Limpopo iiiih! ma demo ajatu kwabwela anthu akunja kudzaletsa atapangidwa hayala Ntanyiwa waulura

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 3 жов 2024

КОМЕНТАРІ • 99

  • @MercyKatongo-p9b
    @MercyKatongo-p9b 3 місяці тому +13

    We won't fear anything even as Zambian s were coming in Malawi guys to fight that evil man chakwela

  • @mellipherjohn7158
    @mellipherjohn7158 2 місяці тому +1

    umakwana mtanyiwa tikuziwa zambili amalawi ambuye azikupasani moyo wautali 🎉🎉🎉🎉

  • @ShaolinThomas-ow8yn
    @ShaolinThomas-ow8yn 3 місяці тому +7

    Inuyo mulungu adzingokuonjexelani moyo wautali basi ,chifukwa mukutimvetsa kukoma

  • @FrynessMoyo-to2du
    @FrynessMoyo-to2du 3 місяці тому +2

    Asilikari anthu ntchito yao ndi kuchinda mahule mutchesi umu😂😂

  • @DavidJackson-ox4xm
    @DavidJackson-ox4xm 3 місяці тому +3

    I support Limpopo FM with Comrade Mtanyiwa.

  • @JuuuKomba
    @JuuuKomba 3 місяці тому +3

    Koma iweyo pokhapa pot awagwila ndakuimikila manja mwamba athuo agwidwad

  • @PeterMphanza
    @PeterMphanza 2 місяці тому

    Nice job comred mwana wa amama kuno ku Zambia

  • @WatsonNtchito
    @WatsonNtchito 2 місяці тому +1

    Mademo akayambire kumamfumu hotel komweko tiyeni tonse tikasokhane popo pa mfumu hotel ku ma room achulidwawo osaopa

  • @FrynessMoyo-to2du
    @FrynessMoyo-to2du 3 місяці тому +2

    Akulu akulu mukulankhula koma sitikumva 😢

  • @UsenLashid
    @UsenLashid 3 місяці тому +2

    Komaso Mr ntanyiwa musalore Kuti anthu 8 amene agwidwawo asatuluke Ayi kufikila chakwela atule pansi udindo komaso dziko la South Africa asawapange rilizi Ayi kufikila lamampho atamuzenga mulandu chakwela

  • @mthawisakaunda
    @mthawisakaunda 3 місяці тому +2

    Akatula udindo chakwerayo, azibale ake onse azachotsedwe ntchto. Galu watitopetsa

  • @Hassankazembe-d3o
    @Hassankazembe-d3o 3 місяці тому +1

    May God bless you comrade Ntanyiwa

  • @BitonFred
    @BitonFred 2 місяці тому

    Anthu akumalawi umbuli, anachotsa peter, ati wabwino chakwera, pano akufuna peter yemwe uja, mmalawi wanzeru sakuyenera kupeleka vote ku president yemwe analephera kale, votelani atsopano osati apeter muthalika

  • @FrynessMoyo-to2du
    @FrynessMoyo-to2du 3 місяці тому +2

    Koma chakwera wandikwana one day ndi kupedza people they call gringo

  • @HevenChiwaya
    @HevenChiwaya 3 місяці тому +1

    Asilikali a ku Malawi ndi ogona tulo zitsilu zimalimbana ndi anthu wamba usayelekeze kuvala kabudula wa makaka ndiye amaonesa mphamvu zawo ati wavala unform yawo mbudzi

  • @BraghtYohane
    @BraghtYohane 3 місяці тому +2

    Ntanyiwa iweyo ndi number one radio yako timainyadira kom athu athawa ziko lili rawo kom kumeneko moto kuti buuuuu mumtimamo angokhuta mphuma lokhalokha km mulimba Ntanyiwa woyeee

  • @FrancisNyayi
    @FrancisNyayi 3 місяці тому

    Apapa ndatanganidwa kuwerenga nkunvesera😂😂

  • @BrunoChakukuma
    @BrunoChakukuma 2 місяці тому

    Ntanyiwa woyeeeee

  • @EllenPhiri-xt8pt
    @EllenPhiri-xt8pt 3 місяці тому

    Kuti muone ku mcp kuli anthu osaoneka bwino okhaokha pamaso ndionyasa ndi mtima momwe

  • @blacksonpeshes5057
    @blacksonpeshes5057 3 місяці тому

    kom mukutivetsa kukoma ndikapanda kuva uthenga kuchokela kwainu sindipuma bwino kod mudarikuti mosemunja

  • @MikeMerecah
    @MikeMerecah 3 місяці тому

    Ma activists athu musakhare chete kunoko akumangidwa mwachisisi mudziwe zimenezi, anthu osatchuka panopa Ali ku area 30 guyz,

  • @MathpeterLemon-ls1ns
    @MathpeterLemon-ls1ns 3 місяці тому +3

    Pano malawi ndi North Korea 😭😭😭

  • @JamesIsaac-zi4kb
    @JamesIsaac-zi4kb 3 місяці тому

    Chakwela ofuna adibwe kanyenya basi

  • @stanleychisasa4343
    @stanleychisasa4343 3 місяці тому

    Boss mbuyomu munatiuza kuti athu aku German ofufuza ndege aja anali okonza miseu lero muti ndi aku butcher which is which
    Big man?

  • @AugustineIshmael
    @AugustineIshmael 2 місяці тому

    Zachamba basi dikilani 2025 vote yanu ndiye nuclear power osati zabibi zanuzi

  • @HalisonSolomon
    @HalisonSolomon 3 місяці тому

    Ndipo chakwera tidzachita kuotcha pamoto chifukwa chankhanza akuchitazi

  • @HalisonSolomon
    @HalisonSolomon 3 місяці тому

    Ankolo ku malawi kulibe a silikali akanakhala kuti alipo zikuchita galu ameneyo mukumuti chokwerayu atamukhazika kale pansi, koma nawo asankha kugwirantchito ndi chipani ayiwala makamulo awo ndi mbuzi za silikali za manu pansi ndi mbuyao chakwerayo tionana chaka cha mawa onse amene akupha ndi chakwera tikhaulitsa boma ili lapita olo ataopseza motani zosatheka

  • @misoMoyo
    @misoMoyo 3 місяці тому

    Limpopo FM ineyo ndimachedwa Ku ntchito kuti ndimvere basi nkhani ZANU mumandidalitsa ine ndi m,ngoni weni weni more fire inuyo a Mr Ntanyiwa

  • @mipeacemakermw9501
    @mipeacemakermw9501 2 місяці тому

    Mwatukwana president 🤣🤣🤣🤣ua-cam.com/video/WRDkQ8s_34k/v-deo.htmlsi=PkGoYsuJRKSW0v4p

  • @EllenPhiri-xt8pt
    @EllenPhiri-xt8pt 3 місяці тому

    Chakwela ndikanankhala kuti ndimatha ufiti ndinakamchosa ineyo manyi akee anthu

    • @EllenPhiri-xt8pt
      @EllenPhiri-xt8pt 3 місяці тому

      Chitsilu chichakwela ndi family yake yonse ambuye tichotseleni munthuyi😊

  • @CadTafa2
    @CadTafa2 3 місяці тому +3

    Apolici a malawi a kuzishipisa

  • @PartsonMdeza
    @PartsonMdeza 2 місяці тому

    nkhanga zaonaaa

  • @JaneLikome
    @JaneLikome 3 місяці тому

    Nice mr ntanyiwa

  • @DuntumaziyaDuntumaziya
    @DuntumaziyaDuntumaziya 3 місяці тому +1

    following you sir

  • @priscillamangata4023
    @priscillamangata4023 3 місяці тому

    Comredy mtanyiwa tikufuna number yanu tizipephela Nanu mulungu azikudalisani kwambili ndipo azikutetezani kulikose komwe mukuyenda

  • @CathrineRamseyJafaal
    @CathrineRamseyJafaal 3 місяці тому +1

    Anthu nonse amene mukudana ndi nthanyiwa mitungati zoswera malambe inu zikukusangalasani mmene akuyendesela dzikoli gule wanuyi achoke alibe phindu

  • @DesireMphatsogama
    @DesireMphatsogama 3 місяці тому

    Tisayembekezere kuti tingamve munthu wakuphayo kuti ndine ndapha mayz ?
    Munona kt wakupha kufufuza chifkwa chomwe wina wafera koma atapha ndiyeyo ?
    Mayankho ndiomwewa omwe tikumayankhulawa coz action ikuchitatu kuoneka yokha ndipo mwachindunji monga kumangidwa anthu then kulowesa zigawenga nde ngt akusakidwa anthuwa kuti aphedwe nde nkumat ena omwe adafa aja anafera zina ?

  • @AjibuTwalibu
    @AjibuTwalibu 3 місяці тому

    Umakwana ya mtanyiwa tili nawenawe my brother

  • @IssahAluba
    @IssahAluba 3 місяці тому

    Chonde AMalawi asatiphimbe maso BOMA ilili osalivera tiyeni pansewu week yamawa osaopa gayz 💪💪🛶🛶🏹🏹⚒️⛏️

  • @Bonisiwentamo
    @Bonisiwentamo 3 місяці тому

    ❤Zowona acc muthu ameneyu AChoke

  • @UsenLashid
    @UsenLashid 3 місяці тому

    Kodi inu apolice ndi asilikali ntchito yanu ndi chiyani kumalawiko? Kodi mukuyang'anila zika Zanu zikuphedwa Kodi inu ndinu apolice opanda ntchito pamodzi ndi iwe wa mkulu wa asilikali utule Pasi udindo coz your usiless man dammit asilikali inu achilungamo menyani nkhondo please

  • @chadreckchibwithala1493
    @chadreckchibwithala1493 3 місяці тому

    zinamizanani pano pa limpopo kwachwera ali pheee kukozanyasi zomwe inapanga dpp . alikuti anthu omwe agidwa aaa opusi mtanyiwa

    • @HalisonSolomon
      @HalisonSolomon 3 місяці тому

      Iwe mutuwako suyenda ngati akutuma a mcp anthu akufinya ndi chakwera wakoyo ngati akupasa ndalama ulibe manyazi wekha otsutsa pano aaaaaaaa ona kolowera

  • @NisharChibisa
    @NisharChibisa 3 місяці тому +1

    Mumakwana

  • @MandalaChaona
    @MandalaChaona 3 місяці тому

    M C P -- Malawi Congress Party
    M C P = Malawi Chikangawa Party 👹👹👹🔨⚒️⛏️

  • @BitonFred
    @BitonFred 2 місяці тому

    😂😂😂😂

  • @maluli5691
    @maluli5691 3 місяці тому

    Asilikali Aku malawi ndi asilikadzi.west Africa asilikali sakunyengelela kulanda boma

  • @shadreckphiri1799
    @shadreckphiri1799 3 місяці тому

    If what comrade is saying is the truth,then Chakwera must be the worst president in Southern Africa.

  • @GeshoMwakitwile
    @GeshoMwakitwile 3 місяці тому

    Nde inu mukuganiza kut olo patabwera peteryo zinthu zingasinthe foundation ya Malawi kuvuta konseko ndi chipani Cha udf olo mutatani Malawi sazasintha

  • @YONA-v5o
    @YONA-v5o 3 місяці тому

    Anthu amenewo ngat agwidwa aphedwe ndinthu cifukwa iwowo anabwela kuzapha

  • @jangiya03
    @jangiya03 3 місяці тому

    Ambuye tithandizeni Malawi waipa

  • @GetrudeBanda-sd1yf
    @GetrudeBanda-sd1yf 3 місяці тому

    Zoonad amalawi azimai tizingoyang'anira nyasizi bvuto azimai timatengrka ndi kathu kochepa

  • @GeshoMwakitwile
    @GeshoMwakitwile 3 місяці тому

    Ukanakhala kut mwina ukutiwuza munthu wozamuvotera koma nawenso ukumpangila peter kampen choti uziwe peter nayenso atatitopesa kale sitikunfunanso

  • @dondamissonchdziwe3958
    @dondamissonchdziwe3958 3 місяці тому

    Hahaha AAA, Malawi poison party, Wanthu anawa votera dala, bolani ife tiri kutali zina ukamva zina Leku kamba anga mwala.

  • @chadreckchibwithala1493
    @chadreckchibwithala1493 3 місяці тому

    mademo mpanga komweko ku lilongwe ayi mkanya

  • @CaptainNyenga
    @CaptainNyenga 3 місяці тому

    😂😂😂😂😂 zabwino zonse wachita bwino wagwidwa tiakonzere konkuno

  • @FrankMulela-qt1wi
    @FrankMulela-qt1wi 3 місяці тому

    Number yotumizila zinthu kwantanyiwa plz

  • @WilliamBandaWili
    @WilliamBandaWili 3 місяці тому

    Mcp mukali kuyalukirayalukiratu

  • @CaptainNyenga
    @CaptainNyenga 3 місяці тому

    Limpopo FM ndi 1

  • @ThokohPrescotKalonga
    @ThokohPrescotKalonga 3 місяці тому

    Malawian kuwopa too much that’s why amakonda kulepheresa mademo so don’t tell us ngati muziwona zoti sizingatheke zochita mademo! Aaa why amakonda kulepheresa mademo

  • @GraceZumazuma
    @GraceZumazuma 3 місяці тому

    Koma Malawi walowa chibwana chakwera anapita ku sukulu koma?pano akusekedwa ndi anthu akunja omwe

  • @ConfusedAstronaut-qv6wq
    @ConfusedAstronaut-qv6wq 3 місяці тому

    Koma chakwera anthawa wauyouyo mbwiyache.

  • @SeephyMfaume
    @SeephyMfaume 3 місяці тому

    MCP Pamtumbo pawo ndithu

  • @MariamAlabi-t3n
    @MariamAlabi-t3n 3 місяці тому

    Ku Malawi aku shooter ma movie rekani amenyane

  • @AnaffSayamika-uh6vg
    @AnaffSayamika-uh6vg 3 місяці тому

    Chakwela ndigalu kwabasi

  • @RhoxinahMalamba
    @RhoxinahMalamba 3 місяці тому

    Chopweteka kwambiri ndi choti ndalama za nkhani nkhani zikuthela kulipira anthu a kunja amene zomwe akuchita mudziko lathu phindu lake opindula ndi ochepa

  • @ConfusedAstronaut-qv6wq
    @ConfusedAstronaut-qv6wq 3 місяці тому

    Asilikira akumalawi ndi wopusa.

  • @HappyMaolid
    @HappyMaolid 3 місяці тому

    It's time to figh now,osagona

  • @CharlesMateya
    @CharlesMateya 3 місяці тому

    Following

  • @PaulineKamwana
    @PaulineKamwana 3 місяці тому

    8:30 musova mcp ,mulithawa dziko mukulifuna

  • @CHIWSABINYAMBOSE
    @CHIWSABINYAMBOSE 3 місяці тому

    Ndichoipadi ichi chigawenga chabechabe

  • @dorisbutao4227
    @dorisbutao4227 3 місяці тому

    Mmmh

  • @AchinaKellz
    @AchinaKellz 3 місяці тому

    Achakwera vomelezani😂

  • @EllinaBitto
    @EllinaBitto 3 місяці тому

    😢😢😢😢😢😢😢😢

  • @ShentrycChinoko
    @ShentrycChinoko 3 місяці тому

    Atanyiwa pathako pako

    • @ShentrycChinoko
      @ShentrycChinoko 3 місяці тому

      Yess

    • @ShentrycChinoko
      @ShentrycChinoko 3 місяці тому

      Zowonadi mchutsuludi chimenechi

    • @EdithKachule
      @EdithKachule 3 місяці тому

      Inu amenewo mungodziyankha nokha muli phee kugwiritsidwa ntchito ndi agaluwo 🥺mxieuw

  • @DavidJackson-ox4xm
    @DavidJackson-ox4xm 3 місяці тому

    Chakwera atha ngati Idi amin sizimuthera bwino ndithu.

  • @FatimanickisJaffer
    @FatimanickisJaffer 3 місяці тому

    Am waiting good news not bad news 😔😔😔😔😔

  • @ShentrycChinoko
    @ShentrycChinoko 3 місяці тому

    Muyiyambe muwone utsi ntanyawa Ali kunja athawa ataba mbuzi kumalawi

  • @DamsonSabitt
    @DamsonSabitt 3 місяці тому

    Paja ninakuwuza kale kuti upite kumalawi mabodza akowo mtanyiwa yiweyo niamene ukumasokoneza anthu infe timapeleka ulemu kwa boni kalindo osati mbuziyiweyo ayi

  • @ChrifordBiziel
    @ChrifordBiziel 3 місяці тому +1

    Ndikut mambodza akowa Pali ine no comment ndizopusa zakozo tithana phwanga galimoto uma user ija nditha kukutumizira komaso pachikwangwani umakonda kucheza paj okay

    • @victorauwana7258
      @victorauwana7258 3 місяці тому +1

      Mwapemphedwa kutu mupange comment?

    • @NizigiyimanaChantal-c2p
      @NizigiyimanaChantal-c2p 3 місяці тому

      😢

    • @SoundmasterElectrical
      @SoundmasterElectrical 3 місяці тому

      Mbudzi iwe uthana ndindani usawone ngat ndife ogona wamva panyo pako

    • @MaryNyirenda-nq3mh
      @MaryNyirenda-nq3mh 3 місяці тому

      Chigawenga iwe chimunthu chopanda phindu chitsilu ulibe manyazi mulungu akukanthan

    • @LukaThawe
      @LukaThawe 3 місяці тому

      Anthu achoka Kuti iwe nawendimbuzi kwambiri ukukofuna kusokoneza amalawi ,chifukwa amalawi ndiopepera kale ndiye azikuvera nyasi zako sata yako

  • @ShentrycChinoko
    @ShentrycChinoko 3 місяці тому

    Chikamabodza chabwela zotani kukamwa ngati manyi

    • @FrancisDay-br7xb
      @FrancisDay-br7xb 3 місяці тому

      Pain MCP

    • @EdithKachule
      @EdithKachule 3 місяці тому

      Dzidyani za magazizo. Mulungu akulangani nkhuku inu

    • @AminahMussah
      @AminahMussah 3 місяці тому

      ukatelo watumidwa nda nzako akuphawo

  • @walesbanda4959
    @walesbanda4959 2 місяці тому

    😂😂😂

  • @CHIWSABINYAMBOSE
    @CHIWSABINYAMBOSE 3 місяці тому

    Ndichoipadi ichi chigawenga chabechabe