndalamazo tilandila nawoo koma Micheal usi ndi Chakwela mukagwere tsitikumvotelani malawi wake sii waleroyi ayi, wagwa nayo iwe galu wamuthu iwe
Aaah koma umphawi sizithu mmmm 😢
Mu misonkhanoyi ndikuona kuti anthu angopemyesesa chetee okuwa ndi ochepa zeedi. Cheteyu kaya anthuwa akuganiza chani?
Watha ameneyo mphamvu zake zatha pamene skc adalowa manda,chilegwalegwa kapeta ngongole last minute,njara chani? Mfiti chedza ndizitsiru zizako koma for ma y nod z not bc,udampeleka dzako iwe woyipa kobasi ine nditenga nawo koma vote yanga nyooo
Kodi gogile zopanda chikole anthu azipasindwa thawi yakampen yokha ?
Mfiti yaikulu iwe garu
KOMA USI PAMATAKO PAKO WAVA ,KODI ANTHU ALI APA NDI A UTM UKUFUNA UTANI NAO KOD ,PALIBEPO WA MCP APA AI KODI USI ULI KU UTM MWINA KU MCP UFATU IWEYO NDI NDALE ZAKO ZOPUSAZO
anakakhala wa UTM original bwezi pamenepo Pali kaliyati achina njawala koma apo Ali ndi chakwela awiri
100%
Ife sitifuna chipani simaphika ayi koma.chitukuko
Anthu landilani ngongole koma vote ku mtima
Mugenden ameneyo mbuzii yamuthu
Palibe kubweza ndalama Zimenezo, Inu zomwe mukupakulazo muzabweza?
Kudya katatu ko nde munene lero mmmmm kale lonseli munali kuti? Kufuna kuononga utm uku 😊
Nthawi yatha kale dzisintha liti iwe galu khobasi
Yudasi mfiti unathandizila chakwela kumapha chilima
Ngongole mpakana liti chitsiru iwe usatinyatsepo eti tibwezera nchani ngongolezo ngat tili ndi business yolongosoka galu iwe
uyu ndimpera kuwiri. Tisamale naye amalawi satigulitsa ku MCP.
Usi nda chakwera ndapao midzu yakachere akumana pasi
Asaaah mbuzi eti umphawi ndi njala ya mmalawi mwauona lero?👹👿😈👽💀
Hmmmm usamachule dzina la mulungu pachabe ndiwe yudasidi a2 sakukunamizira
Uphawi kachitsiludi et🤣🤣🤣
Kodi mwayamba kugwila ntchito ku neef?
Aaaaaa koma ndale eeee dziko ili ngongole ndikupempha kwa azungu basi.
Malawian don't trust this man he is not capable of changing Malawi their is no readership in him
Ine kuno ku Ntcheu ndinalandira kale 1M yangongole koma sindibweza chifukwa ndadya Misonkho yanga iyaaa!! ndipo ndapangitsa kale passport Next month ulendo wa ku Capetown Ukandipezera kuti Manganya
Kavutikeni adhara ....kukhale kunyadira kumeneko south to.....pitani UK or tipezeni Ku USA kuno 😂😂😂😂😂😂 anthu koma ...you are pathetic my guy better ukanayamba business ndikubweza you could get opportunity yoti uzatenge ndalama yambili
A usi si wandale koma akutsiluza nthawi ya chilima mudzamuona akupita ku tikufelanji uyu
Ndipo anthu Ife tichejere ndithu asatinamize thawi yotha yithayi NDI ngongole Kuti tazavoter ayi ndarama Zo tilandire Koma osayiwala m,fiti NDI m,fiti sangasithe kukhala wabwino
Ine nakopekakare mcp bas