A Chimwendo Banda Mphamvu Zoyakhula Za Report La Biyeni Mwazitenga Kuti? - Sizwe
Вставка
- Опубліковано 18 вер 2024
- On Nyasa VoiceBox, Sizwe from Ntcheu seems to have a few issues to address with Honourable Richard Chimwendo Banda, Minister of Local Government, Unity, and Culture, regarding his remarks at a political rally about the air crash that claimed the life of the late Vice President Dr. Saulos Klaus Chilima.
Pa Nyasa Voicebox, Sizwe wa ku Ntcheu akuoneka kuti ali ndi mfundo zingapo zoti akambirane ndi nduna ya maboma ang'ono, mgwirizano, ndi chikhalidwe, a Richard Chimwendo Banda, pa zomwe ananena pa msonkhano wa ndale wokhudza ngozi ya ndege yomwe idapha malemu Vice. President Dr. Saulos Klaus Chilima.
Mwafusa bwin a mfumu adatiphera achilima munthu wosalakwa anthu awa chikangawa mwa ndifusira mfuso la bwino zedi, alira bwanji abiyeni oti anapha yekha chikangawa Mulungu wathu awakatha awa, mfumu zikomo kwambiri Ambuye. Azikusamalani ❤
That's the spirit we need in our warm heart of Malawi 💪💪
Mau amphamvu, long live Sizwe
Osaopa osafooka osagonja malawi dzuka rest well SKC
We are with you
Ine ndikusegula radio FM Ku Malawi ndipo dzina la radio yanga ndi CHIKANGAWA RADIO FM❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤
Imfa ya Biyeni ikundiwawabe mpaka lero honestly speaking ife angoni moyo ukutiwawa za imfa ya Biyeni misozi yathu ikutsikira mimba
Ndipo nde wafikapotu naye uyu😮
Zikomo kwambili amfumu potiyakhulira
Zaona Malawians go konko parliament ayamba kutitola anthuwa alibe chisoni
Achimwendo ndigulu kwakupha chilima kupanda chilima anali ndani a MCP aaa amalawi chakwela ndiamena anapha VP uchitsilu wa MCP akuwona amalawi tikadagonabe ngati 1958 aaa ino 2024 tu
More fire 🔥🔥🔥🔥🔥 big man mkondo wangoni
G0d bless Malawi to all Malawians for the voicecall Friday
Aluta continua angoni
Biyeni anatiphera osalakwa😢
Isvuke madoda 😊
chakwera mwina agwidwa ku malawi koma ngati anathawisa prophet bushiri ku south africa anthu onse kuzunfulira mutu ndiye mu malawi kuzabera mavoti akhoza kubera nfati tiputse
ofunika kusalaza zuma zawo akaluza zapiteni ku Zambia sapanga zopusa
Zauchisilu kodi waletsa kuti anthu asamalire or kutengela za ndale pa maliridwe amalirowa iye adakambapo zalipoti anthu enanu ndizisilu kwambiri nkhani imeneyo or pa court chimwendo zangaluze nkhani imeneyo muvetse bwino
Inu palibe mukuchidziwa court amalidziwa ndi MA criminal, iwe firstonder court umalidziwa iwe? Popeza MA judge a Kumalawi ndi a chikangawa party nde nde chimfupi mwendo wakoyo akhoza kuwina, koma MA judge amene analipo mbuyomu chimwendo wakoyo sangalimbe ndiponso ndiwe galu + Mr chikangawa wakoyo mwana wa hule pantumbo pakonso😢😢😢
@@user-zj1xx1ic2m iweso palibe ukuziwa chifukwa zomwe adalakhura chimwendo sizimezo
Chipwili Cha munthu ngati iwe you don't even know what chimwendo said koma busy kulesa.
Ma bundles opasidwa omwea....
@@wisdomsadyalunda2001 kulesa chani simunave zomwe adalakhula vuto ndilimenero kulira lirani koma osalowesapo Ndale ndiye Pali vuto palibe ngati muli adolo osapita kumademo bwanji
Sizwe tili nanu limodzi dzikoli ndi lathu ili si la chakwera yekha kapena chimwendo yekha ayi tikakumana konko ku citycenter
Ziko ili mwaliwononga mu zaka zochepa .....amalawi tili pamavuto koma mulungu atithandize kuti agalu awa achoke basi anthu osamva zonena za anthu chifukwa cha ndalama zokuba
Chimwendo akuzitenga ngati ndiozindikira kwambiri muno mu dziko lathu la Malawi zoti akumatuma anthu kumapha akuona ngati sitikuona
✊️✊️✊️✊️
Apanenidi amenewa kuwapha anzawo ngati dzinyama zamanyazi ndithu
Zimvele mtolo chimwendo ndizimenezo
Thawi kachitsiru wina alira 😂okutetezani ndiamene akuzakutapani😂
Afumu mwayañkhula bwino
Tiyeni tiyeni tonse lachisanulo a Malawi tigwirizane Chakwela ndimunthu oyipa
Sorry about Malawi zovuta kwambili
Chimwendo banda nkhani ndi imeneyo sindisowanso kukuthanthauzila yalankhulidwa mu chichewa komanso momveka bwino ungoyamba kulongezelatu uthawe
Inu mukulandira bundle yoti muzikapamba zabwino za athu akuphawa musamale heavy..
My warning tishala limozi mmakonbo so mwachulusa kuwerewesha vuduka mitu apa anyokopola muchito so...
Apapa Angoni ayambapo. Wathuyo sangapite chomcho
Chimwendo Banda alibe khalidwe.
Chimwendo ndi MCP ndiyakupha
ARichard chimwendo Banda. Mutu wong'alukawo.
Mwayankhula bwino zedi,uyutu atiuze bwino ndithu
Tikakupelekezani
Akuluwatu awuze mtundu wa Malawi amene adawauza kuti ndege yadzadza mulibe Malo ndindani? Kapena amkadziwapo kathu? Adziwe ichi amalawitu siopusa ndipo zoti akusakaza ndalama zathu tikudziwa ndipo munya mukatuluka m'boma atambwali inu
Ndipo musawasiye aigiputo amenewa
Chitsiru nachimutu ameneyu
Osawopa
Anthu enanu ndinu zisiru pakqganizidwe vuto mulipo ambiri Amene mukutenga maliro aChilima ngati chida chotchukila pandale
Kachimutuyu amangidwe basi chimwendo banda oipa nkhope yomwe mutu omwe
😂😂😂😂
Chakwera unya uwona .
Asambeni sonke Friday Sizwe ukhulumile😂
Lewis Maria Allen Karen Martinez Margaret
Be strong 💪 guys more fire 🔥 don't give up be strong again 💪 🙏 this president is nonsense 😑 🙄
Olo galimoto yavuto siyenda pansewu evn number ngati palibe imafusidwa y.what more ndege
Kukamwa ngati adya manyi
Gokomko .komanso anaziwa bwanji kuti yagwera ncthire ndani mzumzu yeseunja .aphe tonse nyero zawo
Finye ameneyu Chimwendo watikwana ndi nzake chikangawa,was hoping kupanga ma demo akamabwela ku America azapeze anzake atenga mpando
Kod athu inu tupere zananene kom 2020 ija anakuusatu wosafa
Ndipo osaloradi tiyeni tigwilane manja sua napankholoyu achokedi
Chakwera wathawira ku UNGA
Ulindichani kuti Anthu akusake kapolo ngati iwe olakwa ndiyemwe wakupasa phoneyo galu iwe
chisulu ndi iweyo ine sindine ngoni koma ndiwe opusa kwabasi
Kuyankhula kukufunika nkumeneko , osaiwara kupanga action
Gokonko
A MCP la 40lakwanila pa chilima mwapha olakwika muziwona ndipo afinyidwe amenewa akutiwona ngati amalawi zitsilu
Chimwendo umve uliliko ... Biyeni sanali wakwanu .. 5 days
Imfa yachilima ikuwawa ndipo Amalawi nose mukulimbikisa kuti chilungamo chidziwike
Amva kuwawa amenewatu Friday sikale
.
Ndipo wokoma awa
Munthuyi ndichisilu akuti akufuna kusangalasa bwana wake chakwera ......zisilu zokhazokha .....munapha chilima ndipo ndizoona .....boma la zisilu zokhazokha
Ifa ikutipweka ya chilima adafelanji bhiyen.
AMALAWI TIYENI TIDZUKE CHILIMA OLO ADALI NGONI KOMA ADALI VP WATHU WAMALAWI AMCP MWAZIPUTATU UWUWU NDIY MOTO UYAKE MALAWI NDIPO NDEGE KUGWA KUMVURA ANTHU ZOMVALA , AAAAAA AI TILI NDIMAFUTSO CHILIMA KUFA KOMA CHAKWERA OLO OSASUTHIKA NGAT MZAKE YEMWE ADAMULOWESA M,BOMA. MCP 31YRS MULI KUNJA KWAM,BOMA ZANU KUKULOWESANI , M,BOMA KOMA ZOONA CHIFUKWA CHAMAUDINDO KUMUPHA ZANU ACHAKWERA , MWAPANGA MISTECK ZEDI. IYIYI YOKHA IKUMVUTISANI MIZIM YAKWIYA EEEEEEH ACHIMWENDO NANU MUTU ULI PHWIIII NGAT FUWA LAPAUKWATI UZIONAT MUTU KUKULA CHONCHO KOMA OPANDA MZERU. NDIPO NO 1 KUFA UKHALE IWEYO WAMUTU NGAT FUWA LAPAUKWATIWE CHIMWENDO ,CHILIMA MUDAMULAKWIRA , ADALAKWANJI?
Kusakhaledi. Kukulirana. Mitima. Azipani.. Zichepeseni. Gwirizanani. Muwombole. Amalawi. Chonde!!!!!!UTM. Chonde. Zichepeseni. Join. DPP. UDF. AFORD.. Please.!! Mayi. Joice. Banda.and. Your party please. Join. Ngwirizanowu. Ombolani. Malawi
Chimwendo mutuwo umamulemela ameneyi
Ndichi. Nkhumba
Koma abalee akuti tisamulirw biyeni koma tilire chilima ?nzoona zimenezo?ambuye amuyendere munthu ameneyu
Chimwendo Banda ndikanakonda atafufudzidwa bwino bwino apo biii. Tikhala ndi mafunso ambiri osayankhidwa mu mitima yathu. Chinaletsa iye kukwera nawo ndege ija ndani????? Pamene malo analimo ambiri mbiri mu ndeve muja. Mmmmmmmh munatipweteka anthu inu.
Chimwendo chimutu cha chikulucho mutu wopotoka
Tili nanu limodzi angoni
M
Mwasanduka kukhala zisiru kenako mupenga chifukwa Munthu or Anthu omwe mukulimbana nawowo sakukuynkhani mulibe manyazi? Zisiru inu
Kwachema tiyeni tose tigwirsne manja
Mizimu ya anthu 9 songakhale chete
Akuyankhulatu si anthuwa ai
Koma mizimu ikulowa mwa anthuwa mkumawayankhulitsa
Anthu ajatu adaksli.kuchikangawa
Chomwe akuopela chakwela kukaona kunagwela ndege mchiya???
????
Achakwera asavukatu chaka chake mchino
Asambeni muwumodzi muli mphanvu Malawi dzuka dzuka osawopa