Це відео не доступне.
Перепрошуємо.

Kachikenaso Born Kalindo 😂🙌😂😂🙌 pa Chi Sunday 14 July 2024

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 13 лип 2024

КОМЕНТАРІ • 85

  • @user-do2cs8nf4b
    @user-do2cs8nf4b Місяць тому +9

    Ndalama zingowonongedwa anthu angofa mdzipatalamu mankhwala kulibe anthu angofa sisawawa Mulungu akuwoneni mwapaderadera

  • @user-nz7bd7lm4i
    @user-nz7bd7lm4i Місяць тому +8

    Born mulungu azikudalitsa kwambiliiiiiiiiiiii ndipo azikuteteza🙏🙏🙏

  • @MustaphaCassim
    @MustaphaCassim Місяць тому +6

    Chakwera akuwalipira azungu pa ntchito yomwe adagwila pakupha chilima

  • @ExcitedBreakingWaves-oh3zb
    @ExcitedBreakingWaves-oh3zb Місяць тому +5

    Achakwera akuwononga dziko lathu kwambiri.

  • @user-wd9yd1bg9n
    @user-wd9yd1bg9n Місяць тому +4

    Dziko lochitisa manyanzi, nkumati achakwera akugwira ntchito ngati president.

  • @user-fh7sd6gp3f
    @user-fh7sd6gp3f Місяць тому +3

    Tiyamike kubwera kwa tonse Alliance anthu mukung'alula kuti anthu tiziwe zenizeni more 🔥 🔥

  • @officemoyenda-rj2hz
    @officemoyenda-rj2hz Місяць тому +5

    Koma this very very shameful 😢😢😢😢😢

  • @cjaymw496
    @cjaymw496 Місяць тому +1

    Ya balance I think so too😂😂😂

  • @fredsemu7136
    @fredsemu7136 Місяць тому +2

    KOMA CHIKANGAWA ATIPWETEKA NDITHU

  • @MisheckAselo
    @MisheckAselo Місяць тому +3

    Chakwera mchifukwa chake anakapemphera ku CCAP kamutu kataya mission yapheduka, umkaona ngati wapha chilima zako ziziyenda, chilima sanafe akanalipo muona zakuda inu😂

  • @ThokozaniMunkhondia
    @ThokozaniMunkhondia Місяць тому

    A born kalindo,inu ndi mbambande😢😢

  • @edsonnyasulu5394
    @edsonnyasulu5394 Місяць тому

    Koma bon mulungu akuteteze

  • @ClearKondowe-m3j
    @ClearKondowe-m3j 28 днів тому

    Very sorry a Malawi kaya dziko lathu likonzedwa. Yoooo

  • @HappyAbyssinianCat-xt2bm
    @HappyAbyssinianCat-xt2bm Місяць тому

    Mulungu wakiya nawe chakwera waona mulungu wakwiya ndpo mulungu achita nawe iweyo

  • @user-qn2nu4xs9i
    @user-qn2nu4xs9i Місяць тому

    Ati akukonza zinthu!....😅😅😅😅😅😅😅...koma kukonza kunasintha..

  • @ZettaImuranYunusu
    @ZettaImuranYunusu Місяць тому

    Osati Ifeyo Amalawi ai.... But all opposition party's we are with you Trap

  • @user-ik5sz8hc6f
    @user-ik5sz8hc6f Місяць тому

    Ima poyela ndipo aliyense azimva ndithu.Tinasankha satana

  • @crosbeygondwe5403
    @crosbeygondwe5403 Місяць тому +2

    Kung'alulaaaa😂😂😂😂

  • @robertkamtimaleka4394
    @robertkamtimaleka4394 Місяць тому

    a Born Kalindo 42 million yommweyi basi

  • @wonganichakakanyirenda3299
    @wonganichakakanyirenda3299 Місяць тому

    Chakwera iweyooo

  • @user-hh4wn4vf9e
    @user-hh4wn4vf9e Місяць тому

    Auze DC ❤ agaru amenewo

  • @SumanJames
    @SumanJames Місяць тому

    Akalindo sakunama

  • @stevenbanda6665
    @stevenbanda6665 Місяць тому

    Tiuzeni zambiri bwana .kma dziko lathu lomwe kuzunzika

  • @DineoKotjomela
    @DineoKotjomela Місяць тому

    Ma mafia ati😂😂😂

  • @user-oy6dl1pv9e
    @user-oy6dl1pv9e Місяць тому

    The DiiiiiiiiiiiiiiiiiiiiiiiiiCiiiiiiiiiiiiiiiiiiiii

  • @JamesTeacher-b3o
    @JamesTeacher-b3o Місяць тому +1

    Bwana inuyo mmatha kuyankhula ulemu wanu

  • @AufiThera
    @AufiThera Місяць тому

    Wathu wathu born kalindo ✌️🔥 Kung,alula💯💪

  • @HalisonSolomon
    @HalisonSolomon Місяць тому

    KKKKKKKKKK BALANCE KUWAMALIZIRA PANTCHITO YOMWE ANAGWIRA PAKUPHA CHIRIMA NDI ANZAKE SHAME CHAKWERA

  • @user-ck7eb7tb7v
    @user-ck7eb7tb7v Місяць тому

    Munyengo yakung'alula

  • @Mikekajawo-pq9nr
    @Mikekajawo-pq9nr Місяць тому +1

    At we are building Malawi yet ndalama zikutuluka

  • @Musa1828-l5d
    @Musa1828-l5d Місяць тому

    Ndalamq zathu misokho yutha ukupeleka kwazigawenga azipha azibale anthu osalakwa Chakwera sukuwina ase ndakuuza

  • @peternashyo9850
    @peternashyo9850 Місяць тому

    Malawi akulowera kuti abale? Long live the DC

  • @SolomonNjolomole
    @SolomonNjolomole Місяць тому

    The DC ❤❤❤

  • @DineoKotjomela
    @DineoKotjomela Місяць тому

    Ma mafia 😂

  • @Pangolinimw
    @Pangolinimw Місяць тому

    The DC 😅😅😅

  • @user-xx4mt8ox8e
    @user-xx4mt8ox8e Місяць тому

    Mwati ndi Balance?

  • @RitaKainga
    @RitaKainga Місяць тому

    Ulemu wanu the DC

  • @GeoffreyMaulana-rh5rx
    @GeoffreyMaulana-rh5rx Місяць тому +1

    Ng'ona zalusa kufuna kusaulisa Malawi

  • @patrickmacheso5062
    @patrickmacheso5062 Місяць тому

    Mr Bon Kalindo ndinu oyankhuliradi a Malawi tonse, keep it up the DC.

  • @WilliamKawaza
    @WilliamKawaza Місяць тому

    Tell them DC

  • @jamesgama5489
    @jamesgama5489 Місяць тому

    Ayi zikomo

  • @BlessingsMikeyasi
    @BlessingsMikeyasi Місяць тому

    Nazoooo

  • @adzonzicomedy
    @adzonzicomedy Місяць тому +1

    😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂

  • @user-do2cs8nf4b
    @user-do2cs8nf4b Місяць тому

    Chili chonse chingowululika kumwamba kulandire ulemu

  • @AnnastasiaChakwiya
    @AnnastasiaChakwiya Місяць тому

    Ai zikomo achakwera

  • @Leo-fj6gz
    @Leo-fj6gz Місяць тому

    😢😢😢😢😢

  • @user-rs7vx6hc1k
    @user-rs7vx6hc1k Місяць тому

    Koma what is the use of our currency in Zambia? I don't understand this.

  • @BornfiyesignalSignalmtema
    @BornfiyesignalSignalmtema Місяць тому

    The dc

  • @pempheroraynnoxmpesi8713
    @pempheroraynnoxmpesi8713 Місяць тому

    Ya balance 😢
    RIP SKC

  • @user-bd5kw8oq1r
    @user-bd5kw8oq1r Місяць тому

    Choka iwe mbuli zokhazokha zomwe ziimakunvera iwe gawanani ndlmazo paja ndiyo ntchito yanu 😂😂😂mwayi ndi MCP ukudya bwino kamba ka mabodza akowo azipani akumakulipila 😅😅😅uziyamklika wamva

    • @tingamasi106
      @tingamasi106 Місяць тому +1

      Mbuli ndiwe mavuzi okhwimawo

    • @Dysonkhofi
      @Dysonkhofi Місяць тому +1

      Iwenso ndiwe galu,chitsiru

    • @user-bd5kw8oq1r
      @user-bd5kw8oq1r Місяць тому +1

      @@Dysonkhofi fisi,chule,mbuzi,,bulu munayiwala zimenezo zikomo God bless you 😊😊❤️❤️❤️ work up time is almost finished Jesus Christ is coming soon get ready before we die

    • @ednakaluwa5414
      @ednakaluwa5414 Місяць тому

      ​@@user-bd5kw8oq1rutukwana anzako..opanda chifukwa ena akubwexera utchula dzina la Mulungu shame on you.

    • @ednakaluwa5414
      @ednakaluwa5414 Місяць тому

      Vuto u need attention

  • @JamesAlinafe
    @JamesAlinafe Місяць тому

    Tha DDDDD ccccccccc

  • @katalamajames4947
    @katalamajames4947 Місяць тому

    Koma keni nsonda amadya mutu nkhope the same sekeleton ma R. V.sakugwira nchito

    • @zimmekapachika6784
      @zimmekapachika6784 Місяць тому

      😅😅😅😅😂😂😂mankwala anapima sakugwila 😅😅😅😅😅😂😂😂yomweyo galu iwe

  • @GanieAlidih-gu7no
    @GanieAlidih-gu7no Місяць тому

    Kukuyu nyamayake

  • @user-wd9yd1bg9n
    @user-wd9yd1bg9n Місяць тому

    Komanso chibadwireni ine ntchito ya asilikali athu muno mu malawi sindikuiziwa, chifukwa ngati nkuteteza dziko .bwezi atalipanga boma ili held responsible pa nkhani iyi infact predent akadamuchosa.

  • @user-lc3sw8iz2g
    @user-lc3sw8iz2g Місяць тому

    Balance

  • @AndersonChimwala-hz4so
    @AndersonChimwala-hz4so Місяць тому

    koma amalawi

  • @LiamTennessee
    @LiamTennessee Місяць тому +1

    Amazalandila malipilo a ntchito yomwe adagwila

  • @RobertLuka-wy9cl
    @RobertLuka-wy9cl Місяць тому

    Born kalindo 🙏🙏🙏🙏🙏

  • @user-jn7bt1uy5s
    @user-jn7bt1uy5s Місяць тому

    Zovetsa chisoni 😢

  • @JohnConar-kq4hi
    @JohnConar-kq4hi Місяць тому

    The DDDDDDDDDCCCCCCCCCCCC 🤔

  • @kelvinsibande8779
    @kelvinsibande8779 Місяць тому

    The DDDDDCCCCCCC

  • @WilliamBandaWili
    @WilliamBandaWili Місяць тому

    Mmmmm haa?

  • @CharityChikomo-hl1gz
    @CharityChikomo-hl1gz Місяць тому +1

    Ma 20kwachawooo??

  • @chadreckchibwithala1493
    @chadreckchibwithala1493 Місяць тому

    ANTHU PANO MMANGO PANGA MA COMMENT KOPANDA KUSATILA ZINTHU . NDALAMA ZOMWE ZAPEZEKA KU ZAMBIA NDI ZAMAYIKO ANGAPO KUPHATIKIZA MALAWI ANTHU OMWE APEZEKA NAZO NDIZINKA ZA KU RUSSIA OMWE AKUPANGA MA BUSSINES A MA DRUGS OSATI ZOTI BOMA AYI MMM KALINDO ECHI BOZA LENILENI ZINAMIZA ACHILOMWE AKOWO

    • @TysonMwenye
      @TysonMwenye Місяць тому

      Ndiye anthu aku Russia wo angapeze ndi ndalama zathu chifukwa choti akugulitsa ma Drugs? Ifeyo tikamapita ku mayiko akunja timasintha ndalama zadziko lomwe tikupitako.Ndipo tikamaliza business yathuyo tisanatuluke mudzikolo timasinthilatu zamalawi.Ndiye awowo apezeka bwanji ndi ndalama zathu (Mwk) koma kudziko lina chinawakanikitsa kusintha kumalawi konko ndichani ngati ndizachilungamo ndalamazo

    • @tingamasi106
      @tingamasi106 Місяць тому

      Ndalama zama drug mpaka sealed? Iwe ndichimbutumwa wamva

    • @munashemoyo4190
      @munashemoyo4190 Місяць тому

      Kusonyeza kt zomwe zikuchitika dziko muno iwe zikukusangalasa et i uzaziwona ukazakwatila ukasiya kudyesedwako mbudzi yamunthu iwe kape

    • @AmosScott-z9x
      @AmosScott-z9x Місяць тому

      Kape iwe

    • @chadreckchibwithala1493
      @chadreckchibwithala1493 Місяць тому

      mbutuma ndinu osaziwa zinthu alomwe matama basi tiyeni uko .
      mleke kutivuska mngalamuliraso yai chalo ichi jiiiiiiiii peter wanuyo no

  • @user-si8vm5vj8s
    @user-si8vm5vj8s Місяць тому

    Shame on you chakwera

  • @warrenmwambazi8342
    @warrenmwambazi8342 Місяць тому

    Very bad 😊😊😊

  • @FrancoKaunga-rq2ki
    @FrancoKaunga-rq2ki Місяць тому

    Kalindo ndi nyatwa auze zitsiru izi.

  • @DineoKotjomela
    @DineoKotjomela Місяць тому

    Ma mafia 😂