JOHN KAPITO WATOPA NAYE CHAKWERA. Ityoke ityoke Osabisa mau // PART 1

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 26 вер 2024

КОМЕНТАРІ • 308

  • @DanielMaruwo
    @DanielMaruwo Місяць тому +3

    That's number one Mr kapito speaking as a man of integrity

  • @BenjaminKwerengwe
    @BenjaminKwerengwe Місяць тому +1

    Very wise presentation,we have wise Malawians

  • @charlesmuwanya7845
    @charlesmuwanya7845 11 місяців тому +36

    Mr John Kapito has given a true account of the real situation in Malawi. He is a senior soothsayer. He is always for the whole truth. He doesn't mince words & his desire is to set things right.

    • @JoelMpanje
      @JoelMpanje 11 місяців тому +5

      Jst straight to the point

    • @JafaliAkimu-ll1bf
      @JafaliAkimu-ll1bf 3 місяці тому +2

      chakwera ndi chitsiru cha munthu mdziko muno mbava

    • @CatherineBwanali-z1g
      @CatherineBwanali-z1g 3 місяці тому

      koma maiko anzathu zimachitika ngati zimachitika kwathu kunozi kapena nkhani ndiyathu kunjaku....malawi wafika penipeni pomvesa chisoni mmmmm Mulungu atithandize

    • @JacobCimwinga
      @JacobCimwinga 3 місяці тому

      Mr Kapito we are very happy with your insight....Malawi ... needs a Servant not a leader....All our former presidents have travelled and most of them been overseas....but they are failing to bring our country to the international standards....I live in South Africa my passport expired last year...I renewed from the consulate....I paid in Blantyre....but up to now Nothing..I am working here no passport.....
      Immigration is in full corruption..... and disfunctional ...and it's a revenue govt department..Now if they are failing it means that they are bringing the country down.....suck all corrupt officials....we can't be suffering outside the country cause of these rotten officials...... and where is the minister of homeland security.....where is the president.....shame on you guys.....

    • @omarstambuli2105
      @omarstambuli2105 2 місяці тому

      Tilibe ku gahena

  • @EdwinMabviko
    @EdwinMabviko 11 місяців тому +17

    Malawi needs such people to develop!!!

  • @UmaliYunusu
    @UmaliYunusu 11 місяців тому +4

    Very clear message Mr Kapito may God bless you and your family and God bless Malawi country

  • @lyiemax
    @lyiemax 11 місяців тому +8

    Big up Bwana Kapito, you are indeed a great man, I have really enjoyed your explanations 🔥🔥🔥🔥

  • @PatrickTembo-lm1ih
    @PatrickTembo-lm1ih 3 місяці тому +3

    Koma apapa mwayankhula chilungamo ngakhale msogoleli alindimaganizo amenewa likhoza kukhala boma mkhoza kuyendesa boma bwino ❤❤❤❤

  • @mkhulukinyata5198
    @mkhulukinyata5198 11 місяців тому +3

    Well spoken Mr Kapito..Indeed Malawi tikufuna anthu wolankhula dzokupsa ngati momwe alankhulira Mr KAPITO apamu

  • @danielzitande5231
    @danielzitande5231 26 днів тому

    Mmmm abwana akapito apoo ndiye mwalankhura ndipo mulungu adzikisungani NDI uphungu wabwino I like you ❤❤❤

  • @jonas-xh4hz
    @jonas-xh4hz 3 місяці тому +2

    thank you sir kapito for your explanation

  • @FanscioDancun-o9j
    @FanscioDancun-o9j 11 місяців тому +4

    Good explanation sounds like izeck somewhere (kukagwirana ndi azungu 😅😅😅 nice one Mr kapito

  • @ChimwemweMarkBanda-yj7yk
    @ChimwemweMarkBanda-yj7yk 11 місяців тому +4

    Pempho Mr Brian Banda. Would you please visit anthu anchimidzi kuti muone how pple are suffering and see how they are surviving with every days life. Anthu amene adavota akufatu😢

    • @innocentkapachika6591
      @innocentkapachika6591 11 місяців тому

      Take this comment very seriously. Take a chance and visit voters in the the remote areas. For example, come and visit Dedza South Constituency the most Least Developed Constituency in Malawi

    • @SengikhonaDula
      @SengikhonaDula 11 місяців тому

      Eish ndipo very pain full vote lako lomwe kumagona osadya😢

    • @alexdausi5167
      @alexdausi5167 11 місяців тому

      ​@@SengikhonaDulakoma Mesa amati tizidya katatuh everydey

    • @HajraTar
      @HajraTar 23 дні тому

      ​@@SengikhonaDulaso sad malawi okoma uja

  • @stevenchidathas4477
    @stevenchidathas4477 11 місяців тому +1

    I like this Man, Mr Kapito keep on😊

  • @simionkonyane368
    @simionkonyane368 3 місяці тому

    God bless you Mr Kapito wayankhula mfundo zenizeni❤

  • @WysonElson
    @WysonElson Місяць тому

    Exactly Mr kapito and I agreed with u. Keep it up

  • @jaydee1236
    @jaydee1236 11 місяців тому +1

    Brilliant ❤ Mr John kapito

  • @AlexMwambera
    @AlexMwambera 24 дні тому

    Very true we have a leader who has no vision he is totally not knowing what is he doing in government

  • @ChristinaNyirenda-zb1if
    @ChristinaNyirenda-zb1if 3 місяці тому +2

    Good Mr kapito

  • @David-c4g4g
    @David-c4g4g 3 місяці тому +3

    Mr kapita you're true leader

  • @greymasha838
    @greymasha838 11 місяців тому +1

    God bless you and keep it up and this is well said

  • @AllanMwakalenga-wn5ib
    @AllanMwakalenga-wn5ib 11 місяців тому +6

    Kapito umakwana... If possible mungoyima pa u president.. we will vote for you

    • @HajraTar
      @HajraTar 23 дні тому

      😂😂😂zafikapa sitikudziwa kut wabwino ndani Pena nane ndumati bon kalindo akhale president😂😂😂Mulungu atipatse president oyenera

  • @MacdonaldMwanza-t8s
    @MacdonaldMwanza-t8s 11 місяців тому +1

    Big up boss man... you're a great man

  • @ImanRashidi-so4oo
    @ImanRashidi-so4oo 2 місяці тому +1

    Powerful massage

  • @CharlesEliya-d3e
    @CharlesEliya-d3e Місяць тому

    Big up Mr kapito
    And God bless you

  • @Symon-q8n
    @Symon-q8n 10 місяців тому +1

    Thank you Mr kapito mwanena zothandiza ziko la malawi Kodi achakwera mkuva please pasto mrungu akuyang,oneni

  • @alicekalupsya7149
    @alicekalupsya7149 3 місяці тому

    Ur a man full of wisdom.

  • @williamskondowe8795
    @williamskondowe8795 11 місяців тому +3

    Respect Mr kapito otsaopa ,otsapweketsa we're all malawian don't fear lf there's justice

  • @MahmoudZebron
    @MahmoudZebron 3 місяці тому +1

    Ndilibe mau mbili bwana kapito you're good man you're a m'dala 😂😂😂😂😂😂😂😂

  • @allanbanda4388
    @allanbanda4388 11 місяців тому

    100% Mr man matiimilila ifeyo anthu amene tilibe kuthekela kofikitsa nkhawa zathu koyenela kupititsa nkhawa coz anthu tilinazo zolankhula zodzadza mitima komaso chilungamo dziko lamalawi lofunika fix kugwedeza kukhutchumula nyansi tikhale ndiatsogoleli osadzikonda moonjeza amene amalimbikitsa timbamva ma offence ndicholinga chofuna kukhututsa mimbazawo kumamupsinja munthu angakhale olimbikila paiye yekha km Mmmm oky god bless you Mr kapito please musakakhale pansi mubweleso kumalankhula osaopa please thanks

  • @johnmponda9070
    @johnmponda9070 2 місяці тому

    Watching and following from Cape town South Africa 💪💪

  • @EliahLetulo
    @EliahLetulo 10 місяців тому +1

    Kma mr kapita you are the great man ❤😂

  • @chippakaribafox2865
    @chippakaribafox2865 11 місяців тому +2

    Bravo kapito!...respect

  • @StaffordMwasithu
    @StaffordMwasithu 11 місяців тому +2

    Kapito your e a big man ayi pano ndiye ku Malawi sikulibwno ayi.

  • @petertukula1649
    @petertukula1649 11 місяців тому +1

    Mr Kapita Bravo.... awa ndi mau

  • @WilfredYekha
    @WilfredYekha 2 місяці тому +1

    Mr. Kapito, thanks for being there on behalf of the malawians, we gave him our votes in order to see a positive change,we didn't know that we were created autocracy poverty,grave & many more. May God bless Malawi and these guys who are speaking vigorously on behalf of us.

  • @LovelyAzaleaFlower-uc8vr
    @LovelyAzaleaFlower-uc8vr 4 місяці тому

    Well explanation, Malawi needs such people

  • @MoosaSame
    @MoosaSame 11 місяців тому +8

    We're together mr Kapito

    • @AnthonyKhundi-j3u
      @AnthonyKhundi-j3u 10 місяців тому

      Kodi akapito amagwira ntchito yanji kodi abale

    • @AnthonyKhundi-j3u
      @AnthonyKhundi-j3u 10 місяців тому

      A brian banda mulibenso nzeru ndiyesa ndi mankhwala oyeretsa thupiwo mwina ,kodi ndege ku malawi zinasowa liti?

  • @douglasturner2992
    @douglasturner2992 10 місяців тому +1

    You deserve to be a leader...

  • @ShadreckmpManda
    @ShadreckmpManda 11 місяців тому +5

    Mr kapito ukunena zoona koma nkhani yimozi yonkha ndiyankhepo.
    Chilima sangayendese boma ndimunthu wonama kwambiri. Ndiye ngati mutsogoleri ali ndiboza sangatumikire anthu.
    Chilima ndi chakwera ndichimozimozi.
    Chilima ngati akanankhala kuti akufunila zabwino amalawi bwezi atatuluka mu MCP chifukwa akanamuwuza chakwera kuti zimene tinauza anthu kuti tiwachitira sizikuchitika naye ali mphee
    Choyamba kuyendesa ziko ukhale wa zeru and kuzichepesa kwa amene anakukweza. Kuopa Mulungu.

    • @CatherineBwanali-z1g
      @CatherineBwanali-z1g 3 місяці тому

      mfundo ndipo ndizoona

    • @VioletSkiah
      @VioletSkiah 2 місяці тому

      Chilima sadapasidwe mwai ot ayendese boma muzinva ndipo lelo mukuziwa kt chakwela walephela kamba anapasidwa mwai oyendesa boma nde anthu aona kt walephela apapa inu ndiliti chilima ANAYAMBA wayendesa boma ndilkupezeka kt ndionama ?

  • @MariamAlabi-t3n
    @MariamAlabi-t3n 3 місяці тому

    Mr Kapito a man himself he doesn't fear nothing .He is so intelligent

  • @MustaffISAH
    @MustaffISAH 2 місяці тому

    You are indeed real Malawian Mr Kapito and you talking reality

  • @chipanganochirwa5761
    @chipanganochirwa5761 2 місяці тому

    Clear and true speaking.

  • @Mfwanayo
    @Mfwanayo 4 місяці тому

    This Mr Kapito why he's true and direct like this.......shaaaa ndipo ndamkonda bwanj.....in Malawi we also have brilliant and straight people this like

  • @Gwedeza-oz3jv
    @Gwedeza-oz3jv 5 місяців тому

    Great ones Mr kapito

  • @dysonmasiye5736
    @dysonmasiye5736 Місяць тому

    Mr. Kapito is a true Malawian and eish

  • @MikaNamwada
    @MikaNamwada 3 місяці тому +1

    Well said kapito🔥🔥🔥🔥🔥

  • @MathewsPhiri-y3v
    @MathewsPhiri-y3v 11 місяців тому +3

    Brian ndi bambo kapito, boma ili ndi masanje eni eni, ndipo ukunena zoona bambo kapito, Chakwera sankhadziwa kuti angalamule dziko, mu mutu muli gwa! Sadziwa chilichose.

    • @charlesmuwanya7845
      @charlesmuwanya7845 11 місяців тому

      The real situation. Mr kapito is a soothsayer. He doesn't mince words. He calls a spade by its name.

    • @natashayohane
      @natashayohane 10 місяців тому

      Zowona m bomamu muli nyasi

  • @Goliath461
    @Goliath461 11 місяців тому +2

    Paja nyau yonunkha manyi ija amati zinalake chani?la chakwera tachosa koma la nyau yonkha ija😂😂😂

  • @MuhammadSamson-yz1kl
    @MuhammadSamson-yz1kl 11 місяців тому +2

    Respect kapito osaopa achakwera ndi nyani

  • @DoricaGoweka
    @DoricaGoweka 11 місяців тому +1

    Good explanation uncle. The Country need people like you not Chakwera,He must go back to his church not rule the country. The citizens are suffering alot because of him.

  • @EmmanuelGasiten-fo5dr
    @EmmanuelGasiten-fo5dr 3 місяці тому

    True Malawian, Mr Kapito. Okumbira mnzake dzenje, adzagweramo yekha. Lero anadzikumbira okha dzenje ku IMF.

  • @WarriorKB-u3k
    @WarriorKB-u3k Місяць тому

    Malawi its 4 malawians not 4 mr chikangawa tru speaking mr kapito A.P.M our vote

  • @PatrickSomanje
    @PatrickSomanje 27 днів тому

    Exactly mr kapito this president just waste time for poor Malawians , today people suffering no food lot of things happening in Malawi

  • @thokozanichikafa6602
    @thokozanichikafa6602 Місяць тому

    God bless you mwamasuka kuuza a malawi

  • @MikeMadeya-xm4uy
    @MikeMadeya-xm4uy 11 місяців тому +2

    Mr kapito please 2025 please stand for people

  • @jeffchikwapata6933
    @jeffchikwapata6933 3 місяці тому

    I like Mr kapito's explanation

  • @georgesmart3791
    @georgesmart3791 11 місяців тому +1

    More fire mr Kapito🔥 🔥 🔥

  • @raytavares2256
    @raytavares2256 11 місяців тому +3

    How can you say Chilima has not been tested and yet he was arrested for thieving yet still working getting payed on Malawian tax payers? Was he not suspended?

  • @ErimonChilanga
    @ErimonChilanga 2 місяці тому

    Mr kapito god bless you

  • @Benjamin-h4k
    @Benjamin-h4k 2 місяці тому

    Kapito is a genius

  • @AndersonChimwala-hz4so
    @AndersonChimwala-hz4so 11 місяців тому +2

    Big up mr kapita malawi need people like you.

  • @Yasinta-mh3cb
    @Yasinta-mh3cb 3 місяці тому

    Ineyo I don't say much kuopa wat am saying is may the good Lord in heaven protect U in his wings be safe my father it's my prayer eeeesh real man for Ur own parents who is U exactly heeee God save my father his real

  • @bigmount563
    @bigmount563 3 місяці тому

    I am sorry for my self I missed this program, but I koma Mr kapito Mulungu azikudalisani ngati chakwer a sakumva ixi afe ndithu

  • @chikaonekarh
    @chikaonekarh 4 місяці тому

    Our own KAPITO mumatiyimilira koma kunsanva a President,ndakusokosela mkulinga utava!
    Zayekha adaviyika nsima madzi musiyeni timuona 2025 Chakwera

  • @stevenbanda6665
    @stevenbanda6665 2 місяці тому

    Very clear

  • @TisaiwaleTewesah
    @TisaiwaleTewesah 11 місяців тому +1

    Mr kapito i respect you 🙏

  • @YusufujohnSeruweke
    @YusufujohnSeruweke 2 місяці тому

    Ulemu wanu Mr kapito chilungamo

  • @PatricaTchuwa
    @PatricaTchuwa 10 місяців тому +1

    Utsogoleri umadana ndiphuma, lero ndizimenezi manyaka enieni achoke ameneyii chimuthu choyiipa chosava za anthu

  • @frankiechasokoneza5802
    @frankiechasokoneza5802 3 місяці тому +1

    Nde wina adzikati Chakwera yemweyoooo akhomedwa

  • @KennedyPhiri-h9h
    @KennedyPhiri-h9h 2 місяці тому

    You are talking truth brother there nothing happening under ulamuliro wa chakwela mcp

  • @MacDonaldJiyan
    @MacDonaldJiyan Місяць тому

    Kapito , you say infact so God bless you plus

  • @ammaarahkhota7939
    @ammaarahkhota7939 11 місяців тому +1

    ACHAKWERA AKUFUNA KULEMERA SINANGA AKUDZIWA SAKHALANSO PA MPANDO. PALOWANSO ENA .NDIYE OSAMADABWA RATE YAKUNJAILI KUTI .UTSOGOLERI SASITHA NGATI MALAYA .MAPETO AKE ALIYENSE AZINGOLOWA CHOLINGA CHOTI NDILEMELELETU SINANGA CHAKA CHAMMAWA AKULOWA ENA. AWA NDI MAVUTO AWAYAMBA DALA. VUTO NDI IEFE OKHALA KUMUDZI.

  • @NellieMsamala
    @NellieMsamala 2 місяці тому

    Loud and clear mr

  • @George-zd5le
    @George-zd5le 11 місяців тому

    Sir Kapiti ndinu munthu wanseru. Genius man

  • @natashayohane
    @natashayohane 10 місяців тому +1

    Zovetsa chisoni mmene yatulukila maina oti apindule ndi zipangizo zotsika mtengo pa fumu dzina limodzi

  • @DannieChimenya
    @DannieChimenya 3 місяці тому

    Mr kapito God bless you sir

  • @mbaliehaward947
    @mbaliehaward947 11 місяців тому +1

    Boma lavuta ili pangolini amanena zoona respect the DC

  • @lame8
    @lame8 11 місяців тому +2

    Zimangovuta koma chaka China tizapeza wabwinoyo❤ msogoleli wabwinoyo is our hope tizabowoleza tili ndi anthu azelu kumalawi ambiri

  • @jamessheki4293
    @jamessheki4293 2 місяці тому

    Big up Mr Kapito

  • @Thewarrior7093
    @Thewarrior7093 11 місяців тому +2

    I hate chakwera to the extent that i don't even hear about his name being mentioned. All the challenges we're facing is because of his stupid and dull leadership

    • @SheenahMwalabu-iz3pr
      @SheenahMwalabu-iz3pr 11 місяців тому +1

      Was looking for this message 😂😂 me too eish l hate his leadership

  • @henrymbalame222
    @henrymbalame222 2 місяці тому

    Zoonadi zake (ziliko m'nkulinga utatosako!,,)
    Ndipo (Wandisokosera m'mkulinga utanva!,,)

  • @GlacianoChinkonde
    @GlacianoChinkonde Місяць тому

    good speech

  • @LilianKachala-yz2xf
    @LilianKachala-yz2xf 3 місяці тому

    Bambo Kapito now you are Talking. Keep it up

  • @LiynoNazombe
    @LiynoNazombe 11 місяців тому +3

    Palibe angamutsutse mkuluyu

  • @mussamapira801
    @mussamapira801 11 місяців тому +1

    A chakwera Ali ngati chipilala 2angokhala mu office ndiye zinduna zano zimangobwela zainani apa chakwera ku zaina palibe chomwe akuziwa dzikoli akuyendeza ndi zinduna pamodzi ndi banja lawo

  • @FanscioDancun
    @FanscioDancun 3 місяці тому

    This man is speaks the truth

  • @BennettNjedza
    @BennettNjedza 2 місяці тому

    Nice papa you are right ✅

  • @CeciliaKamanga-mx9dc
    @CeciliaKamanga-mx9dc 3 місяці тому

    Bravo kapito 100% agree 👍

  • @LuciaMbisa
    @LuciaMbisa Місяць тому

    Ziko ndi church zosiana achakwera arephera must resin

  • @MaxwellMustafa-ec8fc
    @MaxwellMustafa-ec8fc 11 місяців тому +6

    God bless you sir Mr kapito

  • @LenardJames-t1s
    @LenardJames-t1s 10 місяців тому +1

    Us Malawians we need to have readers from over seaze

  • @FernandosLuciano-bb9or
    @FernandosLuciano-bb9or 11 місяців тому +4

    Uwuwu ndi kantho kapena chilango cha mulungu pochosa msogoleli wabwino peter ndijuika mbava ngothi ndizisilu zones zili mu tonse palibe chomwe chisinthe mpaka 2030

  • @SengikhonaDula
    @SengikhonaDula 11 місяців тому +1

    48 kkkk😂😂😂😅 koma popanda chosintha😂😂😂😅

  • @phillimonzgambo1663
    @phillimonzgambo1663 11 місяців тому

    Good speech kapito

  • @JohnChibalo-wf8gr
    @JohnChibalo-wf8gr 11 місяців тому +1

    M'manja mwa akapito pwa pwa pwa

  • @munashemoyo4190
    @munashemoyo4190 Місяць тому

    😂😂😂😂😂 nkhan ukapolo omwewo bas kujambulisa ndi zungu

  • @WarriorKB-u3k
    @WarriorKB-u3k Місяць тому

    Thats true sakudziwa za boma ,palibe akudziwa za u presdent thts why wangosanduka chigawenga

  • @HanishaissahKagansa
    @HanishaissahKagansa 11 місяців тому +3

    Ndizoonadi alowa m,boma alibe Maso mphenye then nsamadziwa kuti kuyendetsa dziko ndichinthu chomvuta

  • @RaphickBanda-hz4gx
    @RaphickBanda-hz4gx 11 місяців тому +3

    Part 2 please

  • @mbaliehaward947
    @mbaliehaward947 11 місяців тому +1

    Respect Mr kapito