Ku UTM Kuli Ana Pa Ndale (Lyton Mangochi Response) - Mzika Yokhudzidwa
Вставка
- Опубліковано 21 жов 2024
- On Nyasa VoiceBox, a concerned citizen, in response to Lyton Mangochi's claim that Michael Usi is not a true member of UTM, said that UTM is full of amateurs in politics.
Ku Nyasa VoiceBox, mzika yokhudzidwayi, poyankha Lyton Mangochi yemwe adanena kuti Michael Usi si membala weniweni wa UTM, adati UTM ndi yodzaza ndi anthu osachita ndale.
#malawi
Very good speech bwana ziuzeni zitsiru izi zikusokoneza Malawi
Aaaaah uyuso ndi Gwape weni weni za Michael Usi nchimodzimodzi Nankumwa
Inuso Pitani uku mapwala anu ndi usi wakoyo nonse
Pitani kù Dowa muzikalimba mbatata
Zaziiiiiii!
Nthumwi za Dr Chikangawa iziiii😢 Ziphe ndithuf
Zaziii Lyton Mangochi akukamba zowona, Iwe ndiye wabodza
Ndiwe galu kwabasi ndinu amene mukusakisa Malawi
Mumamynyoza ku Tonse alliance panondiye muziyankhula zausiru
Akulu tamva mwayankhulazo za nzeru nzochepa 1 Kyton mangochi sanalakwitse 2 sizikukufunika unboni kuti USI ndi wanu wa MCP 3 mukati mu ku UTM kuli ana pa ndale ndichifukwa chake tinachikonda motsogozedwa ndi malemu inuyo khalani ndichipani cha magogocho 3 president wanuyo alipamenepo chifukwa UTM 4 mwati mumuza manganya njomba zoti agwetse kaliyati tikudziwa kare ndizinene mukuchita simukudziona kupusa nokha 5 paja ndale zanu mumapanga usiku anthu osayamuka basi ndilekere pompa ndingaononge
Iwenso ukuyankhulawe ndi wa Mcp ngati ukumufuna Usiyo ingomutenga ndi chani chomwe chikuonesa Usi kuti ndi wa Utm
Usi chisankhidwire u Vice president sanapangisepo msonkhano ndiliti anapitapo koyasa makandulo umuuze Usi kuti asasokoneze utm
Kape iwe ndiwe wa MCP
Mzika imenei imatha kulankhula mafumu amenewa
wopusa kwambili mkunama wovota ngati ndiwe wekha ngati ndife anthu inuyo ndimene mwampha mramu wathu inu wopusa ife zikutiwawatu muribeso ndiuremu poyankhura popanda sauros bwezi mutauwona mpandowo muziyamika ndarama ndiweyo zikupeteketsa ndikuuzatu sitinapusetu
Kabembe akhale VC wa usi
Iwe mchewa aaaaa ukutani apa kalowe kudambwe ukavale 😂😂😂 kadzole manyi uko shaaa
Ana ????? Tiyeni tithamangisane tione atawine....
Manganya usiye kusokoneza Utm Usi ndi wa mcp
Akuchita kumveka kuti ndi mchewa munthuyu. Kodi anthu a MCP zikukhuzanitu kwambiri kutuluka kwao ku alliance 🤣
Mwalira man
Useless government
Nchoka iwe wa MCP mbuz ya munthu🤣🤣
Tatopa ndi boma la old school
Koma ndiwe galu kobasi,ndimaona ngati ukuyankhula zanzelutu koma ndiwe galu mbuziwe ndipo sudziwa kanthu ndi Michael usi wako yemweyo.
Chilima anapanga mistake kusankha usi kukhala vp sanaziwe kuti ndi udasi.ndichimozimozi azibusa wome anasainira mugwirizana wa mcp ndi utm chilima sanaziwe kuti azibusawo akumugulisa pano azibusa wo abisala chilima atafa.usi apange chake chipani asiyire anawo vuto palibe . And iwe usachuluke zeru amene anayamba ndale zolakwika ndi ndani ndimayesa ndinu mcp
Chigule ichi hiyaa😂😅
😂😂😂 kufuna ndalama iwe a usi apanga chani pamaliro achilima lero akale dolo zoona
Kkkkk Ku utm kuchitika zomwe zinachita Ku DPP ndithu amalawi timaiwala msanga tiyeni tiwaonela akaliyati ndi anjawala
Ndipo iwe ulibe zina nyani iwee
Galu iweyo wamva usalimbane ndi Peter muthalika musiyeninso mangochi chilungamo chiziwike mesa
Ngakhale anapiye amadziwa amayawo pakati pankhuku zambiri.
Uyu ngwa mcp.uku ndikulira alliance yathapo basi.
Iwetu ungovutika. Walowerera zakubanja laweni 😂
Tamajamani za ku MCP kwanu konko man.zaugalu eti
Iweyo ndiwe chitsiru tsopano palibe chomwe ukunena
Ife sitili mbali yanu pangani ZANU basi isiyeni UTM yomwe inawinisa MCP ndipo ikuchoka final. Umva mmbebe iwe.
Ati bungwe la agra 😅😅😅😅😅
Dzingodyani ndalama za blood zo
Manganya siwa utm ndiwa mcp we all know about that
Mcp imadziwatso mulungu
Iwe mbuzi iwe machende ako PA umunthu wake uti iwe zoti usi ndamene amanena maboza ukuona ngat sitikudzea
Kagwere iwe ingodya banzai umwere basi zatha
Iwe ndiwe opepera kwambiri. Anthu akudziwa kuti utm ndiyiti
Ukuziwa chani pandale iwe wa nyau! Chomene umaziwa ndi kuwunika mbewa
Iwenso ndi kape machende ako ndi abambo ako
Mani manyi anu ndi layton wanuyo mulila simunati khaya mwachita kupangana mulila fwiiiiiijnyooooooooo
Machende Ako ndi Chakwera wakoyo
Mutu wankhani muziyika ogwilizana ndizomwe munthu akufotokoza,sono apa sindinamvepo zoti a utm ndi anatu
Usi ndi chisilu iwe nawe iwe
Iwe nfichisilu kwambili nofu a MCP ndi utm anapasa zake nofu ndindani galu iwe
Nyasa Box mukutiyimilira
Gulu iwe Chikangawa wa MCP choka lwe
Aaaa palibe zimene ukuyankhula iwe
Kodi mwadya zingati?
Tikutsikani mukapitiliza kuponya izizi
Iwe NDIwe chikangawa galu wamunthu
Inu omdala mukumveka ngati ochewa okulilongwe ..mukudziwa kuti game yagona apa kuti kuturuka kwa UTM chanu kulibepo mCp agalu inu
Golu
MCP member usatinyanse kagwereko
Fisi iwe garu kwabasi
Osewo sangamake kwa usi angozivuta usi ali ndikuthekera kopanga chilichose ndipo ali ndi sapoti
Mawu
Yooo uyakhuluma lo bhuti
😂😂😂😂😂😂
Iwe ukuyankhulawe uli chisiluso kwambili wamva
Achewa okumba
Ndichitsiluchamunthu chosadziwakulankhula chilimawanzuzidwakwambili mu mcp ndindaniemwesakudziwazoti mcp yaphawanthu 10 kuyambilalelo abamboinu nzimuwa mulungukuloweni mutilankhulitsapambali ufunakunenakuti potianthu ambiliamamwalila imfayachilima tisaiganizile pepa mkuluwanga masomphenyaakulankhulaulibe uchepetse kutamikila mcp please
Chakwela wamupha chilima zasala zosatila Zach
ankakhara kuti ndimunthu wachikondi usi bwezi anawonesa mphavu pamariro azake anapangapo chani kufera ndarama zo unena chani wopenga iwe usiyo ndiwanu ife wathu ndi mayi kariat wamenya nkhondo yayikuru kwaife takubanja or kuchipani mkungo rubwa rubwatu muzayakatu tikazayamba kuwurura zose dikira mzawona anthu wopusa inu
And kangati utm ngati yabalalika iwe chikukhuza chani mutenge usiyo akhale kumbali yako vuto palibe ndi anthu amene ali kutigeranji ko apa tikupanga za utm osati tikuferanji.
Iweyo wunena apaxi ndi za satanic kuyenda njomba yake yiti zakupha anthuzo ngati momwe munayedzekera Chilima?
Inus nde palibes bwanj pamenep nde mwat mwakambap chan zikuvutan tangodikilan
Bvuto kumalawi ndiumbuli umbuli sizinthu ai chipani chimakhala ndi malamulo koma amalawi umbuli umabvuta kwambili
Achitsiru awa angopanga phokoso basi,sukuona kuti mbuzi yako chakwela ndiye akuzuza Malawi ndi chipani chake chokupha ichi
Ndwe galu wa munthu.munthu wakupha iwe.Njomba imene ikuenayo ndye it? Njomba yakupha,chipani chanu MCP chakupha.mulungu azakulangani inu.
Kape wa mcp
Mwana wa chikangawa usatinyaseso apa mumamudziwaso mulungu inuyo Ana oyipa inu.
Tudikira convention kuti manganya abwere kwao kwa Dr. Chikangawa
marlllll
Iwe ndi MCP yakoyo kagwere uko madevils
kodi iwe wawonekeratu kuti wakupasa ndarama zambiritu wosiya moyo sakuziwika ifeyo tikurira mariro ukunama iwe murungu simunthu ariyese ndiwakufa basi ukuyankhura mopusa kwambili
Iwe mapwara anu abambo inu usi anga gwese ndani garu iwe
Iwenso ndiye galu wa munthu ulibe mzeru chakwera ndi emwe anapha chilima kaliati sakufuna u pulezidenti muliradi muonadi
😂😂😂😂😂😂😂😂😂
Aaaaaaaaa iweeee chitsiru iweeee mpatse masamuwo tione amneyo sangawine amneyo iwee opatsidwa ndalama uzingodya ndalamazo
Mwayamba chibwibwi litilo?
Tandipaseni number yake uyu
usiyo anapangapo chani pamariro athu amangodikira u vp basi pari zeru apo munthu wachikondi sasowa mwasewera game yopusa mzayaruka tiyeni nazon
Chokani apa mukudya nawo ndrama za boma inu, ngati mukuti SK anawalako nofu chifukwa cha chakwela iyeyo chakwelayo waima kangati payekha osawina? Agalu inu kagweleni uko
Uneyo ndikupempha autm kuti mukamatukwana ausi mukuyenela muzisuzumila malamulo achipani chanu kuti kodi akuti bwanji ndipo musamale patsogolapa usi akhoza kukhala bwana wanu manyazi adzakugwilani ndiye samalani anjalwala komaso akaliyati
Iwe mcp inawina khamba ka chilima what are you talking about
Galu iwe wa nyau panga zako za mcp mbuzi zikukhuzani ndi chani machende