A day is never complete for me if I do not listen to what the DC has to say. I always look forward to hear his talking points, views, suggestions and general advice.
Mufune musafunee born kalindo asakhara president believe me this is our future president if you like it or not born kalindo is going to be president one day 🤞🏽🤞🏽🤞🏽
Kkkk,Koma Malawi analowadi mphepo,Uyuyu akhale president zoona?,anthu anzeru zawo ophunziranso ali kuti,Malawi si pamajigatu?.Komanso awa ndi antchito a Peter Muthalika.Ikadzawina DPP adzapatsidwa udindo m'boma
Am agree kt report anatulutsali ndi lopanda pake and pamwamba pakuti it's istupit ine mkuti ndizamanyi ndibwino akangokhala chete chabe,a pule kumwambaku ku Mulungu yemwe dzina lake ndi YEHOVA analenga diso lanulo sangalephere kukuonani.
We need people like mr b kalindo in this country ❤❤ l really like the way this guy is doing and l wish if we can choose mr kalindo as a president in our country All the way from cape Town pa boma ❤❤❤❤❤❤
If we know the difference between politics and economics, we will enjoy as a country, our politicians they mix the two together, that's why we are in this situation
A Kalindo andikumbutsa nzathu wina wake apolice anamugwira atangofika kumene kuno ku South Africa anatuluka kundende after 2 months anakabwera qanenepa anthu osamamudziwanso kkkkk pano amangoti mukunena uja ananenepera ku ndende uja? Kkkkk😂😂😂😂
0/10 is not a fair judgement. Attacking the president as a person does not help anyone including anthu ngati ife who will vote not for a political party but capable leadership with sound developmental policies. Abale we need not be misled by people who are promising us heaven so that they can get in on our ticket then to further their political growth . This is home to all of us . These drama issues will not build a nation.
A day is never complete for me if I do not listen to what the DC has to say. I always look forward to hear his talking points, views, suggestions and general advice.
That is really truth.....BIG UP BRAZA....!!!!
Yoh right brother
Mufune musafunee born kalindo asakhara president believe me this is our future president if you like it or not born kalindo is going to be president one day 🤞🏽🤞🏽🤞🏽
Mbuzi ya anthu opusa ndi opanda mzeru nzanu ndi ameneyi
Or atakhala mbuzi its better than crocodile yemwe akungodziwa kupha anthu kuba komanso kuononga
Kkkk,Koma Malawi analowadi mphepo,Uyuyu akhale president zoona?,anthu anzeru zawo ophunziranso ali kuti,Malawi si pamajigatu?.Komanso
awa ndi antchito a Peter Muthalika.Ikadzawina DPP adzapatsidwa udindo m'boma
@@Okalekale misala imeneyi chamba chili thooooooooooo
The real freedom fighter
Komatu mr plezident mukunenepa sopano we malawias we love you plezident
President wa ma bodza ngati abambo ake satana plus APM wopha malubino😅😅😅😅
You are the true fighter mr DC!! your our Samson here in Malawi,. May God continue protecting you until we have rescued from this crockdile's mouth...
Watching from SA the freedom fighter Indeed ❤❤❤ mulungu akutetezeni boss
Kunenepa plus kutchena big up Mr president ❤❤
Chilungamo ndichopweteka Kalindo keep fire burning 🔥 Malawi akufunika anthu ngati Kalindo
THE DC, I REALLY LIKE THE GUY 🔥🔥🔥🔥🔥🔥
Akuti Kodi Mr Kalindo mungayipatse ma percentage angati MCP mu Zaka 4 yakhalayi ( Kalindo says 0 out of 10 😂😂😂) Mwana Olimba mtima Kalindo🔥💪
Ndiyo nsanjeyo or pa cement akuuzani kuti fumbi
Muli uthenga mwa kalindo, kupanda kumvera the DC sindingagone 😅 chilungamo chabwanji ichichi. Kod amamvera achakwera wo? Ndipo nde 0 pa 200 wachita pazaka 4. Chilimatu amatiwawa ndipo kaya wnanu mmamva bwanji? 😢 RIP Saulos Chilima 😢
Boni kalindo the Dc mwana owopsaaa kwambr 💪💪💪💪💪
Kupandatu anthu Ngati Bon kalindo okubawa sitinakawaziwa ndibwenzi tikuungoti boma ndilomweli
Kalindo always stands on truth if leaders listened the country could be developed
God be with you bwana DC you always be side of poor people longing to live
❤❤❤❤ My support to you Mr boon kalindo the DC president wathu
Long live Mr pangolin the DC❤❤❤❤❤
Big man everything you says I agree with you 🎉🎉🎉🎉🎉🎉
Pitilizani big 🎉🎉🎉🎉
The real freedom fighter Mr DC you need face Malema the strong men
Kkkkk my president wandipedza akuti chakwera amavala plastic shoes leather
Out of 10 nd zero tisachedwepo pamenepo😂
Wa mcp sasowa...mfiti iwe
😂😂😂😂😂booon kalindo akuti zero pa ten
Ati pamenepo tisachedwepo😂😂😂😂
We love you here from mpoto Mr Dc
Kkkkkk zoonadi chikangawa anali ovetsa chisoni kalindo sakunama ndipo sadzanamapo
Am agree kt report anatulutsali ndi lopanda pake and pamwamba pakuti it's istupit ine mkuti ndizamanyi ndibwino akangokhala chete chabe,a pule kumwambaku ku Mulungu yemwe dzina lake ndi YEHOVA analenga diso lanulo sangalephere kukuonani.
BON KALINDO NDI MUNTHU WABWINO KWAMBIRI KEEP IT UP MY PRESIDENT
We need people like mr b kalindo in this country ❤❤ l really like the way this guy is doing and l wish if we can choose mr kalindo as a president in our country
All the way from cape Town pa boma ❤❤❤❤❤❤
DC is best chiyembekezo chathu
Pangolin wathu olo aboma amadziwa ❤❤ machine opangira zida za ufulu
God may bless you a good activist
The DC president Wathu Wathu ❤❤
Umakwana bon iwe ndi bakili muluzi komaso mutanyiwa mukuyenela kutetezedwa
Remember one thing, leaders born leaders, not made, it's a gift, chakwela doesn't have it,let's face the fact
Ulemu wanu a Mr president, inuyo msadzafe ayi mmatiyimila
Born kalindo akufinikila anthu angapo timupatse support ndikumanga umodzi molimba kuti tisithe Malawi wathu
Kalindo the top notch
Timamvananu kukoma mapwiya apwiya...........muulupali.❤❤❤❤
Palimbe angabweze galimoto iwe ndiyowamba
Only one man standing love u Mr president onest speaking
The DC MWANA Woooopsa kwambiriiiii 🔥🔥💯
Atasalemo Chakwera ndi Nkazi wakedi😂😂😂😂😂
Boni Kalindo "DC" watching from Nkhotakota
Chilungamo pamtete . Congress yabisala pachipande .
our. freedom fighter
Osaopa, Osatopa, Osafooka ABiyeni Adawaphela dala, Awona matsoka akathithi Ayemusipi
Tsiku la lero fees ya Ku secondary school kuchokera pa 7500 mpaka 40,000 school free
Uyuyu ndi kamuna 😅
Our president boooorn kalindo 🔥 sazatheka
I'm proud on you Mr president of born to suffer of Malawian people's
bigman tsopano bwana kalindo the dc mumatiimirira biggy
Mr DC timenyereni khondo kuipulumutsa Malawi
0 pa 10 😂😂😂 anali wovesa chison chakwera ndi nkazi wache 😂😂😂😂😂chikangawa woyooooo😂😂😂
Bon Kalindo following from Zambia
Fire bwanaa
If we know the difference between politics and economics, we will enjoy as a country, our politicians they mix the two together, that's why we are in this situation
The DC mumayima pa chilungamo inu
❤❤❤❤ Good bless you true story
Munthu wamkulu ameneyo the DC
Iwe usatinamizepo apa iwe Kalindo,zolinga za gulu lanuli ndi zolinga za amene amakupangani sponsor,amakupangani sponsor ndi ndani?
🤣🤣🤣 Dzaka 10 pa u president koma ziliko the DC!!!!!!!
Kuyankhura kwa zeru kumeneko
All in all, the DC is right, politicians think politics is a self riches garden
Kuyankha mwandiiiiii DC ❤
Munthu wa nzeru zachibadwidwe
The nyonyolido mwana wakwathu umakwana
God bless the DC
Ndipo zodabwitsa ndege inyamuka bwanji opanda zipangizo ngati zimenezo President amayenera kufusa responsible people zimene akufusa Kalindo
More 🔥 fire Mr BK ngaluleni
Ameneyo
😂😂😂😂😂 DC mumandiwaza
The DC pangoline our representatives and freedom fighter ❤❤❤
Aborn ambuye akutetezelen kwambili mumati imilila
A Kalindo andikumbutsa nzathu wina wake apolice anamugwira atangofika kumene kuno ku South Africa anatuluka kundende after 2 months anakabwera qanenepa anthu osamamudziwanso kkkkk pano amangoti mukunena uja ananenepera ku ndende uja? Kkkkk😂😂😂😂
Yes Mr DC bon kalindo❤❤❤❤
Mwayankhura bwino ndipo zanzeru kwambiri
The only thing I love about this guy chimayankhura without fear keep telling them the fact
Ameni born kalindo mulungu atimenyela nkhon 🙏🙏🙏🙏
akulu bola musadzasithetu kukhala ngati mtambo uja.Enafe timakunyadirani ndithu muli ndi fundo za bwino.
Watching from S.A.
The one and only the Dc💪🏼💪🏼💪🏼
Kkkkk Simbi zikulu
the DC umakwana
Kodi bwana kalindo sumungayimireko u president
Aaaaa a alibe mzeru awa chamba chili thooooooooooo 😅😅
machine opangira machine amzake more 🔥🔥🔥
Mutiyimile mr Born Kalindo as "PREZIDENTI",2025 .coz nzanuyu mmmm😢
Kaswiri kwambili DC
DDDDCCCC CHILOMBO MWANA WOBADWA MIYEZI 9 Osapita kumagetsi ayi
Mbala iyi wachita kunenena ekha kut akufuna kuthandizila zipani zina ndiwa bodza uyu akumatinamiza kwambir,ungadyese anthu osauka chisiru iwee nyapapi iyi ndi mtambo sakusiyana zao ndi zimozi
MCP inapha chilima ndianthu ena Aja basi palibeso umboni wina tikuufuna apa
Host yu amadziwa ntchito 👍👍👍
Zilooo out of 10😂😂😂😂😂😂
Our great activist the DC
Osadandaula bwana mumangidwanso
The Dccc mwana oopsa kwambiri
Koma Aprezident anenepatu 😂😂😂
Wise man dc
Bon kalindo ndimunthu akumagonetsani tulo inu
😂😂😂 atatsala chakwera ndinkazache
This guy is making sense ndithu...
0/10 is not a fair judgement.
Attacking the president as a person does not help anyone including anthu ngati ife who will vote not for a political party but capable leadership with sound developmental policies. Abale we need not be misled by people who are promising us heaven so that they can get in on our ticket then to further their political growth . This is home to all of us . These drama issues will not build a nation.
Chikangawa lipoti limeneli ukawuze abambo ako iwe ndichisilu kwambiri ukutitenga ngati Amalawife makape eti? Uchoke gwape iwe 2025 A.P.M boma osati iwe,gyz ku Malawi kuno kulibe pulezidenti ichi ndi chisilu timuchotse
Big DC