Omwalira apezeka wa moyo

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 2 вер 2023

КОМЕНТАРІ • 67

  • @SaidShop-nf3qu
    @SaidShop-nf3qu 3 місяці тому +3

    Abare Kodi busayo ndingapeze bwanji abare ndiarogo mwaambuye chonde ndithandizeni

  • @user-eu9xe6wl8b
    @user-eu9xe6wl8b 9 місяців тому +1

    Great work prophet❤🎉

  • @tonyteixeira2463
    @tonyteixeira2463 День тому

    Tolo
    Thoko😅

  • @nimrodkapingatheu5475
    @nimrodkapingatheu5475 9 днів тому

    Anthu awawa anazonzedwa ndi ukulu wa Mulungu.. si azibusa ongofuna kunjoya mmacarpet wa....

  • @user-yy6rj5lc4i
    @user-yy6rj5lc4i 10 місяців тому +3

    Pano zithu sizili bwino ndimakhala ndikuva nkhani zimenezi kwambiri chomwe chimandipasa kulimba mtima kuti ndizoona ndithu ndipo satana akugwilisa ntchito anthu oipa mtima awa kumaononga miyoyo ya anthu kumalimisa muminda.Ambuye atichitire chifundo kwambiri

  • @hawabanda-xs5fx
    @hawabanda-xs5fx 9 місяців тому +2

    Anakakhala azibusa ena bwezi Ali pa screen mulungu apitilize kuwakhuza abusa in Jesus Christ

  • @BdhfbHdhe-pd7nh
    @BdhfbHdhe-pd7nh 10 місяців тому +3

    Ukulu wa Mulungu tauona

  • @IvvyMakuluni
    @IvvyMakuluni 10 місяців тому +1

    Mpimpimpi!!!!!mwabisapo chani a Zulanga....mesa mufuna anthu tidzidziwa chilungamo 😅😅😂

    • @user-lc7ji1gn9w
      @user-lc7ji1gn9w 10 місяців тому

      😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂 kma ndaseka

  • @user-lz1ry1sm4j
    @user-lz1ry1sm4j 7 місяців тому +1

    Too bad. The name of the Lord is a strong tower

  • @richsambakusi424
    @richsambakusi424 9 місяців тому +1

    Azibusa ngat awa mulungu azipitiliza kuwadalisa

  • @user-rv8gi4ro6r
    @user-rv8gi4ro6r 10 місяців тому +2

    Nkhani ndi yakuti mulungu wakwiya

  • @MadalitsoHope
    @MadalitsoHope 8 місяців тому

    Zamphavu 🙏👏 prophet

  • @CatherineDesire
    @CatherineDesire 13 днів тому

    Ndingampedzeko bwanji mbusa amenei?

  • @collinstrevor
    @collinstrevor 10 місяців тому +1

    Ukulu wambuye uwonekere afiti ayaluke sambitu kumampha makolo anzawo

  • @MussaIbla
    @MussaIbla 10 місяців тому +1

    Eish zovesa chisoni kwambiri

  • @esthermakwinja3207
    @esthermakwinja3207 10 місяців тому +1

    Ambuye akantheni afiti on se dziko lilongosoke

  • @JosophineSolobala-hp5ds
    @JosophineSolobala-hp5ds 4 місяці тому

    So sad alot of our relatives akugwilitsidwa ukapolo somewhere ife kumat anamwalila😢😢

  • @BaxterChipofya
    @BaxterChipofya Місяць тому

    Akafukule manda akapange check ngati mafupa palibed

  • @rachealphiri3416
    @rachealphiri3416 10 місяців тому +3

    It happened in Zambia twice

    • @ephraimphiri5789
      @ephraimphiri5789 9 місяців тому

      Nope, it's happened in Zambia more than seven times 'just on TV' about 5-7 years ago...and many more times in the rural areas...

  • @CostaCasimiro
    @CostaCasimiro 7 місяців тому

    Blassa semanal agovati ndi agedo

  • @user-lc7ji1gn9w
    @user-lc7ji1gn9w 10 місяців тому

    Nde mabeluwo kut zinveke bwanji ukubisa chani aaaaa kangaude watani kod😮

  • @BaxterChipofya
    @BaxterChipofya Місяць тому

    Asakhale anyamata okhwima awa akanafukula mpaka pansi to prove that A = B

  • @oswardmwale216
    @oswardmwale216 8 місяців тому

    Aaaa bwanji simunafukule kumaliza mpaka kupeza bokosi kuti muone ngati mafupa alipo

  • @JohnChibalo-wf8gr
    @JohnChibalo-wf8gr 10 місяців тому +3

    Adzibale anga.nsanje to chitipa kwainu nonse mukumapanga masalamusi amenewa kodi mumafuna kuti mupedze chani ? Kodi umakhala umphawi ? kapena kukhwima ? Tiyeni tiyike chikhulupiliro chathu pa mulungu tiyeni tigwire ntchito ndikumapempha kwa mulungu zomwe tikufuna koma tisamafike mpaka pomapha nzanthu muchifukwa chofuna kukhupuka kodi zimenezi kwainu mwapanga idzi zikanakhala kuti mwachitidwa inu kapena mwana wanu mukanamva bwanji ? Nchitidwe uwu utheretu kumalawi inu mukupha anzanu inuyo ndiye mudzapita kuti ? 😂😂😂😂

    • @josephnanyanga2012
      @josephnanyanga2012 7 місяців тому

      koma akutipweteka anthu wokupha azawowo because amatitengera anthu wotitimawadalira andipaseko namba prophet please

    • @user-zc9ku5fw4n
      @user-zc9ku5fw4n 5 місяців тому

      Ndipo ineyo ndipemphero Langa Kwa onse akupanga nchiiiitidwe opha anzawou adzafe mozinzika.ndili munyengo zomwezi nane Ambuye andochitire chifundo Mwana wanga azauke,🙏

  • @dondamissonchdziwe3958
    @dondamissonchdziwe3958 10 місяців тому +3

    Ndi zoona wanthu ambiri sakufa akuma phedwa ndi asatanic m'modzi wa iwo ndi INE inenso ndinaphedwa koma ndina zuka koma munali mu 2015 moti m'mene ndina zukira kunyumba kwa achibale ku Malawiko sindinabwere ndikuopa Kuti mwina achibale sangandirandire koma panopa ndiri ndi Wana awiri chidzukire ineyo ambuye yesu akandithandiza ndizafika kunyumba chifukwa ndina chosedwa kumeneko ndi Wanthu wena awiri woyera mpakana pano wa nthu anandi chosa kumeneko amabwera mpakana pano ndimacheza nawo dziko Lino lapansi likudabwisa kwambiri pempherani kwambiri ambuye yesu afika nthawi iriyonse nanga m'mene ndiriri ine munga ndiziwe kuti ndine odzuka panopa ndiri ku Mozambique malire ndi zimbabwe kunyumba ndiku Mulanje kwa nkanda ku kambenje

    • @peterbakuwo1249
      @peterbakuwo1249 10 місяців тому

      🙆🙆🙆🙆

    • @adamusaidih8570
      @adamusaidih8570 10 місяців тому

      Kkkkkkkkk km ase srias wava kkkkkk

    • @oliviaolivia4979
      @oliviaolivia4979 10 місяців тому

      Koma ambuye akuchitole. Chifundo mupite kwanu akakulandila

    • @mbawabuliyan9704
      @mbawabuliyan9704 10 місяців тому +1

      Akulu inu bwanji Nkhani yanuyo ndiyoopsa kwambiri osabwela poyela nayo bwanji

    • @florencebonga3211
      @florencebonga3211 10 місяців тому

      Ambuye alandile ulemu 🙏

  • @JusticeMakwinja
    @JusticeMakwinja 2 місяці тому

    Tikufuna busayo ndithu

  • @josephnanyanga2012
    @josephnanyanga2012 7 місяців тому +1

    ndikupephako namba ya pulofetiyo ndikupepha

  • @mordecaikachale2497
    @mordecaikachale2497 10 місяців тому +2

    Abel siyani kuliza ma bell 🔔 kubisa mawu ena Pano ndinyengo zoti zibisika za anthu tiziziwa basi

  • @BlessingsBanda-qn7xr
    @BlessingsBanda-qn7xr 10 місяців тому

    Koma anthu ndinu otamba Ana anjoka koma mulungu adzaweruza . Jehovah inu inu ndinu choonadi ndi moyo kazitikhululukirani machimo athu

  • @ChisomoKapanda-jg2uf
    @ChisomoKapanda-jg2uf 10 місяців тому

    Ati amangonda ngati edzi kulankhula kwabwanji uku

  • @CatherineDesire
    @CatherineDesire 13 днів тому

    Amenewa NDE adzibusa a Mlungu not a "can I prophecy!)a busa a receive receive,ma agent a satanic ulaliki ukhare wa ndrama otsati wachipulumutso?

  • @user-dt8nr1zx6e
    @user-dt8nr1zx6e 10 місяців тому

    Taona nawo zikomo

  • @user-zk5nu5fh6l
    @user-zk5nu5fh6l 10 місяців тому

    Izi ndi zowona ndinaziwonapo ndi maso anga

  • @liki-likiladies---lilongwe6963
    @liki-likiladies---lilongwe6963 10 місяців тому +1

    Divine postmortem

  • @marthacassam
    @marthacassam 9 місяців тому

    Zaulendo uno tiona zithu

  • @adamusaidih8570
    @adamusaidih8570 10 місяців тому

    Kkkkkkkkk km ku Malawi gyz kuli ufuti

  • @AmusedSakura-dx1nw
    @AmusedSakura-dx1nw 6 місяців тому

    Lord have mercy

  • @user-ek7vg7ld8h
    @user-ek7vg7ld8h 9 місяців тому

    chifukwa chan anthu akungozuka ku Malawi kokha?

  • @KINGMANMAKALA-hb9gs
    @KINGMANMAKALA-hb9gs 10 місяців тому

    😂😂😂😂

  • @mcsellahntv6896
    @mcsellahntv6896 10 місяців тому

    Ndiye wina amvekele ufiti kulibe. Ur mad.

  • @chimwemwemaquesuwell5841
    @chimwemwemaquesuwell5841 10 місяців тому +3

    Choonde tipatseniko nambala yá openphererawo

  • @YusufMolesi-vr4pn
    @YusufMolesi-vr4pn 10 місяців тому

    Hy

  • @AleksaWilliams-qc6cn
    @AleksaWilliams-qc6cn 10 місяців тому

    Shame😢

  • @AriohChauluka-lm9oo
    @AriohChauluka-lm9oo 9 місяців тому

    M

  • @hawabanda-xs5fx
    @hawabanda-xs5fx 9 місяців тому

    Abusa achilungamo achochi akusowa tikungolimbana ndi ama jecket mtwn

  • @mbawabuliyan9704
    @mbawabuliyan9704 10 місяців тому

    Family imeneyi kuli Anthu ochepa pakufunika afufuze bwino kwambiri munthu akupanga zimenezo aziwike

  • @user-ux8qz1tg7l
    @user-ux8qz1tg7l 10 місяців тому +1

    Number ya abelo pls pls ol ya abusa

    • @SaidShop-nf3qu
      @SaidShop-nf3qu 3 місяці тому

      Gati mwaipeza number chonde tigawireni number yabusawo

  • @patrickjaenda8288
    @patrickjaenda8288 10 місяців тому +1

    Zomvesa chisoni kwambili

  • @user-fq3jz4hl4c
    @user-fq3jz4hl4c 10 місяців тому +1

    Chonde chonde ine kwathu ku Mangochi ndikufuna phone number ya abusa wo please ndili ndi mavutho nso ine yo

  • @BdhfbHdhe-pd7nh
    @BdhfbHdhe-pd7nh 10 місяців тому

    Abelo ukutiona kupusa