Prophet Austin Liabunya: Chimene Chinapha a Chilima Cheni Cheni - Malawi Latest Prophecy (part 1)
Вставка
- Опубліковано 26 чер 2024
- Izi ndi zomwe anayankhula #ProphetAustinLiabunya:
-Chimene Chinapha Dr Chilima
-Explaining My Journey With Dr Chilima
-Mulungu Akuti Chani Pa Tsogolo La Malawi
-Zimene Mulungu Akufuna Dr Laz Achite Kuti Atengenso Boma Mu 2025
-Umboni Wanga Pa Mphekesera Za Kumangidwa.
-Ndi Nkhani Zina Zambiri..
Chilima sanaphedwe thaw unamukwanila
PALI NGOZI YAIKULU, KUSIYA ZA YESU KUYAMBA KUTUMIKILA ZA NDALE,
Only God knows,may the souls of our beloved ones rest in peace
Mulungu akukhululukireni Man
Mbuzi ya munthu, mulungu wasala pangono kt akutopele,
Ok prophert of God
Mulungu adzachilangaichi
Tayankhula zomveka iwe ukuti chani kwenikweni
Kod mulungu wake ndi wa major 1 kod panopa mulungu amangonena zandale
Koma zoti chilima wachita kuphedwa ndi chakwera simukunena bwanji
Komatu iwe
Ndiopenga akufunika mankwala
Milungu ndi yambiri. Ina imamuwuzadi munthu zimene akunenazi. Pajatu satana ndi mulungunso wa dziko lino.
Mulungu wathu satenga mbali mu ufumu uwu wa kumapazi kapene kuti ufumu wa chilombo chopanda dzina
Koma ngati ndizedidi zimene mukuka.bazo kt mudapanga prophesy kt atuluke Avice president mu tose alliance ndiye kt mudolosera chifukwatu adadfa imfa yowawako.aso yosaiwalika
Tizikasaka ma Post amiyezi imeneyo, koma tigwira ntchito?
😂😂😂
😮
Komano ineyo zomwe mukufuna kunena, sindikuvetsa kuti mufuna kunena kuti chani.
Kape uyu osauka akuona ngati atola chikwama oputsa uyu
Iwe ASE usamasewele ndimulungu mulungu si abambo ako chonde chonde usamana ize anthu kuzela kwamulungu musiyeni mulungu akhale mulungu ,,,,tchito zaboma zimafanana ndindale ngati wasata zaziko wasephana ndimulungu man musatichimwise,,Kodi mulungu akuuze iwe ndindani iwe baibulo lake liti
Chilima penapake anali wamwano born kalindo wakhala akunena
I saw your prophecy they is no that condition pliz and you say it with confidence that chilima Will be a president,,chonde venselani kwa mulungu osalankhala za mumaganizo anu
Ndikufuseni mukutumikila utitiuti Mulungu wake 🤔
Your are operating under the power of money
Aaaaaa
🙄
Is good to look something to do not to lies to the people that your poster Kodi ubusa wanji ongokamba zandale
Now you stop preaching jesus .everyday stories we arw tired
Achibale a munthu uyu chonde mutengereni ku mental hospital.
Am crc.
Kodi satana uyu. Ndindani siyeni chilima mzimu wake uuse muntendele
Vomelezani kuti mwaphonya prophecy,false prophet exposed in false prophecy.
It seems like this MAN don’t know what he is saying. “Everything is I think “
Yea, I also noted that. U know the reason? Here, the repeated use of 'I think' is due to his reluctance in mid speach to divulge what he realy knows. So he is trying to remain calm, careful, and at the same time, inoffensive.
YOU DON'T KNOW WHAT YOU PREACHING.
DZIKOMO MULUNGU MWANDIONESA ANENELI ONYENGA.
Sir you don't know how to communicate or deliver, God is not using you because we can't get you at any point
Most of poster they busy to lies
False Prophet in the last days,repent & turn to God.Kufuna kutchuka eti,tisiyeni tikulira maliro ife.SKC RIP😭
He is not a man of God manof chakwera
Musakambe ngati Mulungu ndi brother wanu, that accident was very painful to everyone get something to get famous with, what you are saying is just nonsense remember this CHILIKWANZAKO CHIGWIRE NYANGA you will remember this proverb , Mark my words. Musagwiritse ntchito dzina la Mulungu pachabe.
Aaaa kaya mwina enanu mukumva ine ndepalibe nditolaine