ZOMWE AYANKHULA PA MASO PA A PRESIDENT PA MWAMBO WA ZAKA 60 INDEPENDENT 🙌🙌

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 4 жов 2024

КОМЕНТАРІ • 145

  • @thulanimpphiri6873
    @thulanimpphiri6873 3 місяці тому +23

    Amen munthu wa Mulungu achakwera ndi nduna zanu a chimwemdo kunkuyu zikhale ng'omayo mukaka zisakhale ndwiii ziziva mawu a Mulungu ndizimene zikupangisa Malawi kukhala wawumphawi ndalama akuziononga basi.

    • @EmmanuelNauli
      @EmmanuelNauli 2 місяці тому

      😊😊😊😊😊😊😊😊😊😊😮😅😊

  • @MathewsChilota
    @MathewsChilota 2 місяці тому +5

    Powerful words. We don't need to curse our nation due to painful situations. God will heal our nation

  • @quoniemagalasi9123
    @quoniemagalasi9123 3 місяці тому +9

    This man is one of men sent by God to deliver ❤

  • @LeyahPhiri-sd9xj
    @LeyahPhiri-sd9xj 2 місяці тому +3

    Munthu wamulungu wayankhula, wakumva amve zomwe Mulungu akuyankhula. ❤❤❤

  • @EmilyKamzoole
    @EmilyKamzoole 2 місяці тому +2

    Amen, very powerful message. God bless you, God bless Malawi.

  • @FelistaChiwalo
    @FelistaChiwalo 2 місяці тому

    Amen Abusa, Yehova ndithandizeni kuti ndizipanga zomwe chi Khristu chimanena, Amen.

  • @CharlesPhiri-ds1rk
    @CharlesPhiri-ds1rk 3 місяці тому +4

    Munthu wankulu....powerful massage Glory to Jesus🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌

  • @HildaKumwenda-ho8vz
    @HildaKumwenda-ho8vz 3 місяці тому +3

    Powerful message God bless you pastor ❤

  • @SaamSaaam-g2n
    @SaamSaaam-g2n 3 місяці тому +5

    ABUSA alalikira osati zomwe ayankhula ndipo ndi phunziro kwa tonse osati a President okha
    Tiyeni tisiye zonse mmanja mwa Mulungu popeza Iyeyo adziwa zonse bwino koposa mmene tidziwira❤❤❤

    • @DalitsoDjimo
      @DalitsoDjimo 2 місяці тому +1

      Mwayamba bwino zedi mbale. Anthu tonse tikanamaganiza choncho tikabakhala nidziko lantendere

    • @chimwemwendalama6260
      @chimwemwendalama6260 2 місяці тому

      Yes, inenso ndimmene ndavela ulalikiwu ukupita kwa aliyese ndipo ukumpuzitsa kuti tizikhala okhulupilila koma ma comment ndikuwaona ine apa eeee pakuti kumalawi kuno mmodzi atagoyamba ndi negative comment aliyense alemba zomwezo

  • @HevenChiwaya
    @HevenChiwaya 3 місяці тому +2

    Strong massage this is a lesson to the politicians who pushed a Malaysian people who's dying with hunger poverty

  • @odalachimphepo5257
    @odalachimphepo5257 2 місяці тому +2

    For the first time seeing a preacher without recognizing POLITICIANS 😂😂

  • @tomasvinkhumbu7487
    @tomasvinkhumbu7487 2 місяці тому

    Greatest message pastor God bless you

  • @wonganilungu6352
    @wonganilungu6352 3 місяці тому +5

    Abale ndi alongo timaseva zithu zopanda pake mmafoni athu. Zichotsenimo zoipazo komatu sevani uthengawu waphamvu muziwubwereza×10 kuposa zinazo. Tidzapeza mpumulo woyankhidwa kwa Yehova tonsefe tikawutsatira ndi kuwupempherera uthengawu patokha patokha

  • @VungaQueen
    @VungaQueen 3 місяці тому +3

    Mawu uphudzitsa ndipo achilimbikitso tingavutike motani titsataye chinkhulupiro yehovah ndiye zotse zanthu👏👏👏👏

    • @DalitsoDjimo
      @DalitsoDjimo 2 місяці тому

      Zoona m bale mulungu ndiye yanko tisanyozane pamene takumana nimavuto

  • @HestingsZiba-d6k
    @HestingsZiba-d6k 3 місяці тому +6

    Chakwela yekha ndamene akutikhomelela Malawi siziko losauka chakwela must go

  • @nathannbanda3345
    @nathannbanda3345 2 місяці тому

    This eas beautiful and powerful sermon, great 👍💯

  • @HildaKamfose
    @HildaKamfose 2 місяці тому +1

    Powerful massage amen

  • @WILFREDBANDA-o3r
    @WILFREDBANDA-o3r 3 місяці тому +1

    Powerful message ❤God bless Malawi

  • @Eric-gb9ms
    @Eric-gb9ms 3 місяці тому

    Indeed powerful preaching God bless you

  • @NellieMbisa
    @NellieMbisa 2 місяці тому

    Great message Pastor.......God bless you

  • @PETERSINKADZIWA
    @PETERSINKADZIWA 3 місяці тому +5

    Amene akukondwera ndi utsogoleri wa Mr Chikangawa ndiye kuti Mutu wake suyenda bwino

  • @serakillo8668
    @serakillo8668 2 місяці тому

    Ayi zkm man of god thank for good msg ❤❤❤

  • @florence500
    @florence500 2 місяці тому

    My favorite scripture... book of Job

  • @SalatielMathews
    @SalatielMathews 3 місяці тому +2

    Rev Yasinami Gamma,Mwatiphuzitsa Ambuye akudalitseni kwambiri,

  • @BerthaManyika
    @BerthaManyika 2 місяці тому

    Powerful man of God, uthenga wamveka

  • @Albertngwira-vy3th
    @Albertngwira-vy3th 3 місяці тому

    Amen i love this man of God 🇿🇲🇿🇲

  • @Musa1828-l5d
    @Musa1828-l5d 3 місяці тому +1

    Kuyakhula mopanda matha respect abusa a Gama

  • @phelantunikapikule4624
    @phelantunikapikule4624 2 місяці тому

    Amene ali ndi khutu la uzimu uthengawu wawuva koma amene ali ndikhutu koma osamava, ndiwo ma comment ambiri tikuwawonawa. Amen pastor

  • @feywellkapala7093
    @feywellkapala7093 3 місяці тому

    Powerful message man of GOd

  • @GeorgePhiri-ub2of
    @GeorgePhiri-ub2of 3 місяці тому +4

    Koma azanga mbusa uyu mulungu amupatse moyo wautali

  • @gomesavirgo3987
    @gomesavirgo3987 2 місяці тому

    Y.G is the greatest Reverend of all time

  • @kubengovender6996
    @kubengovender6996 2 місяці тому

    Big up brother man!!

  • @Zeka46
    @Zeka46 2 місяці тому

    🤣😂 God bless you Gama

  • @LytonMfuni
    @LytonMfuni 2 місяці тому

    I knew my rev: never go wrong.🇿🇲

  • @KennyTchapo
    @KennyTchapo 3 місяці тому

    Wat a wonderful preaching

  • @augustinechibbalazi8897
    @augustinechibbalazi8897 3 місяці тому +1

    May God bless His Word through you moderator and may He also plant a heart of philanthropy and patriotism in all political,traditional religious, and legal authorities in Malawi to be once again a Godfearing nation. Amen

    • @RaphaelLudaviko
      @RaphaelLudaviko 3 місяці тому

      malawi wathu ndipamene takhalapo. Amen abusa

  • @vukanifracksonchinkonde7324
    @vukanifracksonchinkonde7324 2 місяці тому

    Wonderful preaching

  • @tiwongehojaney5873
    @tiwongehojaney5873 3 місяці тому

    Powerful message ❤❤❤❤❤😊

  • @khamakhwiliro4093
    @khamakhwiliro4093 3 місяці тому

    Powerful Preaching

  • @chipiesato-ut7hx
    @chipiesato-ut7hx 3 місяці тому

    Powerful message ❤❤❤amen and amen

  • @MikeMakaww
    @MikeMakaww 3 місяці тому

    Great great great apstor of the year

  • @RobertCosmas-bo1uo
    @RobertCosmas-bo1uo 2 місяці тому

    Ulaliki mbambande yobu mwayenkha munali kulimba mtima ndkukhala nacho chikhulupiriro chozama amen

  • @hajisonzanditha1246
    @hajisonzanditha1246 2 місяці тому

    Great preaching

  • @bernadettechoma
    @bernadettechoma 3 місяці тому +1

    Hallelujah!🎉🎉🎉🎉🎉

  • @richardarmittage1693
    @richardarmittage1693 3 місяці тому

    Amen and Amen !!!!! Mau omveka bwino kwabasi

  • @GeorgePhiri-ub2of
    @GeorgePhiri-ub2of 3 місяці тому

    Chonde amalawi tisatembelele dziko lathu chonde mau akulu ochokela mkamwa mwa abusa yasini gama amen

  • @SkevaMustapher
    @SkevaMustapher 3 місяці тому

    Amen amen kuying'alula abusa

  • @LinessStafordsauti
    @LinessStafordsauti 2 місяці тому

    Amen man of God

  • @eunicesaiti
    @eunicesaiti 3 місяці тому +1

    Happy 60th independence Malawi and Long live.❤

    • @SafariBvumbwe
      @SafariBvumbwe 2 місяці тому

      Akulu mwati happy chani kkkkk kumalawi kulibe za happy mganize bwino

    • @inessmsiyambiri8517
      @inessmsiyambiri8517 2 місяці тому

      Eeee zako zili.pabwino Pali malawipa nkumati happy kakaka

    • @eunicesaiti
      @eunicesaiti 2 місяці тому

      60th independence and ufulu.

  • @eliasmpaso2978
    @eliasmpaso2978 3 місяці тому

    Powerful massage

  • @NDIZOTHEKABANDA
    @NDIZOTHEKABANDA 3 місяці тому

    Amen paste!!!!

  • @mablemathuso3903
    @mablemathuso3903 3 місяці тому

    Powerful message

  • @gabiembuhagondwe3629
    @gabiembuhagondwe3629 2 місяці тому

    Yassin gama ndiwaku 49 mama ccap church nt ku 25

  • @RalphZambezi
    @RalphZambezi 2 місяці тому

    Ndipo zobvuta Zambiri zikubwela sakunama

  • @HendrinaWalani
    @HendrinaWalani 2 місяці тому

    Amen so powerful

  • @kadongolakadongola
    @kadongolakadongola 2 місяці тому

    My reverend

  • @georgealabih8979
    @georgealabih8979 3 місяці тому

    True facts in life, ndaukonda uthengawu

  • @BerthaChisoni2
    @BerthaChisoni2 3 місяці тому

    Man of God

  • @BornwellChipango-s9m
    @BornwellChipango-s9m 3 місяці тому +2

    Koma anthu amalalika

  • @engieberlmaguaire5473
    @engieberlmaguaire5473 2 місяці тому

    Powerful

  • @ChikumbutsoTsalangu
    @ChikumbutsoTsalangu 3 місяці тому +1

    Awa nde anadalitsika ndinthu

  • @AtnessBanda
    @AtnessBanda 2 місяці тому

    Amen amen

  • @cynthiakananji1608
    @cynthiakananji1608 3 місяці тому +1

    Osayelekeza kuwapha awa ,taneneratu

  • @GiboTakondwa
    @GiboTakondwa 3 місяці тому +1

    Nkazi wopusa Ngati Mayi gotani hara

  • @desiremlewa
    @desiremlewa 2 місяці тому

    Kutumikila mulungu mwachindinje, pamalawi panga pano palibwanj?🎉 Hellooooooo

  • @RobertChikawonda
    @RobertChikawonda 3 місяці тому +1

    Eeeeeee ulaliki ogwila mtima

  • @MarthaChaima
    @MarthaChaima 2 місяці тому

    Amen

  • @StevenBwanausi
    @StevenBwanausi 2 місяці тому

    Ameen Abusa

  • @GeorgePhiri-ub2of
    @GeorgePhiri-ub2of 3 місяці тому +1

    Amalawi bvuto ulesi ndichikwa chake mtsoleli aliyese akakhala paudindo timati ndioipa akachoka wabwino kodi zooona atsogoleli onse. alamulilandziko linowa angakhale oipa ?

    • @chipi892
      @chipi892 2 місяці тому

      U might not mean what you want to say

  • @paulnyondo7572
    @paulnyondo7572 2 місяці тому

    Uthenga wabwino koma amaopako pangono a kambiri munthawi ngati iyi anaungalura uthenga .😂😂 a pule osawafunanso kkk.

  • @HusseinMoffatt-mi1fl
    @HusseinMoffatt-mi1fl 3 місяці тому +1

    Ayasin ndi mbambandetu ndi weniweni

  • @ShidaMfune
    @ShidaMfune 3 місяці тому

    Amen ❤❤

  • @chiletsobisweck5007
    @chiletsobisweck5007 2 місяці тому

    Mwangozi

  • @MikeMerecah
    @MikeMerecah 3 місяці тому

    Shehe uja amatinamiza koma uyu,

  • @chifundocharles2348
    @chifundocharles2348 3 місяці тому

    Chakwera akuzinyoza yekha aise😂😂 and inuyo mukugwira ntchito yanji if I may ask😂😂😂

  • @hastingsnamasasu8071
    @hastingsnamasasu8071 3 місяці тому

    Amen!

  • @user-sx7fg1NEDG
    @user-sx7fg1NEDG 3 місяці тому

    Amen 🙏

  • @HarryMakwale
    @HarryMakwale 3 місяці тому

    Amen 🙏 🙏 🙏

  • @MosesKhobiri-pr4hg
    @MosesKhobiri-pr4hg 2 місяці тому

    Ndiyitana padzina lanu yenkhova

  • @TwalikiWisiki
    @TwalikiWisiki 3 місяці тому +2

    A malawi sindimakumvetsani koma zowona after all what MCp has done to you in 3 weeks ago mwayiwala kale, kukuyitanani ku msinkhano inu nkupita,, mumati mukamvako chani chatsopano,,a oposition you guys are sleeping to much 😮h munayenela kukana osapezeka nawo pa chikondwelerochi,a MCP akukondelera their successful mission of killing chilima and the other 9, nchifukwa chake lero ali wokondwa,a malawi ndinu anthu osawona,how can you be invited for prayes to pray for the lives lost in chikangawa by the same man who orchestrated their death😢😢😢😢😢😢😢😢😢😢😢😢 Malawians are you nomal ⁉️⁉️⁉️⁉️⁉️

    • @EllinaBitto
      @EllinaBitto 3 місяці тому +1

      Ndipo inu😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭

    • @NatashaBema
      @NatashaBema 2 місяці тому

      Zosayenda

  • @SanhedrinMasauli
    @SanhedrinMasauli 2 місяці тому

    M'busa ameneyu ndi wandale, ananyozapo zipani zina ndikuyamikila mcp,

  • @DalitsoDjimo
    @DalitsoDjimo 2 місяці тому

    Wuthenga wabwino ambuye akudakitseni.

  • @PempheroAlufandika
    @PempheroAlufandika 3 місяці тому

    Ayasini inu ndi munthu wa mulungu ndipo ndinu mlangizi

  • @VincentAndrew-jz2gf
    @VincentAndrew-jz2gf 2 місяці тому

    Khaniyotu ndiyona

  • @PempheroAlufandika
    @PempheroAlufandika 3 місяці тому

    Ayasini inu zitigairani mau amulungu anthu munawasitha

  • @HamanjaManyela
    @HamanjaManyela 3 місяці тому

    Malawi is not poor country

  • @DevisonHala
    @DevisonHala 3 місяці тому

    Muzeni zoona aleke kupha anthu

  • @RedsonKambwiri
    @RedsonKambwiri 3 місяці тому

    Koma Uyudi anadzonzedwa zedi

  • @JosephEthan-l6u
    @JosephEthan-l6u 2 місяці тому

    Koma abusa Bible munalimvesadi ambuye akudaliseni

  • @dysonmakhwira2394
    @dysonmakhwira2394 2 місяці тому

    Kugunda kugwesa

  • @OweniMalokooweni-es9qx
    @OweniMalokooweni-es9qx 3 місяці тому

    Chinyora

  • @lusekeronyasulu8610
    @lusekeronyasulu8610 2 місяці тому

    Abusa aku 25?

  • @lexsonlanjesi2050
    @lexsonlanjesi2050 3 місяці тому

    Nde mwati ABUSA aku 25 eti???😂😂😂😂😂😂😂

  • @LovemoreUlayazulu-ne3id
    @LovemoreUlayazulu-ne3id 2 місяці тому

    Abusa a ku 49 ku nvama ccap church fumbi gheeto

  • @calvinmalinga1774
    @calvinmalinga1774 2 місяці тому

    kumalawi Kuno kulibe akazi opusa

  • @chiefmitengo
    @chiefmitengo 3 місяці тому

    Amene akunyoza Chakwera tsoka Kwa iye.uli ndi tsoka iwe onyoza munthu osalakwa, ngati ndi ulesi wakowo ongofuna kulandira go to page House khalamba yanu ikakupasani za ulele. Agalu inu

  • @SamsonshimokaSteven
    @SamsonshimokaSteven 2 місяці тому

    No the guy knows

  • @AmosPhilemon-y5e
    @AmosPhilemon-y5e 3 місяці тому

    Abusa ndye alalika kut amva tikunena kut zikoli timuchokeramo zikhale

  • @Crysis25
    @Crysis25 3 місяці тому

    Koma azungu akumva?

  • @mablemathuso3903
    @mablemathuso3903 3 місяці тому

    Mulibvumbulotso mu ulaliki uwu,tiyeni timvetsere bwino ndi khutu la uzimu.Ambuye apitilize kukugwiritsani ntchito abusa.