Це відео не доступне.
Перепрошуємо.

KUZUKUTA NKHANI ZOMWE ZACHITIKA.UKU KWATENTHA 🔥🔥🔥🙌🙌

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 25 сер 2024

КОМЕНТАРІ • 100

  • @CHRISSYBALALIKA
    @CHRISSYBALALIKA Місяць тому +12

    Mukaona munthu akuti MCP my vote ameneyo ndi wa family ya chakwera mwina ndi ankolo ake kapena chakwera anakwatira pakwawo which means phindu la chakwera akuliwona ameneyo wachita zolozeka kwawoko

  • @macdonaldmunthali9895
    @macdonaldmunthali9895 Місяць тому +9

    Very wrong decision,the end of utm.chilima was the only leader with great vision and calmness, you can't make decision out of anger.

  • @user-nc4vi1jt5g
    @user-nc4vi1jt5g Місяць тому +3

    Kabambe afunampando ku utm koma autm samalanaeni mtsogoleli wanu autm sankhani kaliati ndiponso pamasankho adzawina anthu tilinae ndichikhupililo enawa tawaesa akanika

  • @user-nj5vu8cd5l
    @user-nj5vu8cd5l Місяць тому +1

    Nkhani ndiyomweyo mwamva bwino zikomo kwambiri pamibawa.. God bless you two guys... Mamakutu wava koma wopanda makutu mawa wazakuwawani

  • @lifayohbenson1994
    @lifayohbenson1994 Місяць тому +3

    Ku utm kulibe mphungwe mpungwe
    Winayo chipani chake ndi odya zake alibe mulandu

  • @user-io2uw2me9f
    @user-io2uw2me9f Місяць тому +1

    Anapha dala chilima cholinga anthu abalalike koma mulungu ndiwadongosolo a utm osafooka osatopa osaopa

  • @SharifChibwana
    @SharifChibwana Місяць тому +5

    Bakili Muluzi tv ndi katundu

  • @user-nv3rf7bl7r
    @user-nv3rf7bl7r Місяць тому +2

    Uku nde kuyankhula kopanga umodzi that's y ndimakukondani amibawa chifukwa mumayankhula chilungamo

  • @DavieChiwale
    @DavieChiwale Місяць тому +1

    Apa a UTM Mukapanda kumva zanu izo

  • @PeterTembo-zj5jk
    @PeterTembo-zj5jk Місяць тому

    Dpp moto❤❤❤

  • @ManzyNgoleka
    @ManzyNgoleka Місяць тому

    vuto inu akulu mukukocha ndale mwachidule nanu mulikuseli kwa enaake

  • @user-gk6bf7xe9g
    @user-gk6bf7xe9g Місяць тому +2

    MCP my vote ❤❤❤❤❤❤

  • @JazzdMonga-v6e
    @JazzdMonga-v6e Місяць тому +1

    Kumupeza wina akuti mcp my vote
    Amalawi ndichani

  • @BillyMhone-jp3kn
    @BillyMhone-jp3kn Місяць тому +2

    Khondo Yochita kutiponyera Mcp kumupanga usi
    LET HIM BE THERE WILL MAKE CONVENTION SOON

  • @hanifahmponda8711
    @hanifahmponda8711 Місяць тому

    Aaa manganya ngati mutu mwake dziyendamo bwino ayi musiyeni ku MCP koko afela nayo limodzi

  • @VincentMbeye
    @VincentMbeye Місяць тому +1

    Yalakwa UTM kuchoka msanga ....awonesa umbuli kwambili

    • @Aqiec09
      @Aqiec09 Місяць тому

      Ndipo usavage wa athu ophunzira umakhumudwisa

  • @daviskamonde4882
    @daviskamonde4882 Місяць тому +2

    Don't lie to us.
    You support MCP.

  • @user-nj5vu8cd5l
    @user-nj5vu8cd5l Місяць тому +1

    Njawala number one, kaluati number two be careful ndi anthu awiriwa ndi anthu oyipa mutima kwambiri
    We love utm kwambiri koma isakhale ya munthu

  • @doreenkaliati3166
    @doreenkaliati3166 Місяць тому

    Zoona zake anganidze mofasa sure ❤❤❤❤❤

  • @JaphetSakala-pq4fl
    @JaphetSakala-pq4fl Місяць тому +2

    UTM motomoto osadandaula

  • @MosesNanchinga
    @MosesNanchinga Місяць тому

    Ma comment onsewa bwanji simukukamba za ndalama ai kma UTM sinalakwitse kuchoka ku alliance coz sanalandire ulemu uku ku MCP atizuza ndlmazo mukukanika kugulira mankhwala zipatala bwnj

  • @TonykalicheloKalichelo
    @TonykalicheloKalichelo Місяць тому +1

    Inu ngat mwin wake amafuna kusazika ndiye mukufuna omusatila atan

  • @lyiemax
    @lyiemax Місяць тому

    Proper narration, big up guys ❤❤❤

  • @RegistermoseskashonKashon
    @RegistermoseskashonKashon Місяць тому +1

    Inu nde munabwela kudzauza amalawi tchutchutchu osat akapilikon enawa ongokamba zinthu zopanda kumutu

  • @user-rf4br1fv2z
    @user-rf4br1fv2z Місяць тому +2

    Mwawathandiza ulemu

  • @DalitsoPhiri-sq5nl
    @DalitsoPhiri-sq5nl Місяць тому

    Skc ankafuna kutchoka after kusalemekdza mgwirizano omwe unalipo ndiyeno kutchoka it's a good move komano to agree with ndikutenga mnthu kunja that's wrong indeed

  • @EdsonNjonjo
    @EdsonNjonjo Місяць тому +1

    Munthu uyu akunena zoona

  • @AlliSaiti
    @AlliSaiti Місяць тому +5

    Athu akuda ndife opanda nzeru

  • @OsmanMasamba-ck4mo
    @OsmanMasamba-ck4mo Місяць тому +1

    Manganya iwetu wagulidwa ndichisilu chinzako

  • @FloraBanda-w7t
    @FloraBanda-w7t Місяць тому

    Koma selina 😂😂😂akut kod akabambe akulowela kut 😂😂😂😂

  • @user-ux9ik4zr5x
    @user-ux9ik4zr5x Місяць тому

    Probably the best program

  • @InnocentEdasi
    @InnocentEdasi Місяць тому +1

    Ndibwino kt atengane okhaokah

  • @StevieTaiza-r9j
    @StevieTaiza-r9j Місяць тому

    Mulungu azikutete bro

  • @user-vm7iz6oz6r
    @user-vm7iz6oz6r Місяць тому +1

    Akumatibera zathu zomwezi zamisokho

  • @EstherManda-ex3bc
    @EstherManda-ex3bc Місяць тому +1

    🤣🤣🤣🤣 nkhani zake

  • @Aqiec09
    @Aqiec09 Місяць тому

    Yea that's very true and I see it ku utm utsogoleri unali wa chilima ena onsewa mavuto bola ku MCP komweko mudziwa bwanji mwina the death of chilima was planned with those who are on top blaming MCP for the death yets amafuna mpando wachilimawo why so early kutuluka mugwilizana without solid proof that is MCP guilty , ine unless pa social media muzabwerese real proof how you saw the killing happen that's when I will find them guilty

  • @ChiyembekezoPhiri-sv8nw
    @ChiyembekezoPhiri-sv8nw Місяць тому

    Njawala ndi kaliati mutiwonongera chipani chathu ndakwiya Nanu heavy kuno kuntheu mutisamale awirinu

  • @Ishriss1999
    @Ishriss1999 Місяць тому

    Ma prophet watu koma atilankhilitsa pambali mxiiiiew

  • @mzeewandembonyirongo2972
    @mzeewandembonyirongo2972 Місяць тому

    Gwende u have fairly advised

  • @user-lg6ym4hz3w
    @user-lg6ym4hz3w Місяць тому

    Kkk😂😂😂😂😂😂😂😂 anzanga afumu owuka

  • @SabinaNkhoma-sf7kz
    @SabinaNkhoma-sf7kz Місяць тому

    Mmmmm km mcp yaonjeza,zot amalawi akuvutika sakuganizako

  • @user-rx7cc7tc6b
    @user-rx7cc7tc6b Місяць тому +1

    MCP 💥💥💥❣

  • @GiftKaunda-f8j
    @GiftKaunda-f8j Місяць тому

    Analysis yanzeru zozama koma imeneyo?

  • @ChristopherKabanga
    @ChristopherKabanga Місяць тому

    anthu atamalankhura ngati mmene ukuyankhulira lweyo anthu akhoza kumachitazinthu mwanzelu

  • @ChrispinKashosha
    @ChrispinKashosha Місяць тому +2

    Mcp ya wina kale

  • @user-he5ol5or7f
    @user-he5ol5or7f Місяць тому

    Gwede is the best

  • @dysonmasiye5736
    @dysonmasiye5736 Місяць тому

    Nduna zomwe zikugawa ndalamazo akumatibera misonkho yathu yomweyi...ifetu maso athu tikuona ndipo tilankhula chaka cha m'ma chino....40million plus just for one meeting business yanji imene akupanga? Apapa zaonekeratu kuti andale amatibera pomwe anthu akufa ndi njala. Ambuye akukuonani ndithu

  • @innocentissah2636
    @innocentissah2636 Місяць тому

    Pamaliro wandale athamangitsidwe

  • @JasonMailos
    @JasonMailos Місяць тому

    😢😢😢😂 ozuka kumandao
    Eeeeee kusokonezatu kkkkkkk

  • @cynthiakananji1608
    @cynthiakananji1608 Місяць тому

    First to comment

  • @MasaukoNyirongo
    @MasaukoNyirongo Місяць тому +1

    😂😂😂😂😂😂😂 koma zinaz abale kkkkkkk kuthamangitsa masiket mudzi kkkk

    • @SamKaposa-i5c
      @SamKaposa-i5c Місяць тому

      😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂Koma abale

  • @AdenaGuest-g4b
    @AdenaGuest-g4b Місяць тому

    Kuwechetamwangajimbilambali

  • @AdenaGuest-g4b
    @AdenaGuest-g4b Місяць тому

    Aaaaa
    Malawi

  • @ZioneMkangadzula
    @ZioneMkangadzula Місяць тому

    utm igawana zida zafikapa angonamizana

  • @chrisgremu740
    @chrisgremu740 Місяць тому +5

    MCP 🔥🔥🔥🔥

  • @AdenaGuest-g4b
    @AdenaGuest-g4b Місяць тому

    Umakwana

  • @PociahMack
    @PociahMack Місяць тому

    Kma nkhani ya a pro andiseketsa bwanj😂😂

  • @PhiriChitani
    @PhiriChitani Місяць тому

    Ndinu a Mcp chokani apa mukuyiwala kuti UTM idayamba yokha without mcp

  • @user-nj5vu8cd5l
    @user-nj5vu8cd5l Місяць тому

    Usi ndi munthu yimodzi yomwe mwini wa UTM

  • @SprianoJeke
    @SprianoJeke Місяць тому

    Kugawa ndalama Koma ma servants ndee ka salary ka mmanja

  • @SprianoJeke
    @SprianoJeke Місяць тому

    As government I think abalalika ndithu

  • @ChristopherKabanga
    @ChristopherKabanga Місяць тому

    vuto amalawi timasapota vitsilu kali ndi ........

  • @user-gk4nu4xr8r
    @user-gk4nu4xr8r Місяць тому

    Of course

  • @GeorgePhiri-ub2of
    @GeorgePhiri-ub2of Місяць тому +2

    akuononga chipani cha utm ndi mai kaliati ndi azao filex njawala anthu awawa ndithu amaliza chipani cha utm samalani

  • @MsondaBanda
    @MsondaBanda Місяць тому

    Ntchindi mulije mu utm

  • @user-kj7hr2jf1l
    @user-kj7hr2jf1l Місяць тому +1

    Zowona utm yisatenge munthu wakunja

  • @atupelemposa4786
    @atupelemposa4786 Місяць тому

    😂😂😂

  • @MayesoKulea-sh8xd
    @MayesoKulea-sh8xd Місяць тому +2

    MCP ☑️

  • @YohaneMotison
    @YohaneMotison Місяць тому

    😂😂😂😂😂😂

  • @PulayaKalaka
    @PulayaKalaka Місяць тому +1

    Mcp mooootooooooooo

  • @user-cb5gh9md4i
    @user-cb5gh9md4i Місяць тому

    Kodi ntchentche zikutanipo pamibawapo

  • @YamikanAbubakary-my4ie
    @YamikanAbubakary-my4ie Місяць тому +1

    Ambuye mulungu daritsani chipani cha mcp 🇲🇼❤️
    🙏🙏

    • @Extratremendouszeus
      @Extratremendouszeus Місяць тому +1

      Ndiwe opembedza mafano
      Mulungu wa Abraham sangadalitse MCP...siwachisokonezo ngat Chakwera wakoyo...usamutchule Mulungu pachabe...ungaone tsoka

    • @user-px6kt8rx2p
      @user-px6kt8rx2p Місяць тому

      Ukunama ukadakhumudwa mcp chiyembekezo cha Malawi ambiri

    • @robertkalima874
      @robertkalima874 Місяць тому

      @@user-px6kt8rx2p MCP chipani chafuko

    • @SamKaposa-i5c
      @SamKaposa-i5c Місяць тому

      Usatchule dzina lamulungu wako pachabe chome iwe

  • @MosesNanchinga
    @MosesNanchinga Місяць тому

    Ma comment onsewa bwanji simukukamba za ndalama ai kma UTM sinalakwitse kuchoka ku alliance coz sanalandire ulemu uku ku MCP atizuza ndlmazo mukukanika kugulira mankhwala zipatala bwnj

  • @Extratremendouszeus
    @Extratremendouszeus Місяць тому

    Abwenza ndalamazi...eni ake akutuwa kusowa sopo...akuoneka a fumbi lokha lokha km ena akuononga mosaopa Mulungu...ayi tiona posachedwapa....nafe tikudikira

  • @AdenaGuest-g4b
    @AdenaGuest-g4b Місяць тому

    Aaaaa
    Malawi