KWACHEMA KUBWEZA MOTO CHAWEZI |

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 6 вер 2024

КОМЕНТАРІ • 76

  • @momuumro
    @momuumro Місяць тому +11

    Mbuzi Chawezi
    Iweyo tangopanga Za MCP yakoyo usalimbane ndi UTM
    Mesa inu a MCP ndamene mwamupha Chilima
    Nde chokhalira mu mgwilizanomo ndichani?
    Chawezi ndiwe mbuzi kwambili

    • @JustinLipipa
      @JustinLipipa Місяць тому

      Ndiwa Mcp uyu, anthu mwawaphera mtsogoleri akhalebe komko

  • @HeinzeVictorMumbai
    @HeinzeVictorMumbai Місяць тому +4

    This chawezii he's MCP member

  • @MAYAMIKOCHALIRA
    @MAYAMIKOCHALIRA Місяць тому +2

    Palibe
    Nkhani apa...ngwilizano unatha ...adekhe why?

  • @user-qz1rp5mh9e
    @user-qz1rp5mh9e Місяць тому

    Iwe chawezi president ananena poyera kuti ayima in public mzake ali pomwepo mmmmm ine si wandale koma mzeru mzako ndi zofoka kwambir

  • @martinnyirongo2892
    @martinnyirongo2892 Місяць тому

    Achewa alibe respect ndipo ndiwophangira kwambiri, utm yachita bwino

  • @MisheckAselo
    @MisheckAselo Місяць тому +3

    Mgwirizano unatha kale mu 2020 kadasala ndikutulukaku☝️

  • @JohnFrank-cg1yh
    @JohnFrank-cg1yh Місяць тому

    Tikuyenela kumapephela tsiku ndi tsiku, nthawi ndi nthawi chifukwa satana ndiwochenjela atha kutigwesa m'mayeseli

  • @aaronziyeretsa6420
    @aaronziyeretsa6420 Місяць тому

    It's a move by DPP and they have allowed kabambe to be leader in order to redirect all UTM followers back to DPP

  • @user-sm6pr9cg2q
    @user-sm6pr9cg2q Місяць тому

    Zomwe adagwilizana chilima adanena pa press briefing kt ndi 5/5 ndy inu mukut anadziwana awili bwanji

  • @Brihippo
    @Brihippo Місяць тому +1

    Komaso muthu akamwalila pamabeera wina basi

  • @user-gj4li2gc8o
    @user-gj4li2gc8o Місяць тому +1

    Kaliat ndi kathyali nfiti yaikaz

  • @user-mh7cc8up4i
    @user-mh7cc8up4i Місяць тому

    Palibe chifukwa cholembela kalata yothela ubalewawo nde asadijile kalata kodi mr chikangawawo atava zimezi anayitanapo a UTM kuti akambilane zakutuluka kwa UTM? Zomatiseka kumaso uwe chawezi uzingodya misokho ya amalawyo osatipusisa mene munkapanga zachipongwe ndichilima ndemumati atani palibeso zodikila myezi mafuna mugule UTM yose nde mwauponda mwakumananazo zanadulila muwona nyekgwe a MCP muwuzeni chimwendo abeleke over muzapenge gwilizano ndi ana achimwendo

  • @user-si7po9sd5i
    @user-si7po9sd5i Місяць тому

    The only wise and rational person who leaves a beautiful place where everything is going well and goes to live with the people who are suffering,will find favor in the presence of the almighty God.

  • @godfreyamos7452
    @godfreyamos7452 Місяць тому +1

    A Chawezi kunali amzathu , muzatha mosakhala bwino

  • @mbelengamavuto2517
    @mbelengamavuto2517 Місяць тому

    Mbuzi iwe chawezi mafuta sangatchipe kuno iwe galu iwe usadandaule ukhala wankulu wa MBC galu iwe

  • @user-ic1zy4zj1c
    @user-ic1zy4zj1c Місяць тому

    Mabwana a chawezi tamuchoseni uyu pa program imeneyi, we need balanced issues, awa ndi achibwana, a Mbuye Mulungu wa zonse mkatheni chawezi yu amen

  • @GiftMathewe-fr3kn
    @GiftMathewe-fr3kn Місяць тому

    Sanalakwise chifukwa zomwa adagwilrizana mungwilizano wawo palibe akuziwa

  • @DysonUmali
    @DysonUmali Місяць тому +1

    Chawezi palibe zodekha MCP is helpless to UTM. What you should focus is MCP agenda

  • @frezarphiri3480
    @frezarphiri3480 Місяць тому

    Ayi choka iwe chawezi utm yachitabwino kutuluka musanga kt akozenyumba yawo even chilima akanavela kalindo bwezi izi kulibe lero winiko amanena zoona kt tulukani mu tose koma sanavele

  • @CathrineBizza
    @CathrineBizza Місяць тому

    Nkona anamuxhotsa ntchito ku mbc uyu xhitsiru wamva

  • @rabsonswathera738
    @rabsonswathera738 Місяць тому

    Kuchoka mungwilizano kwachitika munthawi yake

  • @Brihippo
    @Brihippo Місяць тому

    Timafikila kuti chilima atiyakhule poti wamwalira a Patricia watiyakhula

  • @jameshuwanzulu
    @jameshuwanzulu Місяць тому

    Or ndi dzina lomwelo likungosonyeza kut ndi wa MCP

  • @WisikiBlack-gj4gu
    @WisikiBlack-gj4gu Місяць тому

    Ndipo monga ngati ine ndikuti anakhonza kwambili kutulukako mcp down

  • @user-ql8nf2vb8s
    @user-ql8nf2vb8s Місяць тому

    Ndipo achawezi sawlekeze kuonesa mutu ukakwela galimoto yako tikukhazula tionana aise manyi ako wanva

  • @user-qk2hw4ex3c
    @user-qk2hw4ex3c Місяць тому +2

    Chisilu iweyo simadziwa Kuti Pali ndale kupha chilima

  • @yotamumahomed1313
    @yotamumahomed1313 Місяць тому +1

    Kod iweyo why ukukamira zimenezo ndiwe mbuzi et ?

  • @user-gj4li2gc8o
    @user-gj4li2gc8o Місяць тому

    Utm yagulisa chipani ku dpp

  • @user-ck7eb7tb7v
    @user-ck7eb7tb7v Місяць тому +1

    Iwe apanga nthawi yoyenera, afufuza bwanji za ifa ali ku tonse komweko? Aasa!

  • @leonardmalirana7423
    @leonardmalirana7423 Місяць тому +1

    Ngati, mgwirizano unali wa anthu awiri basi uthepo winayo anatisiya ndiye UTM isiyeni

  • @DamianoGabriel-sh2mf
    @DamianoGabriel-sh2mf Місяць тому

    Chawezi capaign director wa mcp banja likatha palibe za ulemu

  • @user-jn9tz3li3v
    @user-jn9tz3li3v Місяць тому

    Satana akalowa mpovuta kumutulusa, Chawezi amlowa satana.

  • @DysonUmali
    @DysonUmali Місяць тому

    Whether the votes will be minus 20% we don't care . USI and the cabinet ministers can remain at MCP we don't care .The best Usi can do is to start his party and do the alliance with MCP . That will be his correct decision. He must not use UTM emblem because at UTM I don't see his impact achedwa kwambiri.

  • @peterdanie4684
    @peterdanie4684 Місяць тому

    Chawezi great analysis

  • @idilissmuyer2914
    @idilissmuyer2914 Місяць тому

    Pamtumbo panu inuyo mwasowa zokamba mamwapwala anu

  • @UsumanLuwayo
    @UsumanLuwayo Місяць тому

    Ngati Dewesi ali pa banja njofunika kumunyengera mkadzi wake nde kupanga dzoti anthu adzamugwire mkadziyo akuchita chigololo nde iyeyo adzamve, then tidzaone ngati adzadekhe osathetsa banja antil 3 months

  • @samsonmtumbati4855
    @samsonmtumbati4855 Місяць тому

    Programe iyi kulibwino angoyithetsa chifukwa zimene zimakambidwa akumapanga back up mcp so palibe Amalawi yingatithandize Programe yanuyi ayi just suspend it

  • @WisikiBlack-gj4gu
    @WisikiBlack-gj4gu Місяць тому

    Achilima anali odekha mtima, koma ku bwela kwawo ulendo wakunja uja koria,anali ndicholinga chotuluka mu tonse kale, koma tsoka asanaphume kubwela kwaku koria ,ndimene amapita kumarilo akusambala posadziwa kuti awusi chisisi anakamuuza kale chakwela, kodi zonsetu tikuzidziwa koma ndalama ndalama, koma mulungu simuthu

  • @user-qk2hw4ex3c
    @user-qk2hw4ex3c Місяць тому +1

    Chawedzi ndiwe osokonedza

  • @SamukLungu-zg7fl
    @SamukLungu-zg7fl Місяць тому

    Chawezi zinarakoro ndiramunthu wamukazi anakupasayo anakuwononga ndiye utisamare uzapezeka mumavuto mumene umamwera mowa iweyo🆗

  • @vincentkamangamr9062
    @vincentkamangamr9062 Місяць тому

    Chawezi umawoneselatu kuti ndiwe wa MCP all times on this program

  • @DysonUmali
    @DysonUmali Місяць тому

    In life ngati mkazi wakukana olo mutalankhula motani it's helpless to the man.
    UTM is done with MCP

  • @DalitsoPhiri-sq5nl
    @DalitsoPhiri-sq5nl Місяць тому

    Komatu chawedzi pena amayankhula ngati mbuli zedi kodi amene samadziwa kuti alliance ya utm ndi mcp inali yoti five yrs wina akhala president kenako wina azaimeso, ndi chifukwa ichi ndi chomwe chinabwelesa kusagwilizana cz ingakhale Dr late SKC ananena poyera kuti ngati Dr chakwera sakufuna kutula pansi udindo ndiye tiyenera tikavote. Utm kutuluka siinalakwise aii cz mcp siinalemekedze ingakhale imfa ya chilima mzinthu zambiri kumapanga msonkhano anthu akulilabe kenako uziti afulumira kutuluka ukhalike ndithu ngati akukunyemera tazingodya makobidiwo komano usaganize mombwambwana aiii

  • @estonmnthali3719
    @estonmnthali3719 Місяць тому

    Chawezi ndi wa MCP

  • @user-nf3ik3ff6y
    @user-nf3ik3ff6y Місяць тому +1

    Chawezi ndiwe Galu

  • @user-ml4bl2ll2g
    @user-ml4bl2ll2g Місяць тому

    Chawezi samalira ayise we know ukulimbana ndi azipani zotsutsa samalira ayise I know you are there for mcp

  • @SheenahMwalabu-iz3pr
    @SheenahMwalabu-iz3pr Місяць тому

    Kodi chawezi yu mumamutengelanji? Uyuyu adzandilakwitsa one day. Victor or abel, banda are the bes uyu ndiwa mcp. Sadzatheka Chawezi akupeza zabwino ku bomaku ndipo ativuta kulera 😅

  • @patrickmwakilasa7198
    @patrickmwakilasa7198 Місяць тому

    Agalu inu

  • @MaryMlongoti
    @MaryMlongoti Місяць тому

    Chawezi umatha

  • @BehindThecamera-xo1qg
    @BehindThecamera-xo1qg Місяць тому

    Miyezi 4 inachuluka anthu ambiri akanasala ku mcp , achita bwino kutuluka fumbi la kuchikangawa lisanathe .

  • @WilfredChinkono
    @WilfredChinkono Місяць тому

    DK simunthu wamba UTM ikutenga boma 2025

  • @DysonUmali
    @DysonUmali Місяць тому

    Chaweza what you should know is we didn't do a hasty decision . It a fine a decision and you can't change it.
    We are not desperate rather and we as voters cannot take it
    Chawezi you are MCP and no body can listen to your views .
    Member wa nzeru cannot proceed to be in alliance with MCP .

  • @user-si7po9sd5i
    @user-si7po9sd5i Місяць тому +1

    Where is victor

  • @petroszgambo9949
    @petroszgambo9949 Місяць тому

    Useless program

  • @BehindThecamera-xo1qg
    @BehindThecamera-xo1qg Місяць тому

    Ulemu wa chani galu iwe chawezi, umamupasa ulemu munthu oipa

  • @isaihmagani5697
    @isaihmagani5697 Місяць тому

    Chawezi wabodza iwe, sukuyenera kukhara analysis poti zuonekeratu ndiwe wa MCP

  • @leonardmalirana7423
    @leonardmalirana7423 Місяць тому

    UTM IS NOT THE FIRST PARTY TO MOVE OUT OF THIS ALLIANCE , PEOPLE ARE TALKING ALOT BECAUSE IT HAS MANY YOUTH FOLLOWERS SO ZIKUBAYA ANTHU AMBIRI.

  • @PaulChaleka-lb4vx
    @PaulChaleka-lb4vx Місяць тому

    Chawezi ndi wa chakwera

  • @user-lj7lm6ly7z
    @user-lj7lm6ly7z Місяць тому

    Ine anthu awa amandionekera mwa mcp cp eeee ndiye aaaa sinkonda kunvera zamenewa

  • @Raph-kayRaph-kay-g5v
    @Raph-kayRaph-kay-g5v Місяць тому

    Chawezi uzafa ngati garu

  • @Chrissyluwe
    @Chrissyluwe Місяць тому

    Chawez u hv no timing

  • @AliceChipeta-pc3nb
    @AliceChipeta-pc3nb Місяць тому

    Chawezi chawezi chawezi

  • @user-oc8nj3or6y
    @user-oc8nj3or6y Місяць тому

    Ndi ntchito yawo,,,anali kuti? Nthawi yonseyi

  • @user-my5jj5we5j
    @user-my5jj5we5j Місяць тому

    Unuso mukuziwa mugwilizano panalibe

  • @user-cs6zy3ix8d
    @user-cs6zy3ix8d Місяць тому

    Chawez ndi iwe mbuzi

  • @PatrickDisple
    @PatrickDisple Місяць тому

    He knows only how to speak but not to understand what he is speaking. Mr Chawezi 😅

  • @PiusChawinga
    @PiusChawinga Місяць тому

    Wabweza bwanji?

  • @tonnychimbiro
    @tonnychimbiro Місяць тому

    Zinthu zake

  • @chimwemwechiundira6002
    @chimwemwechiundira6002 Місяць тому

    Halayansi yabayatu

  • @ChikuMatemba
    @ChikuMatemba Місяць тому

    we don't like Chawezi on this Program

  • @KestonNGUBO
    @KestonNGUBO Місяць тому

    Zoonad iwe

  • @user-gy8yn6qw2k
    @user-gy8yn6qw2k Місяць тому

    Ineyo i don't like this guy is not the best for me ........

  • @isaihmagani5697
    @isaihmagani5697 Місяць тому

    Chawezi ma comments ako ngooneseratu uli mbali yinayo uli against UTM