LUCIUS BANDA EXCLUSIVEINTERVIEW - 20 MAY 2021
Вставка
- Опубліковано 23 тра 2021
- Banja la a Banda likukumana ndi mavuto pamene anthu angapo akudwala. Lucius Banda wakhala akudwala matenda a impsyo kuyambila December 2020 ndipo wagonekedwa ku chipatala kuno ku Malawi komanso ku South Africa kwa masabata 6. Pano akulandira chilandiro cha dialysis ku Mwaiwathu Hospital. Mchimwene wake Sir Paul Banda naye akudwala matenda a impsyo omwewo ndipo akufunika akalandire impsyo ina ku India. Izi zikufunika ndalama zosachepela 30 million kwacha. Mu banja momwemo, Francis, mkulu wake wa Lucius (mng'ono wa Paul) akudwala cancer yotchedwa leukemia ndipo akulandira chemotherapy. Izi zapangitsa banjali kugwilitsa ntchito ndalama zochuluka ndipo anthu akufuna kwabwino akhala akusonkha ndalama kuti awathandize.
- Розваги
Pawer solder❤ndiwe ngwazi pamaimbidwe
Good to hear how strong your faith is....God is so faithful 🙏AMEN we are with you in prayers.
We will miss him
Get well soon Soldier and your fellow brothers, we love you
Am faith in God
Mlaka ndi more❤❤❤❤❤❤❤
May the healing hand of our Lord Jesus touch you and your brother's.
May God heal them
Uremuwanu mau aphavu
May God Almighty help them all in this hard time they are in.
I wish u all fast recovery, you brought me some inspirations thru music
Keep it up big
Get well soon farmilly
😊😊p😊😊
Za bwino zonse Lucius
Sorry for that my brother god please I’ll them in Blood off Jesus
We love you🙏
Zikomo mumatimilila
But am proud of you soldier, ndinu otchuka koma munakamanga maziko kumudzi kobadwa(Balaka)
May God heal you
Makhazi
Pawer solder❤ndiwe ngwazi pamaimbidwe
Mlaka ndi more❤❤❤❤❤❤❤
Pawer solder❤ndiwe ngwazi pamaimbidwe