ANA NDI ACHIBALE A ZIMAYI WADZUKA KUMANDA KULONGOSOLA

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 24 лют 2024
  • ANA NDI ACHIBALE A ZIMAYI WADZUKA KUMANDA KULONGOSOLA

КОМЕНТАРІ • 86

  • @CatherineDesire
    @CatherineDesire 2 дні тому +1

    Ku mpoto nde kuli ufiti wa serious akapha akapha anthu aphabasi tsamauka ku manda pamene kumwela amauka kumpoto kuli ufiti oyipa!anthu ambiri kumwera akumauka ku mpoto zero🙄

  • @siskanyirenda
    @siskanyirenda 4 місяці тому +5

    Mukamapanga zinthu please khalani serious munthuyo muzimuonetsa tizimuona munthuyo

  • @user-dk8ey5pu5w
    @user-dk8ey5pu5w 4 місяці тому

    Mzimayi ameneyo mugwireni,mumumenye makofi auluru omwe anamutuma. Wamutuma ndi prophet

  • @SleepyAnteater-bh5zo
    @SleepyAnteater-bh5zo 4 місяці тому +8

    Hanifa chonde uzitionetsako muthuyo ngati momwe amapangila azanu

  • @ziyamikanmakowa5981
    @ziyamikanmakowa5981 4 місяці тому +2

    Munthu wabwelayo sakufana ndi yemwe anamwalila ndiye akhalawao bwanji

  • @inessmsiyambiri8517
    @inessmsiyambiri8517 4 місяці тому +1

    Kodi ku lilongweko sanabwereko aaa

  • @user-ih3qe8ho3v
    @user-ih3qe8ho3v 4 місяці тому

    Zonama idzi akuchita kulakatula ngat thano hiyaa 😊

  • @YONA-v5o
    @YONA-v5o 4 дні тому

    Nde inuyo aku banja munthu woti mmakhalanaye simnamu fananitse ndamene anamwalilayo

  • @gracemphande550
    @gracemphande550 4 місяці тому +1

    Ulendo waku Lilongwe ayendako bwanji?

  • @user-rd4ft9nd8t
    @user-rd4ft9nd8t 4 місяці тому +1

    Kodi ku Lilongwe kwake mbali iti koma ngati zili zoona Ambuye alemekezeke

  • @BarnabeMacuane
    @BarnabeMacuane 9 днів тому

    Ndikupemba mamba ya profit ine Kuno ku mozambiaue

  • @user-co4ej4cw8r
    @user-co4ej4cw8r 3 місяці тому

    God have mercy

  • @tiwongehojaney5873
    @tiwongehojaney5873 4 місяці тому +2

    Za satanic izii munthu anamwalila ndi mzimai abwera bwanji zibambo aaa komatu anthu amulungu samalani tili mmasiku osiliza 😮😮

  • @user-hx4mz9nk9g
    @user-hx4mz9nk9g 3 місяці тому +3

    Aaa munthu wamayi kumwalira mpaka kuzabwela ngati nyamata bwino nazotu tizalandila nazo ziwanda zakomweko

    • @ChrissyChakhala
      @ChrissyChakhala 3 місяці тому

      H😊😊😊😊😊😊😮😊😢😢😅😅😅😮

  • @selinaalufasi3150
    @selinaalufasi3150 4 місяці тому +2

    ine sindikumva ataa

  • @user-dh4xl3jb9d
    @user-dh4xl3jb9d 4 місяці тому +1

    Zakumidima izi aaaa

  • @JosèFelixsailessFelixsailess
    @JosèFelixsailessFelixsailess 9 днів тому

    Zoipatu zimenesi

  • @JamLifa-xz8nc
    @JamLifa-xz8nc 3 місяці тому

    Mudzina Lamulungu wachifundo komaso wachisoni khulupilani mwa mulungu mmodzi ekha ndipo wanu sameneyoyo wanu adapita ndithu

  • @janetchinga695
    @janetchinga695 4 місяці тому

    Kuli profet ku Tanzania ku dasalama auka anthu ambiri pitani komweko kubuza dasalama

  • @sarahkamphanga
    @sarahkamphanga 4 місяці тому

    Tipasileni ndithu

  • @arseniomoraisfabiao6342
    @arseniomoraisfabiao6342 3 місяці тому

    Tatiwuzaniko dzina lá a prophet

  • @LufanMenard
    @LufanMenard Місяць тому

    Mmm zavta kwambili😂😂

  • @WysonMpatama-cv1mc
    @WysonMpatama-cv1mc 2 місяці тому

    Kodi a prophet amenewa anakupatsani zingati

  • @danielmaganiza
    @danielmaganiza 4 місяці тому

    Munthu anamwalira Ali wankazi abwela bwela bwanji Ali wammuna mmm😢

  • @kondwanimalikita5604
    @kondwanimalikita5604 4 місяці тому

    Iya za boza izizi zakumidima basi anangotumiza nkhalambyo

  • @JasiGoche
    @JasiGoche Місяць тому

    Nafe timazisowa ndipo zachitikanso ifa yotelo

  • @inessmsiyambiri8517
    @inessmsiyambiri8517 4 місяці тому +1

    Komatu mulandira nazo mzukwa aaaaaosowa munthu wa mmkazi abwera wa mmuna bwanji aaaaakomatu

  • @user-io8ig8xm6z
    @user-io8ig8xm6z 3 місяці тому

    Mau zitolelen muziyankhura bwno bwno man aaha

  • @ConfusedAtv-bs4gc
    @ConfusedAtv-bs4gc 4 місяці тому

    Tangotibweleselani ulendo wakulilongwe Kuti anayendako bwanji

  • @charityamos2183
    @charityamos2183 3 місяці тому

    Komadi akufanana ndi m'bale wanudi kapena zauneneri zomwezi

  • @user-nr8ww2oo4w
    @user-nr8ww2oo4w 4 місяці тому

    Aaaaah komatu anthu mudzikhala serious Pena inu bwanj sanabwele munthu wanu wen wen anafayo mutakhale ndi dziwanda dzaku satanic pa khomo mukumutenga munthu oti simukudziwa zoona zot dziko linayipa inu zimenezo simukudziwa ikanakhala nkhope ya munthu wanu yo bola Koma mukunamizanazo ndizosatheka

  • @livemonkaposka3714
    @livemonkaposka3714 4 місяці тому

    Number ya prophet please

  • @Khadjajemes
    @Khadjajemes 4 місяці тому

    Mwana Wako ungasowe komatu muthetsa nazo chakudya

  • @rashidadan2533
    @rashidadan2533 4 місяці тому

    Zamasiku akumapeto

  • @ConfusedAtv-bs4gc
    @ConfusedAtv-bs4gc 4 місяці тому

    Kodi video imeneyi mumajambulila foni ya tilili kapena ayi

  • @mwale1154
    @mwale1154 4 місяці тому

    Last day

  • @WatsonMayor-lf3ey
    @WatsonMayor-lf3ey Місяць тому

    Eeee ngat boza koma ndozona

  • @Jermah51kennias
    @Jermah51kennias 3 місяці тому

    Sanabwelebe

  • @KennethKachokola-er3us
    @KennethKachokola-er3us 3 місяці тому

    Zoopsatu eesh

  • @slatielchipeni-zy3wb
    @slatielchipeni-zy3wb 4 місяці тому

    Ziwanda iziiii

  • @paulchilola5462
    @paulchilola5462 4 місяці тому

    Aaaa

  • @SaidiMbawa-st6bj
    @SaidiMbawa-st6bj 4 місяці тому

    Zabodza izi munthuyo ndi wina

  • @mercyphiri6867
    @mercyphiri6867 4 місяці тому

    Timve zosatira plz

  • @BeatriceSaulo
    @BeatriceSaulo 2 місяці тому

    Ili ndy bodza la nyooo munthu kumwalira mximai kuzazuka ali mwamuna ndy kut chani

  • @HardyGutu
    @HardyGutu 22 дні тому

    Chipo

  • @LoveNatala
    @LoveNatala 4 місяці тому

    Zamatsiku osiliza owerenga khala maso

  • @user-hs8vn6wc4b
    @user-hs8vn6wc4b 3 місяці тому

    😢

  • @AmaduJuma
    @AmaduJuma 4 місяці тому +2

    Zakumidima izii,akhristu musocherela ,inu munthu oti ndi wanu mungalemphele kumuzindikila?

  • @lasmoboko5989
    @lasmoboko5989 4 місяці тому

    Zabodza zeni zeni kulibe zimenezo

  • @user-ws2xi7ch7z
    @user-ws2xi7ch7z 4 місяці тому

    Inu nkhope take mwaiwala ya munthu?

  • @ShiraSaidi-oz5mx
    @ShiraSaidi-oz5mx 4 місяці тому

    Tionetseni munthuyo

  • @user-tj2vx2xf7e
    @user-tj2vx2xf7e 4 місяці тому

    Koma muzionetsako akulankhulayo ndinso munthu omwalirayo

  • @user-iq3iv8tp8t
    @user-iq3iv8tp8t 4 місяці тому

    Don't stress your self please,munthu àmene mukunenayo ndi scammer amango panga pretend ngati wa asma nditambwali ameneyo he used Kuma panga zakeko ku Lilongwe around kanengo komanso area 43 titamuzindikira maplan ake adathawa

  • @SurprisedDriftwood-ef3lc
    @SurprisedDriftwood-ef3lc 4 місяці тому

    Bodza mukufuna ma comment 5:25

  • @user-hp8du2lx3z
    @user-hp8du2lx3z 4 місяці тому

    Zaziii

  • @user-dk8ey5pu5w
    @user-dk8ey5pu5w 4 місяці тому +1

    Munthu amene anabwera kunamizira ku wa esthma uja ndi mmene ndi amene anadzafufuza maina anu

  • @EvansKatambo-hi3sr
    @EvansKatambo-hi3sr 4 місяці тому

    M'bale wako oti wamwalira angabwere akuoneka ngati munthu wina mkumati ndameneyo zoona?guys come on come on,these so called prophets asokoneza anthu Kwambiri,

  • @user-ju3kj9vy9e
    @user-ju3kj9vy9e 4 місяці тому

    Za ziii

  • @DauglassNkhoma-dj9lp
    @DauglassNkhoma-dj9lp 2 місяці тому

    Mukuti pano alikutoti ifeso kuno tili

  • @osbornleman2500
    @osbornleman2500 4 місяці тому

    mmmmm profit wanama apa

  • @andrewmwachande7612
    @andrewmwachande7612 3 місяці тому

    😂😂😂

  • @DolineDalison-br1et
    @DolineDalison-br1et 2 місяці тому

    😂😂😂😂

  • @BenfordChuzu
    @BenfordChuzu Місяць тому

    Zoopsatu

  • @user-ky4nh4wg7y
    @user-ky4nh4wg7y 3 місяці тому

    Koma zikoli

  • @user-kn3ym1zf3m
    @user-kn3ym1zf3m 4 місяці тому

    Zabodza

  • @user-ln7wg9jn4x
    @user-ln7wg9jn4x 3 місяці тому

    Kkkkk

  • @augustMag
    @augustMag 4 місяці тому

    Funso langa ndi Ili kunena kuti koyamba kunabwera mnyamata amene amaonesa kuti Ali ndithenda yomwe amadwala m bale wanu asma eti? Ndipo abusa anakuyimbirani phone munthu mukamufuna uja anabwera simunamusama pamene wanu yemwe anamwalira ndi mkazi sichoncho tinene kuti athufe tikamwalira timakasitha matupi anthu? Muthu oti anali mzibambo kudziko lapansi pano ndiye bambo uja mwalira pozauka Kwa akufa azauka ndinthupi la mzimai? Koma anthu amene munakhala busy ndi azibusa musamale inutu ameneyo simunthu amene mumamuyembekezera ai ndichiwanda chimenecho chochokera Kwa busa pofuna kuti atchuke ku dziko kuno

  • @AnjelinaKasowanjete-fo8it
    @AnjelinaKasowanjete-fo8it 3 місяці тому

    🤣🤣🤣🤣🤣koma athu muri ndichibwana muthu waikidwa manda kumati wabweraso tangomvomeredzani muthu akamwarira

    • @mphatsomonjeza4371
      @mphatsomonjeza4371 3 місяці тому

      Zina ukamva 😅😅😅kambanga mwala munthu okhala wawo kulephera kumudziwa😂😂

  • @ThomsonNyirenda-df9io
    @ThomsonNyirenda-df9io 4 місяці тому

    Wasting time for nothing I can't believe that

  • @Allieshaibu8612
    @Allieshaibu8612 4 місяці тому

    Malawi ❤❤❤❤❤

  • @ZefaniyaWelios-e5y
    @ZefaniyaWelios-e5y 2 дні тому

    poop?

  • @fredlemani
    @fredlemani 12 днів тому

    Anali yemweyo kapena ayi? Nkhope imasiyana bwanji? Mprothet ameneyo anamutumiza Mulungu kapena ndani?
    You and your prothets are fools and you don't know God.

  • @YONA-v5o
    @YONA-v5o 4 дні тому

    Nde inuyo aku banja munthu woti mmakhalanaye simnamu fananitse ndamene anamwalilayo

  • @JosèFelixsailessFelixsailess
    @JosèFelixsailessFelixsailess 9 днів тому

    Zoipatu zimenesi

  • @EmmaRichard-hr7jj
    @EmmaRichard-hr7jj 3 місяці тому

    😭😭

  • @DauglassNkhoma-dj9lp
    @DauglassNkhoma-dj9lp 2 місяці тому

    Mukuti pano alikutoti ifeso kuno tili