Ndikukhulupira kut Mr President wakhutisidwa ndiripotiyi. Koma ndinakakhala ine ndikanafuna mudziwa 1. Anapopa magazi mkodzo ndi màlovui awanthuwa ndani and why 2.kodi ànaendesa ndege kukasia thupi 17:10 ku nkhatabay y a kasambala ndi ndan
Kafukufuku wa ndege popanda black box palibe chimene chingadziwike. Uku ndi kupusisana chabe. The whole inquiry report tikumva kuti palibe olo point imodzi yokhuza black box why?
@@TrizaGeorge-q8w mukuwapatsa mwayi kod ndichifukwa chiyani a kubanja kwa kasambala amati sakweraso ndege pobwerera mesa anaona kt sanayende bwinobwino inu kakaka kupambana a kubanja amalawi koma
AND LIMPOPO FM WITH COMRAD NTANYIWA HAS DISCLOSED THAT @ BLACK BOX A CHAKWERA NDI NDUNA ZAO AKALISUNGAKU KASÙNGU .KU NYUMBA YA KAMUZU .YA NGULI YA NAWAMBE*** PAMODZI NDI MAVOTE OMWE A MCP ABERA KALE AJA NDI MEC NDI NRB
Kodi a chakwera chikuvuta ndichani kungotula pansi udindo? Feteleza k108,000, chimanga thumba k50,000, report ya covid 19 6 billion simunamange munthu, ma xul fees kudula, ma passport afegi, mec yafeg, NRB ya feg, No smartmatik 2025 let's count one by one.finally this is one of the worst goverment than ever
Mafunso adakali, black box ili kuti, anthu onse ofunika kufunsidwa did they give evidence ie the president & his team? If not, this investigation is yet to start
Koma dziko ili zoona akatiuze kuti oyendesa ndege analekerera mmmm kulakwira mizimu, achibare ndi a Malawi. Atiuze chomwe chimazunguza ndikupotoza ndege mmwamba
Kodi iwe George chaponda vuto lako ndi chiyani palibe chimene wukuchita ku parliament ko angakhale kwanu kumene wukuchokera ukukanika kumanga mulatho kwanuko you're not fit to be opposition leader.
Asazivute ndi kufufuza mitima yathu idafufuza kale okhudzidwa tikunziwa chigamulo pa 16 september nyengo yoipa kkkkkk km yaaah mukusewera ndi mulungu muziona
Kodi papita dzaka dzingati nkhalangoyi ilipo ndege sizimadutsa dela limeneli? koma Black box anachotsa ndindani pakuti munalibe ndipo mpaka pano Black box mulibe mu ndegemo
Abale maganizo anthu siomwe ali mulipotilo ifeyo tisunge maganizo anthuwa bcoz mwai oti tipite tikapereke maganizo anthu unalipo palibe anaipitako kukanena zomwe ifeyo timafuna kuti zikhale mu repotilo kuti likhale loona sibwino amalawi tiphunzire kugwiritsa ntchito mwai omwe tapasaidwa ndipo amachita kunenesa kuti amene akuziwapo zangoziyo apite akafotokoze koma inuyo ndi ine sitinapiteko it will be of no use kumalubwanso apapa imfa ija inatililisa ambiri bcoz its first of this kind mu democracy ndiye otsutsa olamula aliyense zinamukhuza ndithu
Let Njawala commission his party's Commission of Inquiry for the plane tragedy. He seemingly has some special interest apart from what we as Malawians have been informed on the catastrophe.
Amene anayimisa kusaka NDENGE ndani.
MKULU Wa aisirikali ayankhe
Adayichotsa black box ndindani tipemphere kwambri zidziwika in name of Jesus🙏🙏
😊😊😊😊😊😊😊😊
Manyi a report awa , tizapanga inquiry MCP ikazachoka m'boma Chaka cha mawa, onse okhudzidwa azamangidwa including amene anapanga kafukufuku ameneyu.
Ndikukhulupira kut Mr President wakhutisidwa ndiripotiyi. Koma ndinakakhala ine ndikanafuna mudziwa
1. Anapopa magazi mkodzo ndi màlovui awanthuwa ndani and why
2.kodi ànaendesa ndege kukasia thupi 17:10 ku nkhatabay y a kasambala ndi ndan
Nanu tangopelekani black box bsi
Kafukufuku wa ndege popanda black box palibe chimene chingadziwike. Uku ndi kupusisana chabe. The whole inquiry report tikumva kuti palibe olo point imodzi yokhuza black box why?
Basi black box nde dilu
Inenso sindikukhutira za report yi! Mumufune oti muzimunamizayo anthu akupha inu!!!
tikufuna black box basi palibe zoyakhula apa zonse zomwe mukuyakhula APA ndi zamanyi
Inu ndege munthu kugwa ingamuvule munthu zovala ?? Aaaaaaa guys mudzikhala serious
Chakwela chimwendo kukuyu zikhale ng,oma ndinu afiti koma mulungu akukathani posachedwa
@@TrizaGeorge-q8w mukuwapatsa mwayi kod ndichifukwa chiyani a kubanja kwa kasambala amati sakweraso ndege pobwerera mesa anaona kt sanayende bwinobwino inu kakaka kupambana a kubanja amalawi koma
AND LIMPOPO FM WITH COMRAD NTANYIWA HAS DISCLOSED THAT @ BLACK BOX A CHAKWERA NDI NDUNA ZAO AKALISUNGAKU KASÙNGU .KU NYUMBA YA KAMUZU .YA NGULI YA NAWAMBE*** PAMODZI NDI MAVOTE OMWE A MCP ABERA KALE AJA NDI MEC NDI NRB
Nthawi zonse timaganiza kuti imfa ikachitika wina alowesapo zanja lake awa ndimabvuto kwathu kumalawi
Kod ndege yo imayenda pansi mwina bwanji mkut nyengo siinalibwino mkhalango, itafika mkhalangomo inasikira pansi, ngat nyengo siinali bwino bwanji anakakamira kupita
Tien tizilankhula zomveka coz ndege siyingaende bwino pamene mphepo silibwino pamalopo ai Tien tiwamvetsele chilungamo chioneka
Ndege yanji yochosa magazi awathu 💔😭😭😭😭
Apapa ife ngati amarawi tikusogoreredwa ndi mbusa amene usogoreriwo muribemo tsoka rarikuru romwe tiri naro ngati amarawi
Eish
Nonse amene mukupelekera umboni wa report la bodzali mudziwe kuti muli gulu la anthu omwe anapha Chilima ndi anthu 8 ku Chikangawa ndipo Mulungu achita nanu kanthu. Nthawi yanu izakwana popeza iye Mulungu sachedwa komanso safulumira la 40 lizakwana.
Ndimakhara ine bare wanga ndingawsthsmangitse kusekerera zopusaxo
Ngt akwawo alola ndizazizi ndeine mkachaniso anthu andalama salilana coz amaona thumba landalama
Ayi osanyanyala they know better kuti olo akane zomwe aboma akupanga or kupereka palibe chomwe angaphule cz boma ndiboma and sakufuna kuwonetsera mkwiyo wao but let's wait tikasintha boma 2025 September adzawaonetsa awa 😅😅
So black box ilikut
Kodi a chakwera chikuvuta ndichani kungotula pansi udindo? Feteleza k108,000, chimanga thumba k50,000, report ya covid 19 6 billion simunamange munthu, ma xul fees kudula, ma passport afegi, mec yafeg, NRB ya feg, No smartmatik 2025 let's count one by one.finally this is one of the worst goverment than ever
Kwinako tiyeni timusiyire Yehova, Mulungu wathu okhala kumwamba, zikomo.
Za zii apanga bwanji kafukufuku wa ndege popanda black box? Ndinakakhala ine ndikanangoling'amba cifukwa ndiyabodza.
Eti eti zoona zimenezi mxi
Kumwamba kuil mulungu tikalangidwa ndinthu
Mmmmmmmm chilungamo akuchiziwa ndi mulungu
😊😊😊😊😊😊😊😊😊
😮😮😮
Ai akuchidziwa ndi ndi Mr chikangawa Dr lazi
Zonsezi ndi chabe cz mukunena umboni akumva, black box ili kuti Mr kumkuyu???? Black box ndiyokhayo yomwe anganene zenizeni. 😢😢😢
Zoona uyu anayankhula kale kuti ilipo ikusungidwa
Ngat president zisakumukhuza za ngozi apeleke black box basi ndizomwe amalawi akufuna kuti tiziwe chilubgamochake cha ngoziyi
Tikufuna black box nkhaniyatha
komaso. ifengati amalawi lipoti limenelo sitingave. ndege. akuvule.munthu sapato. komaso. inutu munena bwino sitikusiyani. lipoti limenelo abesele. makafe ndichimwenda zachambazo usatiuza zopusazo .anthu munapha.bass.zopusazo..ndege paka imaba ndalama paka kuba bulaki box. inu. zisilu .anthu sakusiyani munya ..anthu okuba ndipha
Iwowo chilungamo achitenga kuti popanda blackbox zaufiti mukhale tu muli inu achakwera akwanu tiziwanamiza choncho
Ikufunika black box ituluke please kumpando
Chomwe munabisila Black Box ndi chiyani?
Ndipo akusunga black box ndi ndani?
Report it nde ayi..bwanji simunalole kuti ma banja oferedwa onse akhalepo
Umbuli kuuika poyela, mu commission of inquiry simakhala achibale aokhudzidwa , vuto umbuli😏
Tachokani apa nanu@@Eliezer-vg1nx
Komanso senior chief Makwangwala wa kwao kwa malemu anali konko mumafuna kuti mkazi wake akakhale kumeneko. Imfa mumaidziwa chotsani umbuli
Apo amafunika aku MDF ena achosedwe tchito or amangidwe anakanika kugwila tchito yawo, komaso president anatipasa report yabodza ngozi itangochitina kumene, komaso atipase evidence yomwe wako airport amayakhulana ndiwamu ndege powafusa zanjila yomwe adusa, n why anayamba kufufuza mochedwa n anaima kaye kufufuza. They told us kut black box ilipo zonse tinva kma pano anatiuza kut inali yoonongeka. Mafuso ndiambili coz sitikuonapo research yanzelu apa. Timaona ma report amzathu mmene amakhalila osati zathuzi
Mcp sizava koma dpp ndi Bomba likafun kulowa bama wina amagulisa chithu joice amagulisa ndege naye chakwela wagulisa lake ndiye dpp ikulowaso
Like a dream when you say chilima died
Iwe kunkuyu don't think that is 1950
Mafunso adakali, black box ili kuti, anthu onse ofunika kufunsidwa did they give evidence ie the president & his team? If not, this investigation is yet to start
ZBS yafika pa manyaka...mpaka kulephera kuwerenga nkhan😅
Mulungu akuoneni akuluakulu ndiboza limene mwanamiza amalawi.
Report li muli be umboni wenwen wapa ground kod black box inja akati idasungidwa bwanji sadakambeko?
Koma dziko ili zoona akatiuze kuti oyendesa ndege analekerera mmmm kulakwira mizimu, achibare ndi a Malawi. Atiuze chomwe chimazunguza ndikupotoza ndege mmwamba
Kodi iwe George chaponda vuto lako ndi chiyani palibe chimene wukuchita ku parliament ko angakhale kwanu kumene wukuchokera ukukanika kumanga mulatho kwanuko you're not fit to be opposition leader.
Brack box ilikuti?
Opanda black box we ll not agree with inquiry
Koma guys ku Malawi ndiye basi sikuzathekasoyi ndithu palibe obwela poyela mkulifusa or Boma ngati akhuthila ndi report lomwe lapangidwa popanda Black Box,,,kodi zoti oyendetsa ndegeyo analephela kuyendatsa bwino anadziwa bwanji popanda Black Box,,,,koma ndithu basi zatha izi eeee komaso malawi
Tili munyengo ya Kunkuyu ndi Alide referee wake Chimwendo
Nchifukwa CHANI nthawizonse pakachitikazinthu zipani zotsutsa zimakonda kugwiritsa ntchito MAU oti A MALAWI AMBIRI akuti. Bwanji osanena zayiweyo ngati munthu ?
China AID kumafotokozera
Asazivute ndi kufufuza mitima yathu idafufuza kale okhudzidwa tikunziwa chigamulo pa 16 september nyengo yoipa kkkkkk km yaaah mukusewera ndi mulungu muziona
Who did they consult? Nanga mlonda uja adatinji
Ni chifukwa chiyani mundege munalibe wa mcp
Kodi nyengo yoyipayo idanena ndi black box nanga mukuti panali kulekelela analekelela bwanji
amene,munkadziwa,box,simunapite,komweko,lelp,mukutsutsa,pa,4nzitanthauza,chiyani,musati,pusise,
Anthu woyipa inu ndipo nonse mwafufuza muzayankhanso, ngati sipansi pano kapena kwa Mulungu.
Vuto la mafuta simungalithe inu, mesa nthawi ya PM linalipo kare?
Umboni uli mu black box. Where is the black box?
Kodi papita dzaka dzingati nkhalangoyi ilipo ndege sizimadutsa dela limeneli? koma Black box anachotsa ndindani pakuti munalibe ndipo mpaka pano Black box mulibe mu ndegemo
Bvuto lathu ndilakuti timadziwa kuyankhula kwambiri kuganiza pang'ono ili ndi buto ku dziko lathu.
Report imeneyi,ine sindikugwirizana nalo,ndi report yabodza yokomera chitsirucho
Liport la manyi lmeneyi report lenileni likubwela next year 2025
Thawi ndi nyengo ikwana
Kodi agalu amenewa akuziwa bwanji kuti woyendesa ndegeyo adatayilila zamanyi bc tangopelekani black bokos
ife,sitikufuna,kupenpha,mavoti,paifa,yachilima,ingoliuzani,dziko,umboni,wanuwo,,ndikunena,tsogolo,yamilanduyi,kt,iyenda,bwanji,osamango,tsutsa,zipindula,chiyani,
Kutseka pakamwa Kwa Amalawi sikuti ndi anthu osaganiza ayi koma kuganiza mozama monga anthu oganiza bwino
Black box mudakasungabe? Nanga mlonda uja anasowanso?
Zanziiiiii report yabodza ngati imeneyo
Bwanji utm ipangiseso wao kafukufuku popeza akafukufuku enawa sakukwanira kwa iwowa
Amene watulusa report limeneli ndi mbuli kwambili komanso samapemphela ndikukhulupililanso kuti kwao kulibeko anthu oti azafa
Izi nde zapatumbo izi nde munena bwanji zimenezo pomwe black box palibe muzanya mukachopa boma
Black box basitu ndiye chida chokhazikitsa bata
Mufufuza bwanji opanda black box mcp chikangawa party
Dziko ndi anthu akee.....
Nkhani iyi,siyoitengela maso m'mwamba,...Zufunika olimba mtima ndi oopadi Mulungu
Kunkuyu naye sangatiuze zopoila ,report lakwawo limenelo
Abale maganizo anthu siomwe ali mulipotilo ifeyo tisunge maganizo anthuwa bcoz mwai oti tipite tikapereke maganizo anthu unalipo palibe anaipitako kukanena zomwe ifeyo timafuna kuti zikhale mu repotilo kuti likhale loona sibwino amalawi tiphunzire kugwiritsa ntchito mwai omwe tapasaidwa ndipo amachita kunenesa kuti amene akuziwapo zangoziyo apite akafotokoze koma inuyo ndi ine sitinapiteko it will be of no use kumalubwanso apapa imfa ija inatililisa ambiri bcoz its first of this kind mu democracy ndiye otsutsa olamula aliyense zinamukhuza ndithu
Mumafuna muthu akapita kukanena chilungamo akamuphe uweso kapena eti ndati nose mumaikila kumbuyo boma lakuphali muli ndi tsoka lalikulu kwambili ndipo simuzapeza m, tendele
Amalaw mulipavuto president wanu sakunena zoveka
Inu mmafunsa okhao amene amaikira kumbuyo MCP komanso inu munadya zophuphu
Ndipo simmayenela kuitanitsa anthu pa umboni koma chidule black box ibwele ituudza yokha mmene zinayendela
Ajawala atiuze paja god papa analipo ndi gawo mwina atiuza ndi a utm
Zaziii ana anjoka dziko ndi laling'ono zizatuluka mulungu simunrhu musathe mau
Komano nanu muzilembe bwino eee okapeleka report la ndege zomwe akumana nazo ndi mai chilima panja peni peni
Yaa, tamuwuza munthu amene anapangayo kuti azikhala serious. tikonza kusogoloku
akhala,akufufuza,,zandege,masiku,ambili,km,inuyo,,osakapeleka,zomwe,mukuzidziwazo,bwanji,lelo,nkumatsutsa,,amalawi,aveziti,
Ikanakhala nthawi ya nyasaland anthu akanakhulupilira koma ma last Born sangakhulupilire
Tikudikila clip yomwe inajambulidwa
amalawi,akudikila,inu,amene,mukutsutsa,kt,mukalengezetse,pawayilesi,ndipamene,timava,zowona,zenizeni,osati,pa,4n,ayi
Nde akumabanjawo alandira nyasizo?ngati ndicomco tu n ndekuti akuvomerezano nazo za report yo cos sanayenereka kutero
Uku nkupepela kwambili kuona amalawi uchitsilu za ziiiiiiiiii
chaka cha mawa sikale choona tizaziwa @fter votes
Kodi inu a utm simukunvetsa pati nanga inu a utm za abuleya lure mukutinazo bwanji tiwuzeni a njawala
Nyasi zanu za report fusek nonse munalo mu report limeneli tidzava black boxs ikabwela poyela komwe mudakabisako agalu inu
kafukufuku wa mkabudura zachamba
Mitumbo yanu nose bwanji simutulutsa black box mubisilanji
Zaugalu basi kd iwe nkukuyu mesa ukt black box ili Malo abwino tabwelesano ikufunika
Mukaba tiziwa ine chiudzu ema@dontcome
Tikufuna black box
Ngozi ya ndenge amafufuza kopanda black box kondowe ndiwe mutumbu opanda nzeru
Chakwera wa kupha uyu uzampeza nzako
Why do you use strange voice instead literal human voice?
Ok nyanja mwagurisa ku songeya ija mdarama zake nizimene mukupangira zopusazo
Let Njawala commission his party's Commission of Inquiry for the plane tragedy. He seemingly has some special interest apart from what we as Malawians have been informed on the catastrophe.
Km mene inarili ngodzi ija mayakho ake akukhara amenewa mulungu Ali nafe😢😢
et et
Akuntundu abwenze mapepara amenewo.akasumire amapanga kafukufukuyo