Ndi zoona wanthu ambiri sakufa akuma phedwa ndi asatanic m'modzi wa iwo ndi INE inenso ndinaphedwa koma ndina zuka koma munali mu 2015 moti m'mene ndina zukira kunyumba kwa achibale ku Malawiko sindinabwere ndikuopa Kuti mwina achibale sangandirandire koma panopa ndiri ndi Wana awiri chidzukire ineyo ambuye yesu akandithandiza ndizafika kunyumba chifukwa ndina chosedwa kumeneko ndi Wanthu wena awiri woyera mpakana pano wa nthu anandi chosa kumeneko amabwera mpakana pano ndimacheza nawo dziko Lino lapansi likudabwisa kwambiri pempherani kwambiri ambuye yesu afika nthawi iriyonse nanga m'mene ndiriri ine munga ndiziwe kuti ndine odzuka panopa ndiri ku Mozambique malire ndi zimbabwe kunyumba ndiku Mulanje kwa nkanda ku kambenje
Abare Kodi busayo ndingapeze bwanji abare ndiarogo mwaambuye chonde ndithandizeni
Great work prophet❤🎉
Tolo
Thoko😅
Anthu awawa anazonzedwa ndi ukulu wa Mulungu.. si azibusa ongofuna kunjoya mmacarpet wa....
Pano zithu sizili bwino ndimakhala ndikuva nkhani zimenezi kwambiri chomwe chimandipasa kulimba mtima kuti ndizoona ndithu ndipo satana akugwilisa ntchito anthu oipa mtima awa kumaononga miyoyo ya anthu kumalimisa muminda.Ambuye atichitire chifundo kwambiri
Anakakhala azibusa ena bwezi Ali pa screen mulungu apitilize kuwakhuza abusa in Jesus Christ
Ukulu wa Mulungu tauona
Mpimpimpi!!!!!mwabisapo chani a Zulanga....mesa mufuna anthu tidzidziwa chilungamo 😅😅😂
😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂 kma ndaseka
Too bad. The name of the Lord is a strong tower
Azibusa ngat awa mulungu azipitiliza kuwadalisa
Nkhani ndi yakuti mulungu wakwiya
Zamphavu 🙏👏 prophet
Ndingampedzeko bwanji mbusa amenei?
Ukulu wambuye uwonekere afiti ayaluke sambitu kumampha makolo anzawo
Eish zovesa chisoni kwambiri
Ambuye akantheni afiti on se dziko lilongosoke
So sad alot of our relatives akugwilitsidwa ukapolo somewhere ife kumat anamwalila😢😢
Akafukule manda akapange check ngati mafupa palibed
It happened in Zambia twice
Nope, it's happened in Zambia more than seven times 'just on TV' about 5-7 years ago...and many more times in the rural areas...
Blassa semanal agovati ndi agedo
Nde mabeluwo kut zinveke bwanji ukubisa chani aaaaa kangaude watani kod😮
Asakhale anyamata okhwima awa akanafukula mpaka pansi to prove that A = B
Aaaa bwanji simunafukule kumaliza mpaka kupeza bokosi kuti muone ngati mafupa alipo
Adzibale anga.nsanje to chitipa kwainu nonse mukumapanga masalamusi amenewa kodi mumafuna kuti mupedze chani ? Kodi umakhala umphawi ? kapena kukhwima ? Tiyeni tiyike chikhulupiliro chathu pa mulungu tiyeni tigwire ntchito ndikumapempha kwa mulungu zomwe tikufuna koma tisamafike mpaka pomapha nzanthu muchifukwa chofuna kukhupuka kodi zimenezi kwainu mwapanga idzi zikanakhala kuti mwachitidwa inu kapena mwana wanu mukanamva bwanji ? Nchitidwe uwu utheretu kumalawi inu mukupha anzanu inuyo ndiye mudzapita kuti ? 😂😂😂😂
koma akutipweteka anthu wokupha azawowo because amatitengera anthu wotitimawadalira andipaseko namba prophet please
Ndipo ineyo ndipemphero Langa Kwa onse akupanga nchiiiitidwe opha anzawou adzafe mozinzika.ndili munyengo zomwezi nane Ambuye andochitire chifundo Mwana wanga azauke,🙏
Ndi zoona wanthu ambiri sakufa akuma phedwa ndi asatanic m'modzi wa iwo ndi INE inenso ndinaphedwa koma ndina zuka koma munali mu 2015 moti m'mene ndina zukira kunyumba kwa achibale ku Malawiko sindinabwere ndikuopa Kuti mwina achibale sangandirandire koma panopa ndiri ndi Wana awiri chidzukire ineyo ambuye yesu akandithandiza ndizafika kunyumba chifukwa ndina chosedwa kumeneko ndi Wanthu wena awiri woyera mpakana pano wa nthu anandi chosa kumeneko amabwera mpakana pano ndimacheza nawo dziko Lino lapansi likudabwisa kwambiri pempherani kwambiri ambuye yesu afika nthawi iriyonse nanga m'mene ndiriri ine munga ndiziwe kuti ndine odzuka panopa ndiri ku Mozambique malire ndi zimbabwe kunyumba ndiku Mulanje kwa nkanda ku kambenje
🙆🙆🙆🙆
Kkkkkkkkk km ase srias wava kkkkkk
Koma ambuye akuchitole. Chifundo mupite kwanu akakulandila
Akulu inu bwanji Nkhani yanuyo ndiyoopsa kwambiri osabwela poyela nayo bwanji
Ambuye alandile ulemu 🙏
Tikufuna busayo ndithu
ndikupephako namba ya pulofetiyo ndikupepha
Abel siyani kuliza ma bell 🔔 kubisa mawu ena Pano ndinyengo zoti zibisika za anthu tiziziwa basi
Koma anthu ndinu otamba Ana anjoka koma mulungu adzaweruza . Jehovah inu inu ndinu choonadi ndi moyo kazitikhululukirani machimo athu
Ati amangonda ngati edzi kulankhula kwabwanji uku
Amenewa NDE adzibusa a Mlungu not a "can I prophecy!)a busa a receive receive,ma agent a satanic ulaliki ukhare wa ndrama otsati wachipulumutso?
Taona nawo zikomo
Izi ndi zowona ndinaziwonapo ndi maso anga
Divine postmortem
Zaulendo uno tiona zithu
Kkkkkkkkk km ku Malawi gyz kuli ufuti
Lord have mercy
chifukwa chan anthu akungozuka ku Malawi kokha?
😂😂😂😂
Ndiye wina amvekele ufiti kulibe. Ur mad.
Choonde tipatseniko nambala yá openphererawo
Hy
Shame😢
M
Abusa achilungamo achochi akusowa tikungolimbana ndi ama jecket mtwn
😂😂 Paja timafera ma jekete... Koma awawa voice yawo ikuchita kumveka kuti ndi a prophet di
😂😂😂😂
Family imeneyi kuli Anthu ochepa pakufunika afufuze bwino kwambiri munthu akupanga zimenezo aziwike
Number ya abelo pls pls ol ya abusa
Gati mwaipeza number chonde tigawireni number yabusawo
Zomvesa chisoni kwambili
Chonde chonde ine kwathu ku Mangochi ndikufuna phone number ya abusa wo please ndili ndi mavutho nso ine yo
Ineso ndikuifuna ngati munaipeza please share
Abelo ukutiona kupusa