Yes, inenso ndimmene ndavela ulalikiwu ukupita kwa aliyese ndipo ukumpuzitsa kuti tizikhala okhulupilila koma ma comment ndikuwaona ine apa eeee pakuti kumalawi kuno mmodzi atagoyamba ndi negative comment aliyense alemba zomwezo
May God bless His Word through you moderator and may He also plant a heart of philanthropy and patriotism in all political,traditional religious, and legal authorities in Malawi to be once again a Godfearing nation. Amen
A malawi sindimakumvetsani koma zowona after all what MCp has done to you in 3 weeks ago mwayiwala kale, kukuyitanani ku msinkhano inu nkupita,, mumati mukamvako chani chatsopano,,a oposition you guys are sleeping to much 😮h munayenela kukana osapezeka nawo pa chikondwelerochi,a MCP akukondelera their successful mission of killing chilima and the other 9, nchifukwa chake lero ali wokondwa,a malawi ndinu anthu osawona,how can you be invited for prayes to pray for the lives lost in chikangawa by the same man who orchestrated their death😢😢😢😢😢😢😢😢😢😢😢😢 Malawians are you nomal ⁉️⁉️⁉️⁉️⁉️
Amene akunyoza Chakwera tsoka Kwa iye.uli ndi tsoka iwe onyoza munthu osalakwa, ngati ndi ulesi wakowo ongofuna kulandira go to page House khalamba yanu ikakupasani za ulele. Agalu inu
Amen munthu wa Mulungu achakwera ndi nduna zanu a chimwemdo kunkuyu zikhale ng'omayo mukaka zisakhale ndwiii ziziva mawu a Mulungu ndizimene zikupangisa Malawi kukhala wawumphawi ndalama akuziononga basi.
😊😊😊😊😊😊😊😊😊😊😮😅😊
Powerful words. We don't need to curse our nation due to painful situations. God will heal our nation
This man is one of men sent by God to deliver ❤
Munthu wamulungu wayankhula, wakumva amve zomwe Mulungu akuyankhula. ❤❤❤
Amen, very powerful message. God bless you, God bless Malawi.
Amen Abusa, Yehova ndithandizeni kuti ndizipanga zomwe chi Khristu chimanena, Amen.
Munthu wankulu....powerful massage Glory to Jesus🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌
Powerful message God bless you pastor ❤
ABUSA alalikira osati zomwe ayankhula ndipo ndi phunziro kwa tonse osati a President okha
Tiyeni tisiye zonse mmanja mwa Mulungu popeza Iyeyo adziwa zonse bwino koposa mmene tidziwira❤❤❤
Mwayamba bwino zedi mbale. Anthu tonse tikanamaganiza choncho tikabakhala nidziko lantendere
Yes, inenso ndimmene ndavela ulalikiwu ukupita kwa aliyese ndipo ukumpuzitsa kuti tizikhala okhulupilila koma ma comment ndikuwaona ine apa eeee pakuti kumalawi kuno mmodzi atagoyamba ndi negative comment aliyense alemba zomwezo
Strong massage this is a lesson to the politicians who pushed a Malaysian people who's dying with hunger poverty
For the first time seeing a preacher without recognizing POLITICIANS 😂😂
Greatest message pastor God bless you
Abale ndi alongo timaseva zithu zopanda pake mmafoni athu. Zichotsenimo zoipazo komatu sevani uthengawu waphamvu muziwubwereza×10 kuposa zinazo. Tidzapeza mpumulo woyankhidwa kwa Yehova tonsefe tikawutsatira ndi kuwupempherera uthengawu patokha patokha
Mawu uphudzitsa ndipo achilimbikitso tingavutike motani titsataye chinkhulupiro yehovah ndiye zotse zanthu👏👏👏👏
Zoona m bale mulungu ndiye yanko tisanyozane pamene takumana nimavuto
Chakwela yekha ndamene akutikhomelela Malawi siziko losauka chakwela must go
1q
@@ElizaMagombo very low
This eas beautiful and powerful sermon, great 👍💯
Powerful massage amen
Powerful message ❤God bless Malawi
Indeed powerful preaching God bless you
Great message Pastor.......God bless you
Amene akukondwera ndi utsogoleri wa Mr Chikangawa ndiye kuti Mutu wake suyenda bwino
Ayi zkm man of god thank for good msg ❤❤❤
My favorite scripture... book of Job
Rev Yasinami Gamma,Mwatiphuzitsa Ambuye akudalitseni kwambiri,
Powerful man of God, uthenga wamveka
Amen i love this man of God 🇿🇲🇿🇲
Kuyakhula mopanda matha respect abusa a Gama
Amene ali ndi khutu la uzimu uthengawu wawuva koma amene ali ndikhutu koma osamava, ndiwo ma comment ambiri tikuwawonawa. Amen pastor
Powerful message man of GOd
Koma azanga mbusa uyu mulungu amupatse moyo wautali
Y.G is the greatest Reverend of all time
Big up brother man!!
🤣😂 God bless you Gama
I knew my rev: never go wrong.🇿🇲
Wat a wonderful preaching
May God bless His Word through you moderator and may He also plant a heart of philanthropy and patriotism in all political,traditional religious, and legal authorities in Malawi to be once again a Godfearing nation. Amen
malawi wathu ndipamene takhalapo. Amen abusa
Wonderful preaching
Powerful message ❤❤❤❤❤😊
Powerful Preaching
Powerful message ❤❤❤amen and amen
Great great great apstor of the year
Ulaliki mbambande yobu mwayenkha munali kulimba mtima ndkukhala nacho chikhulupiriro chozama amen
Great preaching
Hallelujah!🎉🎉🎉🎉🎉
Amen and Amen !!!!! Mau omveka bwino kwabasi
Chonde amalawi tisatembelele dziko lathu chonde mau akulu ochokela mkamwa mwa abusa yasini gama amen
Amen amen kuying'alula abusa
Amen man of God
Happy 60th independence Malawi and Long live.❤
Akulu mwati happy chani kkkkk kumalawi kulibe za happy mganize bwino
Eeee zako zili.pabwino Pali malawipa nkumati happy kakaka
60th independence and ufulu.
Powerful massage
Amen paste!!!!
Powerful message
Yassin gama ndiwaku 49 mama ccap church nt ku 25
Ndipo zobvuta Zambiri zikubwela sakunama
Amen so powerful
My reverend
True facts in life, ndaukonda uthengawu
Man of God
Koma anthu amalalika
Powerful
Awa nde anadalitsika ndinthu
Amen amen
Osayelekeza kuwapha awa ,taneneratu
Nkazi wopusa Ngati Mayi gotani hara
Kutumikila mulungu mwachindinje, pamalawi panga pano palibwanj?🎉 Hellooooooo
Eeeeeee ulaliki ogwila mtima
Amen
Ameen Abusa
Amalawi bvuto ulesi ndichikwa chake mtsoleli aliyese akakhala paudindo timati ndioipa akachoka wabwino kodi zooona atsogoleli onse. alamulilandziko linowa angakhale oipa ?
U might not mean what you want to say
Uthenga wabwino koma amaopako pangono a kambiri munthawi ngati iyi anaungalura uthenga .😂😂 a pule osawafunanso kkk.
Ayasin ndi mbambandetu ndi weniweni
Amen ❤❤
Mwangozi
Shehe uja amatinamiza koma uyu,
Chakwera akuzinyoza yekha aise😂😂 and inuyo mukugwira ntchito yanji if I may ask😂😂😂
Amen!
Amen 🙏
Amen 🙏 🙏 🙏
Ndiyitana padzina lanu yenkhova
A malawi sindimakumvetsani koma zowona after all what MCp has done to you in 3 weeks ago mwayiwala kale, kukuyitanani ku msinkhano inu nkupita,, mumati mukamvako chani chatsopano,,a oposition you guys are sleeping to much 😮h munayenela kukana osapezeka nawo pa chikondwelerochi,a MCP akukondelera their successful mission of killing chilima and the other 9, nchifukwa chake lero ali wokondwa,a malawi ndinu anthu osawona,how can you be invited for prayes to pray for the lives lost in chikangawa by the same man who orchestrated their death😢😢😢😢😢😢😢😢😢😢😢😢 Malawians are you nomal ⁉️⁉️⁉️⁉️⁉️
Ndipo inu😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭
Zosayenda
M'busa ameneyu ndi wandale, ananyozapo zipani zina ndikuyamikila mcp,
Wuthenga wabwino ambuye akudakitseni.
Ayasini inu ndi munthu wa mulungu ndipo ndinu mlangizi
Khaniyotu ndiyona
Ayasini inu zitigairani mau amulungu anthu munawasitha
Malawi is not poor country
Muzeni zoona aleke kupha anthu
Koma Uyudi anadzonzedwa zedi
Koma abusa Bible munalimvesadi ambuye akudaliseni
Kugunda kugwesa
Chinyora
Abusa aku 25?
Nde mwati ABUSA aku 25 eti???😂😂😂😂😂😂😂
Abusa a ku 49 ku nvama ccap church fumbi gheeto
kumalawi Kuno kulibe akazi opusa
Amene akunyoza Chakwera tsoka Kwa iye.uli ndi tsoka iwe onyoza munthu osalakwa, ngati ndi ulesi wakowo ongofuna kulandira go to page House khalamba yanu ikakupasani za ulele. Agalu inu
Iwe ndikape kwambiri
No the guy knows
Abusa ndye alalika kut amva tikunena kut zikoli timuchokeramo zikhale
Koma azungu akumva?
Aimbileni phone muwafuse
Mulibvumbulotso mu ulaliki uwu,tiyeni timvetsere bwino ndi khutu la uzimu.Ambuye apitilize kukugwiritsani ntchito abusa.