BON KALINDO LERO PA 17 JULY 2024 |

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 10 вер 2024

КОМЕНТАРІ • 124

  • @johnmpatama1461
    @johnmpatama1461 Місяць тому +6

    Watching from Stellenbosch Capetown

  • @SaidiMbawa-st6bj
    @SaidiMbawa-st6bj Місяць тому +7

    Anthu safuna ku sogolera dziko ayi amafuna maudindo ndi ndalama palibe chazelu chomwe angachite

  • @SahilluYusuf-sk7es
    @SahilluYusuf-sk7es Місяць тому +2

    He us totally true to convince us ,anyera many I aMCp.Even UTM was there because of Chilima

  • @DanielKatengeza
    @DanielKatengeza 23 дні тому

    Watching from Spain

  • @AlickDaud
    @AlickDaud Місяць тому

    Watching from Botswana the Dcccccc

  • @JohnfosterNkusengwa
    @JohnfosterNkusengwa 24 дні тому

    Watching from cape Town pa boma the DC

  • @OsmanGift-f4p
    @OsmanGift-f4p Місяць тому +1

    Watching from SA cape town langa. Bon kalindo you the powerful do not just leave like that help Malawi from this creaminals

  • @aubreykatembe3081
    @aubreykatembe3081 Місяць тому +1

    Takawabanduledi DC

  • @IssahAluba
    @IssahAluba Місяць тому

    Watching from S/A

  • @DavidJackson-ox4xm
    @DavidJackson-ox4xm 25 днів тому

    The DC'S mwana woooopsa kwambiri chilungamo chiyende ngat madzi umakwana Iweyo

  • @KayRolly-l7n
    @KayRolly-l7n Місяць тому

    Watching frm Johannesburg. This man is wise.

  • @JeanBanda-zy6wu
    @JeanBanda-zy6wu Місяць тому +1

    50+1 is here to stay.... munangoifuna kuti muthane ndi dpp inu mukuithawa zanu musova

  • @EllinaBitto
    @EllinaBitto Місяць тому

    Tell them,watching from Durban South Africa ❤❤❤❤

  • @user-im7sc2my4w
    @user-im7sc2my4w Місяць тому +2

    Chilima anatisiya ,Koma UTM ,mupangisa Kuti chipanichi muwononge ,Kalindo ndizowona akunenazi

    • @VincentMagriva
      @VincentMagriva Місяць тому

      Ndipo they need money olo zot tsiku limene Dr saulosi chilima anakumana nalo mosayembekezela nawonso azakumana nawo anaiwala pa dziko lapansi palibe wamuyaya this is your time ndalamazo ibani koma musamale pot pot baibulo limat tsoka ntunde nd nyanja pot oipayoo wasikira komweko

  • @VictoriaKumwenda-k6o
    @VictoriaKumwenda-k6o Місяць тому +1

    Akaliyati bingu anamwalira mmanja mwanu mnachitapo izi mnali anduna nthawi yimeneyo mlomwe mzanu mnachitapo izi nyifwa yikuwawa kufwa kwa kwachilima ambiri mwasangalala kuti mpeze mavoti koma ziwani kuti maw lanu simkuliziwa

  • @user-gn4mx2es3k
    @user-gn4mx2es3k Місяць тому

    Ine monga Vice DC ndikungogwedeza mutu pa zomwe bwana wangawa akulankhula

  • @AngolanChinga
    @AngolanChinga Місяць тому

    I'm hear cape town khayelisha but i love bon kalindo always God bless you bro

  • @MarvGerald
    @MarvGerald Місяць тому

    Iwedi ndichilombo the DC ndimwana woopsa

  • @GeorgePhiri-ub2of
    @GeorgePhiri-ub2of Місяць тому

    kukamba mosabisa phuma LA mai kaliat ndi bambo njalawa liononga chipani anthu awiri awa ndamene akuchita zinthu mwa phuma kwambili

  • @HamitonFrank
    @HamitonFrank Місяць тому +1

    Watching from Johannesburg the DC

  • @CHRISSYBALALIKA
    @CHRISSYBALALIKA Місяць тому +1

    Kuyankhura chilungamo osaopa aliyense 🔥🔥 more fire DC

  • @JibuzahDrag
    @JibuzahDrag Місяць тому

    Watching from Johannesburg South Africa

  • @ConfusedAstronaut-qv6wq
    @ConfusedAstronaut-qv6wq Місяць тому

    AniBo umakhwana,tikuverani ndithu,kuchokera kuno ku Molere,masambanjati.

  • @VincentMagriva
    @VincentMagriva Місяць тому

    Ndipo they need money olo zot tsiku limene Dr saulosi chilima anakumana nalo mosayembekezela nawonso azakumana nawo anaiwala pa dziko lapansi palibe wamuyaya this is your time ndalamazo ibani koma musamale pot pot baibulo limat tsoka ntunde nd nyanja pot oipayoo wasikira komweko

  • @EmmanuelMalata-r4j
    @EmmanuelMalata-r4j Місяць тому +1

    Mr Born kalindo more fire mumatiyiimlira❤❤❤❤❤❤❤❤

  • @Robertmkango
    @Robertmkango Місяць тому

    Watching from south Africa

  • @OsimanIbnAkim
    @OsimanIbnAkim Місяць тому

    The DC munthu ooooopsa💪💪💪

  • @UlemuKwilambo-o3j
    @UlemuKwilambo-o3j Місяць тому

    Watching from SA, Bloemfontein free State

  • @MariamChipoka
    @MariamChipoka Місяць тому

    Your a hero❤❤

  • @violetpotani
    @violetpotani Місяць тому

    Anthuwa ngamadyera chabe palibe chanzeru chomwe akuchita iwo bola ndalama

  • @SahilluYusuf-sk7es
    @SahilluYusuf-sk7es Місяць тому +1

    Watching from SA pretoria

  • @YusufChipojola
    @YusufChipojola Місяць тому

    From tete Mozambique

  • @ChifundoNinje
    @ChifundoNinje Місяць тому

    Watching from cape town

  • @PaulMwachande
    @PaulMwachande Місяць тому +1

    Mwiniwake oziwa ku ng'alula umakwana THE DC

  • @InnocentnMbale-zq8pk
    @InnocentnMbale-zq8pk Місяць тому +1

    Ndalila ine chomwe akuchita sakuchiziwa zoona chilima azimupanga chonchi chifukwa chandalama

  • @joanaKachiwaya
    @joanaKachiwaya Місяць тому +1

    Ubwino wake wovota ndifeyo tikufuna Mary chilima atuluke aphulitse bomba

  • @KaisiAbdullah
    @KaisiAbdullah Місяць тому

    Watching from Durban the DCEEEEEEEEE my precedent wathu

  • @LindaChikwawa
    @LindaChikwawa Місяць тому

    Mumakwana mr DC uremu wanu

  • @JeanChirwa
    @JeanChirwa Місяць тому

    Zoona D C Walankhula Zoona.
    Keep it Up.
    God Be With You Always.

  • @CharityKangulero
    @CharityKangulero Місяць тому

    Watching from Belleville copetown

  • @STEPHENBJNKUMBIRA
    @STEPHENBJNKUMBIRA Місяць тому

    Koma munthu uyu zimagovuta amalangiza vuto ndi ife anthu 50+1 iwewo akuti akufuna kuyichosa analowa boma ndi chani ngati zili zimenezo ndiye kuti anthu aja sakuyenera kukhala pamene paja

  • @AgnessMzengo
    @AgnessMzengo Місяць тому

    😢😢koma zoona a UTM😢koma mzimu wake utikanthe.... A malawi ndife anthu osachedwa kuiwala..... Evance Meleka anaimba kale # Adzakuiwala, uzasanduka nyasi😢chikondi cha pa dziko lapansi

  • @james-zd2nz
    @james-zd2nz Місяць тому +1

    Watching from jhb

  • @AliKaukutu-bo7cx
    @AliKaukutu-bo7cx Місяць тому

    Watching from cape town Mitchell's plan all the from malawi balak

  • @masterkachingwe7448
    @masterkachingwe7448 Місяць тому +1

    Mai Kaliyati atsongolere UTM kukhala bata and morale

  • @ConfusedAstronaut-qv6wq
    @ConfusedAstronaut-qv6wq Місяць тому

    Agalu a mcp maka makaka pepe kale ndi ndi Chalakwe,aluga kwasiba

  • @YasinMusa-ym8lp
    @YasinMusa-ym8lp Місяць тому

    Dc we love you ❤

  • @salimmkumakumakitombi-yc7pw
    @salimmkumakumakitombi-yc7pw Місяць тому

    I'm hearing live from khayelitcha Barracks ( Capetown)

  • @MarcRero
    @MarcRero Місяць тому +1

    ❤❤❤❤❤

  • @BettyByson-t4z
    @BettyByson-t4z 25 днів тому

    Flom phalombe mbambande bon,

  • @JascoUluma
    @JascoUluma Місяць тому

    Koma umanena chilungamo chokhachokha umakwana l proud of you

  • @Lazarus-qo1sl
    @Lazarus-qo1sl Місяць тому

    The DC kunena chilungamo

  • @PempheroMoleni
    @PempheroMoleni Місяць тому

    Live the DC wa ine umakwana

  • @petertaulo8014
    @petertaulo8014 Місяць тому

    We will stand as UTM forever

  • @user-xv5pr3ji6w
    @user-xv5pr3ji6w Місяць тому

    Tiri pano kumvera ine pat wa patrick, from Pretoria SA

  • @mrcool531
    @mrcool531 Місяць тому

    Akhale phee ali ndi nthawi? Next year elections

  • @Kareemah-y4p
    @Kareemah-y4p Місяць тому

    Koma umanena chilungamo chokha chokha bro mumatiyimilila

  • @JunaKananji
    @JunaKananji 24 дні тому

    Karido Dc❤🎉🎉🎉🎉🎉🎉🎉🎉

  • @MarvinChilombo.flourish
    @MarvinChilombo.flourish Місяць тому

    Kalindo akundisokoneza, akuti a UTM akanadekha kaye. Aaaa nthawi ndimene yatha. akufunika apange strategize za 2025 race. After all, divisions are inevitable in politics coz even Kalindo himself can not name Chilima's successor who will be liked by everyone in the party. UTM is running out of time. Rest well SKC

  • @DOMINICSOKOSO
    @DOMINICSOKOSO Місяць тому

    Ubwino wake Ife tikuyang'ana inu konko make the utm party walks accurate there u r our trust

  • @AmosMkandawire-re9pw
    @AmosMkandawire-re9pw Місяць тому +1

    The DC mwana wowopyaaaaaaa kwambiri tell them the truth. From South Africa

  • @StanleyDama
    @StanleyDama Місяць тому

    Choka iwe nesa unawauza ndiwe

  • @JonathanChimwaza
    @JonathanChimwaza Місяць тому

    Live from south Africa cape Town

  • @ChimwemweKondowe-nj4lx
    @ChimwemweKondowe-nj4lx Місяць тому

    Akhaula amenewo. 50+1 mmesa anayiyambisa ndiiwowo kodi, ndiye lero akuyiopatu powona kuti sangamake.
    Mulingo omwe munamuyezera nawo Peter Mutharika 2025 walunjika pa inu achakwera ndi uhule wanuwo

  • @TemwaKabisa
    @TemwaKabisa Місяць тому

    Ulemu wanu Mr DC ❤❤❤❤

  • @BintonDzuwa-d3p
    @BintonDzuwa-d3p Місяць тому

    Iwe umafuna zimenezi

  • @GeorgeWhite-f1p
    @GeorgeWhite-f1p Місяць тому

    👍💪💪💪

  • @UlemuNewton
    @UlemuNewton Місяць тому

    Zeeeeeeeeee Dccccccccccccccc ❤❤❤❤❤❤❤❤❤kuti khazuuuuuu

  • @iqrahzaheed8633
    @iqrahzaheed8633 Місяць тому

    Kubandura kubandula

  • @MoosaChirwa
    @MoosaChirwa Місяць тому

    Keep fire burning mr

  • @PrinceBlessings-bv5bs
    @PrinceBlessings-bv5bs Місяць тому

    Number one ❤❤❤❤

  • @patrickjaenda8288
    @patrickjaenda8288 Місяць тому

    Katundu waboma

  • @lastchipwere4481
    @lastchipwere4481 Місяць тому

    Ngati pali munthu mmodzi yemwe bon kalindo sangamuzuzule ndi Michael usi,,now i beleive

  • @freedahjere2164
    @freedahjere2164 25 днів тому

    Zamveka ndithu

  • @yassinn5634
    @yassinn5634 Місяць тому

    Kodi inu a Kalindo siinu nomwe mumalimbikitsa kuti UTM choke ku MCP ndipo abwelere ku mene anachokera ku DPP. Ndiye lero mwapeza choyankhula chifukwa zomwe mumayembekezera sizinachitike

  • @user-be5fc3ed1i
    @user-be5fc3ed1i Місяць тому

    The DC mwana wowopsya kwambiri Bon kalindo kuyankhula mosaopa

  • @jacksonmaster2288
    @jacksonmaster2288 Місяць тому

    The D C, mwana oopsa kwambili. Koma kalindo UTM amayikonda kwambili. I will keep saying this now and again

  • @cictechnologies1091
    @cictechnologies1091 Місяць тому

    Munthu uyu ndi wamisara ndareka kumuvera

    • @Charlesnsiri
      @Charlesnsiri Місяць тому

      😢Amakuza ndan kt uzmunvela

  • @HanunKelekesa
    @HanunKelekesa Місяць тому

    Umakwana

  • @JustinLoka-ed4bx
    @JustinLoka-ed4bx Місяць тому

    😂😂 katundu uyoo

  • @NoelBurton-x1z
    @NoelBurton-x1z Місяць тому

    The DC

  • @user-fi7ko7bl6f
    @user-fi7ko7bl6f Місяць тому

    Zosatheka kupha iweo, iweyo ndi mwana oopsa kwambiri ,

  • @user-mx5cx3gl4h
    @user-mx5cx3gl4h Місяць тому

    🤣🤣🤣the DC moto

  • @pemphero-fo9en
    @pemphero-fo9en Місяць тому

    Mwalankhulako zazelutu lero akalindo

  • @OwamiSimeon
    @OwamiSimeon Місяць тому

    Born kalindo the deceeee

  • @sheila5812
    @sheila5812 Місяць тому

    UTM yama kandulo 😂😂

  • @mensuremegrem8330
    @mensuremegrem8330 Місяць тому

    50+1 ilipo ndipo ndilamulo sitilola nanu mulione

  • @TessMjuma
    @TessMjuma Місяць тому

    I wont be a chakwela 😂

  • @VictoriaKumwenda-k6o
    @VictoriaKumwenda-k6o Місяць тому

    Amai chilimawo sakuziwa kuti anzawo ali pachingalalo kugulisa chipanicha amuna awo sakulira chilima koma kuti akusangalala kulira ife timakuziwa

  • @ephraimnogwe6430
    @ephraimnogwe6430 Місяць тому

    50+1 idabwera kuzakhala imene inja

  • @amosbula1249
    @amosbula1249 Місяць тому

    Bon Kalindo akunena zoona

  • @VictoriaKumwenda-k6o
    @VictoriaKumwenda-k6o Місяць тому

    Ndalama yimapangisa munthu kupanda nzelu akaliyati mawwona ngati alindi nzelu koma ayi awagula adpp ndi iweyo kalindo mwagulisidwa simukulira chilima ayi nkhani yake ndikugulisa utm

  • @user-bd5kw8oq1r
    @user-bd5kw8oq1r Місяць тому

    Mbuli iwe thokoza MCP ndi akatundu pa nkhani za chitukuko komaso ukudya bwino chifukwa cha Boma limeneli ukulinyoza koma ndlama ukulandila from opposition 😅😅😅😅 Munda wako umenewu keep it up mpakana MCP iwina the more ukunyoza the more God's grace and popular MCP will gaining more popular 😅😅😅😅😅

    • @Creslevison-vj2sl
      @Creslevison-vj2sl Місяць тому

      Kupusa ndikulankhula mopanda umunthu apa kagwere uko apa

    • @user-bd5kw8oq1r
      @user-bd5kw8oq1r Місяць тому

      @@Creslevison-vj2sl bola wamva ndithu pajatu anthu amakonda Balaba kusiya yesu wina ndinu bola zamveka mukadakhala mukumvetsera uthenga oti ukupulimutsani bola koma za ndale aaah sorry mzeru mulibemo koma opposition ilipoyi or atawona kuti ichi ndi chabwino sangayamikile because alingati satana amatsutsa chilichonse or pasimenti akuuzani kuti mukutithila fumbi nkhani ndi maudindo adziko la pansi kungowavotera mudzanenaso kuti bola yemweuja pa social media sipobweretsera nkhani za kunyumba kwanu ayi kapena kuphunzililapo kutukwana ayiso ndiye sankha wekha panopa ndi chakwera timusapote basi akabweranso wina timusapotenso kuti dziko litikuke koma Izi aaa tikhala pamodzimodzi momwemu

    • @user-bd5kw8oq1r
      @user-bd5kw8oq1r Місяць тому

      Inetu sindinyengerera pochita zinthu because mbuli zophunzila zachuluka koma zosathandiza dziko koma kumasula dziko ndi kuligawanitsa

  • @RamadanShafisha
    @RamadanShafisha Місяць тому

    Inu pezani ntchito yoti muzigwila

  • @MoosaChirwa
    @MoosaChirwa Місяць тому

    Chilimalism😂😂😂😂😂

  • @user-rt6rd1em8y
    @user-rt6rd1em8y Місяць тому

    😂😂😂😂😂😂

  • @user-xd1cm7tm7t
    @user-xd1cm7tm7t Місяць тому

    Dc kuyankhula mopanda mantha 😅

    • @NovassTambala
      @NovassTambala Місяць тому

      Your the best, washing you form cape town graders

  • @EliasKawuwa
    @EliasKawuwa Місяць тому

    Is that activism,or politics? Osangoqasiwa bwanji,Mesa ndi chipani chawo,Mesa iwe unachokamo? Aaaaa asiyeni ndi chipani chawo, ndani safuna kudya?

    • @oskidooscar7468
      @oskidooscar7468 Місяць тому

      Kkkkkkk
      Iyeyi amamuopa manganyanso

    • @sheila5812
      @sheila5812 Місяць тому

      Paja amapangira ma drama limodzi 😂​@@oskidooscar7468

  • @JustinWBanda
    @JustinWBanda Місяць тому

    50+1 kungogwila ntchito erection imozi basi ndale zopanga ndicholingazofuna kuthana ndiwina wake

  • @BrightPhiri-bt6ev
    @BrightPhiri-bt6ev Місяць тому

    Kuchikamwa kwakoko bon kalindo ndichifukwa chake chipan cha utm chatha.mesa umati atuluke mu alliance wakhaula wanyanayo. Ukusokoneza anthu ndiweyo mesa umati atuluke within two months ndiizo sopano utm yamala

    • @MoosaChirwa
      @MoosaChirwa Місяць тому

      Nanga anawauza Kuti azikangana Ngati galu iwe tapeleka report la ndalama zagwidwa Ku Zambia ma box ma box chipani chako cha MCP changoti chete kusonyeza Kuti MCP
      Kuba
      Kupha
      Kuononga
      Kape iwe asiye a UTM alongosole chipani chawo okha iwe usalowelepo

    • @BrightPhiri-bt6ev
      @BrightPhiri-bt6ev Місяць тому

      Kape ndiwe galu ndrama ngati zapezeka ku zambia ndiza boma zapezeka bwanji ku zambia? Dont you know kuti ziko lililose kuli ma scammers? Wamvako zina lachakwela kumene kuja huh? Mbuli yamunthu.wamvako dzina lamunthu wa mcp kumene kuja do research first.

    • @BLESSINGSSTOLO-lt9di
      @BLESSINGSSTOLO-lt9di Місяць тому

      Uli mbali itino?

    • @BrightPhiri-bt6ev
      @BrightPhiri-bt6ev Місяць тому

      What do you mean? Dont go around thy bush

    • @salimmkumakumakitombi-yc7pw
      @salimmkumakumakitombi-yc7pw Місяць тому

      kumavetsa nanu before comment ..mutu wankhani waumva koma kkkkk kungofikira kunyodza .