Times Exclusive with Lucius Banda - 17 December 2022

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 1 жов 2024
  • Times Exclusive with Lucius Banda - 17 December 2022

КОМЕНТАРІ • 138

  • @ericbishopjere4494
    @ericbishopjere4494 7 місяців тому +8

    This was nice interview. I grow up listening to Lucius Banda's music & I like almost them all.

  • @SYLVESTERKAMAU-i1b
    @SYLVESTERKAMAU-i1b 6 місяців тому +5

    Am Zambian, but I have fallen in love with your program.❤❤❤❤

  • @ayamijackson1443
    @ayamijackson1443 Рік тому +9

    Umuthu wachibadwidwe umakhala opindulila aliyese ngakhale mulungu amakondwela nazo well done Mr banda God bless you

  • @samuelkamwendo5845
    @samuelkamwendo5845 Рік тому +6

    I think Lucius is better posotioned to be government spokes person than ajawo ndithu.

    • @falliotphiri688
      @falliotphiri688 Рік тому

      Munthu ngati Lucius is not a good person to a Government spokesperson,,, udindo umene uja umafunika anthu abodza ngati Gospel Kazako...Lucius is too straight, and honest

  • @chrispindambula4921
    @chrispindambula4921 11 місяців тому +1

    Koma munthu amene anganyonze Lucius Banda ndi munthu otembeleredwa. Lucius ndi Paul ndi anthu ofunika kwambiri mu mbiri ya dziko la Malawi kumbali ya music yomwe ndi gawo la chikhalidwe chathu. Adayamba kutukula nyimbo ku Malawi ndi baba amenewa. Munyengo imeneyi tikuyenera kuwapemphelera kwambiri kuwaonetsera chikondi.

  • @IamPenjani
    @IamPenjani Рік тому +8

    The Legend, well spoken sir. May God give you more grace and Good health

  • @mordecaikachale2497
    @mordecaikachale2497 Рік тому +5

    Mr Lucius Ur so intelligent keep the 🔥 burning.

  • @gvtl7201
    @gvtl7201 Рік тому +4

    Brian Banda ndi lucius Banda Agogo awo ndiamozi😂😂😂😂😂

  • @yamikanivictorkawaye9182
    @yamikanivictorkawaye9182 Рік тому +11

    Legends met and well composed questions were been answered constructively.

  • @muchanakasichi5492
    @muchanakasichi5492 Рік тому +3

    I like this guy Banda from Times tv for asking good questions

  • @jezalakaphuka7325
    @jezalakaphuka7325 3 місяці тому

    Interview koma imeneyi akanakhala ena mukanamva akuyankha za a president..... Under the dynamic leadership of fwe fwe fwe.... Lost the big brain

  • @vukanifracksonchinkonde7324
    @vukanifracksonchinkonde7324 Рік тому +3

    Lucious Banda....Get healed in Jesus name.personally I love you sir

  • @newtonsindo5952
    @newtonsindo5952 Рік тому +4

    Lucius has convinced me

  • @RABSONSIKELO
    @RABSONSIKELO 2 місяці тому

    Apatu Soldier unagonjetsa Brian kkk pankhan yabwatoyii

  • @hashimmtelera9536
    @hashimmtelera9536 Рік тому +8

    I like the way he was answering the questions,he is very brilliant

  • @charlesphiri9710
    @charlesphiri9710 Рік тому +2

    Koma Brian!!!!!! Iwe ndiwe munthu ofunika kwambiri

  • @davisghambi7424
    @davisghambi7424 Рік тому +1

    I pity the situation Lucius and his family are going through, but by saying the current government is better placed to helping Malawians is a fallacy. Things have worsened when we were promised Canaan. Start fighting for the poor as you used to and if being part of the government is making you fail to do so, then quit so that you maintain your legacy. Otherwise, wishing you full recovery .

  • @chrispindambula4921
    @chrispindambula4921 11 місяців тому +1

    Mau anzeru Lucius: As citizens, we need to reflect on ourselves to deal with our individual weaknesses rather than always pointing fingers at political leaders. My addition to his point is this: If you don't do something to improve your own living standard, no one else will.

  • @AlgentChilanga
    @AlgentChilanga 2 місяці тому

    Pankhani yabwatoyi pamenepo Brian Banda wasimikiza kuti ochimwenewa he is very clever like ok onsewa ndi adabanda amaziwana wonse ndi amodzi apapa Brian anakumaniza ndithu 😂😂😂.RIP solder L.Banda great wise from you

  • @okoma247
    @okoma247 3 місяці тому

    I don’t like the Interviewer

  • @AbuHafswa
    @AbuHafswa 2 місяці тому

    Ku balakako kuli anthu odziwa kulankhula osati mabwatabwata uh
    Mmmmmmmm

  • @PrinceKachimanga
    @PrinceKachimanga 2 місяці тому

    lucious was a wise..rip😢

  • @bonfesszinkomola6552
    @bonfesszinkomola6552 Рік тому +3

    Wishing the legend well

  • @Prianka567
    @Prianka567 Рік тому +2

    Get well soon and u are really a fighter

  • @lamecklipenga855
    @lamecklipenga855 Рік тому +3

    Powerful points by Lucius and massive questions from Brian Banda, God bless you all.

    • @PedroChachoca
      @PedroChachoca 7 місяців тому

      Thanks broh for your congrats

  • @harrischiwalo5263
    @harrischiwalo5263 2 місяці тому

    Brian went off

  • @MarthaBanda-b8j
    @MarthaBanda-b8j 2 місяці тому

    😢😢😢😢😢 rip

  • @jamestonechiposa6568
    @jamestonechiposa6568 Рік тому +2

    Nice interview. Yobebatu

  • @blessingsmunthali9202
    @blessingsmunthali9202 Рік тому +3

    👍👍💥

  • @kingsleysabola3737
    @kingsleysabola3737 Рік тому +2

    God bless you soldier your the icon

  • @JamesMphingah
    @JamesMphingah Місяць тому

    Anali ndi masomphenya😢😢

  • @johnkamwendo2742
    @johnkamwendo2742 Рік тому +2

    Koma brain Banda ndimakuyamika ulibe ubale

  • @AtupeleKozani-q6m
    @AtupeleKozani-q6m 3 місяці тому +1

    Lucius banda he talk reality 😢

  • @abdulmoosah4309
    @abdulmoosah4309 Рік тому +1

    Lucius is talking from experience he knows what he's talking about exposing people whose stilling doesn't mean you helping people of malawi anthu sakufuna kumva zakumangidwa kwa anthu pomwe anthu akulephela kugula feteleza komanso chakudya DPP imaba UDF imaba koma sizinali chonchi ndipo anthu anali busy kulongosola zawo osati zamboma koma panopa anthu daily kumangkamba zokazokazo chakwela ndamene ali pasogolo pa anthu akuba Lucius akudya ndi chakwera sangakambe zachabe za chakera mr Lucius thank you for failing malawians keep eating the money and enjoy with your family but one day you will need them thank you

  • @beezboi1050
    @beezboi1050 4 місяці тому +1

    The greatest musician who ever lived

  • @chimwemwechiundira6002
    @chimwemwechiundira6002 Рік тому +2

    Loved this conversation

  • @dennissaiwala9405
    @dennissaiwala9405 Рік тому +2

    I have enjoyed this

  • @flonekamwendo506
    @flonekamwendo506 Рік тому +2

    God bless our Legends Lucius

  • @DJMND1234
    @DJMND1234 Рік тому +1

    Honestly speaking Brian Banda ali bwino kwambili ndipo ntchito amayidziwa. 👍

  • @patricknthakomwa5613
    @patricknthakomwa5613 Рік тому +1

    Well spoken Mr Lucious Banda....

  • @goldenbanda1612
    @goldenbanda1612 Рік тому +1

    Kkkkkkk zinazo a Brian mumatisangalasa ambuye akudaliseni mafuno abwino kwa mr Lucius Banda

  • @zamadulasimango6972
    @zamadulasimango6972 Рік тому +1

    So genuine! Humble personality, kind heart. You are loved Angoni!!

  • @rahimmapata545
    @rahimmapata545 Рік тому +1

    Lucius Banda ndizowonadi anthu ena anali m'boma angasangalala ndiye yeyo pano ali m'boma ayenela asangalale koma sangapange nawo katangale kulankhula kwabwino kwambiri

  • @v2-kaj
    @v2-kaj Рік тому +2

    Wishing the legend well.

  • @leonardjika2100
    @leonardjika2100 Рік тому +1

    A NEW VERSION WILL GOVERN OUR LAND SO HELP ME GOD

  • @ceciliamwango1792
    @ceciliamwango1792 Рік тому +2

    Kuyankhula kwanzeru lucius.

  • @ausmanebrino6134
    @ausmanebrino6134 Рік тому +1

    Legend

  • @BusiBusisiswe
    @BusiBusisiswe 11 місяців тому +1

    Mr lucius very good 🔥🔥🔥❤❤❤🙏

  • @chifundonkhoma3642
    @chifundonkhoma3642 Рік тому +1

    Lucius Banda umatha kuganiza, maliro akwanu musandikakamize kulira 😂😂😂😂

  • @hamdanmasuku4800
    @hamdanmasuku4800 Рік тому +1

    Mulungu azikudalitsan Mr chicco Banda

  • @vukanifracksonchinkonde7324
    @vukanifracksonchinkonde7324 Рік тому +2

    Brian you are genuine.

    • @bobkenneth2947
      @bobkenneth2947 Рік тому

      Mulungu ayendere family ya Banda pa zomwe akudutsamo i like the close relationship between Lucius and Paul long live our legends

  • @ChisomoNoel
    @ChisomoNoel Місяць тому

  • @sophiejailos
    @sophiejailos 2 місяці тому

    Chonena ndilibe soldier 😭😭 only God knows why may your soul rest in peace 😢

  • @russell4527
    @russell4527 Рік тому +2

    So there is no one to give this guy a kidney, shame on us, he deserves love, a kidney donation !!!

  • @enricohmw
    @enricohmw Рік тому +1

    Ok

  • @shukuranichinthenga236
    @shukuranichinthenga236 Рік тому +1

    Brian Banda weyo nd Dolo kwambili keep it up ❤

  • @Q_Aura
    @Q_Aura Рік тому

    😂😅😂😂 Koma Brian
    Onelove to the highest degree

  • @DanielDuwe-tc9py
    @DanielDuwe-tc9py 2 місяці тому

    Ambuye akanamapeleka mwai wachiwiri padziko pano mmm,mhsrp Lucius...

  • @SydreckMphamba
    @SydreckMphamba 10 місяців тому

    someone who knows how to talk in public, You impress me Angozo

  • @JoshuaNkhoma-u1i
    @JoshuaNkhoma-u1i 6 місяців тому

    Amalawi timakhulupilira kulima ndiye ngati boma likukweza zipangizo zaulimi dziko likwera bwanji?

  • @DawsonKabotolo-fw3ur
    @DawsonKabotolo-fw3ur Рік тому

    Good point , we are to look ourselves as amalawi and solve our concerns (issues)

  • @oloratosolomon
    @oloratosolomon Рік тому

    Kunena zoona kumapeto Kwa mawu afusa fuso labwino koma Iwo ndimunthu mozi analiwosayamika Bingu anali sogoleri wabwino kumalawi koma sanamike analowesa ndala Lucie's

  • @RABSONSIKELO
    @RABSONSIKELO 2 місяці тому

    May Allah Bless U Sir Soldier

  • @jonathankumalasa
    @jonathankumalasa 2 місяці тому

    Rest well soldier 💔

  • @muhabaulen7912
    @muhabaulen7912 Рік тому

    Kkkkk pano ndi soja wamabwana atsatinamidze Lucius Ali mugulu lakubanawo ndipo palibe chadzeru chimodzi chomwe wakamba

  • @angelicajoseph3080
    @angelicajoseph3080 Рік тому +5

    Thanks forr bringing Mr Lucius Banda , we had missed him. Very intelligent man, am impressed.

  • @johnw.posomanchanel4023
    @johnw.posomanchanel4023 Рік тому

    a Lucius akunamatu apa, yankhani bwinobwino funso loyamba ndi ili likuba ndi liti?

  • @frankmauzauza3819
    @frankmauzauza3819 Рік тому

    kd mukamat boma la New 1 mukutathauza chan ? boma lot latha 3 yrs likhala bwanj ! la New 1 ?

  • @erickhowoya9894
    @erickhowoya9894 Рік тому +4

    Our own musical legend Lucius Banda, answering questions convincingly

  • @Hamidah-g2o
    @Hamidah-g2o 8 місяців тому

    Makwana Banda mupangeso interview ndi nomani chisale

  • @hosema9376
    @hosema9376 Рік тому

    kkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkk koma adha Brian ase akut Lucius akuyakhula ndie uti

  • @BlessingsMhone-lg4ux
    @BlessingsMhone-lg4ux Рік тому

    Where can I get a CD in Mzuzu

  • @carlosalexandreantonio1632
    @carlosalexandreantonio1632 Рік тому

    Kuyankha mafuso mwazeru ndithu, zinthu zabwino zedi.

  • @millionsenenje5010
    @millionsenenje5010 Рік тому

    Munthu mulala kkkkk' maliro akwanu musandikakamize ine kulira

  • @montmphepo3662
    @montmphepo3662 Рік тому

    Maliro a kwanu musakakamize ena kulira... although we are moving from bad to worse

  • @blessingkamanga1781
    @blessingkamanga1781 Рік тому +3

    Thank you Brian and Lucius Banda. Powerful discussion

  • @giftaustin68
    @giftaustin68 6 місяців тому

    Lucius Banda is so wise

  • @QueenTowela
    @QueenTowela 4 місяці тому

    Very intelligent

  • @martinjonam8237
    @martinjonam8237 Рік тому +3

    The way i I love this man im crying 😪😪

  • @richmanjimmy271
    @richmanjimmy271 Рік тому

    NKHANI YOVEKA BWINORUSIYA BANDA TANKHUDZIDWA TOSE

  • @ChristopherKamalizeni-dd6lp
    @ChristopherKamalizeni-dd6lp 6 місяців тому

    Following

  • @ancientnkhata1137
    @ancientnkhata1137 Рік тому

    He is intelligent and wise

  • @maluli5691
    @maluli5691 Рік тому

    Lucius umakhwana

  • @ayandajack6019
    @ayandajack6019 Рік тому

    Brian u know how to ask .kkkkkkk

  • @JojoTyres
    @JojoTyres 3 місяці тому

    Koma Brian banda mmmmm amakakamilatu

  • @CalebeGOLOSI-yp6rc
    @CalebeGOLOSI-yp6rc Рік тому

    I love cos

  • @KayMissinga-hx2js
    @KayMissinga-hx2js 7 місяців тому

    Legend ❤

  • @peterbanda7003
    @peterbanda7003 Рік тому

    Brain aaaaa ndiwachipongwe koma anafunsa mafunso omveka kwabasi

  • @blessingsgeoffrey9414
    @blessingsgeoffrey9414 3 місяці тому

    Rip soja

  • @mrkanyongomrkanyongo
    @mrkanyongomrkanyongo Рік тому

    P

  • @amoschisisi2070
    @amoschisisi2070 Рік тому

    You ate MLAKA MALIRO's money

  • @princembwana9708
    @princembwana9708 Рік тому

    Mr soldier wa amphawi mumatiimila humble number.

  • @kelvinsambo5450
    @kelvinsambo5450 Рік тому

    Nice

  • @victorbanda9039
    @victorbanda9039 Рік тому

    Kulankhula moona mtima ndithu ulemu wanu big

  • @rahimmapata545
    @rahimmapata545 Рік тому

    Lucius atha kuwina ngati wayimila udf anakawina

  • @kachingwefurayide6550
    @kachingwefurayide6550 Рік тому

    Masaka kids

  • @austinharry4135
    @austinharry4135 Рік тому

    Apa timat Njobvu Zakumana

  • @AlexeversonNdilowelela
    @AlexeversonNdilowelela 9 місяців тому

    Obrigado

  • @Hamidah-g2o
    @Hamidah-g2o 8 місяців тому

    Brian ndiye umaseka eeee

  • @paulpaseli6310
    @paulpaseli6310 Рік тому

    Tililadi mosiya bwana takuvani ok