Ma dollars mufupa pa ukwati...koma yaa Denis Mahata uja knows what he is doing n good for this country let's support him. Mind you kulibe zozipenta it's just working for the prosperity of our mother Malawi
Ok kunkuyuu takunva tapangaso apa masam a report la mafitalo which means totally amout fo petrol ls =Ltre's 29,800,000 twenty nine million eight handered Southend. Kudzaso Desilo Totally =4.500,000 Lter's. Four million five hundred thousand litres
Kunkuyu ndi waboza uyu zaka 10 zomwe akuzichulazi MCP inalipo nthawi Ya APM or ndalama ya Rand inali pose potse malawi muno koma pano or utayisaka mene ikusowelamo awatu akusowa chokamba ango siya asamayanguleko fundo dzake ngati mwana weni weni
Because of lack of leadership from the top ndi nduna zawo ndamene akuononga dziko chomwe akudziwa iwo ndikuba basi to proof this information, nkhani za serious samakhala nazo busy koma busy ndizopusa nde lero ndiizi follow denis mahata you will see the directon osti izi za Akunkuyuzi
That’s why the president and his administration are the to solve these problems not always giving unexplainetion no no no you hade failed us a lot if you don’t know what to do just leave our Malawi alone 😢😢😢 please
APM mmene amachoka dziko la Malawi linalindi three months import cover. Kuthauza kuti ku Malawi kuno tinali ndi ndalama zakunja zoti tikanatha kugula zinthu zakunja ngati mafuta kwa miyezi itatu mosavutikila. Mfunso ndi kumati Olemekezeka A Nduna A Kumkuyu ka three month import cover anasiya big man ndi team yake ku mpingo wa mtambo mtambo kaja kanayenda bwanji?
Akamakuwuzani kuti chepetsani zoyenda yenda NDI chigulu KU maiko akunja simumamva apatu mwamaliza ma dollars. Komanso mwabitsa ma dollars ena KU mayiko akunja
kod mesa 2 weeks yapitayi mumayakhula monyera kuti mumakalandila mafuta through pa njanji ndi nzako wakupha uja , nde pano mafutawo Ali kuti ? agalu inu mu 2025, muchoka m'boma
Mr Mahata, Mr Fredo, Mr Kamangila, Mr Kalindo, ngat nkotheka kt anthuwa apange chinthu chimz ziko likhoza kusintha, mothandizana ndi ntanyiwa komaso wabakili tv Malawi 🇲🇼 akhoza kukhala strong 💪
Forex inathera kukalimbikisa mkhondo ya Ayuda ku UNGA
Kodi ndi mayiko angati omwe amagula mafuta through ndalama yakwao man sisanamizidwe ai nkhani ndi mbavazi basi😊
kuyangula kwa bho
Amene aja ndi akamuna, samayankhula wamba
Mayendedwe naonso anachuluka lero ndenge mawa ndege forex ingapezeke
Mahatha mwana wonganiza boooo
Danes is our future president period.
Inu ma dollars amaliza ndi maulendo ....
@@enockkanyerere784 ndipo live amaziwa kut ma dollars ndiochepa koma kuyendayenda bas
He is wise, men
What is this all about mr
Ma dollars mufupa pa ukwati...koma yaa
Denis Mahata uja knows what he is doing n good for this country let's support him.
Mind you kulibe zozipenta it's just working for the prosperity of our mother Malawi
Boma yokuba mulibe experience yoyendetsa dziko chimene mukudziwa ndikuba bas agalu inu
Choka iwe osati zaka 10 wachamba iwe nena kuti Kwa zaka 4 zokhadzi ndiye tawona malodza amenewa wamva iwe kulu nkhuyu
Uyu ndikatundu mzito
Amene uja si Muthu wamba
mahata on fire 🔥 koma kuseliku ma judge akulandila ma Dollar 😅 mapwala anuo mr
Dennis mahata ine ndinadziwa kuti ndidolo nditangowonela interview ija ndipo kudzangopezeka pa ballot paper voti yanga Watergate basi
izi ndizowona br salut
Big up brother man!!
@@kubengovender6996 🔥🎉🙏
Thanks brother
Mukufotokoza nkhwangwa ili mmutu? For what? Sympathy? Hell no
😂😂😂
Kunkuyu ndi odwala magazi achilima akumudzunguza
This guy is really genius
Muvomeleze kuti mwalephela agalu inu
Ok kunkuyuu takunva tapangaso apa masam a report la mafitalo which means totally amout fo petrol ls =Ltre's 29,800,000 twenty nine million eight handered Southend.
Kudzaso Desilo Totally =4.500,000 Lter's. Four million five hundred thousand litres
Inetu mahata amandiwaza kwambili
My vote mahata
Kunkuyu ndi waboza uyu zaka 10 zomwe akuzichulazi MCP inalipo nthawi Ya APM or ndalama ya Rand inali pose potse malawi muno koma pano or utayisaka mene ikusowelamo awatu akusowa chokamba ango siya asamayanguleko fundo dzake ngati mwana weni weni
My Malawi mmmmmmmm atii kuli president mmmmm
Brother Denis zoonadi iweyo ndi mtsongolere wamasomphenya
Koma chakwera atati akutuluka kuja ma dolars apeza
Maulamulilo apita mbuyomu madora samasowa mpamene yafika pano ganizilani maulendo aapresident opanda nao zelu apangisa kuononga madola oodela mafuta sogoleli opanda masophenya
Chikangawa wooyeeeeeeee😊😊😊😊😊😊😊😊😊😊
Komatu dziko muno muli anthu anzeru koma sali pamalo oyenera, this kind of kunkuyu sakuyenera kupezeka pamene alipa.
Chilungamo zedi brother
Because of lack of leadership from the top ndi nduna zawo ndamene akuononga dziko chomwe akudziwa iwo ndikuba basi to proof this information, nkhani za serious samakhala nazo busy koma busy ndizopusa nde lero ndiizi follow denis mahata you will see the directon osti izi za Akunkuyuzi
Mbolo yako fisi iwe kumkuyu ukulamkhuya chifukwa choti wakhuta ndalama eti amzako akudya chitedze
Mahata number one
Auzeni zandègetu kuti amalawiwo adzipanga. Chiganizo cha bwino monga munenera amozesimo
That’s why the president and his administration are the to solve these problems not always giving unexplainetion no no no you hade failed us a lot if you don’t know what to do just leave our Malawi alone 😢😢😢 please
Mahata❤❤❤
Zangongole basi. Ngongole siyingathukule dziko iwe akunkuyu. Dairy bodza amalawi samadya mabodza
ndigaileni ku wap chifukwa ndapombonezeka enable amati ndindale koma apapa inenso ndigwireko ntchito pang`ono please
Nokha mafuta abwela kusowa.mafuta kwatha
Apatu born kalindo.osazamuphweketsa
BMtv is the best TV ever
The future president Denis mahata
D Mahata mbambande
Koma ndiye covid 19 simuzasiya kuunamizila oti kusogoloku muyamba kunamizila ziwawa za ku Mozambique kuti muzuzeso anthu pa Zina.
Kunja kuno kuli ana anzeru koma mbava apsyatangu manjanjawide mfiti ndiso kutchuka mwauchitsiru mbuli!!!!! Ndizomwe zikugwetsa dziko lino,posafuna kupereka mpata kwa oganiza mwaukadaulo ngati achina bon kalindo,,mahata,,kamangira ,, bakili TV and others ndiomwe Ali ndi kuthekera .
MCP kwawo kunatha firs day atangolowa kumene
Kunkuyu matsinya pamaso akuopseza ndan
Koma zimenezi ndizouza ntundu wa amalawi mmmmm kusonyeza kuti mwalephera
Mapwala ako akukuyu osangoti mwalephela
Mnyamata wa nzeru kwambil
Chikangawa angoyenda timawulendo topusaa dollar ipezeka bwanji
Ulendo umene mukuyenda mumalipira ndi chiyani zopusa basi
Ukuona kutuweka zinduzakukanika bwanji ozatula paziudido nanga kungokakamila zinduzizikuye ndakoma kufunapando iweyo nigalu
Atule pansi udindo mr chikangawa
Kodi ndizoona kuti sitima ija idari juice wa shuga votiyanga yasintha ilimbana ndi mashin aja akuti ndi obera zisankho tikungofunako tsikulo bwana
Mukumakhala ndima dolas ochepa koma daily kumayenda kupita kunja pali nzeru
Kkkķkk Mavuto❤
@@0wenNkhambule 🤣🤣
Kkkkkkk
Moses kunkuyu ndiwe chitsilu kwabasii aseee AAAA umatiwona ngatii ndife ana mudziko Muno kapena dzikoli umalitenga ngatii ndila amako iwe pa nyelo pa mako wavaa mbuzi yamunthuu iwe bola mayako akanapita pa chabe kusiyana ndikukubeleka iweyo
Uyu ndinamandwa alibe muzake
Denis tiomboleni please
kaganizidwe kamahata andale sanaganizeko ngakhale dontho
Komano akuluwa nwanji sakunwelano poyela kuti mwina Amalawi amudziwe mwina mkuzamusankha
Anabwera kale poyera km akuluakulu akumupondereza komaso achinyamata we need to support him
Munja anayendela chikwangawa munja ndalama amazitenga kuti amukuuzani kuti chepetsani maulendo koma kusava
Popita ku unga kuamerica anthuwa amalipira ma kwachaaa kapena ma dollars?
@@fanuelbinde 🤣🤣
Mwachidule, tinene kuti zomangongola dzindalama zambirimbiri zija mukupitilizabe???
Ma dollars analipo koma Chikangawa anatenga onse mkumayendayenda nawo mkumapita kokwera njinga plus kutenga anthu 150 kumapita nawo ku UNGA
This government is gone
Denis mahata my vote ❤❤😂😂
kumkuyu ku Malawi kulibe president iwee , machende Ako
Kumvatu timanva,koma timanva monvenura
@@JohnWame-u3l 😂😂🤣🔥🙏
ukatero ukuganiza zokabwerek a ndalama ku ma bank akunja then mugulure mafuta , kumkuyu ma battery Ako komanso mutu ngati choswera malambe galu.
Kod malaw imaendetsedwa ndi ngongole kapena economic activity yake
Ndintunda zedi umeneyu
APM mmene amachoka dziko la Malawi linalindi three months import cover. Kuthauza kuti ku Malawi kuno tinali ndi ndalama zakunja zoti tikanatha kugula zinthu zakunja ngati mafuta kwa miyezi itatu mosavutikila. Mfunso ndi kumati Olemekezeka A Nduna A Kumkuyu ka three month import cover anasiya big man ndi team yake ku mpingo wa mtambo mtambo kaja kanayenda bwanji?
🔥 bakili muluzi tv 📺 😂
Chakwela akanabo mqondo
😮😮😮😮😮
Funso la nzeru America ma dollar amatenga kuti
Kunkuyu plus yr boss dzimachende dzanu bwanji simukuva chisoni ndi anthu tikuopeni poti ndinu satanic mukaudzane nose nyini dzamanu
Komatu bwezi akunena mayi uja wa nkhope ngati ine uja
Chakwela ndamene adaongonga madollas ndikuyenda yenda ndiye Kaya ayenda liti
Koma fuso chakwela akamayenda amalipila makwacha?
Komano mutachepetsa kuyenda yendako mwina zinthu zambiri zilongosokako
Maulendo opanda pake achuluka
Kod mesa munati mafuta azibwera pa train not pa truck?
Et
Mafuna avuta kwambiri 4yrs yanu iyi, komaso maulendo akuchuluka kwambiri akuwononga ma dollars ankhani ankhani mdziko muno, tafika moti mpka kuchita kuwenga truck amene kubwela alimnjila 😂😂😂 ai boma ili salendi izi ndi mbuzi za anthu.
Uyu simunthu wamba
Nkhani ya mafuta yomweyi mpaka zidodo...ngati mwagwesa ndege ina....mmmhhhh
Afanawk ndi katundu osati akukuyu angoba
Kukuyu ndiwe galu wamva eti
Avutikadi chifukwa chopanda nzeru za chipani cha mcp munangobwera kudzaba basi agalu inu anyapapi
iwe kumkuyu pamtumbo pako , forex munakathera ku UNGA , pano ukufuna kumanamiza anthu , zopusa basi , tchende lako kumkuyu
Kukuyu ndimakukonda koma zomwe wayamba kukamba zopanda dzelu mwachidule Mafuta asowa chifukwa sanapeleke ngongole fuso ndalama zinaononga chakwela Kunja zinja bwanji osabweza ngongole
Kunyamura anthu 300 kupita nawo kunja ma allowance in usd 😂😂😂 ine sindidzabweranso kumeneko😂
Akamakuwuzani kuti chepetsani zoyenda yenda NDI chigulu KU maiko akunja simumamva apatu mwamaliza ma dollars.
Komanso mwabitsa ma dollars ena KU mayiko akunja
Chulungamo chibwele poyela
Tikamavutika padziko pano zimangokhala nkhanza zanthu ena
kod mesa 2 weeks yapitayi mumayakhula monyera kuti mumakalandila mafuta through pa njanji ndi nzako wakupha uja , nde pano mafutawo Ali kuti ? agalu inu mu 2025, muchoka m'boma