LIMPOPO FM 05 JULY 2024 NDI COMRADE NTANYIWA, ANTHU OSAZIWIKA BWINO ANAPEZELEDWA MALO OGONA ALENDO

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 3 жов 2024

КОМЕНТАРІ • 190

  • @LoydKamtedza
    @LoydKamtedza 3 місяці тому +5

    Munandisangalasa yomweo chikangawa❤️❤️❤️🇿🇦🇿🇦🇿🇦🇿🇦 osavera Riiimpopo ndi ndimakhala ngati ndataya kofunikila

  • @MiddayDeleza
    @MiddayDeleza 3 місяці тому +20

    Koma ntanyiwa. Respect to you May the almighty God protect you wherever you will go

    • @petroszgambo9949
      @petroszgambo9949 3 місяці тому

      Keep up the good work comrade 💪💪

    • @BeliLikhola
      @BeliLikhola 3 місяці тому

      Ulemu wanu comrade Ntanyiwa.

  • @eliasMwamba-q5f
    @eliasMwamba-q5f 3 місяці тому +3

    Salute comrade ntanyiwa,we love you and all Limpopo FM

  • @ImanRashidi-so4oo
    @ImanRashidi-so4oo 3 місяці тому +3

    Limpopo FM live from south Africa Durban Pietermaritzburg auzeni zoona amenewa

  • @mustafailanga2585
    @mustafailanga2585 3 місяці тому +2

    Ulemu wanu big mani mmatimvesa kukoma kwambili god bless you all the time ❤❤❤❤❤❤

  • @bytonalfred5844
    @bytonalfred5844 3 місяці тому +2

    Ntanyiwa and your fellow comrades excellent well done, and keep it up for the battle you are fighting for Mw nation

  • @Musa1828-l5d
    @Musa1828-l5d 3 місяці тому +2

    Respect bwana Ntanyiwa 🔥🔥🔥

  • @yusufbakali
    @yusufbakali 3 місяці тому +4

    Panopa ine ndinasiya kuvela ma redio ena panopa ndili limpopo yokha basi

  • @Jimmy-m4z
    @Jimmy-m4z 3 місяці тому +1

    My brother your number one keep it up

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 3 місяці тому +4

    Ine mchifukwa chake ndinakana ntchito ya usilikali ndiyapolisi coz fans ya madepartiment amenewa ndiyombwambwana kwambiri, zigawenga zaku Israel and Ruanda zikungolowa mdziko mwathu ngat zikulowa mmanyumba mwawo, chomvesa chisoni kwambiri ndichoti asilikali ndi apolisi angoti vyooooo , vyooooo , osapangapo kanthu

  • @jamiajafali6619
    @jamiajafali6619 3 місяці тому +2

    Antuwo zisilu kwabasi ...Antanyiwa gwilani nchito blo❤

  • @esaMoha-dm4kj
    @esaMoha-dm4kj 3 місяці тому +2

    Mtanyiwwa ulemu wanuw mulungu asinkuphasa moyyo wabwinno ndawi sonse I pray for you all the time amalawi tili phamoto 🤲🤲🤲🙏🙏🙏mulungu dalisani Malawi

  • @DeenesNurudMeke
    @DeenesNurudMeke 3 місяці тому +1

    Tikuziwa zambiri GUYS mmmm Limpopo FM ndikatundu number 1

  • @ibrahimalex7137
    @ibrahimalex7137 3 місяці тому +1

    Ulemu wanu from Limpopo south Africa 🇿🇦

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 3 місяці тому +2

    Agape khombe amandibowa bwanjii eish!, i dont feel good wen i heard names like agape, kumkuyu, chimwendo, chakwela, zikhale, yolamu, vetino phiri, pter kalaya, billy malata, layitoni mangochi, ben longwe too many to mention

  • @EyobeAyala
    @EyobeAyala 3 місяці тому +2

    Chifukwa iyeyu..akupanga zinthu zomwe south African ikhoza kukwiya nanzo.zomwe zingaikidze miyoyo yanthu ife amalawi pa chiswe😢

  • @HanaNyasulu
    @HanaNyasulu 3 місяці тому +1

    Mumatiimirira acomrade timakunyadilani❤

  • @zimmekapachika6784
    @zimmekapachika6784 3 місяці тому +1

    Tafika ndithu kuzamvera our very own limpopo Fm

  • @HappyMaolid
    @HappyMaolid 3 місяці тому

    Am with u Ntanyiwa ahoi!!!From Soweto,osawopa

  • @DaveDambo
    @DaveDambo 3 місяці тому

    Buddy Ntanyiwa ‼️
    Always proud of you ♥️🔥

  • @lyiemax
    @lyiemax 3 місяці тому +1

    I salute you comrade, you are genius

  • @lottiempata2487
    @lottiempata2487 3 місяці тому +1

    God's good always Amen

  • @esaMoha-dm4kj
    @esaMoha-dm4kj 3 місяці тому +2

    Mtanyiwwa osawopha mulungu adalise inuyyo mulungu adalise inuyyo nosse

  • @LoydKamtedza
    @LoydKamtedza 3 місяці тому +1

    Comrade ntanyiwa mulungu azikupasa moyo wautali azikusogolera ndipo mupitiliza kuti pasila choona chamalawi Allah azikuteteza kulikose ukuyenda Limpopo FM ndimanyoya nayo ndikamavera

  • @Angolnanjilayusufu
    @Angolnanjilayusufu 3 місяці тому

    God bless you comrade

  • @ChikumbutsoJohn-rs4tt
    @ChikumbutsoJohn-rs4tt 3 місяці тому +2

    May good God knows everything and palibe chingabisike Mulungu ateteze malawians

  • @RoseMalidadi
    @RoseMalidadi 3 місяці тому +1

    Mtanyiiwa mulungu azikutetezani polowa ndipotuluka

  • @charlesjimu6054
    @charlesjimu6054 3 місяці тому +1

    God bless you ❤

  • @StevenFombe
    @StevenFombe 3 місяці тому

    Even Tv,Radio stations in Malawi are getting lessons though they are silent bravo

  • @eliffagondewe8214
    @eliffagondewe8214 3 місяці тому +1

    🔥🔥🔥🔥Ana Wachepa awa Zina amangoziyambadi...

  • @PETERSINKADZIWA
    @PETERSINKADZIWA 3 місяці тому +2

    Limpopo inabwera kuzakhala

  • @RachealHarawa-xc9gs
    @RachealHarawa-xc9gs 3 місяці тому +2

    Wailesi yokhayo yomwe ambiri akuikonda kunvera panopa

  • @LazarusStanford
    @LazarusStanford 3 місяці тому +2

    Ndili pambuyo pako mtanyiwa

  • @MerryWayson
    @MerryWayson 3 місяці тому +1

    Tinakusowan Mr Mtanyiwa muli bwanji kumeneko kuno tili bwino ndithu

  • @philonampha
    @philonampha 3 місяці тому +1

    27:11 ❤❤❤❤❤

  • @kubengovender6996
    @kubengovender6996 3 місяці тому

    We need some more teachings brother man !!

  • @SindawaPelekamoyo
    @SindawaPelekamoyo 3 місяці тому

    Respect to you bro nthanyiwa keep the 🔥 buuuuuu

  • @yusufbakali
    @yusufbakali 3 місяці тому +1

    It's only champion station in limpopo fm

  • @MervisYobe
    @MervisYobe 3 місяці тому +2

    Chikangawa Ali madzi😅😅😅

  • @GospelSoldiers-sr7np
    @GospelSoldiers-sr7np 3 місяці тому +1

    Mulungu akuulura chinachilichonso ku dziko langa koma vuto dziko langa linasankha kusamva koma limamva china chake chitachitika...Ambuye athandize Malawi

  • @ChimwemweKondowe-nj4lx
    @ChimwemweKondowe-nj4lx 3 місяці тому +2

    Mulungu wayitenga nkhondo imeneyi kukhala yake ndipo palibe yemwe angamenyane ndi MULUNGU.
    OKHA OKHA A MCP AMENYANA NDIPONSO AWULULANA POSACHEDWAPA. IFE TINGOTI PHEEEEEE KUDIKIRA

  • @HannahMwazinva
    @HannahMwazinva 3 місяці тому

    Limpopo FM is number one

  • @RobertLuka-wy9cl
    @RobertLuka-wy9cl 3 місяці тому

    God bless you mr ntanyuwa ❤❤❤

  • @EmanMiles
    @EmanMiles 3 місяці тому

    🎉🎉🎉 to Limpopo FM

  • @LiyayaNyamula-j3b
    @LiyayaNyamula-j3b 3 місяці тому +1

    Yomwey gulu iwe

  • @MaxwellManual
    @MaxwellManual 3 місяці тому +4

    Chakwela sawina wapangila ena kapeni

  • @HallimaMakwinja
    @HallimaMakwinja 3 місяці тому +1

    Zoonadi brother mtanyiwa ifetinapanga mistake kuvotera Chakwera ndigululake komano chakwera aziwekuti wasalandi madzi amodzi

  • @DarwinBobot
    @DarwinBobot 3 місяці тому +2

    Pangolin ..ntanyiwa ....

  • @FaressPatel
    @FaressPatel 3 місяці тому +2

    Kkkkkkkkkk yomwe mwaiputayo chakwera ikuphulikikani

  • @ZondoChirwa
    @ZondoChirwa 3 місяці тому

    Ntanyiwa more 🔥🔥🔥🔥🔥 fire

  • @YasinMusa-ym8lp
    @YasinMusa-ym8lp 3 місяці тому +2

    Achita bwino 😂😂😂arirata😂😂

  • @ChiefJustin-cl8jl
    @ChiefJustin-cl8jl 3 місяці тому

    Limpopo fm ❤

  • @CleverChiumia
    @CleverChiumia 3 місяці тому +1

    Mutitumizire zithunzi za anthu omwe agwidwa ku South Africa.

  • @MosesLackson-l4f
    @MosesLackson-l4f 3 місяці тому

    Comrade umakwana bigup

  • @GRACIOUSKENAN
    @GRACIOUSKENAN 3 місяці тому +2

    Musalimbane ndi manyi woo aaaa muti asilikali alikuti??
    Agalu osaziwa ntchitowo? ntchito zigololo bas.
    ife tiibe ma ninja mmalawi muno aaaa

  • @sulleahmnyimbili1362
    @sulleahmnyimbili1362 3 місяці тому

    Great Job Ntanyiwa

  • @LoveKhobiri
    @LoveKhobiri 3 місяці тому

    God be with u brother

  • @DoricaGoweka
    @DoricaGoweka 3 місяці тому

    Ulemu wanu Comrade ❤

  • @charlesjimu6054
    @charlesjimu6054 3 місяці тому +1

    Tchimo limayitana Lin,zache

  • @LiyayaNyamula-j3b
    @LiyayaNyamula-j3b 3 місяці тому +1

    Yomwey galu iwe umakwan

  • @sharifujoe7633
    @sharifujoe7633 3 місяці тому +1

    Guz Malawi ndiwatu if anyone ali okudzidwa ndikulephera kwa Chakwera tiyen paunsewu tonse pa 10 July

  • @marthablessings1314
    @marthablessings1314 3 місяці тому

    Inde bwana wathu❤❤❤

  • @sweeneykamwendo6251
    @sweeneykamwendo6251 3 місяці тому +2

    Mcp ikupanga zinthu zoopsyeza kwambiri ndipo zamdikwana mmmh

  • @nyanguoipa6996
    @nyanguoipa6996 3 місяці тому +1

    LIMPOPO FM PALIBESO IFE TINGOTI NYADU

  • @mikephiri4092
    @mikephiri4092 3 місяці тому +1

    Amalawi let’s gather together and fight like our fell Kenya’s bakili tv and Limpopo fm thy are doing there parts ife tonse tikutani kapena yathu ija ya Ulemu???

    • @harrisbanda5891
      @harrisbanda5891 3 місяці тому +1

      Not ulemu as such bro, amalawife ndombwambwana kwambiri man, mtanyiwa and bakili muluzi tv alongside bon Kalindo are doing their part for sure

  • @PatrickMulangala-os4by
    @PatrickMulangala-os4by 3 місяці тому

    Respect for you

  • @JafaliAkimu-ll1bf
    @JafaliAkimu-ll1bf 3 місяці тому +2

    boma la zitsiru apolice army chakwera mitumbo ya chamanu

  • @AlinafeChimoto-pp7wp
    @AlinafeChimoto-pp7wp 3 місяці тому +1

    Pa 10 akuchoka bas

  • @ThoccoKakowa
    @ThoccoKakowa 3 місяці тому +1

    Osasiya kunena zowona

  • @rhajabBinIman
    @rhajabBinIman 3 місяці тому

    Be blessed

  • @LatiffKadyamawuseni
    @LatiffKadyamawuseni 3 місяці тому

    Mumakwana ❤

  • @ChrifordBiziel
    @ChrifordBiziel 3 місяці тому +1

    Zigawenga zosadziw dziko akadziwe munthu ali kudimba zoon

  • @TressLuka
    @TressLuka 3 місяці тому +1

    Pitilizani Bigy kubweretsa poyera zobisika kuti tiwachotse ose mwake muno.

  • @CatherineNkhala
    @CatherineNkhala 3 місяці тому

    Be protected sir

  • @AgathaJerard
    @AgathaJerard 3 місяці тому +1

    😂😂😂😂😂😂😂musandikomole antanyiwa ine lero Koma kulizithuuuu 😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂

  • @PatrickMulangala-os4by
    @PatrickMulangala-os4by 3 місяці тому +1

    Walemphela udindo

  • @YasinMusa-ym8lp
    @YasinMusa-ym8lp 3 місяці тому

    Namu bwana mumata ❤

  • @gifthara2460
    @gifthara2460 3 місяці тому +1

    Koma braz mumakwana athawa a mcp

  • @KassimSaizi
    @KassimSaizi 3 місяці тому

    Our channel Malawian channel we love you comrade together with your people ❤❤❤

  • @StellaCharles-dq8db
    @StellaCharles-dq8db 3 місяці тому +1

    Mcp mulungu walange ndinthu ndipo apange kanthu mudzina layesu akutitenga ngat chisiru ndinthu

  • @JefulyPesulo
    @JefulyPesulo 3 місяці тому +1

    Mumakwana ntanyiwa

  • @inamrigala
    @inamrigala 3 місяці тому +1

    Ndipo anapa chilima ndi ameneyo lelo chikuza mawu ndi iyeyo aziwona ndithu atule pasi udindo

  • @EsnartMalewa
    @EsnartMalewa 2 місяці тому +2

    😂😂😂

  • @philonampha
    @philonampha 3 місяці тому

    26:37

  • @PetroJack
    @PetroJack 3 місяці тому +1

    Limpopo ndi katundu uyu😂😂😂😂

  • @EyobeAyala
    @EyobeAyala 3 місяці тому

    Ife kuno ku South Africa kungochotsedwa chifukwa Cha zomwe akupanga chakwela😢azaona konko ku Malawiko zomwe tizapange

  • @RaheemMogoya
    @RaheemMogoya 3 місяці тому +1

    Koma athu aku mcp mulungu achitepo kathu

  • @MabvutoMichaelPanagona
    @MabvutoMichaelPanagona 3 місяці тому +1

    Bambo mu mtanyiwa ulemu ndi wanu mulungu apitirize kukuyang'anirani

  • @AmosBandula-up4yb
    @AmosBandula-up4yb 3 місяці тому

    Tipangeni ad ku group please

  • @GeorgePhiri-ub2of
    @GeorgePhiri-ub2of 3 місяці тому +2

    Kkkkkkkk koma amalawi ena ndinu omvetsa chisoni basi muli Limpopo ndi 1ndi maboza amalwi polani moto please mijedu khani zongopeka anthuni mudzachangamuka liti abale

  • @ShafieIdrissah
    @ShafieIdrissah 3 місяці тому +1

    Chakwera wamupa chilima kuvuna akhale president galu kwabas

  • @MebleNgulinga-hi6rg
    @MebleNgulinga-hi6rg 3 місяці тому +1

    Eyetu ameneyo nde mulungu inuyo ngati mukukwanitsa kutseka anthu pakamwa ndindalama ndiomwewo opusa osusuka achina yudasi Ana anjoka inuuuuu
    Malawi mizimu yambiri ikuzunzika kusowa chisamaliro zinthu zinakwera kuli okalamba Ana amasiye nzipatala kundende ndi anthu onseee mdzikomu ofuna zabwino koma ayi zikuvuta kwacha mwagwetsa mwagwetsanso ma million mukukhonyolera m'matumba mwanu kukhutisa mimba zanu
    Nde pemphero la olira ovutika Mulungu samalisiya amayankha mwachangu nde anthu ayamba kugwidwawa nchiyambi chowululika zinsisi zanu
    I'm repeating all most each and every day kuti you will pay one by one
    I'm not just taking this is prophetic word
    Mulungu ndiokwiya nanuuuuuu anthu amagazi m'manja inu

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 3 місяці тому

    South Africa ikangomuphulisa wagule uja basi, walowa mkati mwana wang'ona ameneyu

  • @MathewKalinkhu
    @MathewKalinkhu 3 місяці тому

    Chakwera woyeeeeeee! Mutu waima, ndipo a Malawi tisalole zopusa

  • @TchumaKanyemba
    @TchumaKanyemba 3 місяці тому

    Yomweyo chikangawa

  • @hanifahmponda8711
    @hanifahmponda8711 3 місяці тому +1

    Kodi agapeyu ndindani nanga tundu wanji wamunthu ku malawi kuno agalu kwabasi ndi MCP yawoyo

  • @RosemaryKhungwa
    @RosemaryKhungwa 3 місяці тому

    Ulemu wanu sir

  • @GeorgeChakuamba
    @GeorgeChakuamba 3 місяці тому +2

    Auze zoona a Malawi iwe umakwana ndipo ndimachita kukuika PA Bluetooth kut maneba amve nawo kkkkkk

    • @SmileMalanda
      @SmileMalanda 3 місяці тому

      😂😂😂😂😂

    • @RiteRoderick
      @RiteRoderick 3 місяці тому

      😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂

    • @Pangolinimw
      @Pangolinimw 3 місяці тому

      umachita bwino

  • @JafaliLysani-nb6bq
    @JafaliLysani-nb6bq 3 місяці тому

    ❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤

  • @zimmekapachika6784
    @zimmekapachika6784 3 місяці тому +1

    Ndipo galu ameneyu akukakamila pampando chifukwa chani mfiti yokupha ngati imeneyi palikundu peni