Ndipo sindikutha kudziwa ngati kuli dziko lina limene limapanga ndale zaumbuli ngati Malawi, ka dziko kakang'ono koma mabodza thooo! And the gullibles believe everything they hear on social media. Those guys cooking these lies are just taking advantage of umbuli wanu omakhulupilira zilizonse izi. Manyazi akugwileni koma
Akalindo pita ku school, osama tchukili zinthu za ziii. We Malawi we are busy following stupid things rather than concetrating on things that can develop our country. A kalindo ndi anthu anu mukusokoneza dziko la mbuli kale ili.
A Chakwera muyaluka chaka chake ndi Chino,, God is watching you,,😂 😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂 olo utapha amalawi onse utsale wekha,koma Mulungu adandiuza kuti akuyalutsa 💯
Basi kungowapotiladi mmanyumba mwawo anthu amenewa, akupanga zimenezi akuwopa kuti akatuluka mboma adzamangidwa nkona akukakamira mipando mind you God is watching
Kkkkk!! Chipani chanji chimenechi koma zitha zimenezi ife si akamuzu aja ayi achawera zukani pano mfuti lolo mmangochi tikungodikila pano ife takakhala tilipanfchito imeneyo pa joni ntanyiwa we are ready
Kod akuluakulu anthuwa phamvu zikuwachulukira et but in the name of Jesus asatanic amenewa chakachino adunsa awiri ndipamene ataziwe kut iwowo siwochuluka nzeru than mulungu
Ndale Za Ku Malawi ,kumangokamba zokupha basi , come to South Africa muwone ndale Za anzanu , Mwana uyu Jullius Malema ,ngakhale alankhule BWANJI boma silipanga ma plan wopha anthu ayi , AAA Malawi fokofu
And according to you wakhulupila zomwe zikukambidwa apa kuti ndizoona? These liars are just taking advantage of you guys pomakhulupilira zilizonse mungave pa social media. Pamene alili Kalindo anthu oti angamuphe mu nthawi in ndi a opposition kuti apeze ma political scores, MCP yoti akudziwilatu zoti munthuyo akulimbana ndi iwo kumupha sindiye kuti azipalamula dala moto. Kumaganiza a Malawi pena
If you want to see people your house today just do that this🎉day you gonna be last day for you mr chikangawa I tell you
Ndiponso live he's gonna also we can't care about chakwela he's full of no nonsense don't try that mapwala ako chakwela
Ndipo chitsilu mr Chikangawa galu okupha @@AngolanChinga
That's no sece people, guys don't play bad games please we are one
@@AngolanChingathat's true ngati atamupha kalindo ulendo uno Dr Chikangawa awona sitizamusekerera mpang'ono pomwe.mnthu watizuzayu kokwana
Ndipo sindikutha kudziwa ngati kuli dziko lina limene limapanga ndale zaumbuli ngati Malawi, ka dziko kakang'ono koma mabodza thooo! And the gullibles believe everything they hear on social media. Those guys cooking these lies are just taking advantage of umbuli wanu omakhulupilira zilizonse izi. Manyazi akugwileni koma
Bon kalindo sangaphedwe olo zitafuta motani God bless kalindo
Mozambique who is presedent
Come to Malawi
God keep mr kalindo continue what you doing don't stop 💥💥💥💥
Muyelekeze muone.kodi Mr chikangawa mwayamba kuzimva mphanvu kuposa mulungu?? Mukufunq kuuyese mkwiyo wamulungu kapena? Muzafaa imfa yowawa
There is no super man in the world, anafa queen ndiye CHIKANGAWA mkachani
Sopano chakwera akufuna akhale eka zikoli😢😢😢
Eya
Ngati angamuphe bon Kalindo , ifenso timupga iyeyo amene watuma zoti bon Kalindo afeyo . Timupha magazi ake ndidzamwa ineyo
Pamenepo ndiye aziwe kuti amalawi ndiwokwiya komaso atopa naye Dr Chikangawayu
Comrade Ntanyiwa,Kalindo & o malawianz we r in this 2gethr A.P.M it's our vote
Ndipo akunama awa chaka chake ndi chino ayelekeze mawali asaliwone namanyi ameneyo mr chikangawa kalindo alipo ndipo azafa nthawi yake ikazakwana ndi mulungu
The DC sangaphedwe i swear.... Something will happen in this country. We will not fear whether the president or what
Anthu oipa kwambili ndi akazi monica chakwera mkazi wa usi mkazi wa kunkuyu akukhala ngati kuleba sanafikeko kodi pobereka mwana zikukhala bwanji pamakhala zowawa kwambiri pls pls osapha anthu
Ndipo Malawi ayaka moto ayensere kumpha Kalindoooo more fire 🔥
Ndipo
Inuuu atelo ndan kod tandiuzen ndiziweee,chakwera kod??? Aaaaaaa panyapacheeee ndthu.......
Awatu afika popepera nawo udindo akusakira pofera ohoo😢
Mulungu achita chotheka pa kalindo
Kuchoka 2020 kufika lero zitukuko zitatu zochoka ku mcp kumpha anthu kugwesa ndege komanso kugwesa ndalama ulendo Uno muziona sitikusiyani
Do you know God of Shadreck, misheck and Abidnego? You never kill Kalindo, Kalindo is son of God ndipo sizichitika believe me
May God protect bon kalindo
Aitu Allah yemwe ndimmodzi yekha amene timamupembeza ife salola kut aborn kalindo aphedwe Allah akuona zomwe akuchita chikangawa ndi team yake
Ameen
Ameen
Yes Mr chikangawa we know u planz try u will see what's gonna happen if u wnt peace free bon kalindo
Akalindo pita ku school, osama tchukili zinthu za ziii. We Malawi we are busy following stupid things rather than concetrating on things that can develop our country. A kalindo ndi anthu anu mukusokoneza dziko la mbuli kale ili.
We are still crying about chilima now if happening this you will see Malawi 🇲🇼
In the name of Jesus bon kalindo saphedwa ambuye timenyereni nkhondo timadalira inu 🙏
Ameen
Ameen
Koma abale Koma ndibusadi muthuyu ambuye mtengeni Muthuyu abwere kwainu ationjeza 😢😢😢😢😢
Sizingatheke kumupha born kalindo zachibwana
A Chakwera muyaluka chaka chake ndi Chino,, God is watching you,,😂 😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂 olo utapha amalawi onse utsale wekha,koma Mulungu adandiuza kuti akuyalutsa 💯
Boni kalindo kungophedwa malawi ayaka moto komaso dziko malawi likhala manja mwa nsilikali
iweyo ndindani ukuyakha zomwe s ukudziwa
A Malawi ndiiwe bwelani poyela tikuoneni
Inu ndinu a chani bwana?@@EdwardRichman-zs5pl
@@EdwardRichman-zs5plndie muziopseza anthu? Mukunamatu man
Ndipo siku likubwera ndipo dziko ndi anthu amalawi omwe mukuwanenawo muzawaona ngati oipa ndipo dziko lizakukulirani siku limenelo ndipo muzalakalaka nthaka itang'ambika kt mulowe pansi koma sizizatheka bet me@@EdwardRichman-zs5pl
Zilibe umboni izi osazitengera palibe amene akufuna kupha Bon kalindo a malawi siyani nkhani zokamba za imfa you will reap what you sow
Ndipo ndizovetsa chisoni kuti ma comments ambiri apa angokhulupilira zilizonse angave, Malawi tili ndi ndale zaumbuli kwabasi
Basi kungowapotiladi mmanyumba mwawo anthu amenewa, akupanga zimenezi akuwopa kuti akatuluka mboma adzamangidwa nkona akukakamira mipando mind you God is watching
Mmmmmm 🙌🙌🙌 ayetsele awona kut dziko ili tiotcha. Aliyense awone kolowera 😢💔💔💔💔
Zimenezo sizingatheke kumupha kalindo
Zitsilu siziphedwa kupha kalindo bora kupha mbuzi ya bele bro usamaname
Nde mukutukwana bwanji,, chilungamo kuwawa,,chikagawa fanz
Oipitsitsa ndi Monica Chakwera Masamuyiwale akuyendetsa nawo dziko la Malawi.......!
Nyanga amasunga ndi zimayi
Komatu pakhala mwazimwazi angoyesela kupanga zimenezo kuti atiphele bon kalindo wathu
Iwe Chakwera mutuwako suganiza ukumapanga mma plan ukupha kalindo ulibe nzelu
Kalindo more fire
Kkkkkkk koma mr chikangawa tayelekeza
Live from kongo 🇨🇩
Koma is this true a real man of like God a chakwera mwafika apa? But why?
Lazaro wafikapo.Dziko lake lokha iye momwe amachita mademomuja alipo anamupangila chiwembu?Ndichifukwa anathawa kuubusa onyenga yo
Angoyesa kuphedwa bon kalindo chakwera one Malawi m'mene izachitikila
Bon kalindo sangaphedwe ay ndipo sizingatheke
Try it, Mr chikanga chakwera u follow him to grave dust to dust u witch craft u died it too wheath u want or not try it today
Akangosowa bon kalindo anthu asasekelele ayi nawonso adzasowa siku limodzi ndwa ku mulanje mwanayo mukampha muona chomupmhela simudzamphatso wina ayi
😂😂😂😂😂 chakwera akuziwa kuti chaka chamawa sazawinaayi ndipo akuziwa kare kuti amalawi sakumufunaayi ndipo akuziwa kare kuti waluza kare ndipo akazaruza akuzifusa kuti kodi nizarowera kuti uzarowereso kuubusa kwako uko kuusatanikikwakouko
Mulungu wathu ndiwazatheka bwanji, no weapon formed against Kalindo will prosper
🎉zodadi ifetadusa mamawa popop km palidi anyamata ochuluka kwambili brother 😢😢 atanyamula zibhonga
Izozo asayelekedze chakwerayo nanga azapha anthu angati?kodi ndi uja mmati m'busa ameneyo?
zatikwana zomwe akuchita chakwera ndipo mulungu sangamusiye choncho ambye tinthandizen
Kkkkk!! Chipani chanji chimenechi koma zitha zimenezi ife si akamuzu aja ayi achawera zukani pano mfuti lolo mmangochi tikungodikila pano ife takakhala tilipanfchito imeneyo pa joni ntanyiwa we are ready
He will not die
May God protect him and be with him
Ameen
Usanamize anthu naweiwe. Usatumizako zachisisimuso bwanawe " unaliko? Uchepa nzeru ndiwe.
Kod akuluakulu anthuwa phamvu zikuwachulukira et but in the name of Jesus asatanic amenewa chakachino adunsa awiri ndipamene ataziwe kut iwowo siwochuluka nzeru than mulungu
Zabodza akalindo ndindani Malawi oti Boma lingade nkhawa Malawi angapinduleko chani ndi akalindo okhawo opanda zochita angatanganidwe Malawi Azeri Ali bize kupeza njira zopezera chuma awawa asiyeni azichedwa ndizibwana
Olo kusowa okuphayo nde mpaka akaphe kalindo munthu ozerezeka ngati ameneyo?? Mulibe zochita zina kodi zokuti mutha kumabweretsa pano eti?? Wat is Kalindo pliz??
Never anamulenga siiwo ndipo BON Kalindo adakangalulabe Mulungu wathu siwakufa afe ndi iwoo
Kungophedwa born kalindo,, nkhondo iyambila popho mosakaikaso ,, chifukwa pano tili lede kuyambitsa nkhondo yakufa kwa chilima anytime ikuyambika muno malawi ,, kungofika pa 30 mwezi uno popanda report kutuluka muzionaso
Nonsense wenna
President waifeamalawi osauka atilekele mulungu awalange lelo lomwe mzina layesu
Kupha Bon Kalindo ndi mistake a Malawi azakwiya ndi okwiya kale ndi kufa kwa Chilima
Chakwera yesera wuone zimenezo ngati munapanga chilima akhale yemwe uja wakwana yelekezani muone
Kodi amangodziwa kupha kokha?ndiolephera adzilenga ndikulemga otsati kupha kokha
The DDDDDDDDDCCCCCCCCCCCC never did bon kalindo never did 🇲🇼🇲🇼✊️✊️✊️✊️✊️✊️✊️✊️the DDDDDDDDDCCCCCCCCCCCC
Limpompo mukusocheretsa anthu osalakwa... pitani kwina
Munya muwona sizitheka bon kalindo anatumidwa ndi Mulungu kuti ayimilire anthu wosauka, Mulungu akukanthani nonse, munapha Chilima inu apa nde zikuchita kuwonetseratu kuti achakwera ndinu amene munapha Chilima tikufuna report la ndege afiti inu bas kumangolimbana ndi anzanu opanda chifukwa Mulungu akukantheni nonse okupha inu
Kodi chikangawa anthu 9 aja sanakukwane?
Kalindo kungophedwa chakwera naye afa basi ndipo angaphedwe ndimanja
Chakwera akuzuza Malawi kwambili
Ndale Za Ku Malawi ,kumangokamba zokupha basi , come to South Africa muwone ndale Za anzanu , Mwana uyu Jullius Malema ,ngakhale alankhule BWANJI boma silipanga ma plan wopha anthu ayi , AAA Malawi fokofu
Ndale za ku Malawi ndi zoputsa kwambiri, Kuno sangapange zoputsazo ayi
And according to you wakhulupila zomwe zikukambidwa apa kuti ndizoona? These liars are just taking advantage of you guys pomakhulupilira zilizonse mungave pa social media. Pamene alili Kalindo anthu oti angamuphe mu nthawi in ndi a opposition kuti apeze ma political scores, MCP yoti akudziwilatu zoti munthuyo akulimbana ndi iwo kumupha sindiye kuti azipalamula dala moto. Kumaganiza a Malawi pena
Mumangonvera nkhani zamabodza ngat zimenezi amalawi chifukwa chani? Zoona mumganvere bodza la ntheretu ngat ili? Aaa koma anthu mumasowa zopanda comment mwanva.!! Zoti born kalindo anayamba kalekale kumangoti akufuna kumupha moti simudziwa? Zaziiii muzitukwana dala boma muli ndimantha kut tsiku lina zizakutembenukirani nkumaopa then nkummadzi pherera pomatumiza mauthenga oti akufuna kukuphani😂😂😂😂😂 muziona!! Ngat timakutumani kut muzinyoza alamulira ife
Kalindo adzamwalira panthawi yake, ndipo enanu mudzayambilaso ndinu kufaaa...
I curse you all team Chikangawa
Bonikalindo can not be killed God be with him sory to someone who make plans to kill bonkalindo
Mmmm mumakamba zomwe zimangogawa dziko muli ndi chiwanda choipa palibe choona chomwe chinabwera choona bolaninso mtambo pali iweyo ndi uja wa muvi wachilungamo palibe chomwe mumanena zaphindu
Chakwela wakulira ku mudzi mu umphawi
Koma chikangawa ukagoyelekeza kupha kalindo uziwaso🛠️🛠️🛠️🛠️🛠️🛠️🛠️🏹🏹🏹🏹🏹🏹🏹🏹🏹🏹🏹🏹🏹🏹🏹🏹🏹🏹🏹🏹🏹🏹🏹🏹🏹🏹🏹🏹🏹🏹🏹🏹🏹🏹🏹🏹🏹🏹🏹🏹🏹
Sangaphedwe sizingatheke ndipo sizingatheke komatu akaphedwa ADC NDE KUMWAMBA KURIBE MLUNGU
Sizithekatu ndipo sizitheka iwo akudana ndi ma damo? Zaziiiii😢
A ndale jahena salinayo patali, cz amakgala anthu a bodza komaso olimba mtima
Once born kalindo kuphedwa kumalawi kuzakhala Moto ndi mkhondo yosatha chikangawa ntchito zawo kupha basi agalu amenewa
Wachita bwino apheso ndi iwe yemwe zikomo kwambili popeka nkhani yabwinoyi mudzakolola zomwezo ndipo mudzaweruzidwa
Kodi iwowo pansi pano anabwera kudzakhazikika?
Zomupha bon kalindo ndizonama ,
Ngati zilizoona tidikilile 3 days from today
sizingatheke ,,,, tili komweko
Old state lodge stlye basi yapafupi ndi moyale basi
Mulungu amugolere born kalindo,,,, tipita kwa chakwela komweko anthu onyasa a mcp oyendela mamina akhosa
Uyu sindimumvela amachulukitsa mabodza,chanel ndi bakili muluzi kawawa wosati izi ayi ,uziwuza wanthu amisala .
Nyasi zokha zokha, zikunenedwa apazi. Why a malawi mkukhala ngati mkusuta ganja zo ganiza zanu, kweni kweni mkufuna chani a Ntanyiwa Nzeru ndizo mlibi let him. Kuganiza ngati khoswe.
Chikangawa chakwera nyama za anthu 9 aja ukalibe ukhuta
God is great Mr DC kalindo he will last long
Bon kalindo ambuye akhale kumbali yake
Munasiya mtalika munthu wamulungu kukasankha wa satanic 😢😢
Vyaboza namwe, vyose vya mbembe pela, kalindo luta ku parliament ndiko ukapangenge ivyo
Mutumbuka wambula mahara
Mtumbuka iwe matako yako
MULUNGU mukuloleranji izi kod kut dziko rathu tizidandaura muthu modzi pangani chotheka tikufuna mphamvu yanu ioneke pa maso pa amalawi tikuvutika ndimuthu modzi chonde mulungu tikufuna inuyo ife talemphera
Koma ichiso ndichaboza ichi zinthu ngati zakuvuta basi tangosiya ukuwona mulungu wakukana kulankhura kuchikamwa kwakoko lilongwe yake iti itapange mademo mawa zaziiii muzipanga kwanuko iweso ndiwe mbuli yophunzira ntanyiwa
Kom amalawi nkhaniyi titaiva mukuti nayo bwanji kod chakwela palibe plan imene anthu angapange
Chikangawa usamale munthu amaluzatu akulamula ose amaluza aja amakhala akulamula
My God protect all freedom fitters
Kodi dzikoli palibe china choti tingamachite koma kuphanaaa
Dziko lomvetsa chisoni 😢😢😢
Ndipomwe muzawawone amalawi moyo wawo
Ndipo agalu aMenewa a mcp akundinyasa kwambili