Це відео не доступне.
Перепрошуємо.

Ogulitsa Ziwalo Xa Anthu Agwida Ku Thyolo.

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 7 лют 2023

КОМЕНТАРІ • 156

  • @augustinechibbalazi8897
    @augustinechibbalazi8897 2 місяці тому +5

    TA you are more a patriotic citizen.May God bless you.Malawi is lacking such leaders even in religious and political fields.

  • @khoviwaedward
    @khoviwaedward Рік тому +25

    This guy is really true Malawian legend.. Wapulumutsa moyo wamwana. The government should recognise him, awards is coming bro

    • @innocentjames_01
      @innocentjames_01 Рік тому +1

      For sure 😊

    • @hanabrighton9903
      @hanabrighton9903 Рік тому +1

      Koma zoona this man must be recognized as a legent

    • @user-nf8tg6ez6u
      @user-nf8tg6ez6u 5 місяців тому

      Mulungu akudalitseni amfumu ndi manjolo

    • @JosephMkandawire-sq7uf
      @JosephMkandawire-sq7uf 4 місяці тому

      Mumagula inu guys

    • @CatherineDesire
      @CatherineDesire Місяць тому

      Anakakhara Ngati Maiko anzathuwa aindithu anakapangapo kachithokodzo ndithu kooneka pa Mfumuyi NDI azakewa Koma🤔mmmm h Malawi a Magadzi mmmm ndukaika anakakhala mwina NDI dzina Lina otsati Malawi coz ma🔥gahena mmmmmh ayi ndithu kuteloko lakwiya bomalo akumipandoko 😂😂😂😂😂😂 Kuti ena apulumutsetso mwana?coz iwowo NDI👹👿👺kare kupha NDI kuononga 😂😂😂😂😂 wafikapo aise Ma🔥lawi iwe🙌ndakuponyera kukhara ngati unalengapo munthu Malawi👹👿👺🤔😔

  • @gesinasutherland9241
    @gesinasutherland9241 Рік тому +7

    long live amfumu ndi Manjolo..Ambuye akutetezeni

  • @olivechikwindi9126
    @olivechikwindi9126 Рік тому +6

    😭😭😭😭YESU akuchedweranji kubwera koma?AMBUYE akudalitseni A/T ndipo akupatseni moyo wautali and Mr manjolo God bless you mukhale wotetedzedwa anthuwa

  • @charlesmpaso2383
    @charlesmpaso2383 Рік тому +6

    Anthu awa akuyenera kukwezedwa udindo komaso akufunika chitetezo.....mulungu oziwa kusamala akutetezeni mu zonse pamodzi ndi ma family anu.... AMEN AND AMEN.U DESERVE AWARDS GUYS.

  • @ChimwemweNthukwa-fw3qj
    @ChimwemweNthukwa-fw3qj 5 місяців тому +3

    Amen Ambuye alemekezeke, amfumu abwino okonda amalawi anzawo!! Ambuye akudalitseni a amfumu

  • @chifundomhango3324
    @chifundomhango3324 Рік тому +8

    Good job Mr Manjolo & T/A❤

  • @rosebanda3613
    @rosebanda3613 Рік тому

    Ulemu wanu manjolo and hands up to Ta. TA you are wise like king Solomon may God bless you with more wisdom

  • @princekabvina1718
    @princekabvina1718 Рік тому +9

    Manjolo he deserve an award,,,well done Mr Manjolo and T/A

  • @moseschizyibwa4463
    @moseschizyibwa4463 11 місяців тому +2

    I like this program. Watching from zambia, Moses

  • @ausbonchimgolo9984
    @ausbonchimgolo9984 Рік тому +4

    Manjolo and T/A they deserve a medal

  • @user-kh9cr9dl7x
    @user-kh9cr9dl7x Рік тому +2

    Really appreciate nkhani izikhala in full video osabisa maina olakwayo ndiokhudzidwawo.

  • @user-ms1ll6hj4u
    @user-ms1ll6hj4u Рік тому +2

    My God bless you mr manjolo ndi
    T/A mukhale ndi moyo fumu❤

  • @jamesngalande4345
    @jamesngalande4345 Рік тому +5

    thats true your heros boma likuyenera kukuthokozani kuti anthu ena akawona atengelepo phunziro

    • @bjmtalimanja5073
      @bjmtalimanja5073 Рік тому

      Pakufunika apasidwe unduna wa za chitetezo mdziko mino.wosati zisilu zomwe chakwera azisankha zija

    • @fosterphiri5366
      @fosterphiri5366 Рік тому

      Mulungu akukwezeni afumu ndakutukulilani muma ja a yehova

    • @juniorbvumbwe9822
      @juniorbvumbwe9822 Рік тому

      Akanagwirisa mawu ot opha nzake aphedwe bas

  • @johndaka6368
    @johndaka6368 Рік тому +1

    That's ws good pran AMALAWI
    Am John from Lusaka Zambia

  • @collinsassenga3711
    @collinsassenga3711 Рік тому +1

    a T A Mr manjolo mulungu akudalitseni, a T A kuyambira lero ndinu mfumu Solomon.

  • @ephraimnjikho9307
    @ephraimnjikho9307 Рік тому +2

    If all Malawians were like Manjolo and the TA, such cases could have been on the decrease.
    People are very hard hearted.

  • @gkay-striker
    @gkay-striker 6 місяців тому +1

    You did a great job

  • @luciachimbalawala3545
    @luciachimbalawala3545 3 місяці тому

    God bless you manjolo and the T/A for job well done im watching from lusaka zambia❤

  • @usherkays4379
    @usherkays4379 Рік тому

    Thanks to the TA for exposing the criminals and protecting the nation

  • @chrissyamanda5510
    @chrissyamanda5510 Рік тому

    Manjolo atetezedwe ndi mwazi wa Yesu
    Ndikutha kuwona kuti moyo wake uli pa chiopsezo koma Ambuye wanthu ngwa moyo ndipo ndi mgonjetsì

  • @williamchanza5338
    @williamchanza5338 Рік тому +3

    This guy s a hero

  • @HenryGulani-fq5js
    @HenryGulani-fq5js 2 місяці тому

    Mlu dzikomo kwambili mulungu Akudalitseni 🙏🙏 ine ndili Joz

  • @chitimbethegreat8560
    @chitimbethegreat8560 Рік тому

    Mr TA well done mwagwira ntchito mafumu ambiri amakonda ndalama and mchitidwe oterewu umakula chifukwa mafumu amatenga nawo gawo koma Inu simunatero ulemu wanu ndi Mr majolo

  • @user-nf8tg6ez6u
    @user-nf8tg6ez6u 5 місяців тому +2

    T/A akutetezeni Mulungu ndi manjolo akupatseni moyo wautali

  • @jamesngalande4345
    @jamesngalande4345 Рік тому +3

    Jesus

  • @collinsassenga3711
    @collinsassenga3711 Рік тому +1

    Chilungamu chiyende ngati madzi, AT ndi mr manjolo mulungu akudalitseni.

  • @Davison-jr6ev
    @Davison-jr6ev 5 місяців тому

    Yes this guy and the TA must gain some thing from the the government for rescued the boys who was about to lose his life,

  • @CatherineDesire
    @CatherineDesire Місяць тому

    😂😂,😂koma Lawez 🙌wafikapo eeeh!dzikomo amfumu Mlungu akupatseni moyo wautali ndithu

  • @johndaka6368
    @johndaka6368 Рік тому +1

    Manjolo akhale wa police am JOHN daka from Lusaka Zambia

  • @MacDonaldkachala-cm5gc
    @MacDonaldkachala-cm5gc 2 місяці тому

    Don't forget the big buyer also hails from the same.........'.............

  • @matiasncalaila4003
    @matiasncalaila4003 Рік тому +1

    Nanga Judgement yatha bwanji? Nanga anthu 5 womwe akugulisapo ndi ati? Amagulitsira kuti? Nanga anthu amenene anagula Boma lichita nawo chiyani? We need Justice. Manjolo Ambuye Akudalitse komanso a T.A pamaganizo yawo ya bwino yofuna munthu wamoyo, tikana luza mwana.

  • @DenisAntonio-bn5ey
    @DenisAntonio-bn5ey 8 місяців тому

    Big up to Mr manjolo and the t.a, 4such a good job done.❤

  • @oliviasullivan1059
    @oliviasullivan1059 18 днів тому

    Nkhani yogulisa ziwalo zinayamba kale kale ndipo ine ndikukumbukira boma likuopyeza anthu kuti anthu asiye kunena boza kuchitisa anthu anzao mantha. Pano anthu ngati Manjolo ndi a T/A ndi osowa. Nchitidwe umenewu uthe mulungu achite nao opha anthu .
    Zikomo a Ntola nkhani Ambuye akutsogolereni mu nchito imenei. Mwapulumusa ena.

  • @user-tf1lk5if6k
    @user-tf1lk5if6k 4 місяці тому

    😭😭😭😭😭 God bless you my brother all the best in your life 🙏

  • @lindsonexton8563
    @lindsonexton8563 Рік тому

    Inu ndi akatundu odziwa kufufuza nkhani, you deserve a medal

  • @janetmanda6412
    @janetmanda6412 Рік тому +8

    After so many years now the secret is out, my question is is the police keep secrets also?

  • @user-nr8cu6we3r
    @user-nr8cu6we3r Рік тому

    Government give thanks to the people for sure they did great job 👏

  • @user-df2me5ro2i
    @user-df2me5ro2i 10 місяців тому

    Well done Mr T/A

  • @ChimzyBinali
    @ChimzyBinali 2 місяці тому

    Ine ndimaona kuti boma litenge mbali ogula ndiogulitsa azirandira chirango chachikuru

  • @user-ts4wy3yr5y
    @user-ts4wy3yr5y Місяць тому

    Mukuloleranji ambuye anthu oipa mtima awa azichita bwino dziko lolenga nokha

  • @paulkaunda6780
    @paulkaunda6780 Рік тому +4

    Dziwalo zimapita ku boma asaname

  • @marynkhata9707
    @marynkhata9707 Рік тому +3

    Afumu anzelu mulungu akudalitseni

  • @ChinsinsiMaseso
    @ChinsinsiMaseso Рік тому

    Boma lichitepo kanthu, big up Manjolo and T/A

  • @user-ou5mx8dg5s
    @user-ou5mx8dg5s Рік тому +1

    Keep it up Manjolo and T/A. May the almighty God, bless both of you.

  • @user-hm9vv4wi9u
    @user-hm9vv4wi9u 5 місяців тому

    Nyamatayu Boma limupase kagalimoto

  • @ayamijackson1443
    @ayamijackson1443 Рік тому +2

    Chochi ndi kumati lamulolonyonga lichoke nooo am saying nooo!!!!! Athuawa akuenela kunyongedwaaja ndiawa for sure ❗❗❗❗❗❗❓❓

    • @hucklyrajabu7137
      @hucklyrajabu7137 Рік тому

      That true my bro wapha mzake naye aphedwe chifukwa kuchotsa moyo wamzako sichinthu chapafupi

  • @PeacefulWildFlowers-sl8er
    @PeacefulWildFlowers-sl8er 6 місяців тому +1

    Mafumu a smart❤❤❤

  • @user-bq1mb4fk1b
    @user-bq1mb4fk1b 2 місяці тому

    Malamulo nkhumi amulungu;Usaphe ";

  • @noahmshanga-rb1xc
    @noahmshanga-rb1xc Рік тому

    Mmmmm! MR MANJOLO and the headman they need to be on the better position and please my fellow youths do not be influenced in such calectors even if things can be bad in life try your best to do the right thing like what MR MANJOLO and the village HEADMAN.

  • @lukainnocent5380
    @lukainnocent5380 Рік тому +1

    Thyolo chilazulo maboma aukape kwambiri kamalawi watunthu alomwe zisiru zokonda kupha anthu moyo wawo ndi waku Mozambique basi

    • @belindansona5296
      @belindansona5296 Рік тому +1

      Kuyankhula mopusa kwinako anthu saphana mxieeee

    • @SirpromiseMatabwa
      @SirpromiseMatabwa Місяць тому

      Mbola yanu malowesa ndale ndikusankhana mitundu eti anthu akuchikwawatu kuthyolo ndikubwalo

  • @SirpromiseMatabwa
    @SirpromiseMatabwa Місяць тому

    Well amfumu amchacha

  • @BeautyMtambo
    @BeautyMtambo 5 місяців тому

    Amalawi tiyeni tigwilane manja kupewa nkadza Kwa abale athu tiyeni tikondani wina ndinzache

  • @RaphaelMusa-x5t
    @RaphaelMusa-x5t 27 днів тому

    It's really fine

  • @augustinechibbalazi8897
    @augustinechibbalazi8897 2 місяці тому

    Malawi is no longer at ease.Laws have to revised

  • @Elvin-dr8tv
    @Elvin-dr8tv 4 місяці тому

    Well-done Manojolo

  • @dalitsochibisa2986
    @dalitsochibisa2986 Рік тому +1

    Zikomo kwa bwana TA and the team who helped to rescue the boy

  • @kingmakala3919
    @kingmakala3919 Рік тому +1

    GOOD JOB BRO🙏

  • @EdsonSichali
    @EdsonSichali 10 місяців тому

    Munthu amene anafika kwa munthu wachilungamo amene anauza aT/A ndiye amene wachilungamo zikomo

  • @PaulThawale-cq7ev
    @PaulThawale-cq7ev 3 місяці тому

    Malawi akufunika atsogoleri ngati awa agog Mulungu akudaliseni

  • @officefileofficefile4771
    @officefileofficefile4771 Рік тому

    Dziko la Malawi atulusidwa amenewo, chisanzo nachimpanti anamutulusa kale Ali kuno ku South Africa, nkhani ngati zimenezi athu m'boma zimakhala kuti zikuwakhuza

  • @ThokoKaipa
    @ThokoKaipa 4 місяці тому

    God is revealing himself to people,,,that child is just innocent and God is watching upon him

  • @lestermhone2710
    @lestermhone2710 4 місяці тому

    Amfumu ndi Manjolo apanga zaumunthu. Boma liwathokoze basi

  • @dolikakamanga203
    @dolikakamanga203 Рік тому

    Good job may God bless you guys

  • @PiliranTChimalizen
    @PiliranTChimalizen 4 місяці тому

    Km a T/A awa ngofunika award

  • @user-df2me5ro2i
    @user-df2me5ro2i 10 місяців тому

    Manjolo u are a king

  • @kingkayaye
    @kingkayaye Рік тому

    on my way to Mr manjolo and Mr T/A they deserve it🏃🏃

  • @charlurquhart5788
    @charlurquhart5788 10 місяців тому

    Mwana obweresa nxakeyu asatuluke cz anauyamba kale

  • @user-gg4pw3zz3g
    @user-gg4pw3zz3g 4 місяці тому

    Manjolo wanena zoona kuti boma ndilo vuto lalikulu anthu ena atagwidwa koma pano anamasulidwa

  • @Davison-jr6ev
    @Davison-jr6ev 5 місяців тому

    Anthu oterewa akuyenera kukalowa mundane moyo wawo onse chifukwa ndizoipa kupha munthu osalakwa

  • @LenackMoyo-jz2fl
    @LenackMoyo-jz2fl 9 місяців тому

    Please those who are doing this dirty thing should face the law.

  • @user-en3ts5cp9l
    @user-en3ts5cp9l 5 місяців тому

    Akanachulukira anthu oterewa bwezi zili bwino amfumu

  • @PeacefulWildFlowers-sl8er
    @PeacefulWildFlowers-sl8er 6 місяців тому

    Ulemu wanu mr manjolo❤❤❤

  • @harrisonmwanga9812
    @harrisonmwanga9812 Рік тому

    Zimenezo zinali nthawi ya kamuzu,yemwe anali ndi lamulo okupha wina naye aphedwetso.democracy yafika ndi zithu zoipa kwambili.

  • @HawaChifi
    @HawaChifi 4 місяці тому

    Strong man manjolo💪

  • @user-qc5hj1gy4s
    @user-qc5hj1gy4s 5 місяців тому

    Tili.mmasiku otsiliza 2timonthy3v 1.....end

  • @steven22issah97
    @steven22issah97 Рік тому

    Just a few people can manage it. Well deserved Mr Manjolo and T/A Ngomano

  • @usherkays4379
    @usherkays4379 Рік тому

    Manjolo deserves a reward from the government

  • @sydneykumisuku1380
    @sydneykumisuku1380 Рік тому

    Few good men!

  • @peterbanda7003
    @peterbanda7003 Рік тому +2

    Iyi ndi mibawadi iyi

    • @samuelmtonga8393
      @samuelmtonga8393 Рік тому

      God bless you Mr T A and Mr manjolo Mulungu akupaseni moyo wautali

  • @greychizaka4088
    @greychizaka4088 5 місяців тому

    True hero

  • @BeautyMtambo
    @BeautyMtambo 5 місяців тому

    Ineyo ndikuyamika a T/A ndi A police amumudzi mulungu awa tsogolele

  • @janetnpaul426
    @janetnpaul426 Рік тому +2

    Chonena ndilibe 😭😭😭

  • @chifundositolo5387
    @chifundositolo5387 Рік тому

    Bwana minjolo ulemu wanu ndipo mu kufunika kukhala wa police

  • @promisemakawa1556
    @promisemakawa1556 Рік тому

    T/A ndi mr manjolo muyenera kulandila award, boma liyenera kukuganizirani, tsoka boma lathuli ndilopondereza

    • @pauldaka7966
      @pauldaka7966 Рік тому

      Tikuyeneradi kudziwa mmene chigemulo chakukhoti chinayendera abale inu

  • @mcdonaldkamanga6919
    @mcdonaldkamanga6919 5 місяців тому

    Title of the song please

  • @bobsaidi7691
    @bobsaidi7691 Рік тому +1

    A tiye Wawa ndi anzelu kwambili

  • @carlossadimba595
    @carlossadimba595 5 місяців тому

    Koma nanga mabwana omwe amagula Ku nchalo Ku chikwawao tiwadziwe nawo ife kwathu mkomweko

  • @ayamijackson1443
    @ayamijackson1443 Рік тому +1

    Ooooo my god 🤔🤔🤔🤔kama amalawi 🇲🇼 mmmmm

  • @blessingsmasakala3285
    @blessingsmasakala3285 Рік тому

    Moti zigawenga zija zikanatutumuka manjolo anali pamavuto agulupu aja akanamutembenukilanso kt iweyo mission ija wailepheresa pazifukwa zilibwino ubale wamanjolo ndi a T/A panopa kamba mission yatheka nduthu

  • @happymguza1136
    @happymguza1136 Рік тому +2

    Mfumu ya nzerutu

  • @isaacmussa2942
    @isaacmussa2942 Рік тому +1

    Boma limadziwa zimenezo koma silichitapo kanthu

  • @user-np4xk9bx3e
    @user-np4xk9bx3e Рік тому

    Mulungu awaonjezere zeru Mr majolo and a T/A

  • @aleksawilliams710
    @aleksawilliams710 Рік тому

    La 4o lakwana ,amenewo asatuluke,,,zinganizani aliwanu mwana

  • @lulukunkeyanih8271
    @lulukunkeyanih8271 Рік тому

    Nfipo ndinalakhala president...ndinakakupasani ...5mita

    • @florakaphanje4664
      @florakaphanje4664 Рік тому

      Amfumu mulungu odziwa kudalisa azikudalitsani munapulumutsa mwana w

  • @user-im4tc9qi4j
    @user-im4tc9qi4j 6 місяців тому

    Trader manjolo

  • @lawrencekathumba7585
    @lawrencekathumba7585 Рік тому

    Khaniyi ndiyopasa chidwi ndayisatila ndikuyinvetsesa,,, I ndikuyamikani nonse omwe munatengapo gawo kuti itifikile,, komanso funso langa ndilakuti bwanji sitinanve m'mene judgements inayendela ku khoti pa mulandu wanyamata ogulitsa anthu aja,, kuti anagamulidwa motani? A T/A angokambapo kuti anakanvela nawo mulandu koma sanakambe kuti anaweludzidwa motani anyamatawo?

  • @kedibonesegametsi2493
    @kedibonesegametsi2493 3 місяці тому

    Mmmmmmm My god 😢😢😢

  • @geee7672
    @geee7672 Рік тому

    Mwana, wapezayi ndi scoop. Atolankhani akuluakulu amagulidwa ndi mapoliticians to avoid this. Break into this industry. This is nothing but tip of iceberg. Mpakana umupeza amene amagula ma albino. Ine ndimakaikila mzimai wakumwanza uja

  • @HassanJailos-hx4qx
    @HassanJailos-hx4qx 6 місяців тому

    Madalawo zosawakhala serious 😮