Izizi zimakhala Zabodza , Zimangokhala zauchiwanda basi pena amakhala kt Wabwelayo wangokhala openga Chabe. It also happened ku Migowi zabodzazi but it ended up kt sanali m'bale wawo
You don't just post someone's face without his/her consent. You can be sued. I guess thats the reason. Komanso a councilor kufikila Popeleka umboni ndiye kuti ndi zoona..
Ine ndimaona ngati omwalirawo ndi awawa ...
Heading mumayika akufuna ma viewers et?
This lady councillor isa good story teller,I like her her narration.
Zaziii basi
Osati wauka koma wapezeka nthawi yodzuka anthu akufa sinakwane ameneyo anangozembetsedwa mumasenga
Wakufa samadzuka mayiwa Ali okwima aaaaa
Mamuna openera ameneyo, munthu akafa sadzukanso. Amapemperowo angomunamiza pomupasa mkazi wina.
Watching from Mfuwe Zambia
Thankyou hainifa pondifikisa mmuzi mwathu
Mwina anangosowesedwa m'masenga nkumakagwirisidwa ntchito eeh mulungu atipase chidziwiso
Aaaaaa zimenezo zikuchuluka hvy
EEE ayi uyuso atiopsa
Nanga zadress lomwe anavala akumwalira anaziwa bwanji😅
Chamba munthu adzafa ndi kuuka mmanda tsiku la chiweluso/kiyama ndiye izi zikuchitikazi zopanda umboni chifukwa ndiza ufiti owoneka ndi maso zomvera anthu opanda chipembezo chenicheni 😢
Amene sanaziwone amayankhul kwambil kt sizoona. Km apropheti alipo kunj kuno akupanga zodabwitsa zimenez taziwona ife
Iiii izi nde ndizoopsa asaaa sizoona ayi😢😢nde ndingathawe mmmm
Zephania from Zambia show the person ti s boza
Khani yopatsa chidwi zikomo man of god
Aaaa sanali akufa kom anangotekedwa mpweya
Izizi zimakhala Zabodza , Zimangokhala zauchiwanda basi pena amakhala kt Wabwelayo wangokhala openga Chabe. It also happened ku Migowi zabodzazi but it ended up kt sanali m'bale wawo
Sidziwanda koma asakhaletu opephelawo atumiza chiwanda chofananako ndimuthuyo
Amakhala kut sanafe,anangosungidwa kumagwilisidwa ntcito nde amathawako kosungidwako
Pena kumakhala kuti mwini wake amene amawasunga matsengayo wamwalira ndi palibenso owasamalira basi awatsegulira kuti adzipita zoopsatu eee
Mmmmm izi ndizidabwisandi
Next waiting
nkhani iyi ndiyabodza ...munthu yemwe akunenedwayo amapanga ngaiti mmmutu simmayenda bwino anangosochererako coz munthuyo ndiwakwa Chinakanaka ..
Watching from ntchisi
It can not happen that's so amazing.
Amati khulupirira ngakhare usanaone brod
Why don't you show the face of the particular person?
Exactly
You don't just post someone's face without his/her consent. You can be sued. I guess thats the reason. Komanso a councilor kufikila Popeleka umboni ndiye kuti ndi zoona..
Tionetseni wokufayo
Zochitika m'masiku otsiriza machenjera amdyerekezi
Osakhulupira kwa tonse owerenga tiyeni tikhale mmaso,wakufa sadziwa kanthu bii
Kodi inu bambo osapeza mkazi wina,ndikupemphera ,ngati mutachita bwino nkudzakumana ku ulemerero wa mulungu
Mayi kd anakupasani zingati moti paka inu muzichimwa chotele
Muziika bwino ma head line anuwa mwatipu tsitsaka a khansala kukhala so ngati ndiwo muukawoka kkkk
Eeeh komanso mafunso ake ambwelera bwanji😅
We need to see her face why don't you show her face?
Ndintawi ya mulungu, ndaionanso ku Tanzania munthu wabwela
Aaaaa tkufun wakufayo ife
Mas ever Dadi isu
Watching from KATETE Zambia
Zam'Zam'masiku omaliza no wonder
Izi ndizo opsa asaa 😥😥😥
Zoyona
Eti osawaonetsa?
God is going to judge one by one.
It will end in tears. Akamazazindikira kuti Prophet akuwabera it will be too late.
A similar episode of 2010. Ask me
Tiuzeni, what happened in 2010?
Ndinzukwa ameneyu
Km athu tikumuseweletsa mulungu
Why don't you show the picture of a person
Part 2 please
Mundkodole akabwera kulilongweko
That's just jiin
Musamatiwone ngati zitsilu ife ayi khani zikungofanana bwanji ndinu agalu kabasi
Angofanana
Amapempere ena akufunika asiyisidwe msanga kumalawiko, akupengetsa anthu kwambiri
Kkkkkk mulungu akuulula zisisi zake
mbwerera za channel
mzimayi uyu?
Headline yamtundu wanji iyii Kodi mumangoziyamba osadziwa malembedwe ankhani etiii mxiii
Chezani ndi waukayo osati akhansala ngat zandele,mafumu kulibe?? Osamatinamizatu
Show us the person pliz
Kumalawi nako
Mibawa ikafike uku
Chiwanda chimenecho
Amalawi tili busy
Munthuyo ndiyemweyo, ngati anafika ndikuyitana ana ake komanso kukumbukira munthu woti anamusambitsa panthawi yaima yake. Ndiye choti, anthu mukayikirenso ndi chiyani?
Kodi anthuwo samamuzindikira meaning kuti anasintha nkhope?
Bodza.... Mzosatheka munthu kufa mkuukanso...... Anali asanafe ameneo
Alady didn't die, a devil is a liar
👿 Demons power😈
I wish l would see the face of the specific person who has resurrected
Ayi sanali wakufa, Koma nzamasenga zija amakonza abathwa aja kapena ndondocha zotenga ndalama zija ndima ziwa bwino za kumeneko nkwamasenga panopa Wanthu ambiri mbiri panopa akuma bwerera nzosadabwisa kumene ndiri kuno Wanthu ambiri akufa akuma bwera ati ku Blantyre mkumene amaka gwira Ntchito mwa A mwenye
Nde mpaka zovala zamunthu wakufa Sept amasungabe
Mwina ndizoona kuli apulofet kulilongwe nsewu wa kasia
Ku Lilongwe ayendako bwanji
Nzukwa umenewo
Nde bwanji mukuti mzimayi uyu??? +
Mutitumizilekonso akabwela kumapemphelo uthenga umenewu
Koma masiku otsiriza timva mkuona zinthu 😮
Tiyamike kumwamba kuti Ambuye akuchita z
Aaaaa osamuona
wonderful
Nde simunayitane A police bwanji!?
Nanga osationesa mumthuyo bwanji???
Muli mzimayi uyu wauka kwakufa ,mzimai wake uti?
Muzatiuzenso kuti kulilongweko mwaendako bwanji
Chikulupililo chani ndi chachabe
Shaaa
Show the face of the risen .
Waoo 😢😢
Zaziiii
Comedy
Tam Navy from Zambia that's total lie
That is not true😂😂😂😂😂 wait for God's judgement. The problem is that these people live for a while and then die forever.
Is this true
timakukondani komanopenapake mukamasakaniza zinthu mumatipatsa peee kuti kodi akutibwanji amenewa
Zozizwitsa sizizatha
Koma ndi omwewo
Za mstsenga munthu samwalira
Why don't you she person's face?
Vdormc
Bible ndi Colani sanena choncho??????
Nkhaniyi isanthere pompho mudzatipasilitso
Iiiiiiii Inu munawagwilaso? Mmmmmmm zolilisa
Zongofuna kuwagunguza mitu anthu basi