Це відео не доступне.
Перепрошуємо.
Kusumira IMF? Uyuyu ndi Future President
- Додати в
- Мій плейлист
- Переглянути пізніше
- Поділитися
Поділитися
Вставка
Розмір відео:
- Опубліковано 14 сер 2024
КОМЕНТАРІ • 116
Наступне
Автоматичне відтворення
BON KALINDO LERO 12 AUGUST WANG’ALURA MCP AKUTI AKUPANGA MA PLAN OFUNA KULIMBANA NAYE KOMA SAMUTHAMakosana
Переглядів 75 тис.
What's the difference between the IMF and the World Bank? | CNBC ExplainsCNBC International
Переглядів 1,1 млн
BRIAN BANDA EXCLUSIVE INTERVIEW WITH JOMO OSMAN CURRENTLY DEPUTY MAJOR OF BLANTYRE CITY. ZINAKUMANAMakosana
Переглядів 85 тис.
👊ЧЕРНИК: Все! Під Курськом НОВИЙ ПРОРИВ. Підходимо до АЕС? Путіна ПРИТИСЛИ. Готують ТРАНЗИТ ВЛАДИ?Сейчас
Переглядів 437 тис.
ЖИТЕЛІ Курська ЗНЕНАВИДІЛИ Путіна! Бункерного ЧЕКАЄ... | ГАРЯЧІ НОВИНИ | ТИЖНЕВИЙ ДАЙДЖЕСТФакти ICTV
Переглядів 715 тис.
Алексей Воробьев - Всё остальное - лишь товар. «Профессор Тод Лебен» (лекция №5) Автор - А.ВоробьевАлексей Воробьев
Переглядів 3,7 млн
KLAVDIA PETRIVNA, МАША КОНДРАТЕНКО - ЇДЕ ДАХ (OFFICIAL VIDEO)Klavdia Petrivna
Переглядів 746 тис.
Paris Olympics 2024 Fulfill Bible Prophecy And Everyone Is TERRIFIED!God
Переглядів 715 тис.
50 Hollywood actors who died so far in 2024listoholic
Переглядів 1,1 млн
Times Exclusive featuring Isaac Osman - 10 August 2024Times 360 Malawi
Переглядів 6 тис.
ABITI WILLIAM DAWOOD kusosombetsa NEC ya UTM...zimvere mtolo kachilungamo kalimo umu👐👐👐LIKI-LIKI Ladies
Переглядів 15 тис.
Enock Chihana kuulura poyela zinsisi zomwe chilima anamuuza asanamwalire zokhunza Tonse AllianceMakosana
Переглядів 232 тис.
Olo Anthu A Ku Kasiya MCP Sakuyifuna - Comrade NtanyiwaNyasa VoiceBox
Переглядів 24 тис.
MALAWI COURT.... TAMVANI IZI ABALE 🤔Jimmy
Переглядів 132 тис.
"New Dawn" in Bangladesh? Nobel Peace Laureate Muhammad Yunus Sworn In as PM After Student ProtestsDemocracy Now!
Переглядів 481 тис.
Imfa la Saulos Chilima. Kulira kwa niece wa Bingu, Abiti Wiliam Dawood.Malawi Page
Переглядів 33 тис.
🤯 ЗДУРІТИ!🔺КУРСЬК: куди дійшли ЗСУ? 🦾 Наступ на Росію ЗВІЛЬНИТЬ Донбас? Новини від ЯніниYanina Sokolova
Переглядів 551 тис.
«Це край, де я родилася й живу! І нікуди я звідси не поїду» #shortvideoСуспільне Запоріжжя
Переглядів 307 тис.
КУРСК в ОГНЕ, кадыровцы грызутся с ГЕНШТАБОМ РФ, а СКАБЕЕВУ послалиТелеканал ICTV
Переглядів 1,5 млн
"СВО” довела РОССИЮ! УРА-патриоты ПРИУНЫЛИ! Гражданская оборона 2024 - 30 полный выпускТелеканал ICTV
Переглядів 1,7 млн
Путин о боях в Курской области: Главное - выдавить противникаAKIpress news
Переглядів 1,5 млн
ВСУ наступают под Курском. Путин требует действий. Эвакуация в Белгородской области. НОВОСТИРадио Свобода. Новости
Переглядів 1,6 млн
Get 10 Mega Boxes OR 60 Starr Drops!!Brawl Stars
Переглядів 5 млн
Azungu amakonda dzisilu monga chakwera
Ndipo nzungu Amazonia zisilu kwambili powagwilitsa ntchito mwauchisilu like chakwela
Palibe chosatheka,ndizotheka ndithu kusintha malamulo amenewo before 2025.ndizotheka ndithu let's give support him.
DENIS MAHATA ndi Thomas Sankara wa malawi 🇲🇼
Ine ndiye ndamukonda
Malawi has a lot of intellectual people and mostly very talented and like late sk they knew that he was wise but was polluted with his mind with corrupt money at the time he was very desperate for saving enough money to use for his upcoming UTM campaign and unfortunately he was assassinated bcoz the other party knew he was getting equipped to severed his relationship with Tonse but the problem was that he also knew that the very ruling party at this moment also stole the same am of money and even more than him. He knew what was under the scrotum of his opponent and he was done and finished, ndale za usiku. Greetings from UK.
Zoonadi brother munthu ameneyo alibwino alibwino ndipo chakwera samaziwa nthandauzo la ( IMF )
Captain Ibrahim Traore 36yrs wasinthiratu dziko lake panopa dziko lonse likusapota Traore koma zisiru za ku Malawi kuno zosakonda dziko lathu lino limangogwadira imf pomwe ndiyokuba
we need young smart men like him look at Ibrahim very young but smart he took over the country couple months the country has been changed. why not us let him be a president and bring changes to our country
IMF kuthandauza kuti freemasons members intentional .koma Satanic mauwa amawabisa ndizolinga zao ndechoti muziwe ndalama ija akakupasa simumapindula zosatilake ndimavuto monga njala kugwa kwandalama yanthu kukwera mtengo kwazinthu ifa pafupipafupi Ngozi zonsayembekezera
Ndipo ndi anthu akupha
Ndagwilizana nazo
He’s young, however super smart, genius, talented young men,he knows how to improve our country being land locked country.
Tiyeni tipange ma demo atsitse zaka akulu akuluwa atitopesa
Any time any day any week any month from now tiwone zomwe sitinaziwone a chinyamata azuka
Uyuyu ndiwoganiza, zitsiru zimangovomera zina zili zonse IMF ndiyokuba koma ife a Malawi timagwadira azungu kupotsa
Wachinyamata ndi amene akufunika ngati president wa Bukina fanso
Ndili pambuyo pake , and zikangotheka zoti aimile u president watenga vote yanga sure
Ndizoonadi azungu samafuna kuti africa ipite pa tsogolo ndinkona amabweretsa ngongole zawozp
Kwambili azungu amakonda zitsilu kwambili koma amwene kwathu kuno mmmmmmmm
Chakwera ndi puppet wa azungu and thats why you see kuti ndalama za IMF zija amati Extended Credit Facility zakhala zikubwera since Chakwera became President and amatiuza kuti their govt has trust of the donors komano on the ground chomwe tikuwona ndi umphawi okhaokha
lets welcome him
Zopanda tchito zimenezo munthu aliyese akakhala kunja kwa boma amaoneka ngati azelu
Inu mayiko onse muwaunawa otukukawa ali ndi ngongole zambiri mbiri ku chokera ku IMF for example south Africa zambia Nigeria just to mention a few
I know this Dennis. He was our university president. He is strong.❤
❤❤❤❤❤ .koma uzamasionese ngope ata kukupanga chiwembu chimwene
❤
he is a supper hero
But he should be careful coz azungu safuna anthu okuda kom Ali anzeru...
Sumaona bakili muluzi tv amakationetsaso mapick omwe achimene akuyakhulacho katundu bakili muluzi tv
❤ tilipa mbuyopake
TIMUVOTELA KUSIYANA NDI MANYI ACHAKWERAWO MBOLA YOPINDIKA YA CHAKWERA, MFANAYO TILINAYO PA MBUYO BOLA ASAMUPHESO
Nokha mukumuyamikila nokhaso mukut ndindan alibe dzina aaàaaa😂😂😂😂😂mwatani kod
NRC Natural Resources College-Tikuchidziwa bwino chipani chmenecho...😅😅
Yes Thomas njala was 29 from Burkina Faso, Abraham Tiro from South Africa was 28 but he asked un comfortable questions to these lolonial masters
Ndimaganizo abwino potengelanso kuti alikunja kwaboma ,
Nkhope yeniyeni yamunthu imaoneka akakhala president wadziko , palibe amadziwa kuti uyuyu alipoyu ndi mwini umbava ndi umbanda ,
Akhale careful with prayers and wisdom. Azungu ngakhalenso mbava zandale kumalawi zimusowesa.
Munthu ameneyo abwele bas 😊
Tell him, he is welcome tinve zomwe akufuna kupanga
Munthu wa nzeru ameneyi, ati Denis Thanthwe Nkhang’a Mahata Eeh 🔥🔥
Kwa ine uyuyu ndi munthu wofunika kwambiri muno mmalawi same like kabambe
Koma nde mwatilongosolera bwino. Great improvement bro. Kp it up
Thanks thanks 🎉🎉
Are countries forced to borrow money from IMF??
Perfect question
Ngati kuli Anthu akuba kwambili pa dziko ndi IMF fiti za Anthu
@@gwatandingo9502 100%
Bwanji sanasumire a president anthu? Mwawona tsopano kuti president mmangompaka zinthu zoti sizimukhudza. Mesa Inu mmati president ndi amene amatsitsa kwacha? President alibe chifukwa anthu mmangomunena popanda chifukwa.
Bola azipanga zakezo mwanzelu, sikuonpa koma moziwa chomwe anguchite akaziwa ndekuti udolo wake ukhaladi odalilika zikomo
Umakhala ndi nzeru zabwino koma ukazitulusa ndikumakhalabe mokhulupila aliyense umaphedwa nde azikhala oziwa. Tikufuna anthu oganiza zanzeru chocho koma azichenjela , osangoganiza then kufa aaa.
Mwana uyu ndi katakwe
Mmmmmmmm brz sadasumile km amangowaunikila anthu
IMF sikakamiza ngongole. Timapita tokha kukagwada. Wamwa Ambuye mtengeni ameneyo.
Izitu ndi zoona ndipo ine ndi zomwe ndakhala ndikumaganiza koma poti tiribe kuthekera kothandizira kusinthako. Anthu oganiza chonchiwa (let's support them)
Za zakazo zikumphinja kwambr look at Burkina Faso president zaka zake 35 akukwanisa kumene km izi zoti president akhala wazaka 35 above szoona zmnezo
That's true bro za zakazi azioneso bwino
That's true
Vuto si IMF koma amene amapita kukatenga ngongole kumeneko
I have loved him most
Dziko la pansi limadani ndi anthu ozindikila take note
Munthu ameneyu Kodi chakwera samupha chifukwa chakwera mmmmmm palibe kalikose. I
😂😂 Muli ndi ma lawyer angat boss?
Ndi chigayo Mr Mahata
Koma muthu amwene ndi dolo kwambili
Vuto ndi asogoleli amafuna za IMF cholinga agawane
The great achievement
Malawian cameras mwabwera inuyo, ask him akupasenso video ya press briefing yomwe anachititsa some two years ago around July 18/8. Ada awawa has what it take to be a leader except the so called age. Ngat presidential age ili open kwa gogo ikhalenso open kwa mwana.
Mmmmmmm atha kukhala president kwakanthawi kochepa, azungu atha kumupha
Tili pambuyo pake 🔥🔥🔥🔥🔥🔥
🎉🎉🎉🎉🎉🎉
Owo
And we need other kind of education,
Chakwera ndi mbuzi kodi ameneyi timakamutenga kuti mbuzi yosaziwa chilichonse
Ali bo kwambili tamulandila
Kodi chilima nayeso mumati ndi wanzelu. Nzelu nsi ku school chifukwa zomwe timamphunzula ku school ndizoti ena analemba or they experienced it
Bola asasowesedwe
Tamulandila ife
Amwene mumvereni Denisyo mofatsa ndiye mubwerenso ndi presentation ina.
Malawi akufunika anthu ngati awa gwenembe amangovomelera chili chonse..
Mwasowatu boss
Amwene chakwera ndi wamkulu kwambirii, computer saikudziwa zangovuta Chilima uja
Taonani 4 yrs yatha kuno ku Ntcheu wapanga chiyaniii
Nsewu opita ku Dzunje panopa zoopsa kwambirii
MCP sikuona kuti paground palibwanjii
Ine siwandale,zithu zakwela kwambirii
Dzikoli likufunika anyamata oganiza mwakuya not malilime
Fertilizer mmmm zafikapa boma likadangonena kuti mafumu ayambeso kulamula anthu awo basi
Boma lalephera
Katangale mmm
Kuvetsa chisoni mafana oganiza bwino akupitaso mmm
Tell them
Biseni chakwela asamuone asowatu kkkkk
@@HamidavioletYassin 🤣🤣🤣🤣🤣 muli ndi Lawyer?
@@MalawianCamera hahaha musiyeni nzanu alire mwamtendere kkk
Ndamukonda uyuyu
Dolo ndiyemweuja bakili muluzi tv bas km iweyo mani palibeso umalankula zogwila ntima kaya umaona ngati timazikonda umakambazi umazinamiza zd bola ungosiya umataya thawiyo zd
Eeeee ndi mwanadi ameneo kma ndi wa mzeru ka bwanji Ibrahim traole ndi mwanaso osakwana zaka 35 km bwanji akumukonda kwaoko ndie anawo amzeruwo kusiyana ndi akulu akuluwa ka
Okay
Kd Mesa ndalama za ku IMF timakapempha tokhaa?
Ali ndizaka 32 not 29
Ndi wa 95 mesa
Tili Pambuyo pake
Palibe zosatheka man bwanji kodi
Ndidolo mfanayo😂
Your talking zoveka zokha zokha
Komano iyeyo Ali nazo ndalama?????
Ali bho ameneyo
Anawo ndie ali bwno km kunoko ndie eeeee sizingatheke
Abwinowa akumaphedwa chonde asamale mwanao
Amupha ngat chilima uyu
Komaso iweyo aseyee ndiwe kape zd umakambs zaukape ulibe zelu zd
Kamer❤❤❤
Ndesudziwaso kulondolalozakhani
Akhalise Malawi tankonda
Kkkkkkkk zachabe
Ayambe kaye u MP then next tym azaimile u President
Big lie alipo ena atha kusintha Malawi
Tayipangani muve
Kodi sheikh mufuti madengo Ali kuti nkhani imeneyo amailongosola bwino ndithu ine ndimamusatila maulaliki ake Osati masheikh anawa satanizm
🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥
Ndindanikwenikweni
Ndili pambuyo pake , and zikangotheka zoti aimile u president watenga vote yanga sure