Limpopo watulukilaso Ntanyiwa kudzathila nchenga mu mpunga wa boma kuwavetsa kuwawa

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 1 лип 2024

КОМЕНТАРІ • 27

  • @sayidimisessa
    @sayidimisessa 2 дні тому +5

    Alemba mmadzi amenewo olo akamapereka R2000 ifekuno ku Johannesburg sitingachite za kanunduzo. Azibale athu kumalawiko akuvutika kaamba ka boma lonunkha mcp

  • @MosesKarengo
    @MosesKarengo День тому

    🤔big up big♥️💪💪💪💪✊✊✊✊✊✊🎉🎉🎉🎉🎉🎉🎉🎉

  • @HafsaAbwanali
    @HafsaAbwanali 2 дні тому +2

    Uthengau upite kwa brother nthanyiwa auze boma la ku South Africa ko kuti dziko lawomo mwalowa zifwamba zochokera Ku malawi zabwera ndiupandu. Nde muziwauza madera. Omwe Ali azifwambawo apolice awangire akaponye chakulinderako azikalima masamba tizigula mashop mu asazatulukenso chifukwa akutengela phamvu kumanja powaona kupusa eni dziko nde anthanyiwa musankhale nchisoni ndi crocodile pple agwidwe basi komweko uthengau ugwirisireni ntchito kuti akamangidwa ena atengereppo phunziro

  • @Henry-vw2cz
    @Henry-vw2cz 2 дні тому +1

    Tipha kuno 💪💪💪

  • @SymonYohane-i5q
    @SymonYohane-i5q 2 дні тому +2

    ❤🎉 mbambande iweyo umakwana ntanyiwa keep it up

  • @user-dn3gp6yi4y
    @user-dn3gp6yi4y 2 дні тому +1

    Anthu awa asatidanitse amphawi ife ndi dziko la south Africa mu south Africa ndikumene tikupezelako thandizo lathu tikumakwanisa kusamalila makolo ndi ana kumamiziku ndiye inu aboma chepesani za chibwanazo muzipanga ku mudzi Koko kuno ayi tikupondani tikakuziwa tikufinyani ndithu akunkuyu samalani chifukwa mwatulusa maso ndi chipani chanu mutha kufa ngati nkhandwe wokuba nkhuku musamale koma

  • @LouisChipanda-ux9dz
    @LouisChipanda-ux9dz День тому

    Akunama amenewo tikangowadziwa akumana ndi ma tsotsi kunoku

  • @sayidimisessa
    @sayidimisessa 2 дні тому +3

    Mr Ntanyiwa mmatiimirira monga ife amalawi omwe tiri panchombo penipeni pa Johannesburg tikukupemphanikuti tazizutseni zipani zosutsa kuti zizipanga zochirimika pa ground kuti boma lokuphali lichoke

  • @user-re7fo3be2z
    @user-re7fo3be2z 2 дні тому

    Tanguwawombela komweko afele komweko akuwononga ndalama za amalawi

  • @DysonNakhaphe-bo4dl
    @DysonNakhaphe-bo4dl День тому

    Man mukutiyimilila and tikudziwa zambili kuzela mwa inu pitilizani

  • @ThompsonMakwakwa
    @ThompsonMakwakwa 10 годин тому

    Awomberedwako chabe kuno!! Asamaletu other wise apita opanda moyo!!

  • @user-rg4du4vu9r
    @user-rg4du4vu9r 2 дні тому

    Shaaaaa km ndaramadi iripaminga et

  • @elizasingano
    @elizasingano 2 дні тому

    Kod anthu akunyamuka ku malawiwo ayenda pa bas ? Ngat ili bus tiziwisen kut ndi bus yanji

  • @KennethKilembe-ex5ro
    @KennethKilembe-ex5ro 2 дні тому

    Great ntanyiwa

  • @vincentbarnes5872
    @vincentbarnes5872 2 дні тому +1

    DPP sikuti inalinso ya bwino mulakwisa kwabasi. Utsogoleri wa DPP kapena MCP sitikuufuna ata pang’ono koma utsogoleri wa masomphenya a Dr Saulos Klaus Chilima

    • @AbrahamTembo-z5k
      @AbrahamTembo-z5k 2 дні тому

      You are one of the wise, just & intelligent people.

  • @user-lk8kj9zv6x
    @user-lk8kj9zv6x 2 дні тому

    Ayitu Mr Ntanyiwa inuyo simugwidwa mulungu sakulola anyapapi amenewa kut akwanilitse zofuna zawo nthawi yawo yoyaluka yakwana mudzingowayang'ana

  • @henrynsiku2108
    @henrynsiku2108 2 дні тому +2

    Tiwagwira kuno ayerekeze kuyambiya kuno Pretoria comrade #MCP must gooooo!!!!!!!

  • @user-ml8lk9dr7t
    @user-ml8lk9dr7t 2 дні тому

    Zilipo njira zina zamwamuna zooneka zoongoka koma tsiliziro ake ndi imfa anzathu tsogolo palibe munthu ukamafa umayamba kugontha mkutu ndizo zikuchitikazi

  • @user-dh1oi8mb4v
    @user-dh1oi8mb4v 2 дні тому

    Ndipo sitikwanitsa achepaaa

  • @HalisonSolomon
    @HalisonSolomon 2 дні тому

    AWAWA GUYS AKANGOFIKA MU JONZ MUNO AKAMABWERERA ABWERERE ATASINZINA , ASABWERERE AMOYO IFE TAGWIRIZANA NDI MA ETA TIKANGOWAPEZA TIKUWAVEKA MA TAYALA NKUOTCHA TIKANENA KU POLICE KUTI NDI ZIGAWENGA ZACHOKA KU MALAWI KUFUNA KUDZASOKONEZA DZIKO LINO, ASIYENI A BWERE TIKUMANA KONKUNO

  • @LindaMakalani
    @LindaMakalani 2 дні тому

    Palibe chochitika mulungu ali nanu cholinga

  • @user-jb5hr4rz2s
    @user-jb5hr4rz2s 2 дні тому

    Timakondwera nanu a bwana

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg 2 дні тому

    Mr Ntanyiwa Kodi ifeso timaika ma comment zikhale ng'oma atigwilaso😢😢😢