Kunena chilungamo. Peter uja zinthu nde ankaonetsadi. Boma lililonse anayesetsa kupanga zofunika. Za kuba ndi izo koma let's see mmene Munthuyo adagwirira ntchito. Sizikufanana ndi Chakwera tu nkomwe. Tikafika kumbali ya nyimbo yi. Ai ndithu bwana Dan Lu katundu mudakwapula. Well talented
ineyo siine wa DPP. ndayesetsa kumukwiyila Dan lu kuti akuimbila za ndale, koma nyimbo iyiyi ndi maifila, beat ili bhoo.. and u r so talented Dan Lu. Koma suti ndingavotele DPP. izi zanyimbo basi.
Zipani mbweee!!!......everyone tryna take down and pull down the other kuti akhalepo iyeyo dziko litukuka bwanji??.....mmalo mopangana support wina akakhala pampando koma mwati ayi tiipitse ameneyu asazawineso timuonele kuti zitha bwanji.. shaaaa!!!....Malawi wanga mayooo hehe
bola inu mumatha kuimba,,,apapa kuteleko akupatsani ndalama (gawo la ma tax athuwa)malawi mukuimva kukomer.. ife nde tatopa ndikumangonamizidwa ndi andale!!! mtendele si msima yokha!!
Ayi zilibwino ena amene akubwelawo ndiwozaba koma pita eyemweyo basi Dan uli bcoz pali anthu ena odana ndi PETA koti ntchito yawo yodula ziwalo inayima pano
Chomwe timadziwa a Malawi ndi kupanga complain basi!!!!......if you are not part of the solution you are part of the problem....osamapaka boma chilichonse. Everyone has potential to make a change......we citizens don't love our country that's y we end up cheering maiko a anzathu nkumanyoza lathu lonwe.....APM kaya MCP kaya SKC....palibe wabwino and wabwino sadzakhalapo mpaka tizaphunzile kukonda dziko lathu....Amen mpingo.....
I like your songs Dan.......and i know that reality is that u even know the message in ur song is totally wrong palibe chomwe akupangapo mdala wakoyo. I respect his brother who did great job to Malwians and iyeso akuloza za brother wake.
Ali pano ndani after kuonena nyimbo yosakoma ya chakwela chikangawa
Ine
😂😂😂ine
Dun luu ndichitsilu basi 😂😂
Ndipo live
Kunena chilungamo. Peter uja zinthu nde ankaonetsadi. Boma lililonse anayesetsa kupanga zofunika. Za kuba ndi izo koma let's see mmene Munthuyo adagwirira ntchito. Sizikufanana ndi Chakwera tu nkomwe.
Tikafika kumbali ya nyimbo yi. Ai ndithu bwana Dan Lu katundu mudakwapula. Well talented
Ndipo live koma manyaka awawa nde mbola
ineyo siine wa DPP. ndayesetsa kumukwiyila Dan lu kuti akuimbila za ndale, koma nyimbo iyiyi ndi maifila, beat ili bhoo.. and u r so talented Dan Lu. Koma suti ndingavotele DPP. izi zanyimbo basi.
Hate him or love him, guy is talented and give him respect for that...love the composition despite everything 😘😘
Fact and true
Mtsogolo ndani??? Peter yekha 💙💙💙✅💪
Here is 2024🌈♥️♥️waiting fo 2025
Iziii nde nyimbo 🔥🔥🔥🔥🤸
Despite his mind of joining unnecessary party of MCP but he makes good compose hits
Dan Lu.....still a legend
ife amalawi tili ndivuto losowa chikondi mmalo moti tikhale athu awumodzi vuto mkunyozana palibe yemwe adzakonzeso dziko lathu ngati tilibe chikondi tikuyenera kuyamikila pazithu zina zomwe ena akuchita ndikuwalimbikitsa kuti dziko lipite pasogolo . Dan Lu kwake mkuyamika pazithu zomwe ena apangapo kutukula dziko adzabweraso ena adzayamikila muthu paiye yekha sangakwanise kuthandiza onse mkusangalala tiyeni tikhale athu okondana kuti dziko lathu likhale chitsanzo kwa ena
Business yako imeneyo
Tiyeni tifikitse 1 million views
Our guy is talented 100%
Dolo katatu my artist since i was born zandale apo mwenewa amatha
Nyimbo zbho Nd izi❤❤❤❤❤❤
Koma nyimbo umakutumula mophyesa mtima ayise..
Tsogoleli ndani ,, Peter yekha ❤❤❤
Eeeh kunena chilungamo Dan lu umatha, komañso peter amatha,,, but time tells,,, zonsezo kulibe lero ulemu wapadziko uli ndi limit
Ndiposo zonsezi kusowa umuthu wa muthu Ali tilibe chilungamo kmaso stitha kumanga umodzi
Zilibho more fire dan lu more fire dpp APM akulamulanso mpaka 2024 wooooo
Big up Dan DPP Niboma ufune usafune Peter yomweyo wina alira .
Keep it up my brother chakwera walephela kusamala anthu
Adadiiiiii my vote🎉
Inde iweeeeeeee Nyimbo ndi izizi💙💙💙✅
Nyimbo Kawawa osati misala wayambayo Dan ..Kodi akupepetula chikangawa?
Making money bro he is a musician not a politician
Ndipo. Nyimbo zomwe zakalezi. Tiziziyika mmisonkhano avulalanazo a MCP okha
Watching from Durban, apitilize ,peter, Dan Lu 🔥
Ine siwandale koma nyimbo iyi anandiyimbila bwino maka paja poti undindo amapeleka ndi chauta pamandimvekela gospel gospel eeeee..
Zipani mbweee!!!......everyone tryna take down and pull down the other kuti akhalepo iyeyo dziko litukuka bwanji??.....mmalo mopangana support wina akakhala pampando koma mwati ayi tiipitse ameneyu asazawineso timuonele kuti zitha bwanji.. shaaaa!!!....Malawi wanga mayooo hehe
Nyimboyi inaimbidwa mwa luso koma the message Aaaa zanu izzo
Winanso ayi Ife tufuna APM basi.....chitukuko chipitirire.Bravo Dan lu
Dpp morefire
despite it's a political song but I have much feeling with this song well composed, good melodies, so danceable.
Tabweraso ife adad ana anu tilandireni ana osochela 2025 we're waiting for you
Hayibooo!!! no comment God will choose by himself for nobody is perfect
Udali kale Daniel Lufani iwe.....pano ndiye aaaaa ukubowa
Iyiyi ndye munapha sound koma na ya chakwela chkangawayi mmmmm mwapepela
Nde mwati kumenya kugwetsa 🤣🤣apa mukuti APM akhale wina ayi mukuziyendetsa bwanji kodi zikukhala bwa 👀😂
This song is so good really love it ❤
That’s you Dan Lufan i like your mingoli keep it up bru listening 👂 you on UA-cam all the way South Africa 🇿🇦
Big up Dan lu nakubaĺi sana sana natamani kufanya colabo na wewe
Wasachisankho lakwika zowona aka joina MCP, ma hit nde amatimenyera
Ineyo nyimbo iyiyi ase sinxasiya kunvera ngakhale ndili wa MCP, imandiwaxa hvy, ndipo unafatsilila, nde padxima speaker dxogunda bwino iwee
😂😂😂
Kuyaruka Dan kusowa ma plan sopano apitara ake ati,ndalama zathu zomwezi misonkho yamthumba mwanthu zimenezo uchisiru uzakupha
Dan lu if u keeping hitting studio lyk diz loool.u wll lose more fans.any 1 agree
These are our taxes indeed man! So what is this guy saying?? Crazy man. Singing sin! ati bwana!
Mungoona kuti mupanga bwanji truth be told Muntharika ngwachitukuko zina kambu
Musova
Muyisova pa nyasa apo Dan lu lekawaka Kuyimbila Agogo awo Anthu akuchoselapo waka mano
Dany lu, tinasowa nyimbo zako za kapeni tikudigila za 2025
Za zii,, ife pambuo pa SKC 2019 BOMAAAAAAA
Nde iti imeneyi
Congratulations
bola inu mumatha kuimba,,,apapa kuteleko akupatsani ndalama (gawo la ma tax athuwa)malawi mukuimva kukomer.. ife nde tatopa ndikumangonamizidwa ndi andale!!! mtendele si msima yokha!!
Awapatsako za cash gate
Zako zimenezo
Apa akudyanso zina ndithu,, kudyera luso
🤣🤣koma ndalama guys..APM🔥
At least sanafufute. Ife tizibwerabe kudzaonera nyimbo ndiyomweyi🎉🎉
Ayise ugwanayo mmadzi 2019 , APM palibe chochitika usogoleri sitikuuonamo ,
Mbola
boma ndi ili likubwera 2025 li dpp oyeeeee
Zinazo ndizake koma masound onse a DPP Dan lu Anamenyaa osati za ku NGO'na zija
Kuja akukakamiza ndie fundo. Zikusowa
Dan lu bwererani
Ku DPP kubwerera sikupusa koma ndi chiyambi cha nzeru
U are number1 malawi♥♥
Akunama, ukubwera boh Dan my Brother. 😘
Kuziphwekesatu kumeneku! Mpaka kukunyngererani apitala?
Am here from fb 😅😅😅
APM kasupe wachitukuko 2019 akupitiridza kutukula Malawi.
Imatikumbusa patali❤🥱❤
Winaso ayi zoona Dan Lu APM yemweyo 2019 kuti moyo buuuuu
follow me i will follow u
Ayi zilibwino ena amene akubwelawo ndiwozaba koma pita eyemweyo basi Dan uli bcoz pali anthu ena odana ndi PETA koti ntchito yawo yodula ziwalo inayima pano
We remember that time things are going well where are you peter mtalika😢😢😢
chikangawa km kuyenda Enda bas
Mwalowaso bwana💪💪💪
Massive Dan Lu.. 2019 APM boma!!!!
This guy I talented sure
APM ndi bwana di... Ndipo winanso ayi ife Dpp
Utm bomaaaaaa manyadzi akugwila
mulipobe? ndi tonse yanuyi?
Winanso ayi dpp woyeee😗
Ambuye atithandize Apm abwelerenso 2025.
Kwambiri kwake
APM woyeeeeee thax Dan lu cop motomoto
Kun ndimemeyo osat chikangawa 😂😂😂😂😂😂have
Umaimba bwino mmakukonda though chipanichi smmachikonda am still ur fan hommie
My vote APM 🔥🔥🔥💯💯
Nyatwa I wish DPP can take over the government again 🔥🔥🔥
Wasochera iwe bwelera
Dan lu ndi dolo❤
APM MY VOTE
Nyimbo koma dzimenedzi
Blue for ntendere kawa Bravo
Very talented man
Ndiwe chi kape...
Came here after Peter kuluza kkkk. Koma zoopsa
Personally lov&love this song
Chomwe timadziwa a Malawi ndi kupanga complain basi!!!!......if you are not part of the solution you are part of the problem....osamapaka boma chilichonse. Everyone has potential to make a change......we citizens don't love our country that's y we end up cheering maiko a anzathu nkumanyoza lathu lonwe.....APM kaya MCP kaya SKC....palibe wabwino and wabwino sadzakhalapo mpaka tizaphunzile kukonda dziko lathu....Amen mpingo.....
Louder for those at the back .Mawu ndithu 😍
Nice song 🔥🔥
Well composed song
Onama iwe magamoto anatipatsa ndi dziko la China otsanamiza anthu iwe uli madzi ndi dpp yakoyo utm 2019 bomaaa
Can we sit down and laugh together now?
Ineeee P yekha basi
Ofunika kukushuta bas , ngati ukufuna dolla
Peza njira Ina , anthu akufa ndi njala ku mamidzi ndi peter wakoyo muli kuti
Yakhulaninso lero😂
😂😂😂😂. Mbali yakumeneko zili pati pano mukudya katatu 🤣🤣🤣🤣 amalawi chomwe timafuna sitimachidziwa
Osati manyaka watulutsa awaa😂
Izizi nde umaphatu not mbwelera mwapanga zija😅😅😅
Ndipo mbwelera😂 or mwana akuseka
Big up Dan Lu tili pambuyo pa Adadi.....2019 APM,Dpp Boma.....Wina Alira..winanso ai ....peter yekha basi
Dpp woyeeee
A chakwera zitukuko ziwili zokha😢
Chirungam si zachakwela zakozo ampwala
Nkona anakutibula anthu akuchilobwe iwe kusamva
Boma ilo❤❤❤❤🥳🥳
Keep it up Dan lu pitilizani zitukuko a Peter kukasungu north tikusalira kuno please
I like your songs Dan.......and i know that reality is that u even know the message in ur song is totally wrong palibe chomwe akupangapo mdala wakoyo. I respect his brother who did great job to Malwians and iyeso akuloza za brother wake.
Koma Chakwera okweza zithuyuu aaa mbola
DPP my vote 🔵 🔵 💙💙💙
A Malawi kodi ndiliti tizaziwe Mulungu? Dan Lu akulephela kungowauzako amalawi chilungamo zoona,, boza ili lamtundu wanji abale? Sibwino koma. Am'pwetekesatu bwana wakeyu.......
follow me i will follow u
Honestly DPP developments were real😂
Tikufuna Peter pano😂😂😂