Agape khombe amandibowa bwanjii eish!, i dont feel good wen i heard names like agape, kumkuyu, chimwendo, chakwela, zikhale, yolamu, vetino phiri, pter kalaya, billy malata, layitoni mangochi, ben longwe too many to mention
Mulungu akuulura chinachilichonso ku dziko langa koma vuto dziko langa linasankha kusamva koma limamva china chake chitachitika...Ambuye athandize Malawi
Amalawi let’s gather together and fight like our fell Kenya’s bakili tv and Limpopo fm thy are doing there parts ife tonse tikutani kapena yathu ija ya Ulemu???
Eyetu ameneyo nde mulungu inuyo ngati mukukwanitsa kutseka anthu pakamwa ndindalama ndiomwewo opusa osusuka achina yudasi Ana anjoka inuuuuu Malawi mizimu yambiri ikuzunzika kusowa chisamaliro zinthu zinakwera kuli okalamba Ana amasiye nzipatala kundende ndi anthu onseee mdzikomu ofuna zabwino koma ayi zikuvuta kwacha mwagwetsa mwagwetsanso ma million mukukhonyolera m'matumba mwanu kukhutisa mimba zanu Nde pemphero la olira ovutika Mulungu samalisiya amayankha mwachangu nde anthu ayamba kugwidwawa nchiyambi chowululika zinsisi zanu I'm repeating all most each and every day kuti you will pay one by one I'm not just taking this is prophetic word Mulungu ndiokwiya nanuuuuuu anthu amagazi m'manja inu
Munandisangalasa yomweo chikangawa❤️❤️❤️🇿🇦🇿🇦🇿🇦🇿🇦 osavera Riiimpopo ndi ndimakhala ngati ndataya kofunikila
Ndipo kwambiri tu mmm
Koma ntanyiwa. Respect to you May the almighty God protect you wherever you will go
Keep up the good work comrade 💪💪
Ulemu wanu comrade Ntanyiwa.
Salute comrade ntanyiwa,we love you and all Limpopo FM
Limpopo FM live from south Africa Durban Pietermaritzburg auzeni zoona amenewa
Ulemu wanu big mani mmatimvesa kukoma kwambili god bless you all the time ❤❤❤❤❤❤
Ntanyiwa and your fellow comrades excellent well done, and keep it up for the battle you are fighting for Mw nation
Respect bwana Ntanyiwa 🔥🔥🔥
Panopa ine ndinasiya kuvela ma redio ena panopa ndili limpopo yokha basi
My brother your number one keep it up
Ine mchifukwa chake ndinakana ntchito ya usilikali ndiyapolisi coz fans ya madepartiment amenewa ndiyombwambwana kwambiri, zigawenga zaku Israel and Ruanda zikungolowa mdziko mwathu ngat zikulowa mmanyumba mwawo, chomvesa chisoni kwambiri ndichoti asilikali ndi apolisi angoti vyooooo , vyooooo , osapangapo kanthu
Dzitsiru
Antuwo zisilu kwabasi ...Antanyiwa gwilani nchito blo❤
Mtanyiwwa ulemu wanuw mulungu asinkuphasa moyyo wabwinno ndawi sonse I pray for you all the time amalawi tili phamoto 🤲🤲🤲🙏🙏🙏mulungu dalisani Malawi
Tikuziwa zambiri GUYS mmmm Limpopo FM ndikatundu number 1
Ulemu wanu from Limpopo south Africa 🇿🇦
Agape khombe amandibowa bwanjii eish!, i dont feel good wen i heard names like agape, kumkuyu, chimwendo, chakwela, zikhale, yolamu, vetino phiri, pter kalaya, billy malata, layitoni mangochi, ben longwe too many to mention
Chifukwa iyeyu..akupanga zinthu zomwe south African ikhoza kukwiya nanzo.zomwe zingaikidze miyoyo yanthu ife amalawi pa chiswe😢
Mumatiimirira acomrade timakunyadilani❤
Tafika ndithu kuzamvera our very own limpopo Fm
Am with u Ntanyiwa ahoi!!!From Soweto,osawopa
Buddy Ntanyiwa ‼️
Always proud of you ♥️🔥
I salute you comrade, you are genius
God's good always Amen
Mtanyiwwa osawopha mulungu adalise inuyyo mulungu adalise inuyyo nosse
Comrade ntanyiwa mulungu azikupasa moyo wautali azikusogolera ndipo mupitiliza kuti pasila choona chamalawi Allah azikuteteza kulikose ukuyenda Limpopo FM ndimanyoya nayo ndikamavera
God bless you comrade
May good God knows everything and palibe chingabisike Mulungu ateteze malawians
Mtanyiiwa mulungu azikutetezani polowa ndipotuluka
God bless you ❤
Even Tv,Radio stations in Malawi are getting lessons though they are silent bravo
🔥🔥🔥🔥Ana Wachepa awa Zina amangoziyambadi...
Limpopo inabwera kuzakhala
Wailesi yokhayo yomwe ambiri akuikonda kunvera panopa
Ndikuuza girl
Ndili pambuyo pako mtanyiwa
Tinakusowan Mr Mtanyiwa muli bwanji kumeneko kuno tili bwino ndithu
27:11 ❤❤❤❤❤
We need some more teachings brother man !!
Respect to you bro nthanyiwa keep the 🔥 buuuuuu
It's only champion station in limpopo fm
Chikangawa Ali madzi😅😅😅
Kkk
Mulungu akuulura chinachilichonso ku dziko langa koma vuto dziko langa linasankha kusamva koma limamva china chake chitachitika...Ambuye athandize Malawi
Mulungu wayitenga nkhondo imeneyi kukhala yake ndipo palibe yemwe angamenyane ndi MULUNGU.
OKHA OKHA A MCP AMENYANA NDIPONSO AWULULANA POSACHEDWAPA. IFE TINGOTI PHEEEEEE KUDIKIRA
Limpopo FM is number one
God bless you mr ntanyuwa ❤❤❤
🎉🎉🎉 to Limpopo FM
Yomwey gulu iwe
Chakwela sawina wapangila ena kapeni
Ndipo kwambiri tu mmm
Zoonadi brother mtanyiwa ifetinapanga mistake kuvotera Chakwera ndigululake komano chakwera aziwekuti wasalandi madzi amodzi
Pangolin ..ntanyiwa ....
Kkkkkkkkkk yomwe mwaiputayo chakwera ikuphulikikani
Ntanyiwa more 🔥🔥🔥🔥🔥 fire
Achita bwino 😂😂😂arirata😂😂
Limpopo fm ❤
Mutitumizire zithunzi za anthu omwe agwidwa ku South Africa.
Comrade umakwana bigup
Musalimbane ndi manyi woo aaaa muti asilikali alikuti??
Agalu osaziwa ntchitowo? ntchito zigololo bas.
ife tiibe ma ninja mmalawi muno aaaa
Great Job Ntanyiwa
God be with u brother
Ulemu wanu Comrade ❤
Tchimo limayitana Lin,zache
Yomwey galu iwe umakwan
Guz Malawi ndiwatu if anyone ali okudzidwa ndikulephera kwa Chakwera tiyen paunsewu tonse pa 10 July
Inde bwana wathu❤❤❤
Mcp ikupanga zinthu zoopsyeza kwambiri ndipo zamdikwana mmmh
LIMPOPO FM PALIBESO IFE TINGOTI NYADU
Amalawi let’s gather together and fight like our fell Kenya’s bakili tv and Limpopo fm thy are doing there parts ife tonse tikutani kapena yathu ija ya Ulemu???
Not ulemu as such bro, amalawife ndombwambwana kwambiri man, mtanyiwa and bakili muluzi tv alongside bon Kalindo are doing their part for sure
Respect for you
boma la zitsiru apolice army chakwera mitumbo ya chamanu
Pa 10 akuchoka bas
Osasiya kunena zowona
Be blessed
Mumakwana ❤
Zigawenga zosadziw dziko akadziwe munthu ali kudimba zoon
Pitilizani Bigy kubweretsa poyera zobisika kuti tiwachotse ose mwake muno.
Be protected sir
😂😂😂😂😂😂😂musandikomole antanyiwa ine lero Koma kulizithuuuu 😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂
Walemphela udindo
Namu bwana mumata ❤
Koma braz mumakwana athawa a mcp
Our channel Malawian channel we love you comrade together with your people ❤❤❤
Mcp mulungu walange ndinthu ndipo apange kanthu mudzina layesu akutitenga ngat chisiru ndinthu
Mumakwana ntanyiwa
Ndipo anapa chilima ndi ameneyo lelo chikuza mawu ndi iyeyo aziwona ndithu atule pasi udindo
😂😂😂
26:37
Limpopo ndi katundu uyu😂😂😂😂
Ife kuno ku South Africa kungochotsedwa chifukwa Cha zomwe akupanga chakwela😢azaona konko ku Malawiko zomwe tizapange
Koma athu aku mcp mulungu achitepo kathu
Bambo mu mtanyiwa ulemu ndi wanu mulungu apitirize kukuyang'anirani
Tipangeni ad ku group please
Kkkkkkkk koma amalawi ena ndinu omvetsa chisoni basi muli Limpopo ndi 1ndi maboza amalwi polani moto please mijedu khani zongopeka anthuni mudzachangamuka liti abale
Ukugona ndiweka
Chakwera wamupa chilima kuvuna akhale president galu kwabas
Eyetu ameneyo nde mulungu inuyo ngati mukukwanitsa kutseka anthu pakamwa ndindalama ndiomwewo opusa osusuka achina yudasi Ana anjoka inuuuuu
Malawi mizimu yambiri ikuzunzika kusowa chisamaliro zinthu zinakwera kuli okalamba Ana amasiye nzipatala kundende ndi anthu onseee mdzikomu ofuna zabwino koma ayi zikuvuta kwacha mwagwetsa mwagwetsanso ma million mukukhonyolera m'matumba mwanu kukhutisa mimba zanu
Nde pemphero la olira ovutika Mulungu samalisiya amayankha mwachangu nde anthu ayamba kugwidwawa nchiyambi chowululika zinsisi zanu
I'm repeating all most each and every day kuti you will pay one by one
I'm not just taking this is prophetic word
Mulungu ndiokwiya nanuuuuuu anthu amagazi m'manja inu
South Africa ikangomuphulisa wagule uja basi, walowa mkati mwana wang'ona ameneyu
Chakwera woyeeeeeee! Mutu waima, ndipo a Malawi tisalole zopusa
Yomweyo chikangawa
Kodi agapeyu ndindani nanga tundu wanji wamunthu ku malawi kuno agalu kwabasi ndi MCP yawoyo
Ulemu wanu sir
Auze zoona a Malawi iwe umakwana ndipo ndimachita kukuika PA Bluetooth kut maneba amve nawo kkkkkk
😂😂😂😂😂
😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂
umachita bwino
❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤
Ndipo galu ameneyu akukakamila pampando chifukwa chani mfiti yokupha ngati imeneyi palikundu peni