Bro mnyamata okanidwa kuti asayomire u pule uja wangoti ziiii kodi adamuchotsa ku conversation ya mcp kapena amupha a mcp kapena a court order basi anango mu deleter kuti asamapezekenso 😎. Chifukwa izo zachinyengozo ine singalowelera kuti ndilowelere tiyamba ndi achakwera zikhale kunkuyu achimwendo ndi ena onse iwowo kuba chinyengo kupha kuzunza zonse😅
Road traffic one of the most corrupt in malawi government
Ku Road traffic Mesa VC anaptako mwa soon....?
Ndipo 500% agree ànd ndakumbukila mawu ajomo kuti azitsogoleli athu nyela basi not zoti tchito imayenda bwanji
ACB has to be involved also to clear the vehicles..... was this done or was by passed ?
Road traffic is rotten fish
Chakwera wayesetsa kuchulukitsa chinyengo mMalawi.
Bro mnyamata okanidwa kuti asayomire u pule uja wangoti ziiii kodi adamuchotsa ku conversation ya mcp kapena amupha a mcp kapena a court order basi anango mu deleter kuti asamapezekenso 😎. Chifukwa izo zachinyengozo ine singalowelera kuti ndilowelere tiyamba ndi achakwera zikhale kunkuyu achimwendo ndi ena onse iwowo kuba chinyengo kupha kuzunza zonse😅
Mmmm kulitu zinthu
Zowona yatsala office imodzi
Question; who changed it's ownership? And how? 😏
@@LouisAndrew-jr1yj 100% that's the right question
Zimenezo ndi mbava za mcp achina zikhale
Ndipo ndizona Road traffic yawonjeza ivn ife madriver tikuvutika ndi anthu awa 040 panopa akuba kwambiri
Triphonia ali ndi ndalama that is why apolidi worked opanda ngati ine mbola... Am a living witness.
@@Kenmoney-xp7tz Akanangoti uziyendera😂😂😂😂😂😂
Iwe kuyendera mpaka tsiku lakufa kupepeza😂 apolice ngasambi
Mmmmm
Am an interested party
Imeneyo ndye Nyasaland kkkkkkkk kulibe za serious chilichonse ndichamasewera
@@JumaSoja 🤣
Zoonadi yasala office imodzi ndipo akuyenera kukafufuza
Chinyengo chidaendapo apa
kod inu za nkhondo ya ku Russia and gaza munasiya
@@Yahiya-wm8nd ku Facebook timaponya daily Kumalawian Cameras yaku fb
Mmmmh ku bagamoyo sungakumvetse