MUNTHU WAMULUNGU kuling'alura boma la CHAKWERA...lalephera

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 1 лип 2024
  • Video from HONEST

КОМЕНТАРІ • 90

  • @harrisonkalimbakatha5339
    @harrisonkalimbakatha5339 5 днів тому +8

    That's a very greatful speech we need such type of people who can't fear but they stand for the right thing keep it up pastor/bishop

  • @AlexManuelMisomali-sv1vn
    @AlexManuelMisomali-sv1vn 5 днів тому +4

    You have spoken wisely and positively to all the audience that's true kuti this government of Chakwera and his tonse alliance have totally failed and destroyed Malawian economy and it will be difficult for the next government to restore it

  • @stanleymollen7273
    @stanleymollen7273 5 днів тому +5

    A patriot.....kuphunzitsa economics momveka bwino...economics 101

  • @ShambululaModel
    @ShambululaModel 20 годин тому +1

    Great on Man of God

  • @paulmanyamba5437
    @paulmanyamba5437 5 днів тому +2

    Akulu mulungu adzikusogolelani mukuyankhula chilungamo ngati munthu wamulungu

  • @user-bu4wn5br5l
    @user-bu4wn5br5l 5 днів тому +5

    I LIKE YOU FATHER AWUZIDWE ZOONA NGAKHALE ALI OSAMVA KOMA TIDZAWONANA PA 2025

  • @user-vb1iq5un5p
    @user-vb1iq5un5p День тому +1

    Kkkkkk mwina tiyese kutenga anthu oti Ali mkanthu kalewa bwanji...anthu ngati Mpinganjira aja ndi amchina Simbi ,,,osaukawa akuwonjeza kuzilemeletsa kaye okhatu.....😂😂😂

  • @user-co2cz2ht8j
    @user-co2cz2ht8j 4 дні тому +1

    This pastor should not get arrested 🔥🔥🔥💯

  • @RabeccaMkandawire-i9j
    @RabeccaMkandawire-i9j 5 днів тому +5

    A Malawi kususuka zithu zoti sizitithandiza kukopeke nditu k500

  • @WilliamBandaWili
    @WilliamBandaWili 4 дні тому +3

    Boma anachita kulilira ili that's y vamunyera chakwera pls anthu apa central region musamuvoterenso uyuyu atipha

  • @paulbanda9638
    @paulbanda9638 4 дні тому +1

    Patakhala kuvota mau anu ndavotera kale,u r a good preacher

  • @user-ui4ux5kc8d
    @user-ui4ux5kc8d 5 днів тому +3

    Ndipo zimafunika kutii uthengawu uwafikire ndithu ukulu amenewa munthu osamva ngati ameneyi sindinamuonepo inee maulendo mbwee mbwee

  • @feehasaidid.r.d
    @feehasaidid.r.d 13 годин тому +1

    Mawu okhala ndichilungamo mkati mwake ndithu pitilizani kuwawunikira anthu bwana

  • @AbdulrazaaqLeyani-k2i
    @AbdulrazaaqLeyani-k2i 5 днів тому +5

    True and lovely words

  • @user-cy9zp4fb2m
    @user-cy9zp4fb2m 5 днів тому +3

    Muli nzeru umu this audio shud reach to the state 🏠

  • @patrickndojime1632
    @patrickndojime1632 4 дні тому +1

    That's true i do respect your massage father keep it up i like the ward's you taling as

  • @user-lu8px7td6p
    @user-lu8px7td6p 5 днів тому +2

    God bless you pastor don't fear for that you know is no clear but to talk people to know

  • @OFG-th3st
    @OFG-th3st 22 години тому +1

    Iyiyi atiwonelele😂😂

  • @AndrewMukhwapa-qj4vo
    @AndrewMukhwapa-qj4vo 5 днів тому +1

    Thanks very much God bless you. Your talking the truth

  • @user-cq2gd5hc4v
    @user-cq2gd5hc4v 4 дні тому +1

    Zikumveka bwino ndithu kuchokera pa mawu amenewa boma la abusa a Chakwera lalepheradi. Zikufunika kusankha moyenera.

  • @WilliamBandaWili
    @WilliamBandaWili 4 дні тому +1

    Akanakhala wins chakwera akanangoimika manja chifukwa zinthu sizilibwino muno mu Malawi walephera yekha anthu chance anamupatsa

  • @AndrewMukhwapa-qj4vo
    @AndrewMukhwapa-qj4vo 5 днів тому +1

    Your talking the truth God bless you thanks very muh

  • @LilianKachala-yz2xf
    @LilianKachala-yz2xf 4 дні тому +1

    Takumvani Abusa

  • @martinmoyo4211
    @martinmoyo4211 4 дні тому +1

    Kudzudzula kulipamenepo koma inunso atsogoleri athu achikatolika mulindivuto. Timakonda kuloza chala anzathu koma ndichani timapangapo polithandiza bomalo.
    Tikati tiyang'anitsitse kumpingo kwathu inuyo atsogoleri a ntchito anunso simumawasala molongosoka mumalipiro. Mwachitsanzo a Gulupa samapatsidwa malipiro abwino komanso a ntchito ena. Ifenso tikonze gawo lanthu mpamene tidzizuzula enawa. You should also set good example in leadership. Zisakomere mbuzi kugunda galu.

  • @user-mj2te7vl6p
    @user-mj2te7vl6p 4 дні тому +1

    Thank you man of God

  • @kingsleymsampha2260
    @kingsleymsampha2260 5 днів тому +2

    Chilungamo chilibe zoti wochimwa ali momwemo ayi. Truth will remain and the wise will choose the right way to go. The foolish will blame the advice.

  • @TopoTopo-bm4vw
    @TopoTopo-bm4vw 5 днів тому +1

    Good advice thanks

  • @BressingsMahele
    @BressingsMahele 4 дні тому +1

    Powerful

  • @giftnyirongo-ey3qy
    @giftnyirongo-ey3qy 5 днів тому +2

    What an intelligent gentleman

  • @hamiltonsolomon3756
    @hamiltonsolomon3756 5 днів тому +1

    Well said......👏👏👏👏👏👏👏👏

  • @user-vu4cz1mt4f
    @user-vu4cz1mt4f 4 дні тому +1

    Zochezatu mukauze
    Tatopa ndimbuz izi
    Mpaka anthu aMulungu kuyamba kuwayankhulisa zandale chifkwa chakuononga ndalama mopusa

  • @clalesschisale3792
    @clalesschisale3792 5 днів тому +1

    Our next Bishop of blantyre archdiocese

  • @user-sb6by9sq5n
    @user-sb6by9sq5n 4 дні тому +1

    🙏🙏🙏🙏🙏

  • @JeanKambala-gm1zr
    @JeanKambala-gm1zr 4 дні тому +2

    Kodi abishop mawuwo basi antha siinu mikuyankhula ndimulungu wakutumani. Tikudikila titsegulenni maso ndi chilungamo

  • @kingsleymsampha2260
    @kingsleymsampha2260 5 днів тому +1

    Samuel told Saul kuti umfumu wanu wakanidwa. Ndiye abusa azingoti zakumwamba?? Kulowa kumwamba ndi umphawi aaaaah

  • @marryphili5419
    @marryphili5419 5 днів тому +1

    That's true pastor we need to use the brain life now is expensive

  • @KennethMchenga-j9c
    @KennethMchenga-j9c 5 днів тому +1

    Very true man of God

  • @mayesojameskatete
    @mayesojameskatete 5 днів тому +1

    Good speech ❤❤❤❤

  • @user-cy4pg1bo5o
    @user-cy4pg1bo5o 4 дні тому +1

    Ku bandura osaopa osafooka kkkk

  • @user-dy3iz1il1d
    @user-dy3iz1il1d 5 днів тому +2

    Oro muthalika a lowe mudzavutika chimodzimodzi musaone kuti akalowa Mutalika ndiye zinthu zisintha ayi mukuzinamiza kwambiri tiyeni tiziwelenga mau aMulungu atiuza zoona awatu ndi masiku otsiliza Buku lopatulika linanana kale kuti masikuotsiliza mudzaona nkhondo kukangana mu maiko osiyanasiya and munthu afzakonda ndalama not munthu nzake ndipo zinthu zambiri zidzakhala zokwera mtengo kwambiri ine ndakambako zokomo abale mwabuye

  • @MphatsoMvula-k6e
    @MphatsoMvula-k6e 4 дні тому +1

    Udatani umuwuza peter wakoyo mbuli ya mbusa iwelenge yohane 10 mbusa wakuba iwe

  • @Patricia_Chisankha
    @Patricia_Chisankha 4 дні тому

    Unenesko uli papa

  • @HedgensChisale
    @HedgensChisale 5 днів тому +1

    Ine ndinauza koma sakuva

  • @gabrielmulowe8481
    @gabrielmulowe8481 4 дні тому +1

    Anthu Ngati awa ndi amene timawacuna

  • @beakab2378
    @beakab2378 5 днів тому +1

    Well said

  • @PrinceKachimanga
    @PrinceKachimanga День тому +1

    i can vote for this pastor in 2025!..if he joins politics.Chakwera has failed this country..

  • @user-lw9su5om5z
    @user-lw9su5om5z 5 днів тому +2

    It's true that they failed

  • @user-gd7xm7xr9v
    @user-gd7xm7xr9v 5 днів тому +2

    Church silimakhala ndi anthu a opposition okha, mliso a m boma, ukulalika mosasamala utha kuyambanitsa anthu m MPINGO. Maka nthawi ya campaign tilimoyi.

    • @user-pn7cj9hb3t
      @user-pn7cj9hb3t 5 днів тому

      Kodi umafuna anene kuti zithu zilibwino zisali bwino? Taganizani kae bwinobwino amwene osathamanga poyakhula taonani kwa nthawi yoyamba anthu a Mulungu kuyankhulapo m'mene dziko likuyendera ndipo ndi ambiri zedi moti mukwanitsa kuwaletsa onsewo? Tadekhani inuyo ngati simukuona manvutowa khala phee muzingodyelera apa sakunena za campaign ayi koma kutsegula maso anthu amene akunvutika, ndipo idakakhala campaign in church bwezi pakunveka ena kumutsutsa pompo koma ngati akumuombera m'manja choncho ndekuti anthuwo akunvomerezana nazo zomwe munthu wa nzeruyu akuyankhula ku mpingo wa Mulungu. Dziwani kuti mudziko Mulungu adalenga anthu anzeru kuposa azitsogoleri anthuwa koma kuzichepetsa kokha kumapambanitsa so you better watch your mouth.

  • @KENETHMAJASA-ud5ee
    @KENETHMAJASA-ud5ee 5 днів тому

    Strong man of God

  • @EdsonKamwendo
    @EdsonKamwendo 5 днів тому +1

    Mbambande Father

  • @user-sr6hc3pv8o
    @user-sr6hc3pv8o 5 днів тому +1

    🙏🙏🙏🙏

  • @user-bd5kw8oq1r
    @user-bd5kw8oq1r 4 дні тому +1

    Popeza mwati ndi munthu wa Mulungu bola tamva koma sanafike kukhala mwana wa Mulungu popeza nayeso ndi wochimwa koma ndi wa bodza uyu Ngati kumpingo kwawo walephera ndiye alonze chala wina angoyesetsa nayeso kutukula dzikolino ndizofunika kugwilana manja koma mukalowetsa ndale ndi mu mpingo momwe ndiye Kuti tigwa tonse ndi nkhosa zomwe or iye sungayendetse dziko ife a DPP zinatikanika kale 😅😅😅

  • @IsaacMusa-py2jm
    @IsaacMusa-py2jm 5 днів тому +1

    Zamphanvu 🙏

  • @user-fd1tu6ku1r
    @user-fd1tu6ku1r 4 дні тому +1

    Chakwera ndi Tambala Wakuda anabwera kuzaononga Dziko lino

  • @user-dp7bc7yy6s
    @user-dp7bc7yy6s 5 днів тому

    Bg amenewo ndiye mau amphav zinthuzi zimafunika kuganiza mozama tisanasankhe otilamulira

  • @MarcosDjussa
    @MarcosDjussa 5 днів тому +1

    Mumakwanila fr 😂😂

  • @JosephAMoses-ne8ji
    @JosephAMoses-ne8ji 5 днів тому

    It is very true that they have failed

  • @DONNEXKhama-bk1gy
    @DONNEXKhama-bk1gy 5 днів тому +1

    Zochezatu😂😂😂😂😂 chilungamo

  • @AchinaKellz
    @AchinaKellz 5 днів тому +1

    Kukhala ngati kachilungamo

  • @user-gd7xm7xr9v
    @user-gd7xm7xr9v 5 днів тому

    Osati zocheza

  • @JamesMalango
    @JamesMalango 5 днів тому

    Ndiponso achepesanso mauwo

  • @Doreen-vw9ws
    @Doreen-vw9ws 4 дні тому +1

    Palibe chomwe amaziwa chipani chosaziwa economy chipani chomvesa chisoni

  • @RonicSouza-sk5ux
    @RonicSouza-sk5ux 5 днів тому +1

    Mau

  • @user-gd7xm7xr9v
    @user-gd7xm7xr9v 5 днів тому +1

    Sizocheza

  • @johnkambala692
    @johnkambala692 4 дні тому +1

    These are part of Malawi disaster

  • @user-ti8ds7iq8z
    @user-ti8ds7iq8z 5 днів тому +1

    Akumanganitu

  • @user-dy3iz1il1d
    @user-dy3iz1il1d 5 днів тому +1

    Uyu ndi wabodza anthu malo poti awauze anthuwa mau achipulumutso akupanga kampeni yandani inu mungafanizile dziko lamalawi la Mozambique or zambiya zambia ndi dzikolimene limagulitsa miyala ya mtengo wapatali komanso muli Ma boulder ambili amatolera ndalama zochuluka komanso kumalawi timabalana kwambiri sizigwiliza ndikuchepa kwadzikolo Mozambique kuli ma madoko awili amene ama bweletsa ndalama plus mogodi anthu amulungu ngati awa ndi amene amapangitsa kuti dziko lisamayende bwino chifukwa amaiwala mau aMulungu amayamba kulalikira ndale mudziko simungakhale m'dalitso ayi toyeni tizipemphera kuti mulungu afalitse Malawi zikomo

    • @user-un6qv6sj3h
      @user-un6qv6sj3h 5 днів тому

      Akunenatu chipulumutso kupulumutsa miyoyo ya anthu apulumuke kunjala kuumphawi kukukwera mitengo ya zinthu Kodi mau oti kupulumukawa amakamba zakumwamba kokha pepani ngati ndakulakwirani koma sitingamakambe zaulemelero ukudzawo pamene apapa anthu tikuvutika

  • @user-pl2lj6mh1z
    @user-pl2lj6mh1z 5 днів тому +1

    Ameen Ameen tikuvutika abale mulungu atikhululukile achakwela chonde mwachose ndithu

  • @MosesLeckson
    @MosesLeckson 5 днів тому +1

    Zoona zake

  • @SaidiMbawa-st6bj
    @SaidiMbawa-st6bj 5 днів тому +2

    Alomwe awa tazilarikilani za ufumu wa Mulungu

  • @PrinceKachimanga
    @PrinceKachimanga День тому

    inu a busa awa akulankhula chilungamo...MCP HAS brought misery in this country.and we are tired of mbuzi zimenezi

  • @YOMALO.
    @YOMALO. 5 днів тому +1

    This is a proof that MCP will reign again

  • @user-dy3iz1il1d
    @user-dy3iz1il1d 5 днів тому

    Uyu ndiwabodza zambia nayo ili pamavuto azachuma munthu wa mulunguyu ndiwabodza kwambiri

  • @victormasambuka8366
    @victormasambuka8366 4 дні тому

    Mu church mumakhala anthu azipani zasiyasyana sibwino kukamba za ndale mufzagawanittsa church as a pastor keep your opinion to yourself

  • @user-kt5bq2wg6v
    @user-kt5bq2wg6v 5 днів тому +1

    Simudayankhule bwino bispo. Munthu wamulungu sanayenera kutero

  • @ChisomoNthukwa
    @ChisomoNthukwa 5 днів тому +1

    Opusa ameneyi zikugwilizana bwanji ndiulaliki

  • @user-gd7xm7xr9v
    @user-gd7xm7xr9v 5 днів тому +2

    Iweso ukulalika zopusa, economics yakuti unaphunzira iwe, you do not compare zinthu zosiyana,, Mozambique ukuchita compare ndi Malawi, kapena Tanzania .... Just chinthu chimodzi like DOOKO,LA PA NYANJA ..... what it earns cannot compare ndi Malawi.Ukawauzenso nawe omwe akutumawo.

    • @marryphili5419
      @marryphili5419 5 днів тому

      Ngati ndiwe wa MCP wuzipase wulemu amalawi tilipa moto sitimasekesekerere ndi mbamva zimenezi

    • @user-pr4xk7wk6r
      @user-pr4xk7wk6r 5 днів тому

      Ndiwe opusa kwambiri ndi MCP yakoyo

    • @simeonbanda4240
      @simeonbanda4240 5 днів тому

      Umva pheni wa MCP ulendo uno

    • @johnchrispine3949
      @johnchrispine3949 4 дні тому

      Point ndiyonena kuti, zinthu zochepa zomwe tili nazo tizigwirisa ntchito bwino.

  • @HarryKandani
    @HarryKandani 5 днів тому +1

    Anthu oipa inu ndi inu nomwe munali pastogolo kulemba ma kalata kuuza anthu kuti avotele agule wa

  • @paulmanyamba5437
    @paulmanyamba5437 5 днів тому +2

    Akulu mulungu adzikusogolelani mukuyankhula chilungamo ngati munthu wamulungu