Mayi Nyumwa John akungotupa mutu kosalekeza

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 6 лют 2025

КОМЕНТАРІ • 188

  • @JoshuamigoweKennedy
    @JoshuamigoweKennedy 7 місяців тому +3

    Ambuye onani mayi uyu akuzum,zika kwambili ndi nthenda koma zonsezi ndikusiya m,manja mwanu amen

  • @ShaneElisha
    @ShaneElisha 7 місяців тому +19

    Mulungu wa David muchilitseni mwana wanu. Zimene mudachita pa ana a Israel pa 2mafumu 2 vs 19-23 muchitireniso mzimayi uyu ndikuti dziko lapansi likulemekezeni🙏🙏🙏

    • @samuzymkwanya8490
      @samuzymkwanya8490 7 місяців тому

      Mulungu away awayendele mwapadela I can fill the pain there going through

  • @MiddayDeleza
    @MiddayDeleza 7 місяців тому +4

    Our almighty God who at in heaven hear the cry of this woman lord for we know that you never fail have mercy upon thus woman lord in the name of jesus

  • @Emmanuel-l6i
    @Emmanuel-l6i Місяць тому

    Ambuye amene munamuchiza Hezekiah atadwara aendereni Mai awa apeze bwino mu ukuku wanu Ambuye 🙏🙏

  • @CharlesMuongola-mt4sv
    @CharlesMuongola-mt4sv 7 місяців тому +12

    Moyo wanga iwe,,,,ulinazo zifukwa zoyamikira Yehova

  • @MoosaMuhammed-se5sd
    @MoosaMuhammed-se5sd 7 місяців тому +1

    Ooooh mulungu wanga ndzakutamandani matsiku onse amoyo wanga mkhuzen mzimayiyu ndi dzanja lanu lamachilitso

  • @charlesRajabu-cc4bx
    @charlesRajabu-cc4bx 7 місяців тому +6

    may Allah almighty afewesele mayiwa kwa Allah ndikomwe timadalira

  • @Bathsheba19
    @Bathsheba19 7 місяців тому +1

    very sad but glad that her husband is still around. God will heal her, the fact that she met Rodwell it"s proof that God is clearing her healing journey.

  • @ChisisiSaynett-nm7uq
    @ChisisiSaynett-nm7uq 7 місяців тому

    Mulungu achilitseni amayiwa muntchifunilo chanu amen

  • @dorisbwanali150
    @dorisbwanali150 7 місяців тому +2

    What God can not do does not exist 🙏 ambuye onetselani Kwa mayiwa kuti palibe chokulakani, palibe chomwe mumalephera,Yehova akhudzeni mwapadela dela 🙏🙏

    • @GloryShaba-nd3mb
      @GloryShaba-nd3mb 7 місяців тому

      What God Cannot Do Does Not Exist #NSPPD 8AM FIRE 🔥 PRAYERS

  • @Mavitoabdulla
    @Mavitoabdulla 7 місяців тому +1

    Mulungu woziwa kuchilisa iyikepo zanja.amen

  • @StellahMatemba-e6j
    @StellahMatemba-e6j Місяць тому

    Eish ziko lapamsi

  • @jacquelinejowatih105
    @jacquelinejowatih105 7 місяців тому +1

    Eish 😭😭😭😭may God heal you mama....please Lord touch this woman and heal her

  • @EstherManda-ex3bc
    @EstherManda-ex3bc 7 місяців тому +3

    Eee Ambuye awachitile chifundo mu dzina la Yesu

  • @chifundomitambo6810
    @chifundomitambo6810 7 місяців тому +1

    Ambuye nchilitseni nzimai uyu mudzina layesu amen

  • @allankapasula8448
    @allankapasula8448 7 місяців тому +2

    God this is too much please touch this woman with you healing hands 👐 please God hear our prayers

  • @Prianka567
    @Prianka567 7 місяців тому

    So touching.God Please do something what she needs is your touch

  • @chimwemwendalumbe2638
    @chimwemwendalumbe2638 7 місяців тому

    This is so touching!!! God please touch this woman

  • @EdwardGeorgeKasabola
    @EdwardGeorgeKasabola 5 місяців тому

    Ambuye Mulungu muyendeleni mayiyu mukhuzeni ndimachiliso anu .Palibe chimakulakani Mulungu wanga muchoseleni ululu mayiwa

  • @JoshuamigoweKennedy
    @JoshuamigoweKennedy 7 місяців тому

    Ambuye ngati munachitisa batrumeyo kuonanso choonde muoneseni mayi uyu amen

  • @mphatsosadiki4983
    @mphatsosadiki4983 6 місяців тому

    Healing Grace

  • @gabrielzande
    @gabrielzande 7 місяців тому

    Yaaaa ALLAH!! may you soften for this Lady please so she be healed!!

  • @pemphoashani4619
    @pemphoashani4619 7 місяців тому +10

    This is disturbing eeeeh! God please see this woman and heal her. Amen

    • @MadalitsoMbewe-f2v
      @MadalitsoMbewe-f2v 7 місяців тому +1

      Eeeish that's indeed Mighty God touch her with healing

  • @NgomaRaheem
    @NgomaRaheem 7 місяців тому

    Ena akuvutika pomwe ena akuba ndalama zanthu eish Allah amuthangatile dzimayiyu mapumidwe ndiovutaso eish

  • @JoshuamigoweKennedy
    @JoshuamigoweKennedy 7 місяців тому

    Ambuye ikani dzanja lanu kwa mayi uyu amen

  • @FaithNyamathanga
    @FaithNyamathanga 5 місяців тому

    Achita kuoneka kuti alipaululu😢😢 Ambuye achiliseni mayi wa

  • @VictoriaWilliam-ms2ft
    @VictoriaWilliam-ms2ft 7 місяців тому

    Ambuye muchitireni chifundo mwana wanu achiritsidwe mudzina la mwana wanu yesu khristu sikukulamulani Koma kukupemphani 🙏

  • @SphiweDunnia-ff9xt
    @SphiweDunnia-ff9xt 7 місяців тому +3

    May the healing river flow over your life mama😢😢

  • @PreciousKumwenda-gh6uc
    @PreciousKumwenda-gh6uc 7 місяців тому

    Lord have mercy😢😢😢😢 touch this woman with your healing hand

  • @JaneNgwira-d7t
    @JaneNgwira-d7t 7 місяців тому

    Pomwe ife nzeru zathu zathera mpomwe mumayambira Yehova wathu pakuti chifundo chanu ndi mphamvu zanu zilibe malire simuwerengera mphulupulu zathu.tikhulupilira muchita chozizwa ndithu.amen

  • @madalitsononiwa1346
    @madalitsononiwa1346 7 місяців тому

    Healing mercies from above mama

  • @tadalanyirenda4744
    @tadalanyirenda4744 7 місяців тому

    Yehova adzakupewetsani ku matenda aliwonse. Sadzakugwetserani matenda owopsa aja munawadziwa ku Igupto, koma adzawagwetsera pa odana nanu.
    Deuteronomo 7:15.
    Get well soon mama

  • @praisekafuliza
    @praisekafuliza 7 місяців тому

    Please God😢😢🙏 get well soon mama... May God see u through

  • @CFMpinganjira
    @CFMpinganjira 7 місяців тому

    😢😢😢😢 so sad. God have mercy.

  • @ShakiraBiton
    @ShakiraBiton 7 місяців тому

    Ambuye akhunzeni mayi ndimkono wanu wamachilitso pakut paiwo okha sangathe koma adalira mphamvu yanu

  • @ShaneaIssa-ph3zz
    @ShaneaIssa-ph3zz 7 місяців тому

    Dear God....😥😭😭

  • @FloridaOssy19
    @FloridaOssy19 7 місяців тому

    Ambuye akudzeni amayi wa ndi zanja lanu lamachilitso 😢😢😢

  • @WilliamHope-rw3ko
    @WilliamHope-rw3ko 7 місяців тому

    Matenda achilendo awa eishh ambuye bwerani muzatiweluze 😭😭

  • @dalitsomthepheya7657
    @dalitsomthepheya7657 7 місяців тому

    May Almighty Lord heal you Mama 🙏

  • @GravelRonald
    @GravelRonald 6 місяців тому

    So touching, anyway God lives. Otherwise atolankhani zifunsani mafunso ogwirika malingana ndi condition yamunthu.

  • @marriammtisu3663
    @marriammtisu3663 7 місяців тому +1

    Allah knows the best
    Chinena ndilibe koma Mulungu yekha akuoneni mwapadera pa ife sitingathe 😢😢

  • @TimothyMoyendah-ih1qq
    @TimothyMoyendah-ih1qq 7 місяців тому

    Mulungu wanga tikudziwa timakuchimwilani tsikunditsiky 😢koma please ambuye muchitileni chifundo nzimayiyu ndipo mupatseni machilitso pamoyo wawo😢😢😢

  • @JohnKalembo
    @JohnKalembo 7 місяців тому

    Eeiishh mzimayi ameneyu ali mu ululu owopsa mmmm Ambuye Mulungu tikukupemphan mpatsen machilitso mzimayi ameneyu chonde chonde

  • @Fay-265
    @Fay-265 7 місяців тому

    Eishhhh mayiwa akuvutika tisanamei

  • @leonardkangoma
    @leonardkangoma 6 місяців тому

    Dzanja la ambuye lamachilitso likukhudzen mama

  • @RhodneyBwa3
    @RhodneyBwa3 6 місяців тому

    Mmmmmmm zosayenda

  • @Freedomchennl47
    @Freedomchennl47 7 місяців тому

    Mmm somvesa chiso Mulungu awayang'anile Mayi amenewa

  • @MathiuzMatungulo-fk5xp
    @MathiuzMatungulo-fk5xp 7 місяців тому +2

    Apapa pakuyenera kuti mathandizo osiyanasiyana awafikire ndipo pakuonetseratu pakhomopo kuti Pali zosowa zambili ambuye atithandize kuti titengepo step tisangoyakhula or only comment ife anthu a kuntandire

  • @FrankNedson
    @FrankNedson 7 місяців тому

    Mulungu akuonetselen machilitao ake aphamvu zodaphitsa mudutsemo munyenho imeneyi mukhala bwn mu phamvu ya Yahweh

  • @HappyAbyssinianCat-xt2bm
    @HappyAbyssinianCat-xt2bm 7 місяців тому +1

    Satana amabweresa zosakhara bwno pa moyo wathu kuti tizimufusa mulungu mafunso osakhara bwno, km inuyo mulungu chitanipo kanthu pa Mai awa yesu mwana wa David muchitilen chifundo mwana wanu amene akuvutika ndi matenda

  • @FelistersBulawayo
    @FelistersBulawayo 6 місяців тому

    God have mecy and heal her

  • @MusaMajudu
    @MusaMajudu 7 місяців тому

    😭😭😭Ambuye mulungu ndinu nthandizo laliyese ambuye ayendereni amai awa

  • @bernadettechoma
    @bernadettechoma 7 місяців тому

    Healing mercies from above 😢😢

  • @gabrielmaluwa1038
    @gabrielmaluwa1038 7 місяців тому +1

    Mmmm very sad 😭... Koma sound musamaike mkati kati mwa interview disturbing

  • @JoshuamigoweKennedy
    @JoshuamigoweKennedy 7 місяців тому

    😂😂😂😂😂😂 zikundiwawa kwambili ndi nkhani yayikulu kunena zoona

  • @frankbanda113
    @frankbanda113 7 місяців тому

    😭😭😭🙆🏻‍♂️ lord please forgive this mum

  • @GertrudeWailley-io1sc
    @GertrudeWailley-io1sc 7 місяців тому +2

    😭😭😭😭 ambuye loweleranipo musakhale chete inu mulungu

  • @alinafeAli
    @alinafeAli 7 місяців тому +1

    Ambuye chitaniponi kanthu pa Mai awa😢😢

  • @BlessingsLuclus
    @BlessingsLuclus 7 місяців тому

    Allah tikupepha chitapo kathu

  • @AtupeleLikwanya
    @AtupeleLikwanya 6 місяців тому

    Rest in peace Mai Nyumwa..you fought a good fight

  • @Stuartkachali45
    @Stuartkachali45 7 місяців тому +1

    Pepan Mai wanga 😢😢😢😢😢😢

  • @PeaceMafait
    @PeaceMafait 7 місяців тому

    This life😢

  • @BrendaDimba
    @BrendaDimba 7 місяців тому

    Healing mercies

  • @aishakachiwale
    @aishakachiwale 7 місяців тому

    Ambuye inu mwini moyo mwini machilitso akhudzeni mwana wanu mayi uyu ndi dzanja lanu la machitso baba m

  • @DONNEXKhama-bk1gy
    @DONNEXKhama-bk1gy 7 місяців тому

    Almighty GOD 🙏 please do favour to this lady

  • @RichardMatemba-pt8tc
    @RichardMatemba-pt8tc 7 місяців тому

    Our heavenly father the creator of everything have mercy with her please

  • @AnastanziaKamanga
    @AnastanziaKamanga 6 місяців тому

    Ambuye ndinu mumadziwa kuchilitsa tikupepha kuti muwachilitse mayi anthu

  • @movieworld12944
    @movieworld12944 7 місяців тому

    Mulungu wachifundo komaso ochilisa akukhunzeni mzina la yesu

  • @MarkKampido
    @MarkKampido 7 місяців тому +1

    The mother is in pain😢😢
    Calling for healing mercies upon her

  • @frazerbanda96
    @frazerbanda96 6 місяців тому

    May her soul rest in peace 😭😭😭💔💔💔💔

  • @hopejere567
    @hopejere567 7 місяців тому

    Ambuye akhudzen mayiwa

  • @glorymtande
    @glorymtande 7 місяців тому

    God have mercy

  • @PromiseMitayi
    @PromiseMitayi 7 місяців тому

    Yehova mulungu wamakamu mpaseni populumikila mwana wanu inu ndi m'busa wathu

  • @asamzymw571
    @asamzymw571 7 місяців тому

    Ndimamudziwa ine zimai uyu ankabwera kwanthu ,, ambuye anafika apa😢😢😢😢 mulungu wazifundo chitan monga mwamau anu chonde chonde

  • @JosophinaKungunde
    @JosophinaKungunde 7 місяців тому

    Mulungu akhudzeni amayi awaa 😢😢

  • @TriciaNyago
    @TriciaNyago 7 місяців тому

    God HV mercy

  • @cathymbawala6576
    @cathymbawala6576 7 місяців тому

    Healing mercies upon her..... she is in pain abale😢😢😢😢😢

  • @chifundomolleni5450
    @chifundomolleni5450 7 місяців тому +5

    Next musazaike background song, its disturbing. Get well soon mama, may God's healing hand be upon you.

  • @Robbenkachulu-lm8ls
    @Robbenkachulu-lm8ls 7 місяців тому

    God touch her with your healing hand

  • @BridgetMayuni
    @BridgetMayuni 7 місяців тому

    Ambuye perekani machiritso kwa mayi mzathuyu kuti apitilize kusamala banja lake. Chonde chonde

  • @LuciaPhiri-e1z
    @LuciaPhiri-e1z 3 місяці тому

    Mulungu awachitire chifundo

  • @AleksaWilliams-qc6cn
    @AleksaWilliams-qc6cn 7 місяців тому +2

    Ambuye azikudalisaniso inu a Lodwell anthu ambiri amathandizika kuzera mwainu

    • @NatashaBema
      @NatashaBema 7 місяців тому

      Ambuye akukhudzeni Mai wanga ndipo ndukuikizani mmapemphero

  • @FatimaMia-l1n
    @FatimaMia-l1n 7 місяців тому

    Mulungu achitilen chifundo

  • @EricCanada-ig9xe
    @EricCanada-ig9xe 5 місяців тому

    😭😭😭😭😭😭 nooooooooo

  • @Florencemaband
    @Florencemaband 7 місяців тому

    Mulungu a hitless çhifundo

  • @JoyceBAllubi
    @JoyceBAllubi 7 місяців тому

    Ambuye mulowelelepo nkhudzeni mwana wanu

  • @andrewtchuwa5368
    @andrewtchuwa5368 7 місяців тому

    Ambuye awachitile chifundo

  • @ShownyYohane
    @ShownyYohane 6 місяців тому

    So sad 😭,

  • @RhodaKalumbi
    @RhodaKalumbi 7 місяців тому

    Ambuye ndiwabwino akuona nyengo zanu asisi

  • @rachelkaunda-sj2xe
    @rachelkaunda-sj2xe 7 місяців тому

    May God see this woman through

  • @TelezaLuka
    @TelezaLuka 7 місяців тому

    Mmmmm life

  • @NaduMbewe-zz6iw
    @NaduMbewe-zz6iw 7 місяців тому

    Pepani mai wanga

  • @SibonisiweThole
    @SibonisiweThole 7 місяців тому

    God heip our sister

  • @AleksaWilliams-qc6cn
    @AleksaWilliams-qc6cn 7 місяців тому

    Mulungu awankhunze amayiwa,mmh alipa ululu mayiwa

  • @DoreemSemu-ho3lt
    @DoreemSemu-ho3lt 7 місяців тому

    Ndamva chisoni😭😭

  • @PaulDiness
    @PaulDiness 7 місяців тому

    😢Mulungu mukhuzen mai uyu

  • @SalomeuniqueBengoh
    @SalomeuniqueBengoh 2 місяці тому

    God have mercy on her

  • @atipatsamada1127
    @atipatsamada1127 7 місяців тому

    Zonvesa chisoni

  • @Zamwano
    @Zamwano 7 місяців тому

    Ambuye atichitire chifundo Mai wathu akhale bwino

  • @NaomiMoyo-x2r
    @NaomiMoyo-x2r 7 місяців тому

    My God mmmmmmm ambuye chonde