Mathembelelo akhale pamutu pa onse amene anakhudzidwa ndi imfa ya a Chilima ndi anthu 9 mwadzi wawo ukhesedwe pamitu pawo omwe anapanga izi Mudzina la Jehovah's...Amen..
Mmmmmmm, koma a Bishop inu mwamaliza zonse, ndipo kumene aliko mutu waima Chakwera ndi boma lake la MCP. Tili pa mbuyo panu Bishop, osafowoka, osatopa .❤❤❤❤
Powerful massage father,mwatiyankhulira ndipo chakwera am sure wamva ndipo akudziwa kuti next year zake zada or atatani ndi manganya wakeyo mfiti zokupha zimenezi zikapume
Powerful gospel,imfa yowawa ngati ya Yesu Christu,ngati yaa Martini Aku Uganda,ngati yaa Postoli Mtima woyera WA Yesu,mutichire chisoni,a Martini Aku Uganda mutipemphelerw Ife,woyera ose akumwamba mutipemphelere ife. Kuyankhula kulalika zomveka .Amen
Mwamvatu a chakwera ngakhale mukubisa umboni anthu akutopelani poti chilungamo nchowawa kuyamba kumanga koma mwa Allah mwini chisoni ndichifundo Ali nafe Ameen mwa Allah
Powerful message,,,we silute you,,,, keep on doing this please
I hope bishop mwatumidwa ndi mulungu ❤❤❤❤
Mathembelelo akhale pamutu pa onse amene anakhudzidwa ndi imfa ya a Chilima ndi anthu 9 mwadzi wawo ukhesedwe pamitu pawo omwe anapanga izi Mudzina la Jehovah's...Amen..
Tsoka kwaiye anatengako mbali pa ifa imeneyi sazaona mdalitso Amen 🙏
Amen
Mmmmmmm, koma a Bishop inu mwamaliza zonse, ndipo kumene aliko mutu waima Chakwera ndi boma lake la MCP. Tili pa mbuyo panu Bishop, osafowoka, osatopa .❤❤❤❤
I will vote next year because of chikangawa accident witnessed by my naked eyes,rest well my handsome VP SKC
Ndpo inenso
❤ love you bro
Muli NDI ufiti
Vote vote basi
Same as me. Ndinkaseka agogo anga akamandiuza zomwe amakumana nazo nthawi ya mcp koma pano sizokuti ndukunva koma kuuona
Powerful massage father,mwatiyankhulira ndipo chakwera am sure wamva ndipo akudziwa kuti next year zake zada or atatani ndi manganya wakeyo mfiti zokupha zimenezi zikapume
Amen amen amve Mr chikangawa fiti
Tiyen tipitilize kuyatsa ma kandulo iziwapweteka daily mpaka kampen wao azakhare opanda mphamvu Amen🙏
Zoonadi❤
Ndipotu zoonadi ambuye kudziwike kuti kuli mulungu pa ifa ya athu amenewa ikhale panutu Pao ndipo china chake chichitike ndithu ❤❤
Thank You very much Bishop for the Wise Preaching,I Salute You..😢😢😢
We need this everyday. Men of God come out and preach the truth 🙏
Mawu amphavu kulakhula mosaopa munthu koma kowopa mulungu
Aaaa yes bishop watokota chilungamo uyu eshiii i lv the way he cud articulate the whole story fearlessly amidst mr chikangawa eshiii
Ine mpakana lero sindikumvetsabe kuti Biyeni anamwalira mmmmmmmmm only God knows
Zoonad
Uthenga usu ngati Chakwera sanawunve pls mutumizileni awunve.
Tony Momadi.
Johannesburg, RSA.
Powerful gospel,imfa yowawa ngati ya Yesu Christu,ngati yaa Martini Aku Uganda,ngati yaa Postoli
Mtima woyera WA Yesu,mutichire chisoni,a Martini Aku Uganda mutipemphelerw Ife,woyera ose akumwamba mutipemphelere ife.
Kuyankhula kulalika zomveka .Amen
Ambuye Mulungu odziwa kuweluza.... aweruze ndithu. MZIMU WA CHILIMA usowetse mtendere aliyense amene anatengako gawo pa infa imeneyi😢😢😢
Amen 😭😭😭😭😭
Amen and Amen🙏
No mtendere mpaka adzafa
Abig message to malawians I salute u bishop
Powerful message, wakuva wamva. Amen 🙏
Amen, that's why am proud of Catholic bishops! 🙏🙏 may his blood be like those of Martyr RIP SKC
Amen and amen, kma2 kudziwike ambuye kt mumatha
Very very powerful , may God continue giving you fearless speeches for Malawians to know the truth of God.
Amen, and powerful
SKC, may your soul rest in peace
Amen bishop🙏🏿 chatsika blood on his hands. God gonna answer our tears. Osaopa osatopa n osafooka we need better Malawi for all not za sikusinjazi
Ambuye yesu akudakitseni Fathar😢😢😢choonadi chimamasura
Amen ndipo mulungu akudalitseni Muthu uyu chilango alandila ndithu mulungu sagona
Bravo Bishop Bravo tell them..They should know that people are watching..RIP SKC 😭😭😭💔
God bless you bishop the power of message
Very powerful message indeed Ambuye akudalitseni father
Uthengawu nde ndiwankaka ndi uchi
Nkaka ndi uchi wabwino 😂😂😂
😂😂😂😂😂
❤❤❤❤ bishop anga akutetezeni Yehova choona chidzatimasula ndiye ndiinuyo abusa, a bishop, onse kuunikira anthu anu amen
Powerful words chilungamo ichi
Kuiponda fadah. Kuipatsa Fire. OSAOPA, OSAFOOKA,OSATOPA.
We love u bishop .......sitikhala chete ai paka mcp ichoke
Lord protect this pastor for us we want more of them to come out . SKC ❤
mzina la Dada nalamwana Nala mzimu utuwa . Amen.
Amen. Pastor uthenga wamveka uyu opanda chilema
Straight to the point amen 🙏 prist
Once catholic always a catholic and our tears for our vp skc will never end until justice prevail
chakwera wazimvera yekha ma umboni apose apo chakwera ndiwe chigawenga ndithu
What a powerful message 😢❤
😂😂😂😂Amen pastor and thank u for reminding us that we don't have a president 😂😂😂😂
Iiiih koma abale😂👐
Pachilungamo palibe Mantha ; osaopa .osafooka. osaopa . Koma tizafela mbendela iyiiih 👉🇲🇼🇲🇼🇲🇼
I love the Catholics they stand on the truth may God bless you all
Osawopa.... kuyankhula koma uku osawanyengelera awa aziuzidwa chilungamo evil people Ambuye achite nanu
Powerful preaching mau Amphamvu
Amen a Bishop tikulira ife Amalawi
Mwamvatu a chakwera ngakhale mukubisa umboni anthu akutopelani poti chilungamo nchowawa kuyamba kumanga koma mwa Allah mwini chisoni ndichifundo Ali nafe Ameen mwa Allah
Amen mtumiki wamulungu,chilungamo mwanena ndithu
Chakwera ndi mbuzi yachabe chabe ..ndichimunthu choipitsitsa pa zolengedwa zonse...matembelero a Mulungu,angero ,komanso onse amene amadziwa kutembelera akhale kwa chakwera oipa kwambiri😏😏😏😏😏
Our God will do it and make us move forward with grace.
Amen. Munthu wa Mulungu walalikira mopanda mantha.
Powerful message to Malawi 🇲🇼
Achita bwino kulankhula ku tchalichi,,atidyenawo akwiya kuteleku,,koma ali mbuu,,
Munthu wa mlungu wayankhula mosaopa nae ndi okhumudwa ndi IFA ya bambo Biyeni
6:52 Kulankhula mosaopa osati enawa. Amalekeza wakuphayo chigawenga kamba Koti wapatsidwa ndalama , uwu ndiye utsogoleli osati abusa ndi asheikh ena Aja aaa anangoziwikiratu Kuti akugulitsa mawu aMulungu Kwa chikangawa (chakwera) ndi ntengo wotsika mukankhanthidwa patsiku lomaliza ndipo mukasowa kothawila ndalama mubazo sizikakuthandizani chifukwa kuzakhala kulibe,
Azibusa ena mzimu ndi mphamvu za Mulungu zinawachokela kalekale angokhala zitsiru kumakalandira ndalama kwa chakwera chigawenga chouma mtima ngati chimenechi chisatana
Mmmmmm achakwera muzivere nokha akuti tilbe tsogoleri nanga inu ndindani kodi?awa akutemberelani mufune musafune simuzalamulanso dziko lamalawi
Indeed chakwera next year azipita bas
The Catholics are very powerful 🔥🔥🔥🔥
Amen,mafunso alipo nmitima mwathu ambuye okha akudziwa
Koma ndizoona izi??
Amen and amen chauta akalange azibusa ena amene a kupanga nawo katangale muboma limeneli amen
Amen
Amen " Katangaleyo olo atamapanga km ine chikundipweteka imfa ya my favorite mzimu wake uwuse mumtendere mpaka kale😭😭😭😭😭💔💔
Ndipo akawafulatile asakawamverenso chisoni
Panopa zomabisa chilungamo zinatha mau awa ndawakonda kulakira kwabwino ndithu Bishop
@@EllieMvoso zopanda nttchito
Kulalika mosaopa. Koma chilungamo chokha chokha. 🇲🇼🇲🇼😭😭😭😭😭😭
🔥🔥🔥🔥🔥 Mr Chikangawaa uveee ndithuuu
Kukhazula mosaopa esh kk
Still can't believe our Biyeni is really gone forever 😢
Amen amen ntumiki anve zimenezi oyipau nfiti
Chilima Rest well 😭😭😭😭imfa yokhumudwisa kwambili
Amen indeed 😭😭😭😭😭 timenyereni nkhondo mulungu kumwambako
I salute you bishop 🙏🙏🙏🙏🙏🙏
If there's change let's change for better Us Malawian
Awwwwwwu😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭Rest in peace Chilima
Mlalikiyu amatha go up mtsogoleri
Zandinvesa chisoni nkatolika kulilila mwana wake SKC😢😢😢😢😢😢
Amen Man of God
yes yes yes my vote will do
Koma ulaliki uwu 💯 perfect
Amen Amen powerful message ❤❤❤🎉
Uthenga wabwino n olongosoloredwa bwino ndithu.ambuye tithangatireni
Uthenga okhathamira bwino Amen
Ulemu wanu 🙏 bishop
Koma chikakagawa mene kunalili muja kuzizira mmmm kumusiya ndithu kukagona ambuye ngatidi mulipo ngatimuzabwerenso ndthu intervine your self
Amen, wakumva amve, osamva akhale?
Chibaluwa chawelengedwa kupita kwa babo chikangawa zivele mtoloooooo kuchikagawakooooo
Amen chikangawa akuva bwanji?kumene aliko munthu oyipa
No mtenderetu
Panyopako chakwera mr chikangawa fiti
Chowonadi chiwoneke abusa thank you.
Chakwera ayerekeze kupha father uyuyu.chilungamo chikuyenda ngat madzi
Chikablngawa ipangitsa kuti ena aluze Zisankho ndipo zoxhitika
Mmmgh am intoxicated with this message
Mau mau Bishop mwalaliksa ndithu
Powerful massage
Uthenga wachoka kwa mulungu live anamutumizira utsiku live live fireeeee
I'm proud to be a catholic
Uthenga uwu umufikire chakwera nimumene anamuphera chirima
Popangira vn ndipati abale amzanga?Km chikangawa chakwera wazimva izi ?SKC rest in peace 💔
Eshiiih kuswa kuswa anthu atopa ndithu
That's what we call prophecy osati ndayankhula ndi Mulungu Mulungu wake utii eeeeee aaaaiiiiii Mcp 2025 boma ndiye kutii chani??? Awaa ndiye mau
Am proud to be a Catholic