A Michael Usi Inu Si A UTM - Lyton Mangochi

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 3 лют 2025

КОМЕНТАРІ • 268

  • @BrightZionga
    @BrightZionga 6 місяців тому +31

    Iwe mangochi umandibowa pazambiri koma leroli wakamba chilungamo ❤❤ the spirit

  • @shadreckphiri1799
    @shadreckphiri1799 6 місяців тому +11

    This is straight forward talk and advice

  • @MEGANABIGAILMNTHALI
    @MEGANABIGAILMNTHALI 6 місяців тому +8

    Munthuyu nthawi zina amalankhula zoduka mutu koma lelo walankhula chilungamo ndakukonda Mr mango hi for this audio.

  • @mayesojameskatete
    @mayesojameskatete 6 місяців тому +29

    Galu ndi gula manganya siwa utm komaso anamupeleka chilima

  • @ChristopherJohn-z5z
    @ChristopherJohn-z5z 6 місяців тому +4

    Apapa ndiri mbariyako or mntaniwa atanva audio yakoyi akunva kukoma mot utamatero anthu akukonda kwambiri the fact u hv say to day congrats Mr Layton big up tufuna chirungamo choncho

  • @RitaKainga
    @RitaKainga 6 місяців тому +1

    Mwayankhula chilungamo malumee,May God bless you!!! Ameneyu adzazunzika nao mzimu wa Chilima

  • @AiwaMedia-sh6vx
    @AiwaMedia-sh6vx 6 місяців тому +1

    Iwe Lyton Mangochi apa wanena mfundo osati yamasewera. Ndamvera each and every sentence looking for a mistake koma mwalankhula zaufumu weniweni.
    I love you

  • @doreenkaliati3166
    @doreenkaliati3166 6 місяців тому +1

    Nkhani iyi ya Straight forward 🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌 ulemu wanu uku kulakhura mwabnzeru manganya or tsiku limodzi lopedzeka pa mwambo oyasa ma candle yoooo or tsiku loyakhulapo zokhudza imfa ya chilimba mmmmm Ambuye akukhululukireni iwe ndi mpeni othwa konse konse iiiih Chilima Rest well tidzakulirani mpaka kale 😭😭😭😭😭😭

  • @SolomonMbewe
    @SolomonMbewe 6 місяців тому +2

    I think you are coming back to your senses Mr Mangochi.... Keep it up.

  • @masterchitabwino898
    @masterchitabwino898 6 місяців тому +1

    Well composed speech keep it up Mr Mangochi. Teach him a lesson

  • @peternashyo9850
    @peternashyo9850 6 місяців тому +11

    Uthenga opanda chigamba, apa ndiye chilungamo.

  • @StevenGJohn
    @StevenGJohn 6 місяців тому +1

    Mr Lyton Mangochi ulemu wanu mwayankhula chilungamo God bless you Mr Mangochi

  • @PollyLysonLutepo
    @PollyLysonLutepo 6 місяців тому +1

    100%. Usi si wa UTM. Angofuna kusokoneza UTM yo.
    Tilitonse mau olawura asiye.
    Ngati zolankhura alibe angosiya. zamadirama ife sitikufuna.
    Ine ndili wakwanu. Kumwitu koku Karonga. Komam'sasiye kudziwitsa anthu choonadi, monga m'nachitira pakatipa.
    Tinali kuganiza kuti nanutso mwagudwa.

  • @DONNEXKhama-bk1gy
    @DONNEXKhama-bk1gy 6 місяців тому +10

    Ine umandinyasa heavy kma lero Mutu wako wayamba kugwila ntchito ❤zanzeru
    Someone hit Like for me

  • @PartLupiya
    @PartLupiya 6 місяців тому +1

    Lero wayankhula mwanzelutu a bro, more fire 🔥

  • @ZebronTembo-u6p
    @ZebronTembo-u6p 6 місяців тому +1

    Mqngochi your right ukunena zenizeni congratulations bro

  • @MadalisoKaujole
    @MadalisoKaujole 6 місяців тому +7

    Bwana Lyton mangochi lero mwakambako mfundo zomveka bwino ulemu wanu

  • @lastonmasoatenganji-bs5gf
    @lastonmasoatenganji-bs5gf 6 місяців тому +4

    Madala madala tsopano, munasowatu😁💗💗

  • @SamangaMushe
    @SamangaMushe 6 місяців тому

    Today it's ur best audio mr mangoch best audio ever muuzenidi achose kachiwanda ka ma drama kkkk

  • @petertaulo8014
    @petertaulo8014 6 місяців тому +1

    Mwanena zoona Mr Mangochi. Manganya akufuna Kuba Chipani!

  • @masterchitabwino898
    @masterchitabwino898 6 місяців тому +1

    Anali ngati Petro yemwe amamuonera Yesu patali ali pakati pa adani kumfunsa uyunso anali waiwo amvereke akunama sindikumudziwa ine ameneyo.

  • @alexsumani6823
    @alexsumani6823 6 місяців тому +8

    Ndipo bwana Mangochi mwang'alula ulemu wanu akulu awa eeeish atipepelesa sure

  • @DaveMakondetsa
    @DaveMakondetsa 6 місяців тому

    mwayankhula bwino kwambili ngati zikadi wa Malawi❤❤❤❤

  • @mphatsosadiki4983
    @mphatsosadiki4983 6 місяців тому +2

    Well spoken.....

  • @JuvenileDebwe-bv8ow
    @JuvenileDebwe-bv8ow 6 місяців тому +2

    Apa pokha Usi avomereza chilungamo kuti anthu alindi maso ndipo amaona ndithu iiiii

  • @CtvnMpina
    @CtvnMpina 6 місяців тому

    Well said big man,thumb up🔥

  • @laurentbutao4084
    @laurentbutao4084 6 місяців тому +3

    Chilungamo chimawawa koma izizi ndi zoona..Malumewa SI a UTM

  • @DaudKYSilindu
    @DaudKYSilindu 6 місяців тому

    Mr Lyton excellent spoken keepitup

  • @CharlesKanuni
    @CharlesKanuni 6 місяців тому

    Mr mangochi took his time to recharge and came back stronger 💪

  • @EvanceWame-v7v
    @EvanceWame-v7v 6 місяців тому +4

    Apa nde wang'alula zeni zeni momveka bwino dziko akulitengela chibwana

  • @ClementbWatches
    @ClementbWatches 6 місяців тому +1

    Lerotu Mr Mangochi mwakambatu mfundo zomveka bwino. Ulemu wanu manganya komwe aliko amve. Chipan chathiko Ife ayi.

  • @JosephMaulidi-m9s
    @JosephMaulidi-m9s 6 місяців тому +4

    AMangochi,apatu mwaonesa umunthu.ndipo mukukhala ngati siinu a Mangochi,koma zikomo. coonadi ncofunika

  • @EmmanuelGasiten-fo5dr
    @EmmanuelGasiten-fo5dr 6 місяців тому

    Bravo, wayamba kuyankhula mfundo zenizeni, zamphamvu.

  • @eliffagondewe8214
    @eliffagondewe8214 6 місяців тому +2

    Well spoken 🔥🔥

  • @FelexMisolo
    @FelexMisolo 6 місяців тому +4

    Apa ndiye wayanbapo kumeneko zanzeru

  • @FatimaSande-lb1hd
    @FatimaSande-lb1hd 6 місяців тому +4

    Uku tu nde kuyankhula kopanda chigamba mau mau. pena nso atipeperetsa a Usi wa Aaaaa inu

  • @EstherBonga
    @EstherBonga 6 місяців тому +2

    Apa wayankhulatu za nzelu even BON Kalindo ajuyamikila

  • @0wenNkhambule
    @0wenNkhambule 6 місяців тому

    Very good Mr Mangochi good Message ❤

  • @TheresaNtodwa
    @TheresaNtodwa 6 місяців тому +5

    Mr. Mangochi awuxeni abambo amenewa chifukwa ndiye akupanga. Zinthu zobowa kwabasi.kasatana kachabe chabe kauzeni kamvetsese

    • @DysonUmali
      @DysonUmali 6 місяців тому

      @@TheresaNtodwa exactly

  • @VictorCustom-my1nv
    @VictorCustom-my1nv 6 місяців тому

    Powerful advice from Mr Mangochi.

  • @BensonMoyo-pf2ci
    @BensonMoyo-pf2ci 6 місяців тому

    Mwayakhura fundo ❤

  • @BrightZionga
    @BrightZionga 6 місяців тому +6

    Ndakuombela mmanja mangochi apa pokha chilungamo chimamasula usi ndi wa MCP

  • @YammsyZebron
    @YammsyZebron 6 місяців тому

    Powerful message

  • @Fanzo-h2l
    @Fanzo-h2l 6 місяців тому +4

    Lyton Mangochi apa walankhulatu ngati munthumuuzeni usi akutitenga ngati ife zitsilu hule wamunthu

  • @DENSONZULU
    @DENSONZULU 6 місяців тому +2

    Ife UTM sangatigulitse .... UTM yachilima ija ilipobe ija yachina Kaliati

  • @LinlyMkunghudzakadzuwa
    @LinlyMkunghudzakadzuwa 6 місяців тому

    Straight talk keep it up

  • @AlexKamowa-u7m
    @AlexKamowa-u7m 6 місяців тому

    Good speaking mr Lyton mangochi

  • @asahelmachila3026
    @asahelmachila3026 6 місяців тому +1

    Long live Impi Biyeni

  • @CharlesChamveka
    @CharlesChamveka 6 місяців тому +3

    Ay Mr mangochi apa pokha mwayesesa kulakhula kwa nzeru

  • @YamzyNedson
    @YamzyNedson 6 місяців тому +2

    Koma apapa zikumveka bwino kwabas Mangochi walankhula mwanzeru chifukwa Manganya samamukonda Chilima .

  • @masterchitabwino898
    @masterchitabwino898 6 місяців тому

    Listening Keenly .....kambani ndithu

  • @Geraldmkwewu
    @Geraldmkwewu 6 місяців тому +3

    Iweso ukuti musiyeni usi ndwe Galu team ya Mr chikangawa fiti agalu lnu

  • @0wenNkhambule
    @0wenNkhambule 6 місяців тому +1

    Good Message Mr mangochi

  • @ebenezerkamanga6016
    @ebenezerkamanga6016 6 місяців тому

    Welcome back Mr Mangochi

  • @williamsalexmbonga
    @williamsalexmbonga 6 місяців тому

    Michael Usi the big man

  • @JonathanMtambo-w6e
    @JonathanMtambo-w6e 6 місяців тому +2

    You. have said. the truth utsi. is not for utm

  • @HamzaMkwanda-bh8dc
    @HamzaMkwanda-bh8dc 6 місяців тому +1

    Respect

  • @tobiasshalla
    @tobiasshalla 6 місяців тому

    Let the Vice President be please !!!

  • @InnocentnMbale-zq8pk
    @InnocentnMbale-zq8pk 6 місяців тому +3

    Mangochi apa nde wandilankhulila ndithu angofusa kutisokoneza ife a UTM

  • @dunstankgombezi2911
    @dunstankgombezi2911 6 місяців тому

    Apa mwayankhula big.
    Osaka asowa poyambira.

  • @ChimwemweKondowe-nj4lx
    @ChimwemweKondowe-nj4lx 6 місяців тому +1

    For the first time I am happy with you Mr Mangochi pa zanzeru zomwe mwalankhula apa.
    I'm sure kuti we're expecting more from you

  • @paulpaseli6310
    @paulpaseli6310 6 місяців тому +3

    Amangochi mukafuna mudye za ausi .

  • @slow-kkamanga4906
    @slow-kkamanga4906 6 місяців тому +1

    very true mangochi

  • @Gwedeza-oz3jv
    @Gwedeza-oz3jv 6 місяців тому +1

    Zanzeru ndizochepa umu kuti mumumvele bwinobwino statement yakeyi yachoka kwa iye manganya mwini kuti awuze mtundu wa anthu kuti akazamati ndine wa mcp anthu asazazizimuke kwambili,
    Ndipo chakwera ali mommu this is propaganda of mcp

  • @MuhaSaibu
    @MuhaSaibu 6 місяців тому

    Mangochi lero mwakambako zanzelu

  • @andiwochishadreck3753
    @andiwochishadreck3753 6 місяців тому

    True talking mangochi

  • @SammyKasolota
    @SammyKasolota 6 місяців тому

    More fire

  • @PatrickMbenje
    @PatrickMbenje 6 місяців тому

    Well spoken

  • @HassanMufase
    @HassanMufase 6 місяців тому

    Wakamba zazelu

  • @zulubeats1071
    @zulubeats1071 6 місяців тому +5

    Bwanji osakayendera ma office a NRB ku southern, eastern and northern regions kuti anthu alandire za unzika mu nthawi yabwino?

  • @LamieTiger
    @LamieTiger 6 місяців тому +3

    Apo Nde wanena zoona a usi Sia UTM

  • @asahelmachila3026
    @asahelmachila3026 6 місяців тому

    Chikangawa will never break the movement's resolve

  • @madalitsomorris6566
    @madalitsomorris6566 6 місяців тому

    Resign, Mr Usi too much drama,
    Well said

  • @DicksonMacheso-lr7oy
    @DicksonMacheso-lr7oy 6 місяців тому

    Fundo zinazo za mangochi ndi zopoila, amalawi tikuyenera kudziwa kuti tonse ndi amalawi koma zinkhulupiro ndi zotsiyana,kutsapedzaeka a Micheal usi ku candle 🕯️ light sichifukwa choti anene kuti si wa utm koma anene zifukwa zina

  • @MaxwellMbesa
    @MaxwellMbesa 6 місяців тому

    Bwana mangochi kubwera kumeneko USI ndi wa mcp akungobisara

  • @DENSONZULU
    @DENSONZULU 6 місяців тому +1

    Mwayamkhula bwino sure

  • @BeatriceMawala
    @BeatriceMawala 6 місяців тому

    Amangochi lero mwayankhula chilungamo pitilizani

  • @PETROLJ-n1t
    @PETROLJ-n1t 6 місяців тому

    Manganya ndichisilu galu ndi mozi mwa anthu ogwesa ndege ameneyo😮😮

  • @chancyphiri
    @chancyphiri 6 місяців тому

    Ndwochenjela mopusa ameneyo

  • @GladysBanda-h2w
    @GladysBanda-h2w 6 місяців тому

    manganya watikwana kale.Mr Mangochi mwabwera

  • @AchinaKellz
    @AchinaKellz 6 місяців тому +3

    Apo wabaya

  • @GiftLichadi
    @GiftLichadi 6 місяців тому

    Good good lyton

  • @KambalameSumayyah
    @KambalameSumayyah 6 місяців тому

    Mangochi go deeper iweeeeeeee

  • @JonathanMtambo-w6e
    @JonathanMtambo-w6e 6 місяців тому +1

    Lyton. mwalankhula zan,zelu. Kwambiri kwambjri. takuyamikila kunokuchitipa

  • @MiddayDeleza
    @MiddayDeleza 6 місяців тому +1

    Apa nde mwayankhula zoonadi 100%ausi si a UTM zinayamba kuwoneka kale kale Chilima alipo

  • @StoneckJali
    @StoneckJali 6 місяців тому

    Mumafuna muzidya naye ngati achipani muziyenda naye mwauponda. Musiyeni zanu agwire ntchito ya boma mufune musafune president wa UTM ndi Usi

  • @lacksonsiyadi943
    @lacksonsiyadi943 6 місяців тому

    Mangochi lero apa nde waza mwakathithi

  • @DafterKhungwa
    @DafterKhungwa 6 місяців тому

    Zoona,kuyimba nyimbo zachinamwali pamsonkhano

  • @WysonAdamu
    @WysonAdamu 6 місяців тому +1

    aLyton APO mwalankhu zoona avaice si a UTM ayi

  • @chimwemwemorris6827
    @chimwemwemorris6827 6 місяців тому

    Zangongore zakezo tilibenazotchito koma asamatinamizekuti ndi wa UTM ai sitikumudziwaife

  • @ThokozaniBilliat-im7lf
    @ThokozaniBilliat-im7lf 6 місяців тому

    Manganya palibe akulakwitsa and zomamena kut sanali wa UTM kapena kut si wa UTM ndikulakwa chabe.Mvuto lomwe Malawi tili nalo ndi nsanje.Chilima anamutenga chifukwa chani Micheal usi ngat sanali ofunikila?.Amene akudzimva UTM kwambiriwo bwanj Chilima sanawaike pa vice president?.Nsanje kusavomeleza phunzirani makape inu

  • @DysonUmali
    @DysonUmali 6 місяців тому +1

    Mangochi wandigwira mtima koopsa

  • @DesmondTaulaye
    @DesmondTaulaye 6 місяців тому

    Mau a mphamvu(powerful voice)

  • @corretabanda7685
    @corretabanda7685 6 місяців тому +1

    Zoona zake

  • @KambalameSumayyah
    @KambalameSumayyah 6 місяців тому

    Mangochi go deeper iweeeeeeee 😂😂😂😂😂

  • @HendrickBanda
    @HendrickBanda 6 місяців тому

    🔥🔥🔥🔥♥️♥️♥️💪💪

  • @ibrahimdyman4356
    @ibrahimdyman4356 6 місяців тому +1

    Wayakhula ndithu za zeru

  • @SoldierWilison
    @SoldierWilison 6 місяців тому +1

    Leroditu alangula zaseru

  • @augustinechibbalazi8897
    @augustinechibbalazi8897 6 місяців тому

    Vice State President, Malawians expect change from rut to prosperity:Genuine philanthropy and patriotism.

  • @rabsonswathera738
    @rabsonswathera738 6 місяців тому +1

    Mau a chilungamo