Amen, Mulungu wathu ndiwamoyo anatulutsa Daniel mudzenje la mikango kuli bwanji ifeyo tikhale ndichikhulupiliro atimenyera nkhondo.a Yudasi wo ndi chiyambi chotchoka mkono ma Bp akubwera simanyengelera
Ife tinavotela chakwela opanda id tinangwilitsa ntchito kalata ya Kwa afumu Lero zikutheka bwanji Kuti tingwilitse Id Why ? Kumwamba kuli mulungu Chakwela sakuwina Ayi,,,,,;:::;:;;;;;;;; mademo akachikeso kunyumba k wa Richard Chomwendo Banda Komaso Kukhala kuswa Katundu waboma.Zilib
Chakwera machende ake ndithu zoona kupha Chilima ashiiiiii 💔💔💔💔💔💔
I support Limpopo FM with Comrade Mtanyiwa God bless you all the time
Number 1 Limpopo fm MBAMBANDE
Pepani chifukwa cha Malilo ,,koma comrade. Mumachulutsa kuyankhula pakhani imodzi ,,kubwereza bwereza,,anthu timadikila kunva zomwe mwabweretsa like Bon Kalindo ,,osati kuyankhula chimodzi chomwecho
Pepeni nkhomled ntanyiwa cha agogo anu ndipo mzimu wao uwuze mumtendele kuchisilam timat Ina linlah wainna ilayih rajiuna
Chikangawa yomwe yoooo😂😂😂😂😂😂
Pepani pepani Mr comrade ntanyiwa tingoti mzimu wawo ukause mumtendere😢
Sorry Mr ntanyiwa. May God comfort you
Comrade inuyo ndi one....may the Almighty God protect you and keep you safe.
Asilikali Kodi izi mungozisiya choncho umboni mutaupeza ?
Asilikali anthu ndio foila mbwanji sakupita kwa dala kadula asa
Condolences Mr Ntanyiwa for the grand's lost. May her soul rest in peace 🙏🏿
Sorry for the lose, May God comfort u and the family
😂😂😂😂mpaka amayo kotooo😂
Amen, Mulungu wathu ndiwamoyo anatulutsa Daniel mudzenje la mikango kuli bwanji ifeyo tikhale ndichikhulupiliro atimenyera nkhondo.a Yudasi wo ndi chiyambi chotchoka mkono ma Bp akubwera simanyengelera
Estamos unidos em oração Ntanyiwa I'm a Mozambican from Mozambique...
Sorry for the lost for your GladMother may her soul rest in peace Cormrade Mtanyiwa
Pepani Mr Ntanyiwa poluza agogo anu mulungu akutothozeni
pepani mr comlade ntanyiwa poluza agogo anu
Sorry sir.. Komabe we love you
Pepan kwambiri Comrade, poluza agogo athu, mzimu wawo uwuse mumtendere
God will expose all those who took part in the evil scheme against innocent citizens of Malawi, and judgement will follow suit
Pepani achimwene 😢,,,
May the soul of your grandparent rest in peace
Sorry Brother NTANYIWA for the Loss. It is sad to loose such a strong pillar. M H S R I E P ✝️✝️✝️
Chilichonse chikuchitika from aboveko chikungokhala pambalanganda kikiiii athawa afa ndi BP
Azabwele Ben longwe tizamudura machende achabuyake akuona ndipo machende ake Ben longwe tikakumana pa 8 aliyese wosokonedza tizazimitsa pompo
Pepani pepani chifukwa Cha kuluza gogo wathu m,zimu wao uuse mutendele 🙏🙏
Koma ntanyiwa iweyo sindimakunvesa iweyo ndi one😅😅😅
boma la zigawenga ili chakwera ndi chigawenga chachikuru ndziko muno
Chikangawa yalavula mizimu chifukwa chake chake ena agendedwa komanso ena BP yashuta
Pepani kwambiri amtanyiwa poluza Agogo anu
Amen ...Comrade from Nguludi
Kkkk manganya satana wachabechabe,
Chakwera l don't think so kut amaliza chaka chino akupuma😞
Olo ine ndikuona chochoso and it's my prayer Kuti nayeso age basi
Inu Dala kadula ndindani kweni kweni kukhal ndiulamulilo phaka kupha munthu Eeee ayi zafika pa wes🤔🤔🤔🤔🤔
Inalilah waina ilaih rajoon
Tikufunaso Michael usi atulukeso UTM chifukwa ndi wabodza Alondole chibwezi cha chakwelacho bas
Chikangawa analowa pa mpando ndi mademo,achokenso ndi mademo ,waononga dziko lathu
Pepani comrade
Pepani Comrade 😢😢😢
Mumatiyimarira inu a ntanyiwa
Napepe brother Mtanyiwa
😂😂 koma comrade avutika chikangawa
Ifa nayonso imaflasha kuti ine kapena iwe ukufuna kufa.
Ndiye wina aziti niwamuyaya kulibe
So sad may her soul rest in peace
My his soul rest in peace timakudyadilani
Pepani comrade mtanyiwa
Pepanikwambir Mr mtanyiwa
pepani achimwene, ineso ndi kumuyamika Mulungu agogo anga amwalila Friday km amwalila alindidzaka 97
Listening
Dr chikangawa akunjenjemera a taona chikangawa forest imupweteka
😂😂😂😂😅
Mulungu akungwila ntchito yake chilima sanalakwilre munthu aliyese 13:57
Rest in peace grand mother of ntanyiwa😓😢😥😓😞
Pepani comrade poluza agogo anu
Mr tanyiwa inuyo munabwera
A vice president adziwona mizimu yakwiya
Amuphonya nayo miyala😂
Pepani Mr ntanyiwa
U vice president wopa Mpha ndichontcho amicable usi iyi simbali yanu Munakangozisiya mufera zaweni Michael usi Kuti Moyo wanu ukhale wawutali bola musiye zomwe mukupanga anthu sakukufunani Ayi
Ulemu wanu comrade
Limpopo inabwera
My she rest in peace agogo
Rest in peace to her
Kod chakweratu afa safika povota ameneuja
Azione ndinthu ameneyo dr chikangawa
Comrade umakwana
Pepani comrade ntanyiwa
Choyambilira ambuye atothonzeni chifukwa cholunza agogo anu.
May her soul rest in peace
Mulungu awafewesere njira yawoyo
Pepani ndithu apume mwa Ambuye
Malawi Chikangawa Party -- Chipani Chosamba mwadzi .
Nyansi zeni zeni.
Mwatasa Mdziko la Malawi, mukuyitha tiyeni nazo poti ndinu "AMUYAYA"
Tikumvera mwachete ndithu!
Pepani infa sisankha.
May de departed soul Rest in peace
Tiuzeni amfumu ntanyiwa ife tilibwino ndithu kuno ku cape town
Agogo athuwo nzimu wawo uwutse muntendele
Ife tinavotela chakwela opanda id tinangwilitsa ntchito kalata ya Kwa afumu Lero zikutheka bwanji Kuti tingwilitse Id Why ? Kumwamba kuli mulungu Chakwela sakuwina Ayi,,,,,;:::;:;;;;;;;; mademo akachikeso kunyumba k wa Richard
Chomwendo Banda Komaso Kukhala kuswa
Katundu waboma.Zilib
Pepani kwambiri Mr ntanyiwa
Pepani Anthanyiwa
Pepani pepani kwambili antanyiwa kamba koluza agogo athu pepani kwambili
Iwe unabwela kusakhala😅
5:29 pepan
Palibe ife tinakhala Ndirande yomweyino koma. Kulibe wapanga ma Demo kuno
Dala kadula Munthu oipa kwambri
Rip
Pepani kwambili kumademo munakakakharakoso kms muzikapangiraso ku malawi ngat ban kalindo azikava kuwawa kwambili samukirani ku malawi chonder
Mukufuna akamupe mwaiponda
Mzimu wawo uwuse mumtendere
Pepani mr potaya agogo
Pepani a ntanyiwa
My condolence to you comred
Wina angwa vimbuza
Ndimakunyadila mtanyiwa komandilibetu number yanu
Mugwidwa nonse asilikali pleasegwiritsanintchitoinformation
Pepani ntanyiwa
😭😭😭😭
Wachitabwino kuntchoka nkono
Sorry Mr ntanyiwa chifukwa chachimenechi
Ben Longwe ndi Gulu
😢😢😢😢😢😢