BON KALINDO LERO UTM YAGULITSIDWA NDI MCP 🤔🤔🙌🙌

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 28 жов 2024

КОМЕНТАРІ • 104

  • @MansonNyamwela-g5r
    @MansonNyamwela-g5r 2 місяці тому +6

    Mr DC, watching you live from dar es salaam, Tanzania.just wishing you a very great Sunday, keep on doing good job.

  • @GreyMwanyimbo
    @GreyMwanyimbo 2 місяці тому +8

    Kalindo wabalalika kuno!!!!!!! This is the game of politics

  • @edsonnyasulu5394
    @edsonnyasulu5394 2 місяці тому +7

    Bwanji manganya asiye utm please

  • @JohnfosterNkusengwa
    @JohnfosterNkusengwa 2 місяці тому +4

    Restening from cape Town pa boma❤

  • @MaryNgola
    @MaryNgola 2 місяці тому +1

    Inutu ngt mumadziziwa kt ndinu a MCP ndibwino musamamvele Za born kalindo,chifukwatu tsiku lina mudzagwa ndi BP,ngt likumulephera boma nde kulibwanji iweyo????

  • @CharityMhone-uk9ym
    @CharityMhone-uk9ym 2 місяці тому

    Inenso munthu uyu ndimamudabwa akayankhula zambiri zomunena chilima pano wafa ..akuonetsa ngati iye amamkonda mmm Ada Inu mdziwen Yesu kusanade...vuto anakumanan udindo..mwamutukwana peter eeeee pano ukutinso peter ndiwabwino😮😮😮😮

  • @rashidadan2533
    @rashidadan2533 2 місяці тому +5

    Yudas anali ophunzila wa yesu , komanso yudas anamugulitsa yesu ,
    History is the best teacher .

  • @jeremiahmalikebu2393
    @jeremiahmalikebu2393 2 місяці тому

    Palibe zogulitsidwa! Zikuchitika ndi Manganya ndi propaganda ya MCP. Koma ma supporter a UTM enieni tili nganganga pambuyo pa UTM ndi Kaliati. Team iri ku MCP yo ikhale komweko

  • @ziyamporoma377
    @ziyamporoma377 2 місяці тому +3

    Iwe Kalindo zangokuvuta kkkk you’ve met your match in Jesse Kabwira…..munatumbwa kwambiri pakatipa nde pano mutsegula mmimba simunati 😂😂😂

    • @ShabaniKuswere
      @ShabaniKuswere 2 місяці тому

      Kodi Jessie Kabwira ndendani?

    • @Martinmkapangakapanga
      @Martinmkapangakapanga 2 місяці тому

      dzeru palibe

    • @GraceZumazuma
      @GraceZumazuma 2 місяці тому

      Dziko la Malawi Lili pa mavuto eeti eeeish 💔😭 which means will be in trouble forever

  • @GregoryMatambo-m6y
    @GregoryMatambo-m6y 2 місяці тому +5

    Osasunga legacy iweyo bwa

  • @DjshukulanGift
    @DjshukulanGift 2 місяці тому

    Usi ndimuthu oyipa kwambili mm ndiapo anamupereka chilima

  • @MazyYanga
    @MazyYanga 2 місяці тому +3

    My president

  • @Cee-H-Cee
    @Cee-H-Cee 2 місяці тому +3

    First to watch

    • @hot265.
      @hot265.  2 місяці тому

      Kukunyadilani
      Thanks 🙏

  • @KennedyPhiri-h9h
    @KennedyPhiri-h9h 2 місяці тому

    ❤❤ zomwe amayankhula uyu ndi zeni zeni and zikuchita kuwonekelatu

  • @OmegaChingamuka
    @OmegaChingamuka Місяць тому

    Mwati M C P ndi yazibekete 😂😂😂😂😂😂

  • @yobesaikonde6166
    @yobesaikonde6166 2 місяці тому +2

    Kalindo drama amatha go ahead we will keep roughing kkkkkk

  • @tasmania527
    @tasmania527 2 місяці тому +1

    Aise Kalindo umandiwaza ndi nthabwala zako. Please keep up the good work ya nthabwalazo- the DC mwana oopsya kwambiri kkkk. Bwanji osangonena kuti umafuna UTM ipite kwa Adadi? Come on man be honest...kodi zakuwawa eti? Nobody should be mad at Kalindo because he's a funny dude.

  • @MisheckZako
    @MisheckZako 2 місяці тому

    Dc

  • @victormbewe7462
    @victormbewe7462 2 місяці тому +1

    Let's admit that politics has become a global problem

  • @MercyHassan-p4e
    @MercyHassan-p4e 2 місяці тому

    😂😂😂😂 mukharise a president anthu anthu aanthu osauka mumatipasa chirimbikitso ndipo timakhurupirila kuti tsiku rina tidzadyera nyama ndipo dima ungakute bwanji kunja kudzawara dzuwa ridzaomba Bon karindo woyeeeeee, timakutsatani ngankhare tiri kutari ndi dziko ra malawi🇲🇼💗

  • @LashidMalindima
    @LashidMalindima 2 місяці тому +2

    Mumakwa adala

  • @NoorRasheed-re5vh
    @NoorRasheed-re5vh 2 місяці тому

    Ukufuna tiziyendela.maganizo ako ulapa

  • @daltonjafali3856
    @daltonjafali3856 2 місяці тому +1

    We salute you our president

  • @esaMoha-dm4kj
    @esaMoha-dm4kj 2 місяці тому +2

    Nkalindo bwanji mullipo mulinkut bwanj malipot andege ankushedwaso after too months guys shonde bk TV mtanyiwwa

  • @lyiemax
    @lyiemax 2 місяці тому

    Zomvetsa chisoni kwambiri, may the spirit of SKC do something on this bad move

  • @GodfrleyTembwe
    @GodfrleyTembwe 2 місяці тому

    Warira mokweza kunooooo 😂😂😂😂

  • @thulanimpphiri6873
    @thulanimpphiri6873 2 місяці тому +1

    Ngat utm inatuluka mu mcp pali chifukwa chani chovalirira makaka pa musonkhano wa mcp. Zimene zinapita kukalandira president ndi makaka a utm ndi zisiru zipanda zeru sizikuziwa kuti uku ndi kwa mcp uku ndikwa utm sizikusiyanisa. Or usi asavareso makaka a utm

  • @JohnNamakonje
    @JohnNamakonje 2 місяці тому

    True

  • @junasssabiwa1996
    @junasssabiwa1996 2 місяці тому +4

    DC

  • @YammsyZebron
    @YammsyZebron 2 місяці тому +2

    The DC great

  • @GodfrleyTembwe
    @GodfrleyTembwe 2 місяці тому

    Akalindo agwira pambali

  • @xinalungu9616
    @xinalungu9616 2 місяці тому

    UTM and Kaliati has no money to run the party.
    If MCP is funding UTM, let them help UTM an alliance partner.
    Dr. Kabambe has 50 followers in Thyolo, considering his last rally. He doesnt have money either.
    Its Utsis camp through MCP n Mary that have money.

    • @mzeewandembonyirongo2972
      @mzeewandembonyirongo2972 2 місяці тому

      Kabambe has money...only that is relatively new in politics and giving out money is not his taste. In UTM Kambala is doing everything by himself. Imagine the whole top guys beg fuel money from him. Money as less than 300, 000 kwacha. They want him to pay. They the rest are not contributing to the party. And seems Kambala is tired. He is being told kuti zabwino zikubwera soon😮

  • @MosesTchauya
    @MosesTchauya 2 місяці тому

    Ndiwe wachipani chanji iweyooo

  • @OnenessLestas
    @OnenessLestas 2 місяці тому

    Kalondo ife MCP timayikonda enafe zokamba zako sizimatisangalatsa ai

  • @PreciousDzonzie
    @PreciousDzonzie 2 місяці тому +1

    Wamisara wamisara wamisara zindikiran nose mumatsata citsiru ici kt ndiwamisala watsara pang'ono kuyamba kutora zinyatsi uyu kkkkk

    • @brightkaunda920
      @brightkaunda920 2 місяці тому +1

      Iweso ndekuti ndiwamisala bwanji ukumutsata?

  • @kondwanivyalema9449
    @kondwanivyalema9449 2 місяці тому

    Mbava zaba Chipani cha SKC

  • @MphatsoMwale-it4xd
    @MphatsoMwale-it4xd 2 місяці тому

    Kalulu mwale from jonz D C tiyenaoni ambalame amenewa

  • @LindaLimbe-fo1oy
    @LindaLimbe-fo1oy 2 місяці тому

    Ulemu wanu bwana Kalindo

  • @Martinmkapangakapanga
    @Martinmkapangakapanga 2 місяці тому

    l like u born

  • @AnnieJutta
    @AnnieJutta 2 місяці тому

    Mr DC sizokanika kung'alula apa ai popeza ndimzanu manganya nenani kuti manganya wagulitsa chipanichi ku MCP ndipo akunama kumwamba Mulungu aliko angoutsa mkwiyio wa Yehova chabe mapangano akeo ndiopusa akuganiza MCP ingakamupatseso u vice president 2025 ndi munthu omvetsa chisoni betrayer

  • @TamikaKaponya
    @TamikaKaponya 2 місяці тому

    No ways....anthu ogulidwa ndi Manganya amenewo not real SKC followers

  • @SlindiryLoveness
    @SlindiryLoveness 2 місяці тому

    Koma akalindo pumani kaye pathe mwezi umozi nkhani yikuwoneka kuti yatha mumutumo ndiye mukhale kaye cheti muzitipasa nkhani zanzeru ndiye kuti aroma alowelerepo kodi UTM ndiya roma koma munthu uyu

  • @DicksonLutere-p9k
    @DicksonLutere-p9k 2 місяці тому

    Kalindo wayamba kulila kuno imeneyo ndiye politics kkkkk

  • @ChawezChinkhuntha
    @ChawezChinkhuntha 2 місяці тому +2

    First comment ❤

    • @hot265.
      @hot265.  2 місяці тому

      Mumakwana
      Thanks

  • @JamesSingini-t4j
    @JamesSingini-t4j 2 місяці тому +5

    Kupita Ku msonkhano wa MCP doesn't mean uzavotera MCP Mr kalindo aaaaaaaaahh,,,aja anapita Ku convention ya DPP ali mu makaka a utm,afford,why smunanene kut ndi a DPP??? Nde palibe chifukwa wa utm kupita kokalandla chakwera coz vote Nd mtima nde musasegule nazo mmimba..

    • @mathewsnachuma8086
      @mathewsnachuma8086 2 місяці тому

      Maganya ayakhule za 5 years tione pomwe uziwe kut siwa utm

    • @FannyWadson-zg4oj
      @FannyWadson-zg4oj 2 місяці тому

      Inu mwaoneka kale vote yanu munama kuti ndi mtima bwanji

  • @BoscoKalua
    @BoscoKalua 2 місяці тому

    a DPP UDF UTM AFORD ndi onse enanu tengani zimene akune bon kalido seriously if not then you are finished completely and forget to be in government in 2025

  • @xinalungu9616
    @xinalungu9616 2 місяці тому

    Bwanji tinene kuti IWE CHILUNGAMO NCHAKUTI ndiwe munthu WA NSANJE kwa anthu amene si a Ku Mulanje or Thyolo.
    Correction.
    Iwe SI PRESIDENT WATHU ayi.
    I we ndi president was anthu 50 amapanga ma demo timawaona aka. Kkkkk
    NSANJE.
    KKKKKK

  • @HarryThomson-n7n
    @HarryThomson-n7n 2 місяці тому

    M matiimiliradi man

  • @GraceMbwana-y8d
    @GraceMbwana-y8d 2 місяці тому

    Amene mekuyankhulanu mukungofuna ndalama ife anatinyasa kale mtambo

  • @kingsleyhopematchaya5184
    @kingsleyhopematchaya5184 2 місяці тому

    Iweyo mesa chili a umamunyozaso lero ukhale ngati umamukonda chili a wosokoneza iwe

  • @AchinaKellz
    @AchinaKellz 2 місяці тому

    apita okha ku chikangawa ife tidangoyikonda utm but the moment they join mcp ife tonse ku dpp basi or atangura anthu 200 ife tikukawinisa dpp

  • @chimwemwenkute3839
    @chimwemwenkute3839 2 місяці тому

    Tge DC booooon kalindooooooo mwana owopsyaaa kwambiri

  • @omarajibu860
    @omarajibu860 2 місяці тому

    Dziko kuwonongeka chifukwa cha dyera, ndalama.

  • @mthelisokadambo8895
    @mthelisokadambo8895 2 місяці тому +1

    Chapompano uyuyu uyu tipita naye ku mental
    Ndale ndi choncho

  • @PaulWilly-ge1tx
    @PaulWilly-ge1tx 2 місяці тому +2

    Zoona

  • @TaweniChavulaKamwendo
    @TaweniChavulaKamwendo 2 місяці тому

    Eee

  • @MoreenSemu
    @MoreenSemu 2 місяці тому

    Aliyese akunena zakuti awina wabalalika kalindo😅😅😅

  • @GregoryMatambo-m6y
    @GregoryMatambo-m6y 2 місяці тому +2

    No logic why kuveka anthu ma t-shirt yet you know kuti ndi anu kale kkkkk . Aaaaa kulowerera za catholic Kkkk fotseki

  • @CassimMbalaka
    @CassimMbalaka 2 місяці тому

    Mulungu salakwitsa kalikose akuwoneni pokuyikani nose wokhudxiwa pa ifa ya chilima

  • @EsetaGerate
    @EsetaGerate 2 місяці тому

    ❤❤❤❤

  • @HarrietSainetStone
    @HarrietSainetStone 2 місяці тому

    😢

  • @MarkBannda
    @MarkBannda 2 місяці тому

    Kalindo, you don't have evidence you are just making pipo to fight

  • @Paworo-h5r
    @Paworo-h5r 2 місяці тому

    Awuzeni anthu azipita kumunda si nthawi yochemelela zipani iyi. Inu ndi amene mumabweletsa njala every year

  • @ElizabethMulinde
    @ElizabethMulinde 2 місяці тому

    Mmmm zabodza izoo

  • @MulowokaBlessings
    @MulowokaBlessings 2 місяці тому +1

    A DPP adadi Anu amene ananena kuti ovotera MCP amwa mutnjani KOdi amawauzao ndi a Malawi?olo ndaku Mozambique?a Kalindo misara yakulisa yendani ku Mental

  • @GraceMbwana-y8d
    @GraceMbwana-y8d 2 місяці тому

    Choti muziwe adale simuzatheka mpakana kalekale ifetinakuziwani

  • @StephenPrinceScale
    @StephenPrinceScale 2 місяці тому

    The DC😂😂😂

  • @ElesonChalemera
    @ElesonChalemera 2 місяці тому +1

    A Mr kalindo ingojoinani ndale chifukwatu mmm zomenyera ufulu zakukanilani ndithu sizikuendapo

  • @worldamazingvideoz9416
    @worldamazingvideoz9416 2 місяці тому

    Wamisala anaona nkhondo

  • @GiftMaiden-g5w
    @GiftMaiden-g5w 2 місяці тому

    Live show

  • @ephraimkadamika
    @ephraimkadamika 2 місяці тому

    No utm singathe utm yeni yeni tikuyidziwa

  • @JonathanMtambo-w6e
    @JonathanMtambo-w6e 2 місяці тому

    This. was already planned before. chilima was killed

  • @ChicoBanda-kq7py
    @ChicoBanda-kq7py 2 місяці тому

    Pitilizani bwana

  • @DumisaniMhango-e4i
    @DumisaniMhango-e4i 2 місяці тому

    Or atagula sitingavotele awa akanganya awa

  • @JimmyMhone-b5p
    @JimmyMhone-b5p 2 місяці тому

    Manganya wagulisa chipani cha UTM kung'ona

  • @bridgetmajor3646
    @bridgetmajor3646 2 місяці тому

    Ndare ndi Mabozatu

  • @macchitsulo2986
    @macchitsulo2986 2 місяці тому

    Munthu amene angavala zovala za utm koma ali wa chipani china magulu ake ali ngati iweyo the DC

  • @sauuladi6753
    @sauuladi6753 2 місяці тому

    Zakeyo

  • @MaikNkhoma
    @MaikNkhoma 2 місяці тому

    Inu munapenga palibe zazelu mungakambe

  • @moseskapelekeza8849
    @moseskapelekeza8849 2 місяці тому

    Mukuva kuwawa man

  • @MulowokaBlessings
    @MulowokaBlessings 2 місяці тому

    Akalindo zipitani chabe ku DPP uko

  • @TelinaNjanje
    @TelinaNjanje 2 місяці тому

    ⁱᶠ ⁱᵗ ˢᵒ ᵗʰᵉⁿ ᵗⁱᵏᵃᵛᵒᵗᵉʳᵃ ᵉⁿᵃ

  • @RobertMisheck-w1v
    @RobertMisheck-w1v 2 місяці тому

    Awanso mutu wamaminawo

  • @MathewKalinkhu
    @MathewKalinkhu 2 місяці тому +3

    A MCP ndi mbulidi zoona, sasiyatsa za boma ndi chipani, mai awa azitengela pa mgong'o.

    • @ziyamporoma377
      @ziyamporoma377 2 місяці тому

      @@MathewKalinkhu Inuyo mukamayankhula ntudzu mumasiyanitsa ?

    • @LukaThawe
      @LukaThawe 2 місяці тому

      Ndipo mbuli ndiyeyo

  • @isaacybanda-s6e
    @isaacybanda-s6e 2 місяці тому

    Mumatha inuyo bwana

  • @ChilindeHarry
    @ChilindeHarry 2 місяці тому

    Za chamba zokhazokha.

  • @Cee-H-Cee
    @Cee-H-Cee 2 місяці тому +2

    First to watch