Mr John Kapito has given a true account of the real situation in Malawi. He is a senior soothsayer. He is always for the whole truth. He doesn't mince words & his desire is to set things right.
Mr Kapito we are very happy with your insight....Malawi ... needs a Servant not a leader....All our former presidents have travelled and most of them been overseas....but they are failing to bring our country to the international standards....I live in South Africa my passport expired last year...I renewed from the consulate....I paid in Blantyre....but up to now Nothing..I am working here no passport..... Immigration is in full corruption..... and disfunctional ...and it's a revenue govt department..Now if they are failing it means that they are bringing the country down.....suck all corrupt officials....we can't be suffering outside the country cause of these rotten officials...... and where is the minister of homeland security.....where is the president.....shame on you guys.....
Pempho Mr Brian Banda. Would you please visit anthu anchimidzi kuti muone how pple are suffering and see how they are surviving with every days life. Anthu amene adavota akufatu😢
Take this comment very seriously. Take a chance and visit voters in the the remote areas. For example, come and visit Dedza South Constituency the most Least Developed Constituency in Malawi
Mr. Kapito, thanks for being there on behalf of the malawians, we gave him our votes in order to see a positive change,we didn't know that we were created autocracy poverty,grave & many more. May God bless Malawi and these guys who are speaking vigorously on behalf of us.
This Mr Kapito why he's true and direct like this.......shaaaa ndipo ndamkonda bwanj.....in Malawi we also have brilliant and straight people this like
Brian ndi bambo kapito, boma ili ndi masanje eni eni, ndipo ukunena zoona bambo kapito, Chakwera sankhadziwa kuti angalamule dziko, mu mutu muli gwa! Sadziwa chilichose.
Good explanation uncle. The Country need people like you not Chakwera,He must go back to his church not rule the country. The citizens are suffering alot because of him.
How can you say Chilima has not been tested and yet he was arrested for thieving yet still working getting payed on Malawian tax payers? Was he not suspended?
Ineyo I don't say much kuopa wat am saying is may the good Lord in heaven protect U in his wings be safe my father it's my prayer eeeesh real man for Ur own parents who is U exactly heeee God save my father his real
I hate chakwera to the extent that i don't even hear about his name being mentioned. All the challenges we're facing is because of his stupid and dull leadership
A chakwera Ali ngati chipilala 2angokhala mu office ndiye zinduna zano zimangobwela zainani apa chakwera ku zaina palibe chomwe akuziwa dzikoli akuyendeza ndi zinduna pamodzi ndi banja lawo
Uwuwu ndi kantho kapena chilango cha mulungu pochosa msogoleli wabwino peter ndijuika mbava ngothi ndizisilu zones zili mu tonse palibe chomwe chisinthe mpaka 2030
That's number one Mr kapito speaking as a man of integrity
Very wise presentation,we have wise Malawians
Mr John Kapito has given a true account of the real situation in Malawi. He is a senior soothsayer. He is always for the whole truth. He doesn't mince words & his desire is to set things right.
Jst straight to the point
chakwera ndi chitsiru cha munthu mdziko muno mbava
koma maiko anzathu zimachitika ngati zimachitika kwathu kunozi kapena nkhani ndiyathu kunjaku....malawi wafika penipeni pomvesa chisoni mmmmm Mulungu atithandize
Mr Kapito we are very happy with your insight....Malawi ... needs a Servant not a leader....All our former presidents have travelled and most of them been overseas....but they are failing to bring our country to the international standards....I live in South Africa my passport expired last year...I renewed from the consulate....I paid in Blantyre....but up to now Nothing..I am working here no passport.....
Immigration is in full corruption..... and disfunctional ...and it's a revenue govt department..Now if they are failing it means that they are bringing the country down.....suck all corrupt officials....we can't be suffering outside the country cause of these rotten officials...... and where is the minister of homeland security.....where is the president.....shame on you guys.....
Tilibe ku gahena
Malawi needs such people to develop!!!
Very clear message Mr Kapito may God bless you and your family and God bless Malawi country
Big up Bwana Kapito, you are indeed a great man, I have really enjoyed your explanations 🔥🔥🔥🔥
Koma apapa mwayankhula chilungamo ngakhale msogoleli alindimaganizo amenewa likhoza kukhala boma mkhoza kuyendesa boma bwino ❤❤❤❤
Well spoken Mr Kapito..Indeed Malawi tikufuna anthu wolankhula dzokupsa ngati momwe alankhulira Mr KAPITO apamu
Mmmm abwana akapito apoo ndiye mwalankhura ndipo mulungu adzikisungani NDI uphungu wabwino I like you ❤❤❤
thank you sir kapito for your explanation
Good explanation sounds like izeck somewhere (kukagwirana ndi azungu 😅😅😅 nice one Mr kapito
Pempho Mr Brian Banda. Would you please visit anthu anchimidzi kuti muone how pple are suffering and see how they are surviving with every days life. Anthu amene adavota akufatu😢
Take this comment very seriously. Take a chance and visit voters in the the remote areas. For example, come and visit Dedza South Constituency the most Least Developed Constituency in Malawi
Eish ndipo very pain full vote lako lomwe kumagona osadya😢
@@SengikhonaDulakoma Mesa amati tizidya katatuh everydey
@@SengikhonaDulaso sad malawi okoma uja
I like this Man, Mr Kapito keep on😊
God bless you Mr Kapito wayankhula mfundo zenizeni❤
Exactly Mr kapito and I agreed with u. Keep it up
Brilliant ❤ Mr John kapito
Very true we have a leader who has no vision he is totally not knowing what is he doing in government
Good Mr kapito
Mr kapita you're true leader
God bless you and keep it up and this is well said
Kapito umakwana... If possible mungoyima pa u president.. we will vote for you
😂😂😂zafikapa sitikudziwa kut wabwino ndani Pena nane ndumati bon kalindo akhale president😂😂😂Mulungu atipatse president oyenera
Big up boss man... you're a great man
Powerful massage
Big up Mr kapito
And God bless you
Thank you Mr kapito mwanena zothandiza ziko la malawi Kodi achakwera mkuva please pasto mrungu akuyang,oneni
Ur a man full of wisdom.
Respect Mr kapito otsaopa ,otsapweketsa we're all malawian don't fear lf there's justice
Ndilibe mau mbili bwana kapito you're good man you're a m'dala 😂😂😂😂😂😂😂😂
100% Mr man matiimilila ifeyo anthu amene tilibe kuthekela kofikitsa nkhawa zathu koyenela kupititsa nkhawa coz anthu tilinazo zolankhula zodzadza mitima komaso chilungamo dziko lamalawi lofunika fix kugwedeza kukhutchumula nyansi tikhale ndiatsogoleli osadzikonda moonjeza amene amalimbikitsa timbamva ma offence ndicholinga chofuna kukhututsa mimbazawo kumamupsinja munthu angakhale olimbikila paiye yekha km Mmmm oky god bless you Mr kapito please musakakhale pansi mubweleso kumalankhula osaopa please thanks
Watching and following from Cape town South Africa 💪💪
Kma mr kapita you are the great man ❤😂
Bravo kapito!...respect
Kapito your e a big man ayi pano ndiye ku Malawi sikulibwno ayi.
Mr Kapita Bravo.... awa ndi mau
Mr. Kapito, thanks for being there on behalf of the malawians, we gave him our votes in order to see a positive change,we didn't know that we were created autocracy poverty,grave & many more. May God bless Malawi and these guys who are speaking vigorously on behalf of us.
Well explanation, Malawi needs such people
We're together mr Kapito
Kodi akapito amagwira ntchito yanji kodi abale
A brian banda mulibenso nzeru ndiyesa ndi mankhwala oyeretsa thupiwo mwina ,kodi ndege ku malawi zinasowa liti?
You deserve to be a leader...
Mr kapito ukunena zoona koma nkhani yimozi yonkha ndiyankhepo.
Chilima sangayendese boma ndimunthu wonama kwambiri. Ndiye ngati mutsogoleri ali ndiboza sangatumikire anthu.
Chilima ndi chakwera ndichimozimozi.
Chilima ngati akanankhala kuti akufunila zabwino amalawi bwezi atatuluka mu MCP chifukwa akanamuwuza chakwera kuti zimene tinauza anthu kuti tiwachitira sizikuchitika naye ali mphee
Choyamba kuyendesa ziko ukhale wa zeru and kuzichepesa kwa amene anakukweza. Kuopa Mulungu.
mfundo ndipo ndizoona
Chilima sadapasidwe mwai ot ayendese boma muzinva ndipo lelo mukuziwa kt chakwela walephela kamba anapasidwa mwai oyendesa boma nde anthu aona kt walephela apapa inu ndiliti chilima ANAYAMBA wayendesa boma ndilkupezeka kt ndionama ?
Mr Kapito a man himself he doesn't fear nothing .He is so intelligent
You are indeed real Malawian Mr Kapito and you talking reality
Clear and true speaking.
This Mr Kapito why he's true and direct like this.......shaaaa ndipo ndamkonda bwanj.....in Malawi we also have brilliant and straight people this like
Great ones Mr kapito
Mr. Kapito is a true Malawian and eish
Well said kapito🔥🔥🔥🔥🔥
Brian ndi bambo kapito, boma ili ndi masanje eni eni, ndipo ukunena zoona bambo kapito, Chakwera sankhadziwa kuti angalamule dziko, mu mutu muli gwa! Sadziwa chilichose.
The real situation. Mr kapito is a soothsayer. He doesn't mince words. He calls a spade by its name.
Zowona m bomamu muli nyasi
Paja nyau yonunkha manyi ija amati zinalake chani?la chakwera tachosa koma la nyau yonkha ija😂😂😂
Respect kapito osaopa achakwera ndi nyani
Good explanation uncle. The Country need people like you not Chakwera,He must go back to his church not rule the country. The citizens are suffering alot because of him.
True Malawian, Mr Kapito. Okumbira mnzake dzenje, adzagweramo yekha. Lero anadzikumbira okha dzenje ku IMF.
Malawi its 4 malawians not 4 mr chikangawa tru speaking mr kapito A.P.M our vote
Exactly mr kapito this president just waste time for poor Malawians , today people suffering no food lot of things happening in Malawi
God bless you mwamasuka kuuza a malawi
Mr kapito please 2025 please stand for people
I like Mr kapito's explanation
More fire mr Kapito🔥 🔥 🔥
How can you say Chilima has not been tested and yet he was arrested for thieving yet still working getting payed on Malawian tax payers? Was he not suspended?
Mr kapito god bless you
Kapito is a genius
Big up mr kapita malawi need people like you.
Ineyo I don't say much kuopa wat am saying is may the good Lord in heaven protect U in his wings be safe my father it's my prayer eeeesh real man for Ur own parents who is U exactly heeee God save my father his real
I am sorry for my self I missed this program, but I koma Mr kapito Mulungu azikudalisani ngati chakwer a sakumva ixi afe ndithu
Our own KAPITO mumatiyimilira koma kunsanva a President,ndakusokosela mkulinga utava!
Zayekha adaviyika nsima madzi musiyeni timuona 2025 Chakwera
Very clear
Mr kapito i respect you 🙏
Ulemu wanu Mr kapito chilungamo
Utsogoleri umadana ndiphuma, lero ndizimenezi manyaka enieni achoke ameneyii chimuthu choyiipa chosava za anthu
Nde wina adzikati Chakwera yemweyoooo akhomedwa
Ndipo
You are talking truth brother there nothing happening under ulamuliro wa chakwela mcp
Kapito , you say infact so God bless you plus
ACHAKWERA AKUFUNA KULEMERA SINANGA AKUDZIWA SAKHALANSO PA MPANDO. PALOWANSO ENA .NDIYE OSAMADABWA RATE YAKUNJAILI KUTI .UTSOGOLERI SASITHA NGATI MALAYA .MAPETO AKE ALIYENSE AZINGOLOWA CHOLINGA CHOTI NDILEMELELETU SINANGA CHAKA CHAMMAWA AKULOWA ENA. AWA NDI MAVUTO AWAYAMBA DALA. VUTO NDI IEFE OKHALA KUMUDZI.
Loud and clear mr
Sir Kapiti ndinu munthu wanseru. Genius man
Zovetsa chisoni mmene yatulukila maina oti apindule ndi zipangizo zotsika mtengo pa fumu dzina limodzi
Mr kapito God bless you sir
Boma lavuta ili pangolini amanena zoona respect the DC
Zimangovuta koma chaka China tizapeza wabwinoyo❤ msogoleli wabwinoyo is our hope tizabowoleza tili ndi anthu azelu kumalawi ambiri
Yes
Anangokhala ndi nsanje kumuchosa peter pampando
Big up Mr Kapito
I hate chakwera to the extent that i don't even hear about his name being mentioned. All the challenges we're facing is because of his stupid and dull leadership
Was looking for this message 😂😂 me too eish l hate his leadership
Zoonadi zake (ziliko m'nkulinga utatosako!,,)
Ndipo (Wandisokosera m'mkulinga utanva!,,)
good speech
Bambo Kapito now you are Talking. Keep it up
Palibe angamutsutse mkuluyu
A chakwera Ali ngati chipilala 2angokhala mu office ndiye zinduna zano zimangobwela zainani apa chakwera ku zaina palibe chomwe akuziwa dzikoli akuyendeza ndi zinduna pamodzi ndi banja lawo
This man is speaks the truth
Nice papa you are right ✅
Bravo kapito 100% agree 👍
Ziko ndi church zosiana achakwera arephera must resin
God bless you sir Mr kapito
Us Malawians we need to have readers from over seaze
Uwuwu ndi kantho kapena chilango cha mulungu pochosa msogoleli wabwino peter ndijuika mbava ngothi ndizisilu zones zili mu tonse palibe chomwe chisinthe mpaka 2030
48 kkkk😂😂😂😅 koma popanda chosintha😂😂😂😅
Good speech kapito
M'manja mwa akapito pwa pwa pwa
😂😂😂😂😂 nkhan ukapolo omwewo bas kujambulisa ndi zungu
Thats true sakudziwa za boma ,palibe akudziwa za u presdent thts why wangosanduka chigawenga
Ndizoonadi alowa m,boma alibe Maso mphenye then nsamadziwa kuti kuyendetsa dziko ndichinthu chomvuta
Part 2 please
26:58 27:00
Respect Mr kapito