Dan Lu Ft. APM - Winanso Ayi (Official Music Video)

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 15 жов 2024

КОМЕНТАРІ • 248

  • @PromiseMartin-uu4wf
    @PromiseMartin-uu4wf 25 днів тому +24

    Ali pano ndani after kuonena nyimbo yosakoma ya chakwela chikangawa

  • @ISHMAELSHAIBU-kn4on
    @ISHMAELSHAIBU-kn4on 5 місяців тому +20

    Kunena chilungamo. Peter uja zinthu nde ankaonetsadi. Boma lililonse anayesetsa kupanga zofunika. Za kuba ndi izo koma let's see mmene Munthuyo adagwirira ntchito. Sizikufanana ndi Chakwera tu nkomwe.
    Tikafika kumbali ya nyimbo yi. Ai ndithu bwana Dan Lu katundu mudakwapula. Well talented

    • @ChimwemweRajab
      @ChimwemweRajab 25 днів тому

      Ndipo live koma manyaka awawa nde mbola

  • @siphiek6312
    @siphiek6312 5 років тому +6

    ineyo siine wa DPP. ndayesetsa kumukwiyila Dan lu kuti akuimbila za ndale, koma nyimbo iyiyi ndi maifila, beat ili bhoo.. and u r so talented Dan Lu. Koma suti ndingavotele DPP. izi zanyimbo basi.

  • @priscillachimango8962
    @priscillachimango8962 5 років тому +16

    Hate him or love him, guy is talented and give him respect for that...love the composition despite everything 😘😘

  • @BeckieMw
    @BeckieMw 22 дні тому +1

    Mtsogolo ndani??? Peter yekha 💙💙💙✅💪

  • @preciousmaononga
    @preciousmaononga 2 місяці тому +7

    Here is 2024🌈♥️♥️waiting fo 2025

  • @VanessaDaudi-xk6pr
    @VanessaDaudi-xk6pr 24 дні тому +1

    Iziii nde nyimbo 🔥🔥🔥🔥🤸

  • @HajiWhite-bp4zu
    @HajiWhite-bp4zu 25 днів тому +4

    Despite his mind of joining unnecessary party of MCP but he makes good compose hits

  • @trymoo8479
    @trymoo8479 18 днів тому +1

    Dan Lu.....still a legend

  • @williamslahman8998
    @williamslahman8998 5 років тому +5

    ife amalawi tili ndivuto losowa chikondi mmalo moti tikhale athu awumodzi vuto mkunyozana palibe yemwe adzakonzeso dziko lathu ngati tilibe chikondi tikuyenera kuyamikila pazithu zina zomwe ena akuchita ndikuwalimbikitsa kuti dziko lipite pasogolo . Dan Lu kwake mkuyamika pazithu zomwe ena apangapo kutukula dziko adzabweraso ena adzayamikila muthu paiye yekha sangakwanise kuthandiza onse mkusangalala tiyeni tikhale athu okondana kuti dziko lathu likhale chitsanzo kwa ena

  • @DEBORAHMSUZI
    @DEBORAHMSUZI 24 дні тому +1

    Tiyeni tifikitse 1 million views

  • @BridgetKanyika-r6g
    @BridgetKanyika-r6g Місяць тому +1

    Our guy is talented 100%

  • @EllasNgoma
    @EllasNgoma 22 дні тому

    Dolo katatu my artist since i was born zandale apo mwenewa amatha

  • @PatrickJemus-q8w
    @PatrickJemus-q8w 12 годин тому

    Nyimbo zbho Nd izi❤❤❤❤❤❤

  • @BlakRedGrin
    @BlakRedGrin 5 років тому +3

    Koma nyimbo umakutumula mophyesa mtima ayise..

  • @TracyMagaso-q6w
    @TracyMagaso-q6w 25 днів тому

    Tsogoleli ndani ,, Peter yekha ❤❤❤

  • @ManzyMaker
    @ManzyMaker 7 місяців тому

    Eeeh kunena chilungamo Dan lu umatha, komañso peter amatha,,, but time tells,,, zonsezo kulibe lero ulemu wapadziko uli ndi limit

    • @RuthRaphael-k2j
      @RuthRaphael-k2j 7 місяців тому

      Ndiposo zonsezi kusowa umuthu wa muthu Ali tilibe chilungamo kmaso stitha kumanga umodzi

  • @arnoldfungulani9800
    @arnoldfungulani9800 5 років тому +2

    Zilibho more fire dan lu more fire dpp APM akulamulanso mpaka 2024 wooooo

  • @dysonthindwa4697
    @dysonthindwa4697 5 років тому +2

    Big up Dan DPP Niboma ufune usafune Peter yomweyo wina alira .

  • @ChikumbutsoChikaphonya
    @ChikumbutsoChikaphonya Місяць тому

    Keep it up my brother chakwera walephela kusamala anthu

  • @EllenLwara
    @EllenLwara Місяць тому +1

    Adadiiiiii my vote🎉

  • @TalandiraMsiska-iw3qd
    @TalandiraMsiska-iw3qd 25 днів тому

    Inde iweeeeeeee Nyimbo ndi izizi💙💙💙✅

  • @JohnBanda-ux9fy
    @JohnBanda-ux9fy 24 дні тому

    Nyimbo Kawawa osati misala wayambayo Dan ..Kodi akupepetula chikangawa?

    • @WonganiTiyese
      @WonganiTiyese 24 дні тому

      Making money bro he is a musician not a politician

  • @TameeraInglis
    @TameeraInglis 7 днів тому

    Ndipo. Nyimbo zomwe zakalezi. Tiziziyika mmisonkhano avulalanazo a MCP okha

  • @mavuschitseko7757
    @mavuschitseko7757 2 роки тому +1

    Watching from Durban, apitilize ,peter, Dan Lu 🔥

  • @PetrosSamuel-rs9wk
    @PetrosSamuel-rs9wk 7 днів тому

    Ine siwandale koma nyimbo iyi anandiyimbila bwino maka paja poti undindo amapeleka ndi chauta pamandimvekela gospel gospel eeeee..

  • @sarahmugawa249
    @sarahmugawa249 5 років тому

    Zipani mbweee!!!......everyone tryna take down and pull down the other kuti akhalepo iyeyo dziko litukuka bwanji??.....mmalo mopangana support wina akakhala pampando koma mwati ayi tiipitse ameneyu asazawineso timuonele kuti zitha bwanji.. shaaaa!!!....Malawi wanga mayooo hehe

  • @Alex-vr1yb
    @Alex-vr1yb 6 місяців тому

    Nyimboyi inaimbidwa mwa luso koma the message Aaaa zanu izzo

  • @beinhardkausiwa7107
    @beinhardkausiwa7107 5 років тому +3

    Winanso ayi Ife tufuna APM basi.....chitukuko chipitirire.Bravo Dan lu

  • @smartchitimbe2450
    @smartchitimbe2450 Рік тому +1

    despite it's a political song but I have much feeling with this song well composed, good melodies, so danceable.

  • @SakinaMohammed-r8p
    @SakinaMohammed-r8p Місяць тому +4

    Tabweraso ife adad ana anu tilandireni ana osochela 2025 we're waiting for you

  • @lovenessbanda9762
    @lovenessbanda9762 5 років тому

    Hayibooo!!! no comment God will choose by himself for nobody is perfect

  • @beniekamoto8227
    @beniekamoto8227 5 років тому +5

    Udali kale Daniel Lufani iwe.....pano ndiye aaaaa ukubowa

  • @HytenStima
    @HytenStima 25 днів тому

    Iyiyi ndye munapha sound koma na ya chakwela chkangawayi mmmmm mwapepela

  • @MellissieChideru-id4ub
    @MellissieChideru-id4ub 22 дні тому +1

    Nde mwati kumenya kugwetsa 🤣🤣apa mukuti APM akhale wina ayi mukuziyendetsa bwanji kodi zikukhala bwa 👀😂

  • @LewisHudsonNkhonjera
    @LewisHudsonNkhonjera 4 місяці тому

    This song is so good really love it ❤

  • @chawingamanase4790
    @chawingamanase4790 5 років тому +3

    That’s you Dan Lufan i like your mingoli keep it up bru listening 👂 you on UA-cam all the way South Africa 🇿🇦

  • @marianyati7003
    @marianyati7003 7 місяців тому

    Big up Dan lu nakubaĺi sana sana natamani kufanya colabo na wewe

  • @LusunguMkalira1996
    @LusunguMkalira1996 25 днів тому

    Wasachisankho lakwika zowona aka joina MCP, ma hit nde amatimenyera

  • @mphatsomtoso2506
    @mphatsomtoso2506 2 роки тому

    Ineyo nyimbo iyiyi ase sinxasiya kunvera ngakhale ndili wa MCP, imandiwaxa hvy, ndipo unafatsilila, nde padxima speaker dxogunda bwino iwee

  • @leymaskeva5820
    @leymaskeva5820 5 років тому +5

    Kuyaruka Dan kusowa ma plan sopano apitara ake ati,ndalama zathu zomwezi misonkho yamthumba mwanthu zimenezo uchisiru uzakupha

    • @starmondaychikwax1277
      @starmondaychikwax1277 5 років тому

      Dan lu if u keeping hitting studio lyk diz loool.u wll lose more fans.any 1 agree

    • @brown8350
      @brown8350 5 років тому

      These are our taxes indeed man! So what is this guy saying?? Crazy man. Singing sin! ati bwana!

    • @sintasintchaya5020
      @sintasintchaya5020 5 років тому +1

      Mungoona kuti mupanga bwanji truth be told Muntharika ngwachitukuko zina kambu

    • @olivelikwaya785
      @olivelikwaya785 5 років тому

      Musova

    • @0wenNkhambule
      @0wenNkhambule Рік тому

      Muyisova pa nyasa apo Dan lu lekawaka Kuyimbila Agogo awo Anthu akuchoselapo waka mano

  • @TPSQUAREsqure
    @TPSQUAREsqure 6 місяців тому +3

    Dany lu, tinasowa nyimbo zako za kapeni tikudigila za 2025

  • @wellocenjobvuyalema6456
    @wellocenjobvuyalema6456 5 років тому +1

    Za zii,, ife pambuo pa SKC 2019 BOMAAAAAAA

  • @francisbwerera9975
    @francisbwerera9975 5 років тому +6

    bola inu mumatha kuimba,,,apapa kuteleko akupatsani ndalama (gawo la ma tax athuwa)malawi mukuimva kukomer.. ife nde tatopa ndikumangonamizidwa ndi andale!!! mtendele si msima yokha!!

  • @CeciliaKalua-g9y
    @CeciliaKalua-g9y 21 день тому +1

    🤣🤣koma ndalama guys..APM🔥

  • @Roseta0629
    @Roseta0629 20 днів тому

    At least sanafufute. Ife tizibwerabe kudzaonera nyimbo ndiyomweyi🎉🎉

  • @billiechunda8786
    @billiechunda8786 5 років тому +2

    Ayise ugwanayo mmadzi 2019 , APM palibe chochitika usogoleri sitikuuonamo ,

  • @moureenmolesi
    @moureenmolesi 10 днів тому

    boma ndi ili likubwera 2025 li dpp oyeeeee

  • @lifnetmakoka2175
    @lifnetmakoka2175 24 дні тому +1

    Zinazo ndizake koma masound onse a DPP Dan lu Anamenyaa osati za ku NGO'na zija

  • @GetrudeBanda-sd1yf
    @GetrudeBanda-sd1yf 22 дні тому +1

    Dan lu bwererani
    Ku DPP kubwerera sikupusa koma ndi chiyambi cha nzeru

  • @husnahaslam6
    @husnahaslam6 5 років тому +3

    U are number1 malawi♥♥

  • @coollovelyk314
    @coollovelyk314 5 років тому

    Akunama, ukubwera boh Dan my Brother. 😘

  • @everlardngwira2112
    @everlardngwira2112 5 років тому

    Kuziphwekesatu kumeneku! Mpaka kukunyngererani apitala?

  • @CharityJuwawo-k6x
    @CharityJuwawo-k6x 25 днів тому

    Am here from fb 😅😅😅

  • @wilsonmudaudi
    @wilsonmudaudi 5 років тому +3

    APM kasupe wachitukuko 2019 akupitiridza kutukula Malawi.

  • @Cee_Busy_Mw
    @Cee_Busy_Mw 24 дні тому +1

    Imatikumbusa patali❤🥱❤

  • @manhaj5743
    @manhaj5743 5 років тому +2

    Winaso ayi zoona Dan Lu APM yemweyo 2019 kuti moyo buuuuu

    • @ajallan7051
      @ajallan7051 5 років тому

      follow me i will follow u

    • @inuragreen7387
      @inuragreen7387 5 років тому

      Ayi zilibwino ena amene akubwelawo ndiwozaba koma pita eyemweyo basi Dan uli bcoz pali anthu ena odana ndi PETA koti ntchito yawo yodula ziwalo inayima pano

  • @EfacyNkhoma-j8h
    @EfacyNkhoma-j8h Рік тому

    We remember that time things are going well where are you peter mtalika😢😢😢

  • @WiliWili-y2d
    @WiliWili-y2d 20 днів тому

    chikangawa km kuyenda Enda bas

  • @OscarChris-jn1wo
    @OscarChris-jn1wo 4 місяці тому

    Mwalowaso bwana💪💪💪

  • @kachalaphoebe4480
    @kachalaphoebe4480 5 років тому +5

    Massive Dan Lu.. 2019 APM boma!!!!

  • @kingsleymsampha2260
    @kingsleymsampha2260 4 місяці тому

    This guy I talented sure

  • @violetpotani
    @violetpotani 25 днів тому

    APM ndi bwana di... Ndipo winanso ayi ife Dpp

  • @billiechunda8786
    @billiechunda8786 5 років тому +1

    Utm bomaaaaaa manyadzi akugwila

  • @ajilukalitendere105
    @ajilukalitendere105 5 років тому +1

    Winanso ayi dpp woyeee😗

  • @MercyNkhoma-b6h
    @MercyNkhoma-b6h Місяць тому

    Ambuye atithandize Apm abwelerenso 2025.

  • @frezarphiri6141
    @frezarphiri6141 5 років тому

    APM woyeeeeee thax Dan lu cop motomoto

  • @GodfryMasina
    @GodfryMasina 22 дні тому

    Kun ndimemeyo osat chikangawa 😂😂😂😂😂😂have

  • @winniemfunda8618
    @winniemfunda8618 4 роки тому

    Umaimba bwino mmakukonda though chipanichi smmachikonda am still ur fan hommie

  • @Jaydee-mw4
    @Jaydee-mw4 21 день тому

    My vote APM 🔥🔥🔥💯💯

  • @LewisHudsonNkhonjera
    @LewisHudsonNkhonjera 3 місяці тому +2

    Nyatwa I wish DPP can take over the government again 🔥🔥🔥

  • @Uladimbwana-fr9ev
    @Uladimbwana-fr9ev 22 дні тому

    Wasochera iwe bwelera

  • @rosemagombo359
    @rosemagombo359 3 місяці тому

    Dan lu ndi dolo❤

  • @MarthaMpausa
    @MarthaMpausa 13 днів тому

    APM MY VOTE

  • @NiccoGama
    @NiccoGama 22 дні тому

    Nyimbo koma dzimenedzi

  • @lucasnanjalla4385
    @lucasnanjalla4385 5 років тому

    Blue for ntendere kawa Bravo

  • @Chiku723
    @Chiku723 Рік тому

    Very talented man

  • @k-1985
    @k-1985 25 днів тому

    Ndiwe chi kape...

  • @ireendanbwanali3938
    @ireendanbwanali3938 4 роки тому

    Came here after Peter kuluza kkkk. Koma zoopsa

  • @lindahchisemphere9220
    @lindahchisemphere9220 4 роки тому +1

    Personally lov&love this song

  • @sarahmugawa249
    @sarahmugawa249 5 років тому +1

    Chomwe timadziwa a Malawi ndi kupanga complain basi!!!!......if you are not part of the solution you are part of the problem....osamapaka boma chilichonse. Everyone has potential to make a change......we citizens don't love our country that's y we end up cheering maiko a anzathu nkumanyoza lathu lonwe.....APM kaya MCP kaya SKC....palibe wabwino and wabwino sadzakhalapo mpaka tizaphunzile kukonda dziko lathu....Amen mpingo.....

    • @nellietsonga4609
      @nellietsonga4609 5 років тому +1

      Louder for those at the back .Mawu ndithu 😍

  • @marthamwenelupembe1188
    @marthamwenelupembe1188 2 роки тому +1

    Nice song 🔥🔥

  • @smartchitimbe2450
    @smartchitimbe2450 25 днів тому

    Well composed song

  • @rooneymaster4861
    @rooneymaster4861 5 років тому +4

    Onama iwe magamoto anatipatsa ndi dziko la China otsanamiza anthu iwe uli madzi ndi dpp yakoyo utm 2019 bomaaa

  • @PemphoMononga
    @PemphoMononga 8 днів тому

    Ineeee P yekha basi

  • @jameskavina197
    @jameskavina197 5 років тому

    Ofunika kukushuta bas , ngati ukufuna dolla
    Peza njira Ina , anthu akufa ndi njala ku mamidzi ndi peter wakoyo muli kuti

    • @tiyabanda7555
      @tiyabanda7555 7 місяців тому

      Yakhulaninso lero😂

    • @MzadziWanga
      @MzadziWanga 24 дні тому

      😂😂😂😂. Mbali yakumeneko zili pati pano mukudya katatu 🤣🤣🤣🤣 amalawi chomwe timafuna sitimachidziwa

  • @thelastship2455
    @thelastship2455 25 днів тому

    Osati manyaka watulutsa awaa😂

  • @gracekachingwe6879
    @gracekachingwe6879 25 днів тому +1

    Izizi nde umaphatu not mbwelera mwapanga zija😅😅😅

  • @waishansambo79
    @waishansambo79 5 років тому

    Big up Dan Lu tili pambuyo pa Adadi.....2019 APM,Dpp Boma.....Wina Alira..winanso ai ....peter yekha basi

  • @aubreychiphwanya7622
    @aubreychiphwanya7622 25 днів тому

    Dpp woyeeee

  • @CharlesAfiyah-m7w
    @CharlesAfiyah-m7w 25 днів тому

    A chakwera zitukuko ziwili zokha😢

  • @ShoziInoki
    @ShoziInoki 22 дні тому

    Chirungam si zachakwela zakozo ampwala

  • @jackiempulula3670
    @jackiempulula3670 5 років тому

    Nkona anakutibula anthu akuchilobwe iwe kusamva

  • @Mervic-vm8eo
    @Mervic-vm8eo 3 місяці тому

    Boma ilo❤❤❤❤🥳🥳

  • @fosterjames2985
    @fosterjames2985 5 років тому +2

    Keep it up Dan lu pitilizani zitukuko a Peter kukasungu north tikusalira kuno please

  • @michaelchibambo3832
    @michaelchibambo3832 5 років тому +2

    I like your songs Dan.......and i know that reality is that u even know the message in ur song is totally wrong palibe chomwe akupangapo mdala wakoyo. I respect his brother who did great job to Malwians and iyeso akuloza za brother wake.

  • @FannieMasese
    @FannieMasese 25 днів тому +2

    DPP my vote 🔵 🔵 💙💙💙

  • @markseniorkamoto4844
    @markseniorkamoto4844 5 років тому

    A Malawi kodi ndiliti tizaziwe Mulungu? Dan Lu akulephela kungowauzako amalawi chilungamo zoona,, boza ili lamtundu wanji abale? Sibwino koma. Am'pwetekesatu bwana wakeyu.......

    • @ajallan7051
      @ajallan7051 5 років тому

      follow me i will follow u

  • @hopekiescharley4471
    @hopekiescharley4471 25 днів тому +1

    Honestly DPP developments were real😂

  • @INNOCENTMzumara
    @INNOCENTMzumara 21 день тому

    Tikufuna Peter pano😂😂😂