Broh panopa ndpamene ndikumamva zoona.zake pitilizan kutiunikira koma after kulephera kumugwira wa Bakili Muluzi TV komas Ntanyiwa muone adzimanga aliyense apa angoyamba kumene
Chikalayayo ndi wawusilu walandila ndalama km kungoluza onsewo azakhala ma lova azawonas tizalemba ntchito ena nosenu a mcp mpakana ndi ma judge omweso ntchito yawo izawathla kmaso azamangidwa ndi awusilu mesa ndi Andale amene apolicewo
A malawi tidzuke tipepherere dziko lanthu makamaka 11:pm and 02:pm popephera timupephe Mulungu Atipulumutse.
Zoonadi zimenezi popanda kudalira Ambuye tili madzi
Ndipoe.zoona
Osamatengera malamulo mmanja dikirani chilungamo chioneke 👏
Chilima analakwitsa yekha kuwinitsa mcp lelo akuvutitsa otsala
Ndinayake
Vuto apolice aku Malawi alowa mcp agalu okhaokha a mcp komaso chakwera mboloyao
Chiwembu cha abambo ake asikono Ichi. Maganyatu ndi owukira nd mfitiso
Apapa Malawi yense timayenera kupanga mademo a emergency
Ndipo izi ndizoona
Amafuna kupha munthu koma opha SKC alikuti?
Ndiusi ameneyo manganya Ngati anapeleka chilima akalephele kumupeleka kaliyati
Kodi mwayamba za one party system
Thanks for the update
Any time!🎉❤
MCP chifukwa chiyani ikumawatengela a Malawi kuntoso a kweni alakwanji koma
Mmmmmh mayi kaliyati sanamvekepo ndi mbiri imeneyo zalowa ndale iziiii
Kodi zafika poti apolice kulesa anthu kuti asatenge ma placards?mpaka ma placards kusungidwa kuseli kwampando?ok
Mwaona inu ana amma 2000 zomwe munapanga? 1 million jobs ija ndiimenei
Vuto ndife 😂😂😂😂
Eeee koma mcp a zoona ng'ona ndi ngona mcp sizasintha
Vuto la opposition yogona, kumangana sikungathe
Bola muzimanga umboni ulipo,,osati misonkho yathu ipitenso apa
Amalawi mizimu zukani,monga nzika ya chimalawi,yambaponi kutibula,mpolice aliyese ndi odelela kwambili.
Aah police yaku Malawi penapake💔
Chosecho imavala jombo yophulika
Munthu wake ndani?
Aliyense wandale ndioipa bas ndipo ife ndiomwe timapanga zopusa kumataya nthawi yathu
Koma zoona zimenezi achakwera mbiri yanu isaonongeke chifukwa cha anthu anu oipa mtima chifukwa chipani cha mcp anthu akchita kunenakuti. Ndi chakhaza kwambiri pamene chafika aliyese akuopa kufikira pafupi
Police yathu ikugwlisidwa ntchito ndiandale basi zitsiru zapolice
Broh panopa ndpamene ndikumamva zoona.zake pitilizan kutiunikira koma after kulephera kumugwira wa Bakili Muluzi TV komas Ntanyiwa muone adzimanga aliyense apa angoyamba kumene
Zosezo. Ndizaboza. Akufunakupasa. Poizoni. Mapulaniawo. Alichocho. Pakufunika. Kuchitapokathu. Akweni tialuzaso. Ngati chilima bomaili. Liphaathu
Apapa akuonjezera mkwiyo wa anthu
Kmaso sizikufunika kupephela kma kupita kukagona kupolice
Amafuna kuphaa muthu kutiko kapena zalowa kundale. Muthu wake ndani , palowa ndale apapa sizonamizana. Ayiwala kuti ndamene analowetsa boma
Ine ndine wakumudzi ndimafuna boma limeneli litandimanga a police angazaone polekela sure
Zopusa basi kwacha mumango ngwesa basi pangani zoyendesa ziko mmmm
Boma ndilomweli tingositha president ndi apolice
Chikalayayo ndi wawusilu walandila ndalama km kungoluza onsewo azakhala ma lova azawonas tizalemba ntchito ena nosenu a mcp mpakana ndi ma judge omweso ntchito yawo izawathla kmaso azamangidwa ndi awusilu mesa ndi Andale amene apolicewo
Vuto apolice aku Malawi amakhala Ngati Siaku Malawi
Akufuna tibweleleso ku one party system. Akukanika bwanj kunena mulandu wenewen omwe amangila mmmmm
Muli busy kumanga anthu malo moti mukhale busy kusaka njira yomwe mungapezere mafuta dziko. Mcp ndiyochitisa manyazi poganiza koma chalakwe amaganiza ngati mwanadi ndithu, zina umangoona waziyambadi.
Ndye mwati chalakwe kkkkk
Akupanga zopusa kwambiri anthuwa
Kmatu aboma akuyesa zida
Zachamba chikangawa chakwera garu 😮
Koma mulungu akuchitileni chifundo pa nkhaza mkuchitila anthu zikutikhuza kwambiri zimene zikuchitika mziko mwathu muno ngat mtsogoleri kulibe zoona chitanipo kanthu achakwera
Mbava zosowa pogwila
Maro Moti azirimbana ndi dzikori kuti Kodi dzikori rikuyenda bwanji koma akurimbana nd chirima amene amumangayo ndi skc Muzimu wakhe uwuse mumutendere
Malo mosaka Mafuta mwayamba kusaka Anthu😄
Izitu zomwe zikuchitikazi ndi khaza kwa amayi chifukwa chani koma ziko mukuliwona ngati ndilanu
A polisi musayiwale kuti mnzanu waphedwa ndi MCP yomweyo
Apha chilima ndi witika muwamanga liti?
Sizachilendo m c p kupanga nkhanza
Manganya Manganya Manganya manganya
Munthu wake uti yemwe akuti amafuna kumumpha mmmm
Police yakumalawi is very useless amumanga bwanji muthu mulibe umboni wina uliwonnse, this is proper gander srious.
Iiiii koma ndale
Apapa akanamangidwa wa mcp akanawalola kuti amuone m,balewao koma pot ndiosusa alibe ufulu
mbuye menyeleni nkhondo,malawi okoma uja waonongeka,ivani kulira kwathu
Kungowonjezela mkwiyo kwa aMalawi. Ma plan anu sayenda MCP
A police opusa awa
Mukuwopa chan titulusilen munthuwanthu
Yakuphandiyakupha mcp anapha chilima kasambala Mia
Zarowa ndare izi
Tumizani mafuta anthu akufa sanafike kuchipatala muwasaka anthu kuti atani
Amalawi ufulu wathu tinaugulitsa povota nthawi ijayi mmmmm
Tichilape😂😂😂😂😢
Amafuna kupha Muthu koma chakwela anapha mumugwila lit
Manganya usi ndiwe mfiti ndi chingawayo
Magalimoto asilikali ose aja amapita uku
Apangisa zosezi ndi manganya ndi chikangawa
Zoopsa
Wathilila mchenga mpunga
Ma plan amanganya awa
Boma ndilomwelii😁
nkulu wina wake akuti quarter chani kaya sangapiteko muona
Umboni mulinawo
UTSI ALIKUTI?????
Zonsezi ndi manganya tikamati ngoyipa bamboyu mwaonatu
Chipani cha nkhanza osamakasaka mafuta bwanji
Apolice akumalaw ndiofoira kwambiri
Iiiiii koma boma ili ayi ndithu
Kod moyo umeneu nduyekut ufulu wathetsad chikangawayu
Manyazi akuwagwira apolice akuwaletselanji ma poster a, ikasaka mafuta kumene
Eti amwene mafuta Akusowa akusaka anthu
Yesaya 54v17
Mumtima ndi muthumba salowana
amafuna kupha ndani?
Kayasotu sakunena
Malo mokasisa mafuta aja amati alingambwi ngambwi aja koma satana alipantchti
Mcp ndye chipani choyipa ichi
Tiyeni mahdemo
Mcp chidure avomere kulephera
Malo mokasa mafuta, mukumanga anthu
Munthu amafuna kupha yo Ali kutiko poyamba anena kuti chakwera tsopano tiva zoti tsopano
Sakumutchuladitu
A police omvetsa chisoni kwambili
@@WhyteSmart Heavy
Komatu bambo a sikono longosokani
Zovesachison mcp mbuzzi
Aaaa koma police yaku malawi
Zaukape man
Koma mcp amuziwe yesu
Iiiiiiiiiiii koma machimo
amafuna kupha munthu kuti
@@alexsumani6823 kayaso man😂
Kodi peter sanamange jese ndi sungama mwazionalero agwepe inu
Takasambeni uko uli mbuu apa ngt unagona paphulusa mwana wa njoka iwe