Kalindo is trying his best,chikufunika osusa agwirane manja!,ku UTM apereke mpata kapena position imene Mary chilima angatenge icho chiperekeranso mphanvu ina yapadera muchipani.
Mayi chilima to be president, braund banda,mwana wachilima awa kaliyati, awa musankhemo mumozi ankhale president mwana wa chilima anyamata ose ankhala ndi chidwi
What if mrs Chilima is not a politician? Komanso akuti anthu azilowa kuchipinda ndi candle nkumakatchula dzina la Chilima kodi Chilimayo wasandukano mulungu?
Brayani Banda ndimunthu wa chikondi ndi ziko Lake mayi cilima tiwona ngati chilimayo alipo anthu tivota ambiri mwana wachilima anakonda achinyamata ndiye achinyamata ose ali ndi ife
Your the best the DC bon kalindo❤
Thanks sir for ur update
Bon kalindo amalankhula zoona zokhazokha koma anthufe timangoti ndi wama comedy let's support him as malawians
Kalindo amatha kwambili❤
Wamisala anaona nkhondo,,lero Bon kalindo mukumuyamikila koma mmene munkamunyozela siizi😂😂😂😂
Ati amakutengan ngat manyi😂😂😂😂 chi booooniiiiii kalindoooo
Kuyankhula mopanda mantha ngati wakhalira mfuti Bon kalindo 😮😮
Ndpo inu
Uyu ndiye activits yemwe timamudziwa, Bon kalindooooooo!! Mwana owopsa kwambiri.
Yomweyo fadaa🎉
Born kalindo🔥🔥🔥🎷🎷
I love you so much
God bless you Kalindo
Umakwana
Good advice sir.
True
Uyu ndiye ❤
❤❤❤❤❤❤❤
🎉🎉🎉 following
Always your the best all the time mr president Bonie Kalindo
The DC🔥🔥🔥
U always stand in true mr Bon l love u more than
Salute
Good advise Mr born kalindo thank you 😅
The DC
Zikomo bwana DC UTM yitulukedi kumeneko iyime pa yokha basi
Khan nd yoona
Chilungamo chimamasula go ahead the DC
Mbambande Bon Kalindo
Like this guy or not , but he is very sharp
Mumaitha bwana d c ndi more pachilungamo😊
Mr Kalindo mukutitsegula mmaso kwabasi keep it up
Umaitha bon
Mumatiimilira a bon
Utm siingatuluke mugwilizano ngakhaleso atatuluka palibe chazelu chomwe angapeze
Big up to you 🎉🎉🎉🎉🎉 umatha kung'alura
Komatu bon kalindo amayakhula ngati wamisa koma ndizoonadi zimene amayakhula anhtu inu muzichenjera
President wathu Mr DC
Kalindo amalankhula zoona uyu ndi mpulutsi.
The DC mwana ohopya kwambili
Bwana DC mumatiimilira
Good advice
Powerful spetch
DC Huma kwana
Kalindo is trying his best,chikufunika osusa agwirane manja!,ku UTM apereke mpata kapena position imene Mary chilima angatenge icho chiperekeranso mphanvu ina yapadera muchipani.
the dc
Tiyeni tiyeni tiyeni Mr DC
Kulankhula mwachilungamo. UTM tsegulani maso. Tulukani mu tonse alliance monga akunenela Bon Kalindo please.
A MCP asakupusitseni ife tili mbali yanu ndi SKC osaopa, osatopa, osafooka 💪
Mr DC 2025 woyyeee.
My vote kalindo umatha umatiimirila
Bon kalindo akunena zowona lelo muchoke ku mcp mukapitiliza ndiye kuti mukusangalala ndi ife ya chilima chipani chimene chingawine ndi UTM kampeni wake zikolose lapasi lipanga saport
President wathu wathu,Mr Kalindo lero ndilomwe tidziwedi kuti UTM ipitilira ndipo SKC waphera chilungamo.
Kmat uyu tiyen Tzimuvela zimene amayankhulaz
Ah b
kalindo umakwana ase
Kalindo more 🔥 ❤
The DC kkkk konda u ife
Big up de DC our pool p
A UTM uthenga ndiumeneo zili ndiinu kunyalanyaza kapena kutengapo kanthu km mawa pangatalike muzawakumbukira mau a Bon sadutsa pachabe
Sanena boza uyu
Chilungamo ndimwano❤ The DC pick up man
Our freedom fighter ndiwe kawawa ndithu
Bon kalindo umakamba zoona
😹😹😹 iwe umakwana aaa nilinje mau
Kalindo good advice
Mumatha
Mayi chilima to be president, braund banda,mwana wachilima awa kaliyati, awa musankhemo mumozi ankhale president mwana wa chilima anyamata ose ankhala ndi chidwi
DPP+UTM+UDF+AFORD....
MCP out 2025..
THE DC PANGOLINI 💪💪💪💪💪
Umakwana winiko
In short Utm ibwerere ku DDP....tigwetse vinyau tikinze dziko
Wise man
It's true bwana president woyamba wa anthu osauka muno Malawi
The Dc bon kalindo ❤
What if mrs Chilima is not a politician? Komanso akuti anthu azilowa kuchipinda ndi candle nkumakatchula dzina la Chilima kodi Chilimayo wasandukano mulungu?
Musapusisidwe a utm mcp sichipani .muzifunse kuti kodi chilima chamupha ndichani kodi mukugona a utm, tsegulani mumaso
Na pa Bone Kalindo palibeso same same Mtanyiwa anthu awa amanena chilungamo chokhachokha
The Dc bon kalindo 🎉🎉🎉
The DC ,lankhula chilungamo bas
Usazafe kalindo uzangotsowa ngati eliya
The DC agogo anga akufuna azakuoneni
Tidziwe basi.
Ma traitor tiwadziwa lero
A UTM mukapanda unvera za bon kalindo muzalira moyo wanu onse
Good Good news
Very true
Ndipo a mcp ndi athu ochenjela ndi kuipa komwe ndipo chilima amusasa lelo akuyanja otsalao mukapusa akumezani
The DC mulomwe wathuwathu odziwa zinsinsi
Amakwana koma ❤
boooooon kalindo!
🎉More fire!!!!!!!!!!!
Brayani Banda ndimunthu wa chikondi ndi ziko Lake mayi cilima tiwona ngati chilimayo alipo anthu tivota ambiri mwana wachilima anakonda achinyamata ndiye achinyamata ose ali ndi ife
My vote umakwana
The problem is anthu akumudz unthengawu suwapeza cz of social media
Mzimu wa bwana Chilima uwavuta.mukaone maruwa ngati akukanika kufa .musamale kwambilitu.
Palibepo zomwe mukulusapo zazelu zimodz modzi zosavekaso mkomwe
Koma manganya asamuwelengele ndiwa MCP kuyambila kale
Makwana mr keep it up
Sadzalaga munthu Asana dzudzule big mukulankhutu inu
The DC😊
The Dc mawu ako a koma akagonela
Mumakwana bwana born kalindo
Nice