Ngati a Usi ndi a UTM, achitapo Chiani pa kumangidwa kwa Kaliati? Ngati sachitapo kanthu ndiye kuti ndi Iwowo amapangitsa kuti pa Convention yomwe akhale nayo azayende poyera. Kariati ndi m'modzi amene amawanjenjemeletsa. Koma ngati ndi amodzi a UTM a joiner azawo ku Police. Koma ngati ndi nyenga sangapite. Chifukwa Chakuti pamenepo amasangalala. Koma akunama.
A Malawi kumbukilani kt Vice president wa dziko ndi wa UTM ali ndikuthekela komanga munthu amene akulimbana naye ,osamangoti boma ayi. Unkutheka kt upo ukunenedwawo akulimbana ndi manganya tadekhani kaye ndizandale izi mukuvutika ndi inu anthu ovutika
We love you Mamie always on ur side
Allah akangolowela nyengo zonse zisinthilatu mama
Anyamata a UTM ponyani miyala kuli bwino civil war yiyambike
God bless you akwen
Afuna kumupha achakwera ndi ndale ayika poison mu selo anthu oyipa inu koma chomwe mungadziwe palibe wamuyaya mulungu akuchitireni chifundo simukudziwa chomwe mukupanga
Bravo Malawian 🇲🇼 ✊️✊️✊️
More fire people bravoo
Viva UTM, I love you Mamie, osaopa ndipo osafyooka
Viva UTM ❤🎉🎉🎉🎉🎉
Tiyambepo mademo lelo tigone konkuno sitigaive imeneyo tiyeni konko🏃🏃🏃🏃🏃
UTM komko ndikumene kwatuluka zimenezo chifukwa kuli chimkulirano cholimbirana mpando wa president.
Tisamangoti Chakwera onani kae mmene zikuendera za ndale kuyambira ku Chipani chaocho.
Chakwera tamunamizira zinthu zambiri koma akutitsutsa ndi Mulungu. Mapeto ake tikanthidwa Ndi Mulungu ngati tingamaweruze kuti ndi Chakwera tisadafufuze bwinobwino.
ZIKOMO KUMPANDO
Viva akweni ngamo abusawa tribalism kwambiri kwake ❤❤❤❤❤
Ngati a Usi ndi a UTM, achitapo Chiani pa kumangidwa kwa Kaliati?
Ngati sachitapo kanthu ndiye kuti ndi Iwowo amapangitsa kuti pa Convention yomwe akhale nayo azayende poyera.
Kariati ndi m'modzi amene amawanjenjemeletsa.
Koma ngati ndi amodzi a UTM a joiner azawo ku Police.
Koma ngati ndi nyenga sangapite. Chifukwa Chakuti pamenepo amasangalala. Koma akunama.
Tayatsanipo aaaaaaa akutiwoonjedza Panja akawoona Kt munth akumuremphera amamubaya Jackson amutulutseko wanthuyo
Viva UTM osaopa
Tiuzeni tilipo ife akaziotche tiphwanya police imeneyo
UTM moto kuti buuuuuu.go,koko.ahlomwe,onse ku mwela tiyeni koko police ya pa 18 isatizolowele.
Mumatiimilirq mom❤❤
The biggining of Mai Kaliati successful political journey
Iyambike bas
Osa wopa osa fooka malawi 2025 tichose satana chakwela 💪💪💪
Umakwana mammy
Bravo mama💪💪💪
Kkkkk zokambirana ayi awoneseni kt amarawi munatopa aporice opusa jombo zawo zinatha kare kare timanyumba tawo tonvesa chisoni
Iwe osakayambitsa bwanji ukufuna akayambitse anzako?bweraniko ku joniko muzidzayambitsa inuyo
@@ElizabethZiyadi kwacha ikugwa deiry tibwera boma rikasintha anthu akasiya kudya chiteze
Sakuyankhulilanji chifukwa chomwe amangila bwanji kumangot ndi mulandu wa srs zopusa bas
Ndiye nanga ngati nkhani zake zili zomwezi amanama
Koma apolice Aku Malawi ndi chani mukuwoneka ngati mwayamba kupenga misala
Viva UTM
Zangovuta I need ndikanakhala pafupi kwangotalika ku l city
MANGANYA ndiyemwe akudziwapo kathuu tamufusan ndiyemwee akukwedzera MOTO kt akwen amagwidwee
I can see very chaotic situations Happen next, probably civil war
NDI jocka uyo ndintengo omweuli ndizipaso zakupya ayamba kuugenda.
Awuzeni za chamba ayi
Tiyatsa police imeneyiiiii
Vuto loweta ng,ona ngat mphaka wannyumba ndiizi , awa munawakweza muntengo nokha.
Guys let's just demonstrate
Ndathokoza a UTM pa zimene mukuchita pamenepo
Gendani miyala polisiyo
Nde ukakhala mmalawi uzipanga zirizonse wafuna? No! We need to be civilized at all cost
PK awina, mtsogoleri akamangidwa amawina
Anapha chilima lelo akufuna kupha amayiwa dzonakoma amalawi tingo yang .Ana atitolatu uyu
Tili nanu mayi tikukuikizani mapephero mulungu yekha ndi amene akudziwa
Akuyankhula zopanda nzeru
Dziko ndila amalawi silamunthu Osama ophezana apolice mupandidwa zikutiwawa ifeyo sitikuwopani nanu
Auzeni Kuti simukuopa ,chilima anafa kale musope
Kodi azipani Zina zosutsa ali Kuti?
Tengani ma pic a apolice wo tiwasaka mmakomo ndipo tiwanyenyanyenya
Osaopa
Amenyedwe apolice
Km mai wanga sadalakwe atulutseni
Vuto la zipani zosusa zikakhala zogona everything can happen
Zifukwa zopangira mademo zikuchulukirabe osaopa osafooka osatopa
Viva Malawi viVaaaa
Manganya ukunama wadya magazi a mcp sizitheka
Khwiya iwe,Koma kumeneko,tiye nawoni osalola
❤❤❤❤❤❤❤❤
Otchani chipolice chawocho abele amenyen apolicewo
A Malawi kumbukilani kt Vice president wa dziko ndi wa UTM ali ndikuthekela komanga munthu amene akulimbana naye ,osamangoti boma ayi. Unkutheka kt upo ukunenedwawo akulimbana ndi manganya tadekhani kaye ndizandale izi mukuvutika ndi inu anthu ovutika
Exactly
Usi ngwa mcp mungovela zakamanjekete munthu asayakhule mcp mwatitopetsa situkufunani kamuzu amavuta pano alikuti mpando womwe muliwo amcp ngosiyilana
Osawaselelera