APM Sanaluze Zisankho Mu 2019 Ndi Mu 2020 - Innocent Mutholo

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 20 вер 2024
  • On Nyasa VoiceBox, Innocent Mutholo, says that in his opinion, when he analyses the number of votes cast for APM in 2019 and 2020, APM won the election free and fair.
    Pa Nyasa VoiceBox, Innocent Mutholo, wati malinga ndi maganizo ake, pamene amasanthula mavoti a APM mu 2019 ndi 2020, APM adapambana pachisankhocho mwaufulu.
    #malawi

КОМЕНТАРІ • 106

  • @TrizaGeorge-q8w
    @TrizaGeorge-q8w 4 місяці тому +15

    Apapa chofunika tilape mulungu akhululukile Malawi chifukwa chakwela akadapanda kulamulila dziko la Malawi dziko la Malawi kukanakhala khondo yoopya chifukwa athu amafuna chakwela kwambili ndipo mulungu adalola kuti ateteze Malawi kusakhale khondo koma chakwela alamulile kuti athu adziwe kuti sakwela si muthu oyenela kutumikila dziko ndipo amaene amafuna chakwela aona okha kuti chakwela si muthu

  • @isaaczuze
    @isaaczuze 4 місяці тому +5

    Uku ndiye kuyankhula kwenikweni kwas chilungamo .....
    Mr game changer ayi ndithu mumaziwa kuyankhula kwambili

  • @user-te3ps3kf2t
    @user-te3ps3kf2t 4 місяці тому +2

    Very true,amalawi avutika mokwaila,chifukwa cha adindo anjiru,mwaona zimene amapanga Mulungu, disorganized of Ministers chifukwa mulungu anakwiya,zonsezo Mulungu akuona,tionana 2025 sitilola zopusa zilizonse kudzikolanthu la Malawi

  • @paulbanda9638
    @paulbanda9638 4 місяці тому +2

    I by myself personally I agree with this man, game changer he is 100%right, anaba boma a tonse alliance,

  • @MorrisMapiri
    @MorrisMapiri 3 місяці тому +1

    50+1 must be abolished

  • @PhilipMatolino
    @PhilipMatolino 4 місяці тому +2

    Im agree with you game changer

  • @PatrickGonagona
    @PatrickGonagona 4 місяці тому +2

    Zoonad kwambiri Mr. Gama changer💪💪

  • @marryphili5419
    @marryphili5419 4 місяці тому +3

    Koma chakwera mulungu akuwone Malawi panopa wukuvesa chisoni Kuti wudye mavuto okhaokha

  • @yohanedaudi1740
    @yohanedaudi1740 4 місяці тому +2

    Very true

  • @FelixMatebule
    @FelixMatebule 4 місяці тому

    Uku ndiye kukamba Mr game changer continue fighting for Malawi, Malawi open your eyes

  • @MikeTheu-ic2dt
    @MikeTheu-ic2dt 3 місяці тому

    ❤❤❤❤❤ zowona DPP Vot kujoni Kuno kwatopesa mwina tingabwere kwa2

  • @ErustusPhiri
    @ErustusPhiri 3 місяці тому

    Come on Brother man game changer.

  • @SuzgoDhlamini
    @SuzgoDhlamini 3 місяці тому

    I agree with you Game changer🎉

  • @User_n6-8n
    @User_n6-8n 4 місяці тому +1

    God remember us🙌🏾

  • @ibrahmdoka7486
    @ibrahmdoka7486 4 місяці тому +1

    Manyaka aboma...mbuli zenizeni zankhanza

  • @spargomw
    @spargomw 4 місяці тому +2

    Ma Judge aku Malawi ndi adyera, amagwira ntchito akuyang'ana Umphawi wawo😂😂😂😂😂. Alipo oweluza wa Chilungamo ndiye Mulungu basi.Ma judge nawoso akayankha Milandu pamaso pa Mulungu.Kazilandiran ndithu ma Envelope'wo nd zomwe zikakhale Mboni zanu kumwamba

    • @timothymhone2340
      @timothymhone2340 3 місяці тому

      Ngwira tnchito akupasa ndalama msatiputsitsepo apa

  • @RaymondKaumba
    @RaymondKaumba 2 місяці тому

    Opusa ndiwe everywhere in the world in elections ldentity is a must.
    Ma demo ukapanga wekha

  • @Edwardtolo
    @Edwardtolo 3 місяці тому

    Chulungamo ukuyenda ngati madzi okumva wamva osamva asamve ndipo tikumvutika kwambiri kuno ku malawi chifukwa cha MCP Chakwera Chakwera ndi Chilima UTM 😢😢😢 Abuye chitanawoni anthu amenewa

  • @ivychithyoka1551
    @ivychithyoka1551 3 місяці тому

    And God remains big judge even if earthly judges rule otherwise

  • @AlexBilliat
    @AlexBilliat 4 місяці тому +2

    Tikufuna anthu ngati inu

  • @Ljk-k4g
    @Ljk-k4g 3 місяці тому

    Keep it up brother

  • @juliochiwalo
    @juliochiwalo 3 місяці тому

    Ngakhale mayi Jane Ansah anenanso kuti APM ndi amene anawina ndipo chisankho chinayenda bwino

  • @hanifahmponda8711
    @hanifahmponda8711 4 місяці тому

    God bless you malawi wafika pa Zimbabwe lelo 2025 kumvota no ID ngati akufuna dzimenedzo polembetsa mamvoti popo pakakhale elembetsa ma ID chilinga aleyetse atsalephele kumvota chifukwa cha alibe ID dzikalepheka apo bolani vote ilepheleke adzilamula popanda kumvota kutsiyana kuti atibele tikuwona Maso anthu alephela chimene akufuna adzilamulilbe chiyani kuwopa mulandu bwanji

  • @YasinMusa-ym8lp
    @YasinMusa-ym8lp 4 місяці тому

    Kunena soona malawi wata boma lamalawi rochimtisa manyasi chivukwachani kumalawi kukukanika 🇱🇾😭

  • @chifundocharles2348
    @chifundocharles2348 3 місяці тому

    That judgement was not fair indeed

  • @LembeniMtenje
    @LembeniMtenje 4 місяці тому

    Zowona big brother 🙏💕♥️

  • @chrischiwere7279
    @chrischiwere7279 4 місяці тому +2

    Zoonadi zolanda

  • @WitnessMaulidi
    @WitnessMaulidi 3 місяці тому

    Osawopa Bwana tili nanu

  • @ENNOCHHILL
    @ENNOCHHILL 3 місяці тому

    Totally true

  • @user-te3ps3kf2t
    @user-te3ps3kf2t 4 місяці тому

    True,

  • @LovemoreSalima
    @LovemoreSalima 3 місяці тому

    Ndizoona. Anaberadi

  • @ivychithyoka1551
    @ivychithyoka1551 3 місяці тому

    Gooooio !!!!!

  • @MonicaChunga-wg6xz
    @MonicaChunga-wg6xz 3 місяці тому

    Mutichitire chifundo mulungu pautsogoleri uwu

  • @ChifundoNinje
    @ChifundoNinje 3 місяці тому

    💪💪💪🔥🔥🔥

  • @MaxonKambazithe
    @MaxonKambazithe 3 місяці тому

    Achule awa achoka basi tizikavota ngati amalawi zoona ndithu

  • @FranklinNdovi
    @FranklinNdovi 3 місяці тому

    Two blind persons can not lead each other properly for both of them are unable see what is ahead of them.

  • @LivielMabvuto
    @LivielMabvuto 3 місяці тому

    Kwambiri kwake aliyenxe amadziwa kut APM anawina

  • @ENNOCHHILL
    @ENNOCHHILL 3 місяці тому

    Alekeni athana okhaokha a tonse alliance wo. Ayamba kale.

  • @StevenLeoJana
    @StevenLeoJana 4 місяці тому

    Amen

  • @TracyZiyaya-nz4pd
    @TracyZiyaya-nz4pd 3 місяці тому

    Maka maka chilima mulungu athane nawe ndipo unapanga zonyasa kwambiri ku dziko lino lamalawi

  • @IssaKapalamula
    @IssaKapalamula 3 місяці тому

    Munthuyo ndi sapota wa dpp, ndiye mukuona ngati anganene za nzelu?

  • @BistonNjobvu
    @BistonNjobvu 4 місяці тому +1

    Koma antnhu amaziwa kutsata nkhani

  • @DavidPhiri-o6w
    @DavidPhiri-o6w 3 місяці тому

    Kodi APM , mukunena galu wakupha ma albinos ndi kuba ndi chisale

    • @DIRECTORJARVMACK
      @DIRECTORJARVMACK 3 місяці тому

      Mukuganiza ngati mwanatu mesa achakwera amamufufuza sanamupedze ndi mulandu uliwose

  • @EmmanuelGasiten-fo5dr
    @EmmanuelGasiten-fo5dr 3 місяці тому

    Mulungu awalange ma Judge amenewa.

  • @RaymondKaumba
    @RaymondKaumba 3 місяці тому

    Pitani ku court .mbuzi
    Iwe .
    Kulira kwa mbuzi

  • @MaxonKambazithe
    @MaxonKambazithe 3 місяці тому

    TIZALOWA AMBIRI PAMSEU

  • @ErustusPhiri
    @ErustusPhiri 3 місяці тому

    MCP, yawonga zambiri.

  • @ShaffiMilias
    @ShaffiMilias 4 місяці тому

    Fire 🔥🔥 plus 💪💪

  • @ivychithyoka1551
    @ivychithyoka1551 3 місяці тому

    Eeeeeeee Apm anaberedwa

  • @NicholasJames-cb7du
    @NicholasJames-cb7du 4 місяці тому

    Big man bwanji simutumiza ma audio a dj munyanane pepani ngat ndalakwisa kufusa

    • @nyasavoicebox
      @nyasavoicebox  4 місяці тому

      Simukulakwitsa tiyesela tiziponya mungoti tipatsa ka mpata pang’ono

  • @JosephMwambe-rz2oy
    @JosephMwambe-rz2oy 3 місяці тому

    Zoona zimezo

  • @Kradle-h4o
    @Kradle-h4o 3 місяці тому

    Zen zen

  • @RaymondKaumba
    @RaymondKaumba 2 місяці тому

    Ukubisala chani
    Kuwola mmkamwa

  • @uchizJoelMumba
    @uchizJoelMumba 4 місяці тому

    Ndiye ngati ukulimbana ndi majaji mbale wanga ndi dpp yakowo mulipamabvuto ndithu amene akutumawo akupweteketsa mbale wanga

  • @HevenChiwaya
    @HevenChiwaya 4 місяці тому

    Kodi monse munayambila muja kuti mupita pa mseu muzapitapo liti pomwe zinthu zikupitilila kuwonongeka???

  • @RaymondKaumba
    @RaymondKaumba 2 місяці тому

    Mfiti ndiwe

  • @amiduclement2142
    @amiduclement2142 3 місяці тому

    Kodi ku mcp kuribe wina wazeru

  • @Chiso2019
    @Chiso2019 4 місяці тому +1

    A munthalika amagona kwambili that's why analandidwa dziko....nanuso mukuyankhula kwambili koma action zilo

    • @ShabaniKuswere
      @ShabaniKuswere 4 місяці тому

      Kupewa sikupusa anapewa nkhondo

    • @TrizaGeorge-q8w
      @TrizaGeorge-q8w 4 місяці тому

      Ndipo ndizoonadi mulungu samalakwitsa amafuna athu amuone chakwela kuti si muthu oyenela kutumikila Malawi

    • @ibrahmdoka7486
      @ibrahmdoka7486 4 місяці тому

      Umafuna Peter apange nkhondo mbuziwe

    • @ibrahmdoka7486
      @ibrahmdoka7486 4 місяці тому

      A judge amenewo tidzawamanga

    • @SolomonNjolomole
      @SolomonNjolomole 4 місяці тому

      Kuyankhula kwabwanj uku mumafuna ayambitse nkhondo?

  • @ivychithyoka1551
    @ivychithyoka1551 3 місяці тому

    Speak Game changer!!!!!?

  • @phillipstamaley7901
    @phillipstamaley7901 3 місяці тому

    Chakwela woyeeee mcp m'paka 2063

  • @MonicaChunga-wg6xz
    @MonicaChunga-wg6xz 3 місяці тому

    Chitsime chakudya chimaoneka chikaphwa

  • @Homeofpeace321
    @Homeofpeace321 4 місяці тому

    Panopa MCP yayamba kuchotsela masiku, DPP yayamba kuwengela masiku

  • @BertharrySecurity
    @BertharrySecurity 4 місяці тому

    Chilungamo chimawawa,Koma mnthu wayankhula chilungamo uyu.

  • @paulbanda9638
    @paulbanda9638 4 місяці тому

    Chi christu nthawi zina sichiri bwino, a chakwera ndi a khristu, zikuchitikazi ndi panichimeti kwa amalawi onse, chakwera ndi tonse alliance ndiakuba anaba boma kuli ndalama kukhala bwanji

  • @HassanMufase
    @HassanMufase 4 місяці тому

    MA judge pawo pawo ndthu

  • @MasiyeDayton
    @MasiyeDayton 4 місяці тому

    Kkkkkkk game change ❤

  • @SolokingChimzy-yt7dj
    @SolokingChimzy-yt7dj 4 місяці тому

    Chakwela Ali ngat Hule wa pa saloon yemwe amazazionesa ngt munthu wabwino koma Ali ooopsa kuposa hule yemwe Ali ku Bar

  • @GanieAlidih-gu7no
    @GanieAlidih-gu7no 4 місяці тому

    💪🏼💪🏼💪🏼💪🏼💪🏼

  • @BensonMalaulo
    @BensonMalaulo 4 місяці тому

    Mumakwana Mr game changer

  • @SALIMASSAN-vr8ld
    @SALIMASSAN-vr8ld 4 місяці тому

    Ndip iwey ulem wak srs chilungam chikuveka bwin kwambir

  • @MiddayDeleza
    @MiddayDeleza 4 місяці тому

    Mulungu akuwona zonsezi tsiku la 40 lidzawakwanila anthu amenewa

  • @LilianKachala-yz2xf
    @LilianKachala-yz2xf 4 місяці тому

    Mau Amphamvu ngati amenewa tamva ndithu

  • @gladysbonongwe1038
    @gladysbonongwe1038 4 місяці тому

    Dzuka Malawi dzuka

  • @gladysbonongwe1038
    @gladysbonongwe1038 4 місяці тому

    Majaji ndi amene ayika amalawi pamoto

  • @RaymondKaumba
    @RaymondKaumba 3 місяці тому

    Galu iwe

  • @marryphili5419
    @marryphili5419 4 місяці тому +1

    Malawi panopa akuvesa chisoni machine opanga mapassport sakugwira ntchito panopa machine wopangira ma ID akuvutaso Koma chakwera wuziwe komwe wuliko Kuti wulamuliro wako ndi mulungu yemwe ndiwokwiya ndi iwe

    • @SolokingChimzy-yt7dj
      @SolokingChimzy-yt7dj 4 місяці тому

      kkkkkkkk......Nebukadinezera uyu

    • @DIRECTORJARVMACK
      @DIRECTORJARVMACK 3 місяці тому

      Ku Lilongwe kuli machine 8 opangila ma id pomwe ma district ena ndi zero

  • @uchizJoelMumba
    @uchizJoelMumba 4 місяці тому

    Galu wa dpp kulila mobangula ndiye sunati ukanalila mcp 2025 boma kale

    • @mafukenimasangwi5487
      @mafukenimasangwi5487 4 місяці тому

      Dzinazi osamatengela kut bambo anu anali a mcp kapena a dpp koma kumaona kut nziko mwathu zinthu zikuyenda? kapena ayi ngati mumamwa tea sikuti ndi azibale anu nso onse akumwa tea ayi akuvutika mukatengala ku muziti simunaati muziwe kut azibale anunso ali mugulu lomwelo lomva zowawa

    • @FelleCasim
      @FelleCasim 4 місяці тому

      Zitsilu za nyau inu wamzelu angavotele mcp panomso?

    • @DIRECTORJARVMACK
      @DIRECTORJARVMACK 3 місяці тому

      Kumalikonda dziko lako osati umoyo wako ayi anthu akumva kuwawa

  • @IsaacMusa-py2jm
    @IsaacMusa-py2jm 4 місяці тому

    Mau amphanvu 👊 👊

  • @Littlefair7
    @Littlefair7 4 місяці тому

    Mutholo ndi anzako achina Ben Longwe mupeze zochita, what you're doing is not activism, this is stupidity of its highest order, mwasanduka oyankhukira zipani, zopusazi tasiyani, ngati mukufuna u activist pitani ku school mukaphunzire osati kumasokosa ndi zopusa zanuzi.

    • @EvanceEdson-fz1vn
      @EvanceEdson-fz1vn 3 місяці тому +1

      Akunena chilungamo, chilungamo chimawawa. Why 50+1, why alliance yet anakana a mec fresh vote registration? Don't you see kut the same rules of 2019, could apply for the fresh 2020 election

  • @UmariBashiri
    @UmariBashiri 4 місяці тому

    Zoonadi munthu wamkulu

  • @IssakeMateyo
    @IssakeMateyo 4 місяці тому

    Kkkkkkk

  • @BintonDzuwa-d3p
    @BintonDzuwa-d3p 4 місяці тому

    Simungavumeleze

  • @ClementMisozo
    @ClementMisozo 3 місяці тому

    Very true