Bon he is talking the truth, but u can see other people they talking sheet, be very careful my fellow Malawian, we must wake up guys, zinazi sizotengela kupita ku school, khalani pansi moganiza bwino, malangizo awuleletu awa,all the way from johannesburg
Zooona zokhazokha, Chilima wakhala duuuuu a Malawi tikulira, olo one day osalankhulapoyi mmene m"boma mukubedwera ndalamamu, nde atifune pano? Ine ndamitsikatu, he won't get my vote
The problem with Kalindo is that he wants to be the master minder of Chilima. But he has to understand that Chilima has brains. My instincts also tells me that he is indirectly campaigning for DPP.
In your minds but he talks vry true posatengera za ndale,,,,,and all of this akuya khula ndizoona,,,, nokha mukuziwa mene adalankhulila chilima mu campaign ya 2019 analankhula zambili mbili zokomera Ife achinyamata koma ndzt wakwanilitsapo,,,,,inuso musamangosutsa zilizonse you supposed to see the true
Iwe sukuimirira a Malawi koma chipani china chomwe aliyense akuchidziwa. Ukulimbana ndi Chilima nthawi zonse bwanji? Kodi kwinako kulibe zofooka zawo. Usawaike a DPP ngati ndi Angelo lero. Sitinaiwale zomwe amachita padzana paja. Tikudziwa kuti mtunda wa kwanu ndi omweo. Usatinamize ife takana.
Boma la Chakwera silizakhala labwino kwaiwe only if utakhala Minister. Unduna sapatsa zitsiru ngati iwe. Anthu a kwa Chulu akakuthibula bwera uzazione. Kulira 4 years kufuna udindo kkk😂😂😂😂
Bon Kalindo you have gained a supporter!!!!
Honest speaking Mr DC Big up
booooon kalindo Mo fayaa. keep on to give us truly updates. inu mumalankhula chilungamo chokha chokha
Bon he is talking the truth, but u can see other people they talking sheet, be very careful my fellow Malawian, we must wake up guys, zinazi sizotengela kupita ku school, khalani pansi moganiza bwino, malangizo awuleletu awa,all the way from johannesburg
Who spoke that spoke?
Go ahead Mr kalindo we are following you
Komatu a Kalindo munthu osamuipitsa choncho. Inu musamunene Chilima kuti oipa lero. Mwagwira naye ntchito limodzi. Kuipa kwa munthu amadziwa ndi Chauta basi. Inunso muli ndi zonyansa zanu.
khala chete iwe
aaaaah kuipa kwa munthu amakuziwa ndan? mxiew
Mr kalindo moto 🔥 🔥🔥
man of integrate😂😂😂 Bonnnnnnn Kalindooooo mwana oopsa kwambiri from Njeza village ..T/A mabuka, mulanje😊😊😊😊😊
Yes you are really talking
Chakwera ndi Chilima wooooyeeee,muwaphe A Malawi onse mukatha mutenge mitemboyo muitafune Mukhute,popeza ndalama mwawa bera Kale,koma muziwe masiku amatha ndikugona adaku voterani wokha samaziwa zoti Chibwenzi chankhwangwa chokoma pokwera, Amalawi mukaza voteranso awa izo ndi zanu wanthuwa ndi aka Nyimbi Anunkhisa Malawi.
Kalindo is matured now
Chisilu mbuzi 😢😢😢
Mukunena zoona big, koma mmalawi opusa akuona ngati chilima ndiwabwino
Bwana Born Kalindo pqjatu ndinu amene munamukakamiza Chilima kuti avomere kukhala vice president lero mukumunyozaso . Komaso inuyo mumatiuza kuti sindinu wandale koma chosecho mukuwauzaso anthu kuti akqvotere aford , udf kqpenda dpp.
Mbambande mr presdent bon kalindo kwathu kwa chulu zinthu sizilibwino tikukhalangati tili mkamwa mwa mikango
Kodi inu mumkamuuza chilima ngati ndani? Osachita naye msanje. Pangani zanu akulu
Shaaaa this was days ago
DC ❤❤❤
Zooona zokhazokha, Chilima wakhala duuuuu a Malawi tikulira, olo one day osalankhulapoyi mmene m"boma mukubedwera ndalamamu, nde atifune pano? Ine ndamitsikatu, he won't get my vote
Ndipo nkhaniyi ndioona big up DC
Bwanji adzangotiimra bon kalindo yomweyo pa u president,akuoneka ali ndi nzeru kwabasi
Ipondeni Fadala........ You're a real son of Malawi........
Zoyankhula za bon kalindo zatitopetsa tsopano, katakwe ndi bakili muluzi tv
Zakutopetsa not zatitopetsa bwana
Ingosiyani osamamvela bas,,,,, za ziiii
The problem with Kalindo is that he wants to be the master minder of Chilima. But he has to understand that Chilima has brains. My instincts also tells me that he is indirectly campaigning for DPP.
This is true. Kalindo is 4 dpp
In your minds but he talks vry true posatengera za ndale,,,,,and all of this akuya khula ndizoona,,,, nokha mukuziwa mene adalankhulila chilima mu campaign ya 2019 analankhula zambili mbili zokomera Ife achinyamata koma ndzt wakwanilitsapo,,,,,inuso musamangosutsa zilizonse you supposed to see the true
I fully agree with you, Kalindo is taking advantage of illiterate masses.
Which brains dear, you talking about??? No he is bad man also,can he preform good speak today how??
Koma kumanidwa udindo kulira mpakana 4 years
Apadi akunena zoona zaka zonse takhalayi chilima ali.duuuh nde angabwele kwa ife kutiwuza chani ??
Kalindo to the people
Kalindo ndiwamisala uyu
Chilima sanalakwise kanthu, cholinga akawukira muzimunena kuti amangowukira kulikonse? Apa pokha nde ayi, boma ili tinalivotera chifukwa cha Chilima, nde atulukeko chifukwa? Mesa kuli mavoti ake, musiyeni Chilima akhale, nthawi ikakwana ayankhula
Aziyankhula zichani Nanu Inu chilima wanuyo
Ndizoona ndikugwilizana nazo
Nkhanira yakwachulu yokha mwapala. Miyambe mwazimvetsa zinthu mmene zikuchitikora. Bwerani ndi ma demo anuwo tione ngati simuyaluka
Vchifukwa choti azakhala pa u president ndichifukwa achakwera amuphera.....
Chifukwa chani mdziko mumalowa anthu osaziwika bwino
Musamuipitsile mbiri a chilima inunso simulibwino.
Yes DC akunena zovona
Bon kalindo ulemu wanu
Dzapangeni nawo compete bwanji because it seems mukudziwa zambiritu
Zoona amasankha tsogoleri ndi mulungu. Inu musaweluze
Akunena zoona kalindo
anatipwetekesa asabweleso
iwe ndikumenya bwanji mulimbana ndi DC wanga
Tabalirankon aku mwera usabwere ndi mademo Ako pano pakati chita kwanuko
Ndiye tivotele ndani utiuze kalindo manyi ako
Amakomadi akamwalira munthu sure
Chilima usogoleli mlibe ose ndi adyera same like chakwera 😅
Zitsiru ndizomwe zingakhulupilire chilima opusa omwewa ndizomwe zikunamizika chilima zaupresdent alibe nazo ntchito koma iye azingodyelera mimba yakeyo
Kalindo akufuna atibalalise Ali ndi reason behind
Yaaa
Munthu amakondedwa anamwalira Pamalawi
Impossible ngati munthu akugwira ntchito mmboma sangayankhulepo zotsutsa boma man limenelo nde bodxa
Uyu ndi wamisala chilima ndi otumidwa so sakadaima mkuyankhula mudakati ndi oukira
Akutitenga ife uchitsilu pomwe achitsilu ndiyiwowo amalawi asukutsula ngati tinachotsa mbuyawo kamudzi chifukwa chankhadza chakwela nde ndanitso galu kwabasi
Chilima waonetsa kudekha ndipo sadaukire koma kalindo ndale zidakulani
Dziko likamaonongeka mtsogoleri wabwino sadekha ....chilima akudekha zichani pamene zinthu zikufoila mdziko muno
Ndizoona zimene akuankhula karindo chifukwa nthawi yakampeni ndiiyeyo amene amanyamula thumba la 50 kg sichakwera iyayi
Chilungamo chimawawa,Koma DPP ayi ziko linaliko bwino mnthawi yimeneyo
Aka ndi kachilungamo
Uzitiuzanso za DPP ifeyo lero? Moti ukakhala umati aMalawi angamvere ndithu iweyo kkkk
Kalindo ngati ndi chamba uzavula galu iwe ukukhale wachilungamo ndiwe mulungu?? Ndiwe galu kwambiri usatibowe uziyankhulira amako ndi anthu akwanuko
u a big fool
Iwe sukuimirira a Malawi koma chipani china chomwe aliyense akuchidziwa. Ukulimbana ndi Chilima nthawi zonse bwanji? Kodi kwinako kulibe zofooka zawo. Usawaike a DPP ngati ndi Angelo lero. Sitinaiwale zomwe amachita padzana paja. Tikudziwa kuti mtunda wa kwanu ndi omweo. Usatinamize ife takana.
Boma la Chakwera silizakhala labwino kwaiwe only if utakhala Minister. Unduna sapatsa zitsiru ngati iwe. Anthu a kwa Chulu akakuthibula bwera uzazione. Kulira 4 years kufuna udindo kkk😂😂😂😂
Aaaa chilima angoputsisa MCP tsingapase utsogole chifukwa chakwela akumva kukoma ndibanja lawo lotse nso dzoti chilima akudziwa chilungamo koma manyadzi uchitsilu mutayeni tiwone 2025 dzizatha bwa
Zoonadi zianthu zoipa kwambiri 😂😂😂😂😂😂😂
Eh komatu akulu awa chilima anakulakwilani chani muja munayambila kumunenamuja mpakapano or kukuyankhani osangomusiya bwanji ndiwankulutu ameneuja amadziwa chimene akupanga nde zinazi ife mumatinyasanazo zomalimbana ndimunthu oti samakuyankhani
Chilima ndi witch craft mbuzi mwana wajoka amati tizidya katatu madzi awulere magetsi awulere fetelizer wochipa. chilima ndifiti kwambili
Zinthu zake
Kkkkkk
The DDCccccccccccc
It a better to dellete this video. You have cursed him
Lero akuti anali tsogoleri wabwino tooo bad
Izi ndi nkhani za amalawi ngakhale a president anayankha nkhani ya America mu chichewa, translate in English nonsense
Kkkkkkkkk