Those that think that Dr. Joyce Banda is a spent force in Malawian politics are cheating themselves and at the same time misleading others. Dr.Joyce Banda is and will still continue to be a highly respectable force in Malawian politics. There are so many good and great things Dr. Joyce Banda has done for Malawians and continues to do which Malawians of good will and sound reasoning will never forget. Long Live Amayi!
Kkkkk Joyce banda amakhala mu fernbrook estate muno pa Stage wood street apa ife tinali kumuona tsiku ndi tsiku and olo amufunse anena kuti zoona. Ku America Joyce adakhalako liti ? Joyce amakhala mu fourways/ Johannesburg Fernbrook estate - kenako anasamukila ku Dainfern ndikomwe anamumangila kuti abwelere ku Malawi zaku America mukuzitenga kuti agalu inu
Sangasiyane ngwilizana wawo ndi wamaganzi kuteloko mayi Joyce Bandah ,,ngankhale muli akulu Anga Koma lmfa yachilima mudziwapo kanthu inuyo ,,
Mutu wanu ndiobonga amai Inu, mgwilizano wa DPP ndi UDF siwamagazi?
@@PhillspicJerechokani inu mulibe mzeru palibe chomwe mudziwa mmutu mwanu mwangodzadza manyi umuuzeso chakwera kuti machende ake anapha chilima
@@Musa1828-l5d Ndiwe mwana phone ndiyako koma uziona Zotukwana komaso owatukwana
Obvious....she can do anything for money shame
Akuziwadi kwambili mmayi oipa uyuuuuu alape
Those that think that Dr. Joyce Banda is a spent force in Malawian politics are cheating themselves and at the same time misleading others. Dr.Joyce Banda is and will still continue to be a highly respectable force in Malawian politics. There are so many good and great things Dr. Joyce Banda has done for Malawians and continues to do which Malawians of good will and sound reasoning will never forget. Long Live Amayi!
Asatanic okhaokha ndi Mr chikangawa iyah..
Ndiye china nkumati Mutharika wakula? ifetu tikungofuna fertilizer tizidya nthalo yambiri
muthalika simukumufuna
Ndie padakali pano mukudya anzathu?
@@MartinmkapangakapangaEya munthu wa nzeru angafunenso nkhalamba
Fertilizer nde mutharikayo
@@AmosScott-z9x mmmmm mabodza achimwene awa 5 years adalamula ija inu phindu mudapezapo chani
I love this man eeshhh
Ine ndivotela utm,dpp,aford ndi udf basi
Akuluwa nzeru mulibemo. Iye akuti mgwirizano sunathe pamene amai ananena kuti anauzidwa MCP ikalowa ku convention ndiye kuti mgwirizano watha
Joyce Banda osavotera ndikape ndi munthu mmodzi safunira amalawi zabwino mutayeni
Komatu zomatenga amalawi ngati nyape zanuzo ife timadya nawo musatitole osaukafe musamale,,,,kulankhula kwabwanji uku? Timve ziti? Muona ngati ndi nthawi zopusitsana panoso?
Titamakhala ndi anthu ngati awa mziko olankhula chilungamo bwedzi ziko likuyenda bwino
Bakili muluzi TV yokha nde ya nzeru zinazi zimakhala ngat mwa chiphwilikiti
Politics at its best. PP is still with MCP. This is a strategy of dividing votes in the south. Amalawi akupenya masiku ano sangapusitsidwe
Agalu inu asatanic okhha okha,tikumana 2025
Gashiketi yokhayokha kulibetu ndege yogulitsa kumalawi anagwetsa chakwela ndiye akadzawina maiwa
😂😂😂😂😂
Cashgeti people's paty
Mmphuno mwako
Nkhani yabwino hvy
Moonse NDinu amane mukuzunza Malawi ,vote Kwa Dadie basi
Anthu ngati pa msonkhano wa fumu wa macopoun
Chokhacho achimwene mwauponda mcp ndimbola
😂😂😂😂😂😂 Inu munaziyipisila mu trauser chifukwa cha tonse alliance simuzawinanso agalu inu😂😂😂😂😂
Ulemuwanu amai ine ndichisanzo chabwino ulamulilowanu unatisithadi achinyamata mmalawimuno munasitha dziko lamalawi masiku owelengeka amalawi tiwakumbukile anapangazabwino❤
koma ambuliwu amalawi changamukani
Ndimwe wa tonse alliance mavwele yinu
Kondwani Nakhumwa chikapeta Chakwera bwana mkonzeke kukalowa Ku state house 2025
Your Back ground music ndibwino kuyichosa zizimveka boh boh
Treu
Zamanyi basi mesa Joyce Banda yo ndi mfiti anatigulisa kwa chakwela yo hiyaaaa
Kodi mukadali ku mcp eeeti?? Ayi tamva
Mwasowa chochita Kodi ?
Kanyamata aka boza ngati katsikana ka 15 yrs old
Zinawakanika awa analamulira dzaka za Bingu ziwiri basi koma Bambo uyu wakhura za nzeru Koma mai athuwa akuba
Inu muli ku Mcp musatiputsitse kuteroko nde kuti kutsogoloko chachiziwikire midzapanga mgwirizano ndi mcp
Ingotulukani ku mcp inu
It only happens in a federal government
Kuonekerathu kuti muri pamodzi ndi Mcp mkufuna kunamiza amalawi muona pa 2025
Mabindi (masanje) APM my vote
Kutaya vote my friend kumeneko think nicely
Kagwere uko mufuna muphe tonse ndi chifunga tikakuviterani @@damianokachingwe3531
Eti munthu wanzeru zoona angavotele Peter kkkkkkkkk
Kkkkk Joyce banda amakhala mu fernbrook estate muno pa Stage wood street apa ife tinali kumuona tsiku ndi tsiku and olo amufunse anena kuti zoona. Ku America Joyce adakhalako liti ? Joyce amakhala mu fourways/ Johannesburg Fernbrook estate - kenako anasamukila ku Dainfern ndikomwe anamumangila kuti abwelere ku Malawi zaku America mukuzitenga kuti agalu inu
😂,,,😂😂 palibepo Cha nzeru apa
Mfundo za ziii
10:14
Inu palibe chanu chipani cha satanic chakwela palibe za vote
Mai Joice banda imfa ya chilima akuidziwa
Hahaha koma ndale kkk
Salu zikugawidwa koma sakuvala mudzifuse
Zilombo za chakwera
Kod chilipo chipan ichi et
Kuyankhula kwamanyi uku nkotani
Kunena zoona mulamuliro wanu amayi zinthu zimaenda km ife tili pambuyo panu mai 2024 moto kt buuuuuuuuuuiiiiiiiii
A Joice Banda tazisiyani izi. That time you had that opportunity because of death and you can't win your dreams.
Adadiiii moto buuu!!¡
Kkkkk koma anthu akafuna kum'bera wankulu eeeee amanama koopsya. M'bereni Ali ndi ndalama zomwe anaba kuzera mu Caschgate tuyeni naoni musamukhumudwise m'beleni
Ubwino wake mwavomereza kuti mafumu akuvutika.Mavutowo ndye akuta wina aliyense
Kkkkkk kuiyang'alura😂
Moni kwa mr Chikaonda ku chipani kwanuko 😂😂😂
Za ziiiiiiiiii kwanu kunatha Inu limbani mtima
❤❤❤❤❤ 50 +1
Kod chivunde first name ndindan
Koma timvereni ma followers anu background sound yo muchotse ikumatisokoneza
ATUMIDWA KUTAPA MA VOTE A KUMMWERA A DPP.
Musapepelese anthu Mai inu
Ndiye ngati akukayikirana kuba chitenje what more ndalama za boma?
50+1🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥
Joyce chipani chako ndi chakwanu konko ndi zisilu zakozo
Zaziiiiiiii tixivaso za mcp pano
Chasowa chochita inu
Koma ndiye mutimatiza
Zee one films
Aaaaa awa ndi anthu okuba
mukuwapusisa amalawi awuzeni Zoona
Awa angomasuka basi atulukamo mu gwilizano wa Tonse alliance
chivunde ali nd mfundo mbambande koma chipanichi chamuchepela kwmbr
Tinadzidzukadi zoona Ng,alulula basi ,tachika nacho kutali
Anthuwa atiwonjeza ife ovota atifuna pompano
Good
Mcp zake zada basi
kodí zílimótero et
Musezeseni katundu muzakana kumutura pasogolo
Hi
Achakwela mundu jwamatama
AGALU kwabasi inu mbavu satanic nokha nokha simungawinenso afiti inu ndi chikangawa wanuyo
Mhuu!!!
Tikuvoteran may tavutika mokwana
Kutereku zolinga zao nzimenezi? Mwayaluka. That's why speech ya mai sikumveka mutu wake kkkkkk
Zaazii kuti ziveke bwanji inuyo
Kkkkk kwachema ku pp
Vinyo watha
Aimed basi
Chaka cha mawa chakwera no vot
Hhhh kom inu mupangisa kuti chakwira awine hhhh
Amapocholol
😅😅😅😅
😂😂😂😂
Ine vote yanga ilikwa may
Kkkkkkk Kkkkkkk Kkkkkkk