My gracious God have mercy on Malawians to transform their nation from rut to prosperity or vision 2063 will remain a political requiem to satiate the destitutes.Let callous religious and political leaders change their minds.
Koma chilungamo Malawi anachagamuka mcp ngat simukuziwa munalowa chifukwa kunali ma demo ndiye mukuona nga anatha? Mukufunika kumangolapilatu apa no chance
It is true that opposition leaders are dormant whether they like or not but they are. We Malawians are tired and worried about them. May be they're receiving some money which makes them silent, please work up!!!!!!!
Kodi Mr Kalindo, simungakoze ulendo osawadziwitsa ma president a opposition kuti akadzuke...?. Chifukwa Boma la tonse mmm likuning'inatu heavy as tsabora., Chakwera must resign ndithu 💔💔💔💔
Peter nayenso akugona kwambiri.....Chikangawa mmene amasokonezera 2020, Nde mukudikira a Malawi kut aonde kaye kenako akuikeni pa mpando inu muzidzanjoya.kodi a Peter ,kufatsa kumeneko kwamtundu wanji ....check out
Iwe ndye ndi president wa amphawidi ,mmatiimilira keep it up Mr kalindo!!!
Mvuto amalawife mantha much
Man this guy is talking sense, there's wisdom in it
Mr kalindo keep pressurising the opposition side to take action to save the pple who are suffering under this government
Ambuye azikusamalira pena paliponse pomee ungamapezeke present wathu❤❤❤
Mofaya Mr keep on pressing
The DC🔥🔥🔥🔥🔥
My gracious God have mercy on Malawians to transform their nation from rut to prosperity or vision 2063 will remain a political requiem to satiate the destitutes.Let callous religious and political leaders change their minds.
Ndipo inu opposition yangoziii kumangomvera ma audio a achina horn kalindo,,ntanyiwa,, bakili muluzi TV kma osapanga support zobowa Bwanjiso
Umakwana koma kalindo suyangana nkhope ukafuna kungalura chilungamo
Km kalindo umakwana 😂😂😂😂 ati manyaka ngati awa sitikuwafuna ayi
We olways behind u mr bon
UTM alliance aford zintheka
Intro yokhayo...mwalamwalatu 🔥🔥🔥
Koma chilungamo Malawi anachagamuka mcp ngat simukuziwa munalowa chifukwa kunali ma demo ndiye mukuona nga anatha? Mukufunika kumangolapilatu apa no chance
Mumakwana ❤❤
Malawi freedom fighter. we love you The ...DC
Intro yasintha, tsopano akuti "Chi Boonie Kalindooooh"
The DC 🔥🔥🔥🔥🔥
mwana ooooopsya kwambiriiiiii
Bwana kalindo ingoyambisan chipani chanu tizakuvoteran coz a opposition sali serious kumene
It is true that opposition leaders are dormant whether they like or not but they are. We Malawians are tired and worried about them. May be they're receiving some money which makes them silent, please work up!!!!!!!
My boss booon kalindo,our freedom savior and fighter.
Powerful 💪💪💪 Ife sitikuwopa tili pa buyo pako
opposition yakedi yaziiii atupele ndia DPP angokhala ziiii akungoyang'anira basi koma akufuna kuvoteredwa
Mkulu uyu tidzamulira one day,he got love for his country
Mmatilimbikisa ndi kutipanga lerise up Amalawi ife ❤🔥🔥
Do all you can do to awake the opposition leaders
Ine ndi nchewa koma mcp ndi agaru nyasi zisatiipitsire mbiri uchitsiru umenewu udayamba ndi kamuzu, kuno pakati mcp yaluza ndale mpaka kupha azawo
Si Mchewa iwe, DPP inkazunza aChewa omwewo.
Am not really happy with the way opposition is handling the public affairs,,
Ichi nde ndichi booooni kalindo🎉
Koma zikoli mmmmm zafikapoo
Tiyipatsa Moto 🔥🔥🔥🔥🔥
God bless 🙏 you kalindo😅
Zikuchita kuonesekatu kuti ngakhaleso a tawina a opposition palibe chomwe chingasithe
Our pangolin tilinawe limodxi Bon osaopa,osafooka,
Ma bodza sangawine olo atatani ine ndineso mchewa awawa kapume
Let kalindo to run for Presidency
Mulungu azikudalisani a president athu anthu osauka ife
Achewa yo siwose ena anyasidwa nayoso utsogoleri umeneu.
Mwina akufuna muchite kwagwira Malo obisika kuti azuke inu zoona ife achinyamata tikuchita mantha kubwelera kwathu kuti tizikapanga ma business kuopa ulamuliro wa khaza omwe uli dziko lathu lomwe tabadwira zoona koma kumati kuli inu omwe mumazitcha kuti ndinu Andale mumathaso kukalowa nyumba ya malamuro zukani zukani atsogoleri athu kwakwana tsopano Atupele ,, Peter muthalika,, Chihana,, Joyce banda,, Inu bambo asikono,, Ndikunena ndinuyo Timothy mtambo ,, ndi ansanu onse ,, tachangamukani please chotsani nyazi zimenesi
Ndiposo ndizoona kumene kuti achewa ndi ambili kuposa mitundu yose ku Malawiko
😊
Ipatseni moto🔥🔥🔥
Karido ❤❤❤🎉🎉
The DC
Chi born kalindo❤
Aford UTM alliance tidusa popanda opikisana nawo.
MCP is now bringing tribalism but just to remind them that Yao ndintundu waukulu kwambiri Malawi yonse
The DC❤❤❤❤❤❤❤
Opposition achuluka dyera sangagwilizane
Kodi Mr Kalindo, simungakoze ulendo osawadziwitsa ma president a opposition kuti akadzuke...?. Chifukwa Boma la tonse mmm likuning'inatu heavy as tsabora., Chakwera must resign ndithu 💔💔💔💔
😢😢ndip Eeeee atiphweteka
@@agnesgwaza9165 Ine daily mtima kuwawa ndikamava ma challenge awo kuti mpaka 30 years
Raster kumbuyoko amakhala ali cheucheu😂
Opp0dition yadyetsedwa dekhani ndi mcp
❤❤❤
Mr SSS
Mbambande madala mumakwanila
Ulem wan boss man tiri pambuy pano
❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤
You are talking sense bro
Welcome the dangerous child
Peter nayenso akugona kwambiri.....Chikangawa mmene amasokonezera 2020,
Nde mukudikira a Malawi kut aonde kaye kenako akuikeni pa mpando inu muzidzanjoya.kodi a Peter ,kufatsa kumeneko kwamtundu wanji ....check out
Osusawa sakutithandiza
When are we protesting
Koma why sakuyamkhulapo za manganya ku mcp
Chakwera anapha Chilima
Good Messnge Chakwela you mast go
Mwatukwana president 🤣🤣🤣🤣ua-cam.com/video/WRDkQ8s_34k/v-deo.htmlsi=PkGoYsuJRKSW0v4p
ThE dC😂
Inu puppies wa MCP sichipani cha fiti
Zowonadi anthudi agona.ifa ya anthu onse aja sangawa vote ataa.
Mumakwana ❤❤
The DC